Ndipo CHAKWERA wationesa amcp ndi oipa kwambiri ,Chilima amalakwa chiyani ndiy mfutso lathu daily mupephero lathu mulungu atiyakhe zatikhuza KWAMBILI tikulira kupha anthu 9 what is meaning of this? Ndale zophana zabwanji ? Achakwera MULIBE Muthu inu Santana iwe Chilima kukuikan Paule inu kubweza chipongwe chonchi AI mwaphadi tikuona APA ndipo YEHOVA sakhalat chete inuso mupita
@tingo315526 күн бұрын
Jealous ndi ufiti zoona, Chakwera and mcp is evil to the core
@user-nf3ik3ff6yАй бұрын
Chakwela you mast go
@YohanePatrick-lc2lqАй бұрын
Iwe uli ku soth Africa upite ukavote osamango kamba ayi dzoputsa basi utm yachani ife tili ku mbuyo kwa dpp basi chifukwa tikudziwa kuti ndiyachitukuko anawa ayi akuba anachoka ku dpp anapita ku mcp akubanawoso kumeneko uladi ndiena otele dpp motooooooooooooookutibuuuuuuuuuuuuuuuuuuuuuu2025 bomaaaaaaaaaaaaaaassaaaa
@user-gg6uh2wo4xАй бұрын
Gud news
@KellyHart-pi4hdАй бұрын
Abwana Ndikufuna Ndikuwuzeni dziko ra Malawi sitikufunika mtsogoleli wanyowani chifukwa dziko likakhara ndi atsogoleli ambili wopuma silimayenda bwino ,Coz atsogoleli wonse amarandirabe ndarama zaboma ndiye muganize Kuti tili kale ndi awili Chakwera Akhara wachitatu dziko lizayenda bwanji ?mayiko anzathu mtsogoleli wopuma amamutsakirq zufukwa amumange cholinga asamamulipile kuwopa kuwononga ndarama zaboma, ndiye chikufunika apa tibwelele Ku Dpp Ngati ayi basi timutsiye Chakwera Apange zofuna zake