Mumunvesese munthuyo akuti anali odabwa osati amaziwa akanati anene then boma likanamufinya kt abwerese umboni nde zikanamuvuta ndiyeyo@@EllinaBitto
@SinyoroMoyo3 ай бұрын
Mwina anauzidwa tsiku lonyamuka akanatani nanga .koma ngati anadziwa kale nde Naya amangidwe
@NikolasNanawe3 ай бұрын
amwen inuso mboza pitan ku nkhoti gt mukunena sowona mumafuna munkhale ndi maviews bas amalawi zopanda zeru😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂
@Ishmael3762 ай бұрын
Pitani Kaye classe Mr man
@user-lf6qf2tw5o3 ай бұрын
Mkudikila chan abale ingoyankhulan.kumutundu wa Malawi kt anthu amve km mkamakhala chete chonchi mkudikila chibanz
@martinsailesi17313 ай бұрын
Nkamwa mukuchita kumveka kuti chiyawo chikulemera. And malongosoledwe akao akuchita kumveka opanda confidence. School yochepa koma kukhala wodziwa kwambiri , ndinakuuzani musalekele standard 3
@JoyceBanda-k8t3 ай бұрын
Tisayakhule zambiri tiyeni tidikire tidzave zambiri muthaw yake
@DanielGeorge-l4h3 ай бұрын
Ndiye iweyo umadikila anthuwo kuti afe kaye😢
@EnelessLundu-sn8om3 ай бұрын
Iwe opusa kwambiri...ukuulula anthu atafa kale ndiye ukufuna titani ..ngt mizimu ikukuzunza usatinyase ife apa
@LeonardMhone-cg1tk3 ай бұрын
Mulungu ndiwa mkulu,zonse zikuturuka praise God 🙏
@HarrisonMwanga-xy4sc3 ай бұрын
Anauzidwa,ndege isananyamuke,mpaka kuyisiya ndegeyo mpaka kunyamuka.ambwiye,mwazi wa a chilima uli manjamo.soka,kwa iye,amene anaziwa za chiwembuchi,koma kusiya osanena kathu.moto,wa sulufule ukhale pa mitu pawo,ndi ana awo.
@MaxwellChiwaya-tv7kn3 ай бұрын
Inu inu musakhale ngat boma simulidziwa munthu anakawauza ndani poti oyenera kuwauzawo ndi aboma omwewo or muli inu mungatani tiyeni tidzingoziona choona chenicheni chidziwika athu ndi maso
@HarrisonMwanga-xy4sc3 ай бұрын
@@MaxwellChiwaya-tv7kn munthu yu anali pamenepo ena ndikumuudza chinali chisisi cha anthuwo koma kumeneko kunalibe wa UTM, kapena,onse ogwila ntchito pamenepo amaziwa,za ichi,nanga bwanji osanena kwa munthu,opangidwa chiwembu yo kuti bwana musakwele,umu,pamene mulungu anamunong'onedza,kudzela mwa wina.uyutu,angofana ndi Judas,opasidwa, ndalama kukaziponya,pa kachichi.chifukwa,zizamuwawa paka Kale.
@ChristopherKamphanje-o8l2 ай бұрын
Ok abwana mukunena zimenezo munthu atamwalila kale bwanji mukudziwa kuti kubisa chinsisi kumakhala kuti iwenso ukuvomela zoyipazo kuti zichitike basi inunsu muzigugude pamtima mwapambaso pachimenecho
@HarrisonMwanga-xy4sc2 ай бұрын
Ndiye awa asamabwele,pano kumanena,zoti wina anawaudza kuti,ndege,igwa,ndipo kumamuona Vic president akulowa,mundegemo,kumaziwa pasi pa mtima akukamwalila,koma osachita kathu ndiye akubwela,pano,kumatiudza zitithangata chiyani.akufuna,kundiudza, kuti kumeneko kulibeko wa UTM ogwila ntchito pamenepo? kapena nonse ogwila ntchito ndi MCP?chinabvuta ndi chiyani kukaudza mmozi wa UTM bwana asakwele.kodi,olo unganaona bwana chilima galimoto yawo ikubwela koteloko,ndikukaima ku sogolo,sakadaima?akadafona aziwe,kuti chikuchitika ndi chani.olo,unganalemba pa katoni.akadawelenga.
@EdsonNjonjo3 ай бұрын
Chindele iwe, ndiweso one of them sanakupase ndalama eti
Utadziwa za chiwembucho, sunawauze anthu bwanji chilimayo asanamwalile kuti awone njila yina yomutetezela? Nde apa adzuka mukamaulula zanu ataphedwa kale?
@dysonfysonchifundo22843 ай бұрын
Koma chomwe tingadziwe chakuti pali zina zimayendela ma level, zikanatheka iye kulankhula koma remember osauka alibe mbalume or zomwe akunena zili zothandidza sidzimaphula kanthu. Words of God imfa iliyonse Mulungu amalola koma, Tsoka wakubweletsa imfayo.
@ChifundoChiwanda-ru3pg3 ай бұрын
Nde chomasiya osanena mpaka ndege inyamuke ndi chani? Osatiuzaso basi coz miyoyo ya anthu ofunika inatayika kale ungangotikwiyitsapo l
@PatriciaMbewe-xn7ke3 ай бұрын
Eti eti wandibowa bwanji ameneyu
@MosesKalenge2 ай бұрын
🤯🤯🤯💔💔💔💔💔💔💔💔💔midzim ya anthu onse, 9 ikusowetse mtendele ndinthu ulape😌 😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭
@JohnMeleka-s1t3 ай бұрын
Akanika kukulipila kd uwulula lelo aaaaa km amalawi tulo take
@elias.m.chunga3 ай бұрын
Mbuli simasowa, failing even to speak English clearly😂😂😂
@cynthiataulo52113 ай бұрын
Inunso muli part yachiwembu, you knew and you stayed quiet and now you're busy telling us, where is your conscious. You'll guilty for rest of your life. Zamkutu basi
@GiftGift-d6u3 ай бұрын
How came you kept all this inform before the aircraft depart,,,, 9 life's lost here...
@chrispinmlambamalemboc32282 ай бұрын
Fooolish guy who follow the checks on a military plane.cant we justlet the souls rest in peace.Lets not just focus on VP but other families list their breadwinner's
@AliJack-e6r3 ай бұрын
Mwalowesa chibwanatu guys
@MalawiPage3 ай бұрын
Eti...
@NancyNyirenda-v9o3 ай бұрын
Ndipo inu anthu akungokhulupilila zilizose koma ambuye atithandize ndithu
@wezzieneba92383 ай бұрын
What is it going to benefit now? We have lost a legend, a father of many, a husband to someone, a future leader in whom we had hope. You should have been in the forefront kupulumutsa moyo wa a VP ndi anzawo enawo. At least, kulolera kuchotsedwa job and save them. I wish you would have broken the protocol, run and kneel in front of the VP as he goes to board the plane and then talk to him so that he doesn’t board the plane. Guys this is painful, indeed.
@YoungMwacho3 ай бұрын
Waboza uyu. He seems not Malawians from his chichewa accent. If he new why did he let the people perish like that. This is stupid narration.
@nenaningola3 ай бұрын
Ati ndudikira investigate😂 aah
@smithh.njirayafa58473 ай бұрын
I have stopped to support MCP because of this
@andsenJeke3 ай бұрын
Skc has gone forever inu mumadziwa ndithu God should intervine malawi wants to know the truth of what was actually happened
@ChimwemweMuhelliwah3 ай бұрын
Ndie ndiwe chitsiru,,ukuti umadziwa kt ndege sibwelera..mbuzi iweyo,,bwanji sunanene ku U TM members... ndie chilungamo chanji uwuze aMalawicho?
@Homeofpeace3212 ай бұрын
Chilima Munamupha Uja Nzimu Wake Ukukudandaula Iwe Chichakwela, Chinchewa Chakupha Iwe Umanama Kuti Ndiwe M busa , U president Wanji Okupha Naye Nzako? Iweyo Suzafa? Sitikukufuna 2025 Chitsiru iwe
@madalitsomorris65663 ай бұрын
Why now, how do we know it's true what you are saying, Osati pusisa pano, Malawi will never be the same,
Km2 mukungobwata ayao inu! Shiiii umagwila ku airport yake ya usku or kapena zomwez tuziziwazi . Zsyen this z serious issue, uyu ndwaboza.mboli yakonxo
@ClementAnusa3 ай бұрын
Iwe munthu opusa maganizo kwambiri, you think anthu angakhale ndi chidwi pa mfundo zakozo , what do you think will this silly information help us? Never do such a mistake wamva
@VictorKachulu-y3n3 ай бұрын
Five moba yaku Malawi ili pa social media pitani ku Court mukanene umboni wanuwo because anthu opusa akumverani koma ozindikila kuti Satana akugwilitsa ntchito social media sakhulupilila zonena zanuzo ndiye ngati muli a nzeru pitani ku Court musawope, Ngati mukuwopa kutenga mabodza anuwo ku court mukuwopa chiyani mudiwuza mbuli zimenezo inetu ndine wa DPP koma si zonse kumangowombera mmanja ndi nyasi zomwe ayi ndinu omvetsa chisoni manyazi bwanji DPP wooyeeeeeee Mulungu amayika munthu pa mpando wotsogolera komaso amachotsa yekha ndi cholinga ndawonera a Dad (APM) koma savomereza kuti Mulungu analanda ndilo vuto lili ndi atsogoleri athu 😊😊😊😊awa ndi maganizo anga ndimmene ndikuwonera work up time is almost finished Jesus Christ is coming soon get ready before we die
Zikundiwawa kwambiri mukamaulula pano pomwe mumadziwa chilichonse anthu asanamwalire inunso munatengako gawo pa imfa ya anthu aja
@johnmalupia17543 ай бұрын
Ndiwe chitsilu usapusitse anthu sugwila ntchito ku Airport komaso ndiwe galu, kodi achawa bwanjinu bwanji mumachuluka mbuli? Osamangopita ku mzikiti ku ka swala bwanji a galu mi dyomba inu dzitsilu
Koma anthu akupekatu eeee. Mukulipidwa zingati kodi? Anthu ndiye tili busy kugwirizana nazo zoyankhula za makapewa atangokupeperetsanipo apa. Palibe choona ngakhale cha mzeru wayankhula uyu.
@Rodrick-m8h3 ай бұрын
Nde inuyo bwanji osatiuza zoonazo
@mussahalfraid63953 ай бұрын
@@Rodrick-m8h aaaa kuteroku inunso ndi mmodzi okhulupilira mbwererazi? Vuto lake mu mtima mwanu mwakhazikika zoti Chilima anachita kuphedwa ndiye kamba ka zimene zili mmutu mwanuzo chilichonse chokambidwacho chikumakhala choona kwa inuyo. Mudziwe kuti kagulu kambiri kamene kakupanga mislead anthu ngati inu sikalinso Ku Malawi kuno anthu ake ali kunja akungopeka nkhani inu muzikhulupilira mabodzawo.
@MasegoModukanele-xg2hj3 ай бұрын
Umbuli wa athu ena ndiumenewu mosemuja pano uzikati kati mwango funa kuthila mchele kuti zikome ndiye simunazitenge bwino mwaphonya
@TemboMedison2 ай бұрын
sizikupindula chilichose zimene ukulankhulazo Bola ukadalankhula kale
@andrewkalima3 ай бұрын
Ase khala chete ulibe thandizo lililonse pano siposewelera ndikumatchula maina a anthu zikuchita kumveka kuti ukungobwebweta potengera zomwe anthu akulankhula samala usatisokoneze tinatopa nazo za anthu oziikamo ngati akuziwa zomwe zimakhalira yet you are totally blank,If you had more evidence you could come the very same day.Be carefully
Mphaka weniweni iwe. Ndiwe chisilu wanva? Umadziwa kuti imfa imene ija imatiwawa kwambiri? Vuto ndiloti ambilinu mumangowona pa a Chilima basi koma enafe pano tilibe potsamila. Ndiwe galu kwabasi
@judithchaima3 ай бұрын
Umadikira anthu afe, pano ukudikira report? Imfa ya a Chilima ndi anzawo inatipweteka kwambiri ife ngati mzika za malawi ndipo ndi imfa yosaiwalika choonde osaseweretsa maliro Mulungu akulangani inu
@mustaffahhemmad3 ай бұрын
No evidence how can we trust this. Why you don't want to mention your name..komanso tatolapo chayani pa video imeneyi.. muziponya ma video opanda chikaiko apa
@MosesPhiri-l6e3 ай бұрын
Uvek ngt mwa law signal bwanj edit or wat If u know the damn truth umbon wak uli kt mwin ufun more comments
@MeliaDivala-sl5yk2 ай бұрын
Nde kungouzidwa kt musaipange check iwe nkuziwa kale chomwe chinachitika,mutu wako ndthu.Ukamangiwa ukuona ngt amalawi akhala nawe ntchto
@yowasschitsosa53483 ай бұрын
Unatani uwauza anthuwo kuti asakwele ndegeyo, moti uri serious kumapeleka uthengau anzako atataya abale awo ndwe chitsilu iwe