ARINDI MWANA AGWILITSE. mpungu Joseph nkasa

  Рет қаралды 72,102

NYINBO ZADZANA

NYINBO ZADZANA

3 ай бұрын

Пікірлер: 100
@user-xc3fh3ej4v
@user-xc3fh3ej4v 2 ай бұрын
Nkasa is the one of musician advisor in the country of malawi.....kp it up🤝
@user-xc1gk6bw6m
@user-xc1gk6bw6m 19 сағат бұрын
Wanukha malawi🙏🙏 may God bless you my fadah ❤❤❤❤
@GiftMathewe-fr3kn
@GiftMathewe-fr3kn 18 сағат бұрын
Very nice song❤
@YusufChipojola
@YusufChipojola 12 күн бұрын
Nice mr mkasa sakumva a poster
@anusahjenala1063
@anusahjenala1063 3 ай бұрын
Mwalowa mmalo mwa soldier ndinuyo sopano😊
@user-tv2ic6xd4d
@user-tv2ic6xd4d 28 күн бұрын
Chakwera adzivere yekha uthenga wabho Mr Nkasa
@CosmasJohn-zn4qd
@CosmasJohn-zn4qd 4 күн бұрын
Umakwanira mkasa big up
@user-cb2cv9fz7m
@user-cb2cv9fz7m 3 ай бұрын
Ndipo chakwera ambuye MULUNGU akuone munthu kuipa mtima ngat imfa eee ndipo chakwera wamuonga Malawi
@augustMag
@augustMag 3 ай бұрын
I like this song indeed Mr you are saying the truth All Malawi is Smalling
@user-rc3ze2oi7u
@user-rc3ze2oi7u 3 ай бұрын
WANUNKHADI MALAWI 🇲🇼 MR NKASA GOD BLESS YOU
@user-uz1yp6ni8o
@user-uz1yp6ni8o 8 күн бұрын
Mayo dziko langa
@user-ut5nx5vd6p
@user-ut5nx5vd6p 27 күн бұрын
This man is very creative I'm telling you.mr nkasa more love to you sir
@JoshuaMataula
@JoshuaMataula 2 ай бұрын
Phungu Mulungu apitilize kukupatsa. nzeru zochuluka kuti upitilize kutisangalatsa more fire
@ungweruwinthu6907
@ungweruwinthu6907 3 ай бұрын
What a song.. Big up Nkasa. Sugar Ali pa 3700 now.. Malawi wanukhadi
@giftbanda4518
@giftbanda4518 2 ай бұрын
I love this song. You've said it all Phungu
@ThokohKalonga-je9rx
@ThokohKalonga-je9rx Ай бұрын
Big up mr Nkasa nice song
@AaronWiniko
@AaronWiniko 11 күн бұрын
Legend
@user-jk8sh7fh2d
@user-jk8sh7fh2d 2 ай бұрын
I like this guy too much amaganiza movuta kwambili na nyimo iyi siyandale koma ngamo bsi kuswakuswa sakugawa ma sweet I like once again i like it.
@PatsonYusufMaulana-rj9lf
@PatsonYusufMaulana-rj9lf 22 күн бұрын
Big up my brother,that's Joseph Nkasa whom I know 100,,%
@lastonkandiyado4526
@lastonkandiyado4526 3 ай бұрын
Big man kuzatulukila sopano ndi waduka ndi Malawi ndizona simukunama ayiii God bless you always
@user-yz5yt3vj6w
@user-yz5yt3vj6w 3 ай бұрын
Koma Nkasa umayiponyeradi kwakuya, ❤woyimba koma uyu
@AgnesNkukumila
@AgnesNkukumila 2 ай бұрын
Nice song keep it up
@FugieKholowa
@FugieKholowa 22 күн бұрын
This guy iiiiiiii born for his country
@madalitsoyakobe2123
@madalitsoyakobe2123 Ай бұрын
🔥🔥🔥
@user-pf5er7gc9s
@user-pf5er7gc9s 26 күн бұрын
Beautiful song
@user-oq5rg5mz7q
@user-oq5rg5mz7q Ай бұрын
❤❤❤
@ObreinMhone-hs4vq
@ObreinMhone-hs4vq Ай бұрын
I like his music it's straight and true
@user-op3nx5qt4q
@user-op3nx5qt4q 8 күн бұрын
Ndithawira kuti 😢😢😢 passport ndi license atseka Malawi watha basi
@VernacioChintedza
@VernacioChintedza Ай бұрын
Nice tune big up nkhasa
@InnoPondani
@InnoPondani Ай бұрын
Song with a massage❤
@samdiverson9733
@samdiverson9733 2 күн бұрын
Nkasa umakwana chakwera has to understand the message
@user-im4bs7fk9o
@user-im4bs7fk9o 3 ай бұрын
I like this song very much the meaning is still elevant &power😂
@LazarusBwanali-qw5qc
@LazarusBwanali-qw5qc 13 күн бұрын
Nkasa ndi akamuna
@AlickMwaza
@AlickMwaza Ай бұрын
Kkkkkkkkkkk kuimbatu ndikumeneku
@user-wp5rk5zk7t
@user-wp5rk5zk7t 2 ай бұрын
Davide mbewe woyeeeeeeeee
@LovemoreKachingwe-nm8bz
@LovemoreKachingwe-nm8bz 3 ай бұрын
Big mutchuleni munthuyo kkkkkk mumakwana ndinu prophet
@JamesNgwamire
@JamesNgwamire Ай бұрын
nice song tinenereni basi
@Robert-bx8sp
@Robert-bx8sp 2 ай бұрын
Ñice song
@majendauzananilimitedi2049
@majendauzananilimitedi2049 18 күн бұрын
"galimoto yomwe yaononga nsewu yomweyo singakoze, pakufunika katapila adzakonze"
@MadandoChannel
@MadandoChannel 3 ай бұрын
Eddie longwe Dada general 2025
@CalmBackpacker-lw7ol
@CalmBackpacker-lw7ol 24 күн бұрын
Nyimbo yabwera muthaw yake
@Cleva-dd1qd
@Cleva-dd1qd 25 күн бұрын
Ndi mommo phungu
@user-et6we9mx5h
@user-et6we9mx5h 2 ай бұрын
Mr chakwera please Malawi akuvutika kwambili tavani kulila kwa anthu
@user-nf3ik3ff6y
@user-nf3ik3ff6y 23 күн бұрын
Mukasa umakwana❤
@KayifaSkeffa123
@KayifaSkeffa123 18 күн бұрын
Akupaseni galimoto chondechonde😅😅😅😅
@user-wv5hz8ce3i
@user-wv5hz8ce3i 3 ай бұрын
Ndipo inu zachabetu kwathu komwe ngati ndife obwela mhh
@Alomwe
@Alomwe 3 ай бұрын
Mr Chakwera please tamvani kulira kwa Malawi
@MasterMalekwa
@MasterMalekwa 8 күн бұрын
😢😢😢
@LovemoreKachingwe-nm8bz
@LovemoreKachingwe-nm8bz 3 ай бұрын
Wanunkhadi Nyasaland Maka nthawi ino eeeeeeeeeee
@DanielMoses-yp6qc
@DanielMoses-yp6qc 3 күн бұрын
Kkkkk
@user-cr7iy2tc6f
@user-cr7iy2tc6f 3 ай бұрын
😢😢😢😢 nyimbo iyi inali vumbulutso
@fostenkachinga9945
@fostenkachinga9945 3 ай бұрын
Nyimbo iyii muli uthenga 😢😢😢
@GenesisYafika-cs5nm
@GenesisYafika-cs5nm 2 ай бұрын
Awuze phungu anthu opanda chfundowa,adyera
@Enockjosephy2528
@Enockjosephy2528 3 ай бұрын
Mumakwana big
@mcdonaldgerard9707
@mcdonaldgerard9707 Ай бұрын
Nkasa nthawi zonse amalangiza, komanso kunena chilungamo angokhara osaganiza bwino ndi atsogoleli wo🤔🤔
@user-og9fq6yu9p
@user-og9fq6yu9p 3 ай бұрын
Auze Zions wanunkha
@yamikanikhanga4527
@yamikanikhanga4527 3 ай бұрын
Apadi ofunika D 7 ikonze Malawi
@user-ww3fe2bz2u
@user-ww3fe2bz2u 3 ай бұрын
Zoona big
@grivinmaniwa166
@grivinmaniwa166 2 ай бұрын
Ndiye kuti mavuto a dziko la malawi ndi ogonera. Chifukwatu pomwe ena akuona ngati nyimbo iyi ndi yatsopano koma ayi ndithu ndi zaka za kumbuyo
@Hobiexd-ji9kz
@Hobiexd-ji9kz 3 ай бұрын
Zoo na big
@Henry-vw2cz
@Henry-vw2cz 2 ай бұрын
Double salute mkasa
@user-bq8gb7tb1l
@user-bq8gb7tb1l Ай бұрын
Tokota nkasa,koma nsaku musiye asauka yekha ndi mowa wake,zolinga ndi zofuna
@Cleva-dd1qd
@Cleva-dd1qd 25 күн бұрын
Ndi choncho phungu
@Buleyaprophet
@Buleyaprophet 3 ай бұрын
Kkkkk mutchuleni timuziwe
@geraldlukhere1159
@geraldlukhere1159 3 ай бұрын
Mkunena chakwela was ma trip uyu Kodi?
@andrewchirwa2193
@andrewchirwa2193 3 ай бұрын
Malawi wanukhadi mukuziwakale
@user-im4bs7fk9o
@user-im4bs7fk9o 3 ай бұрын
Usinda
@user-tr4fv6ry9q
@user-tr4fv6ry9q 26 күн бұрын
Big up phungu,we like your music
@user-ur6uh5nm8b
@user-ur6uh5nm8b 2 ай бұрын
Phungu umakwana
@user-yd7di3cf8q
@user-yd7di3cf8q 3 ай бұрын
A malawi kuvutika chifkwa cha vote yao ai zikomo
@regsonhara1725
@regsonhara1725 3 ай бұрын
Komabe zina zikusapotabe kusangalala kuti anthu akuvutika
@ShabaniKuswere
@ShabaniKuswere 24 күн бұрын
Etieti zomvetsa chisoni Ku Malawi
@user-yk9ib1bg2b
@user-yk9ib1bg2b 3 ай бұрын
Koma ndiye wanuknkhadi Malawi lazaro wanunkhitsa Malawi
@user-vq7fz5zu4d
@user-vq7fz5zu4d 5 күн бұрын
Beautiful song ❤
@user-hp8du2lx3z
@user-hp8du2lx3z 3 ай бұрын
Amalawi tili pamoto
@user-ur6uh5nm8b
@user-ur6uh5nm8b 2 ай бұрын
Atupele muluzi azakoza dziko❤
@user-jk8sh7fh2d
@user-jk8sh7fh2d 2 ай бұрын
Eeeh this guy dyela too much like father like son, koma ngati akuganiza atupele and chilima waiphonya
@akimsakala327
@akimsakala327 3 ай бұрын
Ndipo zoonaditu
@user-pj3qi7gb3s
@user-pj3qi7gb3s 2 ай бұрын
Mkasa ndiwe mulosi ndipo ulosi wako ndiwolondola
@user-gl4wc9pq4e
@user-gl4wc9pq4e 3 ай бұрын
Zovuta
@McphersonMsulira-zx2lj
@McphersonMsulira-zx2lj 3 ай бұрын
Mapasaport ayamba kutuluka pamtengo wa 14500
@MaidakaisiNkota-oo5tz
@MaidakaisiNkota-oo5tz 3 ай бұрын
Timadabwa kuti otiyankhulira aja alikuti
@Daniel-wk7uj
@Daniel-wk7uj 3 ай бұрын
IZI tinasankha tokha timati tiyese achinyamata komanso opemphera lero ndi izi. APM amadziwa ndipo anatiuza kuti ngati tikufuna mavuto tivotere CHAKWERA koma ngati tikufuna zabwinobe bola DPP koma ife tinasankha kuvutika ndi anthu amulungu komanso wachinyamata oganiza bhooo.Lero mavuto okhawokha.
@user-pj3qi7gb3s
@user-pj3qi7gb3s 2 ай бұрын
Amkasa 5000 ilipo gaileni number yanu ndikuthokozeni
@user-uc1pd1tc2x
@user-uc1pd1tc2x 3 ай бұрын
😂😂😂😂😂Chakwera wanunkhisadi Malawi mfiti ameneyi zedi ya MCP
@nkopedafter831
@nkopedafter831 3 ай бұрын
😅😅😮😢
@user-uc1pd1tc2x
@user-uc1pd1tc2x 3 ай бұрын
@@nkopedafter831 😃😃😃Nthakati yoopsa zedi tiigwetsa Chaka chammawa ibwelere kumakalima maganyu😃😃
@user-be5fc3ed1i
@user-be5fc3ed1i 2 ай бұрын
Welcom Nkasa kp it up chinyimbo cha heavy Malawi is on for sale koma ndiye wanunkhirathu
@dicksonmlera2777
@dicksonmlera2777 3 ай бұрын
Malawi is on the market
@user-dd1qq5xq1k
@user-dd1qq5xq1k 3 ай бұрын
Malawi for sale
@NYINBOZADZANA
@NYINBOZADZANA 3 ай бұрын
Yamaha man please subscribe 🙏
@user-zu4wc1kw2j
@user-zu4wc1kw2j Күн бұрын
Ndeno nyimbo zako ngat menezi ungapeze 10k views...anzako akulemelelatu zomwe zija iwe busy zandale...fokol
@estonmnthali3719
@estonmnthali3719 3 ай бұрын
Kkkkkkkk
@hardwickkameta1681
@hardwickkameta1681 10 күн бұрын
Legend
@user-ec3xh4pc6t
@user-ec3xh4pc6t 2 ай бұрын
❤❤❤
@DaudJulius-hz8uy
@DaudJulius-hz8uy 3 ай бұрын
Boni kalindo ndi atupele Muluzi akhonza kusintha zinthu tiese amenewa
@user-hs6sh3xz1f
@user-hs6sh3xz1f 3 ай бұрын
Upole moto kkk
@symeonjoffreymapondera9530
@symeonjoffreymapondera9530 3 ай бұрын
Ndiye umbuli
@henryphiri6100
@henryphiri6100 3 ай бұрын
Atupele ndi Peter Muthalika
@user-oq5rg5mz7q
@user-oq5rg5mz7q Ай бұрын
❤❤❤
ANASAKHA OLAKWIKA.mpungu Joseph nkasa
6:53
NYINBO ZADZANA
Рет қаралды 3,7 М.
Can you beat this impossible game?
00:13
LOL
Рет қаралды 62 МЛН
ANAMVA - Phungu Joseph Nkasa
6:03
ZAMAKEDZANA
Рет қаралды 82 М.
MAI JANE  ANSAH ABWERA POYELA KUKAMBAPO ZA CHISANKHO CHA 2019!.🇲🇼
40:06
Peter Nsauka -akwatila chiwaya 🔥🔥
3:23
Peter Nsauka
Рет қаралды 170
Phungu Joseph Nkasa - Mose wa lero
7:20
Nyimbo za ku Malawi
Рет қаралды 418 М.
Kucheza ndi wa Sataniki Mpakana Waziwulula Yekha
20:20
Morton Baghaya
Рет қаралды 55 М.
Joseph Nkasa  -  Ma Millionaire  (Full Album)
51:42
Prime Time Malawi
Рет қаралды 35 М.
AKUFUTSA .mpungu Joseph nkasa
5:17
NYINBO ZADZANA
Рет қаралды 6 М.
JOSEPH NKASA./ SIWANDALE
4:23
MalawI Music Of All Times
Рет қаралды 10 М.
Skeffa Chimoto Apresident new Audio Official
8:35
Yathu Music Official
Рет қаралды 115 М.