JESSY KABWIRA KUTOKOTERA DPP & APM
17:30
14 сағат бұрын
MDYANGU COMEDY SERIES 31 JANUARY
28:44
19 сағат бұрын
Пікірлер
@ShaffieOmar
@ShaffieOmar Сағат бұрын
Bushiri my vote
@franciscoduartie5762
@franciscoduartie5762 Сағат бұрын
Chiphwanya wachesula Prosper
@ShaffieOmar
@ShaffieOmar Сағат бұрын
Leah
@AlickJam
@AlickJam Сағат бұрын
Ma fund aja akat azifikila mmanja mwa anthu ngat awa bwez anthu ambiri atathandizidwa
@CharlesKapwanya-r2x
@CharlesKapwanya-r2x 2 сағат бұрын
Zonsezi chakwela bc moyo ukuzuza kwambili
@HalimaBwanali-f4g
@HalimaBwanali-f4g 3 сағат бұрын
Azinena chilungamo lelo alipoyera
@MalliamAli
@MalliamAli 3 сағат бұрын
Mulungu azikudalitsani bwana
@raytavares2256
@raytavares2256 3 сағат бұрын
First lady mai busa😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂Hilarious indeed calling ndidza pafupi poo
@MasankhoKausi-b2j
@MasankhoKausi-b2j 4 сағат бұрын
Mbambande
@TamUs-u2h
@TamUs-u2h 9 сағат бұрын
My vote to Chalakwe , president opandadi tsankho, ene akuti akazolowa m"Boma azasamutsa ma office from LL to BT kkkkk, Tele si tsankho ili? Koma ma cadets ndinu otembeleledwa
@chiefmitengo
@chiefmitengo 9 сағат бұрын
Nkhani yabwino ya ma school ngati iyi, Tele munthu obadwa Kwa amake ndithu ndikumadana ndi izi? Ma cadets chitani manyazi msanje si sikuthandizani, ndale sitidya AI koma chitukuko. Ndipo musazinamize kuti DPP izalowaso M'boma ng'oooooo
@EnockMpaha
@EnockMpaha 10 сағат бұрын
Ama mwafika apa down thawi yomweyo kkkkkkkk
@LimbikaniHaulesi
@LimbikaniHaulesi 13 сағат бұрын
Katundu
@Malani41
@Malani41 15 сағат бұрын
This a joke. No need for leaders!!!
@PaulKambalame-l2e
@PaulKambalame-l2e 15 сағат бұрын
Kukhala ndimunthu ngati uyuyu ndichinthu chonyaditsa ku dziko ndipo tikuyenela kumuchita cover monga mdalitso wathu koma ife ndiameneso tilipatsogolo kumuipitsila mbili tsono tikamati anayenda bwanji kuchokela ku south Africa timafuna aphedwe? eshiiiii amalawi tilindimsanje ameneyi anathawila kwawo ndipo Kaya anthu akuluakulu aboma anathandizilapo zakuchoka kwake kuchokela ku south Africa anthu amenewo sanalakwitse ndipo mulungu awadalitse anachita zotamandika komatu Steven kayuni anthu amakudandaulani mulindi khalidwe lolakwika sinthani please 🙏🙏 achisaleso anakudandaulani kobasi apa ndiuyuso man of God akukudandaulani inutu mwazi wamwana wa prophet shepherd bushiri ulipa mutu panu😭😭😭mau anga nawa kwa man of God pitilizani kukhala munthu olimba mtima vuto munabadwila dziko la anthu amsanje inu musabwelele mbuyo Kaya nkhani zachifundo pitilizani kugwila ndithu osafoka tizazindikila koma mochedwa mulungu akadzathana nanu padziko lino lapasi 🙏🙏🙏
@GrecianKamwendo-s4l
@GrecianKamwendo-s4l 17 сағат бұрын
Kkkkkkkk chiphwanya watani zimayi
@PeterBendeka
@PeterBendeka 17 сағат бұрын
Watch ING From jouberg mulibo guy's
@JamesMachunga
@JamesMachunga 18 сағат бұрын
Koma umphawi ndiwovutadi president ndi duna zake zigoba ndalama za Malawi inu mukuchoka pamenepo kumagona ndidyala anthu Inu womvesa chisoni ndithu
@noriesingini
@noriesingini 18 сағат бұрын
Watching from Lilongwe kawale 2 nanjati
@Georgejames-d4z
@Georgejames-d4z 18 сағат бұрын
Kkkkkkkk koma chuma
@noriesingini
@noriesingini 18 сағат бұрын
Prophet mulelemba big man he is a talent man
@ShillahYohan
@ShillahYohan 19 сағат бұрын
Madoba doba sopano mwatbiliwa mbuya
@AlicksonMakata
@AlicksonMakata 19 сағат бұрын
Koma eeeeee anthu inu mwafatsapo.
@GeorgeKhonje-q3u
@GeorgeKhonje-q3u 19 сағат бұрын
Mwana wamkango😊😊
@MaxwellNamwela
@MaxwellNamwela 19 сағат бұрын
Ine watching from lower shire-chikwawa mmalawi Momuno!!
@KelvinBandah-o5v
@KelvinBandah-o5v 19 сағат бұрын
Lies of kasakula
@StoreRoom-j7u
@StoreRoom-j7u 20 сағат бұрын
😂😂😂😂😂😂
@ShadreckEsauh
@ShadreckEsauh 20 сағат бұрын
HKkkkkkkkk
@GreyGrant-jr4fs
@GreyGrant-jr4fs 20 сағат бұрын
Adah awawa kkkkk
@langsonmndalanga
@langsonmndalanga 20 сағат бұрын
Maka ifee kuno ku Northern gate what's ever kulibe chitukuko tingoona ma tunker akutidusa kuno ku Karonga koma sitiziwa kumene akupita
@YunusFikra
@YunusFikra 20 сағат бұрын
Jelousy basi? Ochewa sazatheka😂😂😂😂
@geofreydzinyemba6107
@geofreydzinyemba6107 21 сағат бұрын
Ulemu wanu guys
@LawrenceBelson
@LawrenceBelson 21 сағат бұрын
Mpaka kuonesa chimimba koma namachende iwe
@MaggieGirl-n6b
@MaggieGirl-n6b 21 сағат бұрын
Koma mumandivesa kukoma anthu inu
@AlefaKhumalo
@AlefaKhumalo 22 сағат бұрын
Nde agan azionatu kkkkkkk😂😂😂😂
@kumbusemu9446
@kumbusemu9446 22 сағат бұрын
Eee koma mercy uli ndimwano iii
@kumbusemu9446
@kumbusemu9446 23 сағат бұрын
Watching from Groenkloof Pretoria
@Littlefair7
@Littlefair7 23 сағат бұрын
Funso lokuti anatuluka bwanji ku south africa ndi lopanda phindu, nditakhala ine sindingabwerenso ku ma interview anuwa.
@EbstoneKonzani-q7x
@EbstoneKonzani-q7x 23 сағат бұрын
Prosper wakumana ndi zotani ku subi
@EbstoneKonzani-q7x
@EbstoneKonzani-q7x 23 сағат бұрын
Mabanja
@daviemakhumula4932
@daviemakhumula4932 Күн бұрын
Awe
@MdapataBlessings
@MdapataBlessings Күн бұрын
, c.
@NiyaMwawa
@NiyaMwawa Күн бұрын
😂😂😂😂
@chifunirokandeya4647
@chifunirokandeya4647 Күн бұрын
Koma Mulelemba😂😂Aroma amalemba mwa chani...
@Collen-d3p
@Collen-d3p Күн бұрын
Mukumbutseni wayiwala shoti ameyo😂
@PriscaMphuwa-iw4mm
@PriscaMphuwa-iw4mm Күн бұрын
🎉🎉🎉
@JonahJere
@JonahJere Күн бұрын
UTM MY VOTE
@georgeamosi9931
@georgeamosi9931 Күн бұрын
Prosper
@TreezahKapandasalu
@TreezahKapandasalu Күн бұрын
😂 😂😂😂
@FaheemChipojola
@FaheemChipojola Күн бұрын
Arsenal a Gun 🔫 the ganizani