Amene kupanga za size make gather here kkkkkkkkkkkk koma malawi izi ndiye iti
@stanleykundembo7765Сағат бұрын
Mulungu simunthu a malawi mwanva verse limene Michael usi wamaliza nayo mulungu akufuna kutichenjeza kuti tichenjere nalo boma ili la chakwera chifukwa ndilamwazi wangomaliza ndi verse limeneli mosazindikila popeza mulungu akafuna kuyankhula ndi ana ache amadzela munjira zosiyanasiyana ina mwa iyo ndi imeneyi koma Michael usi sakuzindikira.
@WisikiBlack-gj4gu47 минут бұрын
Awusi inuyo sitikukulupililani ndinu ofoila , kodi iweyo bwanji wangoti ziiii pakafufuzidwe a report laifa ya chilima
@ExcitedBreakingWaves-oh3zb23 минут бұрын
Andale mumakonda kubisala mwa mulungu pamene simuchita zamulungu.
@thulanimpphiri6873Сағат бұрын
Manganya akuyesesa kuti aziwe mau a Mulungu koma akulephera kutuluka munyumba ya falawo
@GiftMusorola-l2o49 минут бұрын
Kodi mchifukwa chani mbuli zina Zama socials media Ku ma Facebook amalimbana Ndi manganya mukutaya nthawi bambo Ake Ndi mai ake anamupitisa Ku school mbuli inu zinakukanika mzanutu Sazasauka Vice president siudindo wamasewera azadya pashoni yake mpaka Kuga iwe ukukukuta mano
@WisikiBlack-gj4gu44 минут бұрын
Tilibe nazo tchito zokukuta Mano ifeyo koma tufuna ulamulilo wa bwino, uli iwe atakhupela bambo ako ungalakhule zimenezo
@sydneysitima50932 сағат бұрын
The talk of no relevance today,the government & leadership no one has trust with
@tasmania52710 минут бұрын
You don't have trust in the government and leadership, but others like myself do have trust in the leadership and its government. Do not generalize your dislike of the current regime because some of us see a future prosperity being laid as a foundation now. We were in Malawi when companies were closed by the previous regimes. We were in Malawi when irrigation schemes and cattle ranches were left in shambles. We were in Malawi when the Capital City was neglected. We were in Malawi when roads wore a new face of potholes. We were in Malawi when MDC was rendered unnecessary by the regime after Kamuzu...the list is endless. Those who hate Chakwera do so due to tribalism and not due to his failures. Musamakhale anthu amkwiyo popanda justification. Play a role as a citizen of the country to help feed your family or develop the country. God hates laziness and anger plus pride.
@Patrick-kambalaСағат бұрын
Km munthu ngt akukanika kumanga church chitukuko adzachita bwanji?.. ndatchula dzina ngt😂
@mishecksipolo715358 минут бұрын
THIS IS JUST A NOISE MAKER.THE SHORT DEMON
@saidimwanyali8969Сағат бұрын
Kodi David mbewe ndi kuyambisa chipani kuja akupita Ku MCP
@MafosayilesiСағат бұрын
Galu iwe Pali mfundo apa
@FidesChandamaСағат бұрын
Usamale iwe a gift ponde ponde ali mmodzi ngati iwe koma adamusowetsa ndiye iwe ndindani
@VitumbikoKaunga54 минут бұрын
Ukanakhara wachifundo bwenzi ukupha anzako mbuzi iwe
Iweyonso ndiye galu weniweni osawuka uhule wamakolo ako unakupangisa kuti jkhale osawuka manganya is VP WA dziko la Malawi ngakhale kwazungu akuziwa kuti kumalawi VP Ndi manganya
@GiftMusorola-l2o45 минут бұрын
Umafuna adankhe vp mbuli yakumuzi zosaphunzira ngati banja lako
@stevenmwamadi303541 минут бұрын
Kape iwe usanditayise thawi yanga iweso ndi crocodile team wamva
@stevenmwamadi303541 минут бұрын
@@GiftMusorola-l2o kape iwe usanditayise thawi yanga iweso ndi crocodile team
@stevenmwamadi303535 минут бұрын
@@GiftMusorola-l2o voice president wakuphayo anapha nawo chirima manganya ndi crocodile wakoyo wamva iwe kumayenda ndi dziko ase
@SEEJSHJEFFREYСағат бұрын
Palibe chamzeru akalankhula awa
@samanthamuller7643Сағат бұрын
Mbunzi iyi usi
@EmilyKanyikaСағат бұрын
Chikangwa
@ShuqItwaСағат бұрын
Usi ndi munthu oipitsitsa uyu, mavesi ngati munthu opemphera