Why simukunena number ya asilikali omwe aphedwa a ku Malawi?
@fastMalawi5 күн бұрын
Atatu🇲🇼
@MariaDandazaraJSDmoio2024e5 күн бұрын
Kulimba azake chifukwa chiyan
@fastMalawi5 күн бұрын
Eti eti
@JosephyMakunganya6 күн бұрын
Sometimes I don't understand why We Malawians( we )go there,this is not only peacekeeping there is something Behind 🤔
@fastMalawi6 күн бұрын
Kwambiri 🤝
@BernardKalongah6 күн бұрын
Chakwera , pamodzi ndi azimzake akulimbana ndi kufuna kukhala olemera kwambir padziko lonse la Malawi, osati kuthandiza anthu / dziko , Koma kuthandiza mimba zawo komanso mabanja awo okha ,chimene tikudira apa ife ndi anthu angat omwe Angapezeke pa top ten ya anthu olemera pamalawi, I am show kwangangotsala chabe kanthawi kochepa kwambir ,tiwaonetse agalu amenewa,mbava, alesi ,
@fastMalawi6 күн бұрын
Kwambiri 🤝
@rashidadan25336 күн бұрын
Ntchito ya usilikali ndiyomweyo palibe kuthawa
@fastMalawi6 күн бұрын
Ndipo kwambiri 🤝
@BernardChikopa7 күн бұрын
Zooona anthu andale kaya akalowa kimenekunja kaya amamwa magazi achani chifukwa onse saganiza za anthu....koma mimba zao eeeee,,tikapuma kumwamba...
@@fastMalawiDRC ndiyomwe asilikali amabwela ndi mamilion enawo ankhoza kupita kunkhondo koma akusakako gold
@fastMalawi6 күн бұрын
@UsumanUsumanwillo zosaendatu
@UsumanUsumanwillo6 күн бұрын
@@fastMalawi kwambili
@UsumanUsumanwillo6 күн бұрын
Eyetu nkhondo sangangonyamuka amalawi ndi ma South Africa kuli ma Uganda ,Rwanda American zonsezo chifukwa cha kuluna boys mupange vedio ya kuluna boys machete muone mmene amakhapila anthu sakulakwisa koma ndilamulo la military
Kurankhura kopusa azanu ataya miyoyo yawo azibare awo akulira Inu basi kumarankhura kopusa kuteroko enanu Chirima mumamukonda kuposa Mulungu eti?Ofa lero safa mawa Oro iweyo ukhoza kusowa ngati Mulungu angafune cz Miyoyo yathu iri m'manja mwa Yahweh
@SliviaJosephy9 күн бұрын
@@SusanaMakanga ndiye iwe chakupweteka ndichani zautsilu basi awatibule kumene onse athere komweko ntchito zake zolembana pachibalezo,,, tachokani apa nanu fokofu,😏
@UsumanUsumanwillo6 күн бұрын
@@SusanaMakangasukulu ndiyofunikatu akanalowa nkalasi anthu akutelowo sakanayakhula nkhondo ya military ndiyovuta kupanda asilikali mwinaso anthu akuitanidwa kuti kuluna boys bwezi atatipeza mu africa
@SailotaSamuel9 күн бұрын
Tune your voice please 😮
@fastMalawi9 күн бұрын
🙏 I'll Try
@DicksonKamwendo9 күн бұрын
Rip our Sodiers u have done ur best trying to bring peace in Africa.