No video

Chifukwa Chenicheni Chomwe Shepherd Bushiri Akumangira Mzinda Wa GOSHEN CITY

  Рет қаралды 199,871

Hanifa Mw

Hanifa Mw

Күн бұрын

if you like my content and would like to support me further, please
PayPal
➡️To Donate please use PayPal www.paypal.me/...
Business/Sponsor Inquiries //hanifamw.suggestions@gmail.com
Mu November mchaka cha 2021, pamene mlaliki Shepherd Bushiri pamodzi ndi mkazi wake Mary anathawa belo mdziko la South Africa mkubwera kuno ku Malawi, anthu ambiri anayesa kuti basi watha ndipo sangapangenso chilichonse cholozeka. Hotel yake yotchedwa Sparkling and Spa yomwe ili mu dera wa Rustenburg mdzikolo inayamba kupita pansi popeza malonda sankayenda. Ndalama zomwe amkazipeza kuchoka mu chopereka chaku tchalichi kamba kakuthawaku izi zinayima. Kenako ali ku Malawi analengeza za scholarship yomwe iye akufuna kuthandiza ana osowa fees mma sukulu osiyanasiyana. Apa anthu sanamukhulupilire popeza amkati alibe ndalama ndipo amapanga izi pongofuna kutchuka.
Komatu Bushiri wadabwitsa ndikututumutsa anthu ambiri posachedwapa atalengeza kuti akumanga mzinda m’boma wa Mangochi womwe akuwutcha kuti Goshen City.

Пікірлер: 124
@LovenessLester
@LovenessLester Ай бұрын
That's a great city for many Malawians let's learn how to appreciate this our man of God 🙏
@alfednjolobvi1591
@alfednjolobvi1591 2 жыл бұрын
Bushiri ur a great man that's why ur very blessed I wish if Malawi having too many people like u Bushiri who thinking about there homeland ur great indeed keep it up God bless you more
@richardchaupe7231
@richardchaupe7231 2 жыл бұрын
I salute Bushiri, he is one of a kind Creating jobs for the young people
@teddybanda8989
@teddybanda8989 2 жыл бұрын
That guy has got gold mines here in zambia 🇿🇲 and different countries
@allenchilekw5698
@allenchilekw5698 2 жыл бұрын
Where in Zambia?
@joeljere4385
@joeljere4385 2 жыл бұрын
He is doing great work to develop Malawi
@andersonmasamba457
@andersonmasamba457 Жыл бұрын
t
@josephkaputa8502
@josephkaputa8502 2 жыл бұрын
He is agood man coz he is dealing with poverty,big up B
@michealmwimba6084
@michealmwimba6084 Жыл бұрын
I just like the way you express yourself in chichewa its so amazing and keep up the good work
@lucksonlongwe1658
@lucksonlongwe1658 2 жыл бұрын
Best wishes to man of God. Continue your work. God is with you.
@madakasosoch4322
@madakasosoch4322 Жыл бұрын
He is going great work to develop Malawi
@naongarluhanga3218
@naongarluhanga3218 Жыл бұрын
Hard workers always think about changing things .All the best man
@joebanda3732
@joebanda3732 2 жыл бұрын
You are doing extremely well Sir I like your tone. U got a very bright future. God will exalt you this year. Stay focused and pray more
@stevechizaka9908
@stevechizaka9908 2 жыл бұрын
Dziko la malawi silimatukuka ndi nkhani ngati zimenezi. Munthu ngati akumanga town yamakono ngati imeneyi mudziko lathu.ife bwezi tikuonesa chikondi kwaiye ndikumulimbikisa osati kumufookesa pazinkhani zopanda Pache. Anthu akatangale akuwaziwa kale bwanji osamakawafufuza amenewo
@mussawilliam5684
@mussawilliam5684 2 жыл бұрын
Vuto ndilokuti ife a malawi makamaka kumipandoko kwachuluka achule kwambili mwachisanzo ine ndili kuno ku south Africa ndapedza ndalama ndithawile dziko lakwathu adzafuna kundifufudza ndiye uchulewo ugalu a aphaka Bushili akufuna kutukula dziko lakumalawi ndiye pakupedzeka agalu ena monga amulaka malilo ndijelasi yao kudzolowela kuvutika ugalu basi Bushiri akufuna kutukula dziko lamalawi
@isaacschamatwa3596
@isaacschamatwa3596 2 жыл бұрын
such a very good tone,Bushiri is doing such a good job
@mollymadzibane
@mollymadzibane Жыл бұрын
My Father My Prophet you are doing great job . You are creating work also for Malawians generation . I tap into your Annointing my Prophet . May God bless you all your Enemies will Scarter one by one Molly limpopo
@richardmadaka287
@richardmadaka287 Жыл бұрын
Goshen City is a product of powerful vision
@biggyk7740
@biggyk7740 2 жыл бұрын
I will always support bushiri he is a true citizen of Malawi
@maxwellmustaffaalickalick1745
@maxwellmustaffaalickalick1745 2 жыл бұрын
Ife anthu akuda ndichoncho sanje kwambiri i respect him a lot
@williamlahman2787
@williamlahman2787 2 жыл бұрын
Let him to fulfill his duties,. He's so young, hope will do mo than that. All those jealous people must fall. Almighty bless him
@machonabanda5752
@machonabanda5752 2 жыл бұрын
Hanifa you are the best ♥️♥️🙏🙏
@hoekboy1102
@hoekboy1102 2 жыл бұрын
I salute you Bushiri I will be Uber driver there
@harrietmwika8695
@harrietmwika8695 Жыл бұрын
Love the Bushiris keep it up and God bless.
@simonndou5236
@simonndou5236 Жыл бұрын
Good work Prophet Bushiri
@jestinanamkonda1495
@jestinanamkonda1495 2 жыл бұрын
The annointing of Papa Bushiri breaks the yokes of poverty. Try it. You don't know the businesses Bushiri has. Why being so rough without the knowledge of his wealth and Riches. He is the third richest person in Malawi nde mumati ndalama azitani nazo? They devil will never be happy with a progressive person
@benitozack6523
@benitozack6523 Жыл бұрын
Don't be jealous with someone who is doing great work,because that city will change many Malawians
@richardchaupe7231
@richardchaupe7231 2 жыл бұрын
Please do the same content in English to enable none Malawians understand Unless you are from Zambia and some Zimbabwians can understand
@brucewarchild2156
@brucewarchild2156 2 жыл бұрын
It's none of foreigners business
@chifundonkhoma3642
@chifundonkhoma3642 2 жыл бұрын
Kkkkkkk OK fine.... Please people stop being jealous,instead of focusing on your demonic poverty , you waste time with whom YAHWE blessed... Learn to love one another.. Learn to thank God......
@agnessmpungalume1446
@agnessmpungalume1446 Жыл бұрын
Just wow Beautiful masophenya
@Fanny-h9r
@Fanny-h9r 2 күн бұрын
Boozaa anthu ake ati omwe alembedwa ntchitowo mphekesela ya boza iyii
@englishboy6570
@englishboy6570 2 жыл бұрын
Vuto la amalawi ndinsanje basi
@jestinanamkonda1495
@jestinanamkonda1495 2 жыл бұрын
That is the problem of Malawians
@jtpi8362
@jtpi8362 2 жыл бұрын
Ndi izi mukuziona ku ma comments kuno, anthu a nsanje akumunyozabe m'malo moyamikila kuti a Malawi ambiri apeza ntchito kumeneko, komanso dziko lathu litchuka ntchito imeneyi ikatha.
@willardakidy6916
@willardakidy6916 2 жыл бұрын
Akulephera mapulesident kutukura dziko lanthu ineyo ndingoti Malawi mwana tingathe kumaloza chala kwaathu kuti town yakwathu iyo mulungu pasongolo basi
@mederinausain6913
@mederinausain6913 Жыл бұрын
Bushili ndi one akupotsa president ulemu wanu a bushili za ndare simupanga nawo koma kukwedza malawi pa sogolo ..koma muzandilembeko tchito
@trymoo8479
@trymoo8479 2 жыл бұрын
Ohhh? At least
@ThomasMwandila-tn7cf
@ThomasMwandila-tn7cf 5 күн бұрын
Murekeni munthu atukure marawi
@bashiriyusufu1224
@bashiriyusufu1224 2 жыл бұрын
🔥🔥🔥Wabwela ngat coming 💪💪💪
@user-gs7wc3nx3q
@user-gs7wc3nx3q 2 ай бұрын
Akurephera chakwera kutukura ziko.rino angoononga ndarama chakwera chito zamanja ako zikuchitire umboni bushiri
@chifundonkhoma3642
@chifundonkhoma3642 2 жыл бұрын
Komatu anthu mupole moto... Mmalo mopanga njira zothana ndi umphawi omwe satana anakutembererani nawowo.. Mukulimbana ndiwo mulungu adawadalitsa, kutaya nthawi ndi za zii limbikirani kupemphera siyani msanje, mulungu adzaona mokudalitsira musiyeni Shepherd Bushiri apange zothandiza human kind
@gloriabanda6552
@gloriabanda6552 2 жыл бұрын
this is great💯
@simonndou5236
@simonndou5236 Жыл бұрын
We need ro underatand in english too. Inam in South Africa.
@bobkenneth2947
@bobkenneth2947 2 жыл бұрын
A Malawi Munatani kodi kumangovuta pa zinthu zopanda pake MAJOR 1 akufuna kutimagira Town mukufuna kumufufuza chiyani at least he's creating jobs zomwe Atsogoleri athu saangakwanitse koma kuba basi ndi ma slangs and fluent English opanda pake hands of BUSHIRI Manga Town SHEPHERD...👏👏💪 Let Them Talk, Idiot's come on Homies If you want someone to investigate I'm gonna show you where to go Pitani ku TONSE ALLIANCE that's where you'll find thieves,mbava,akamatule,matsotsi,wawii,🤞😊
@wisdomktitus660
@wisdomktitus660 Жыл бұрын
Aaa pajatu Malawi is full of kaduka,,enawa angofuna amudyere
@duduzilesimelane9208
@duduzilesimelane9208 Жыл бұрын
Man of God who only does God mind not him
@williamjusten6646
@williamjusten6646 2 жыл бұрын
Great job
@anthuochukapazambiaelishas4978
@anthuochukapazambiaelishas4978 2 жыл бұрын
Perfect
@AllanChingwazala
@AllanChingwazala Ай бұрын
Ndimafunisisa utazakhara president malawi ikhoza kukhala yopambana ngat wakwanisa kumanga ndalama zayekha kulibwanji athakhala president buchiri ndimakufila kuzakhala president ndizabwerera kumalawi
@thekuhespodcast
@thekuhespodcast 2 жыл бұрын
The first to comment and hopefully will be the first resident of Goshen 😂
@lilianmazila7688
@lilianmazila7688 2 жыл бұрын
L
@user-gs7wc3nx3q
@user-gs7wc3nx3q 2 ай бұрын
Bushiri uzangokhara president
@thomphalavi5027
@thomphalavi5027 4 күн бұрын
Mzinda umeneu u kubwera ndizolinga chilipo akufuna ku Malawi kuno ndpo zomwe anthu awa zolinga zawo zikwanilitsidwa ndipo akufuna Malawi ankhale mbali imodz yaa tow omwe amachita za satana
@limpopolimpopo2623
@limpopolimpopo2623 2 жыл бұрын
A Malawi sanje mlekeni atukule dziko lathu la Malawi
@mbumbajilowele6511
@mbumbajilowele6511 2 жыл бұрын
Greatest man
@promise3693
@promise3693 2 жыл бұрын
Nsanje aMalawi iiiii munthu akapanga chinthu basi zokamba mbweeee
@webbyasterchengo4006
@webbyasterchengo4006 2 жыл бұрын
That's why ziko lamalawi lizakalabe losauka mphaka kale kale amufufuza bwanji ngati ziko lamalawi labeledwapo nsaja basi ziko losafuninara anthu zabwino
@victormsika1538
@victormsika1538 9 ай бұрын
Ndipo iyi nde ndi mfundo ndithu
@mikegoodblessyoumenofgoodm3482
@mikegoodblessyoumenofgoodm3482 2 жыл бұрын
Moti musangalale akubwelesa Chitukuko ku malawi sanjebasi
@johnboscozgambo71
@johnboscozgambo71 2 жыл бұрын
Thanks for budget
@innocentkandulu2825
@innocentkandulu2825 2 жыл бұрын
That's great
@praisemkutumula3348
@praisemkutumula3348 Жыл бұрын
Great ideas
@duduzilesimelane9208
@duduzilesimelane9208 Жыл бұрын
I like profet he only does God mind not his
@chrisschikozera7271
@chrisschikozera7271 2 жыл бұрын
Ppl are serious wth him ......for show bushiri is doing good jobs for better malawians
@johnbihali9883
@johnbihali9883 Жыл бұрын
But your report doesn't relate with the title of your presentation. Improve pliz
@beautyandnatureofafrica5334
@beautyandnatureofafrica5334 2 жыл бұрын
Nsanje amalawi.. Musiyen bushiri atukule dzulo lathu
@ayamijackson1443
@ayamijackson1443 2 жыл бұрын
Gays tangoyamikilani muthuyu popangachiganizo chotukula zikolovesa chisonili ngati palizolakwika aakoze ndimulungu
@olipamaseko2693
@olipamaseko2693 10 ай бұрын
Zokaikitsa ndalama zake aaa
@victormsika1538
@victormsika1538 9 ай бұрын
@@olipamaseko2693and so???? Nde mukufuna kuti munthu atani kodi. Olo Chakwera atasiya kupusa kwakeku this country can’t still go further because of people like you. Bitter and pathetic person
@AminaPhiri-pp9tw
@AminaPhiri-pp9tw 6 ай бұрын
Zoona zake afufuzidwee munali asadiki miya muzikomo olemera oti amatha kukuthandiza boma lo koma sanafikepo apo fufuzani ndithu
@phikamomo9755
@phikamomo9755 Жыл бұрын
Nice job
@geoffreychimutu6654
@geoffreychimutu6654 Жыл бұрын
More fire
@manuelsamuel293
@manuelsamuel293 2 жыл бұрын
Let him to do what he want to do and moreover he is doing that in his country, so let those dogs who has jealous with him to smile urine
@giftphiri595
@giftphiri595 2 жыл бұрын
A Malawi ambiri amadana ndi chitukuko amafuna kuba chabe, Bushiri asaope munthu.
@victormsika1538
@victormsika1538 9 ай бұрын
Nzoona ndithu
@newdavidomw
@newdavidomw Жыл бұрын
bushiri ndi munthu modzi wachuma yemwe akuyika pa map malawi
@vitumbikochirwa2830
@vitumbikochirwa2830 Жыл бұрын
Enemies of progress.Bushiri is doing this for the betterment of the country. This is malawi property,bushiri is just engineering.its the government which is going to benefit
@tuntufyesichinga1071
@tuntufyesichinga1071 Жыл бұрын
Okay?
@nelsonkausiwa4754
@nelsonkausiwa4754 Жыл бұрын
Major one
@mabvutochimkondenji910
@mabvutochimkondenji910 2 ай бұрын
uyu akhale vice
@bonimpoya1439
@bonimpoya1439 Жыл бұрын
Malawi goas on
@kondwanileonard9868
@kondwanileonard9868 Жыл бұрын
Is right
@user-ng2nu6xn9x
@user-ng2nu6xn9x Жыл бұрын
AKADAKHALA KUTI ANTHU ENANSO AMAKHOBILI AKU MALAWI ALI NDI MOYO AKUONETSA A SHEPHERD BUSHIRI PANOPA MALAWI AKADAKHALA ATATUKUKA KOOPSYA
@victormsika1538
@victormsika1538 9 ай бұрын
Ndipo nzoona kunoku anthu ake ngansanje yauchitsilu nayo
@naongarluhanga3218
@naongarluhanga3218 Жыл бұрын
No need of AcB because he z not apolitician
@collinsassenga3711
@collinsassenga3711 Жыл бұрын
Maiko azathu anthu ngati amene ndi amene amatukura dziko,
@squatmansaidi561
@squatmansaidi561 Жыл бұрын
Kkkk kma guys mawu awa akuyenera munthu wa ndemvu ku face
@phirisandfore643
@phirisandfore643 Жыл бұрын
Papa help me to change my life
@hendmorsoni32
@hendmorsoni32 Жыл бұрын
Malawi akukanika kutukuka chifukwa chansanje
@snetawailiyasa3215
@snetawailiyasa3215 2 жыл бұрын
Ok
@marcelolemos1484
@marcelolemos1484 2 жыл бұрын
Humm
@VincentChikopa-mm6ig
@VincentChikopa-mm6ig 2 ай бұрын
Muuze bushili mon
@olipamaseko2693
@olipamaseko2693 10 ай бұрын
Aaaa ndalamazi aaaa
@cadohjabu5565
@cadohjabu5565 2 жыл бұрын
Mlandu Ukudikila ku South Africa Aonetse chitsanzo chabwino
@innocentchirwa3677
@innocentchirwa3677 2 жыл бұрын
Wabwera mwa coming
@lonmediatech5864
@lonmediatech5864 2 жыл бұрын
Iwe anthu azakumangisa.
@fedinadisakala2380
@fedinadisakala2380 2 жыл бұрын
Sanje amalawi musiyeni munthu atukulemalawi
@frankkamunde4575
@frankkamunde4575 2 жыл бұрын
nsanje ndimene yakula nsinkhu
@sidickbadat1086
@sidickbadat1086 2 жыл бұрын
You have to screen this man the so called Prophet, whenever he got his money and how he made it, because this doesn’t look normal at all.
@rasheedbanert7086
@rasheedbanert7086 Жыл бұрын
Zasatanic basi mboli yako iwe
@amosnyirenda5712
@amosnyirenda5712 2 жыл бұрын
Zot zikuyenda chifukwa cha a Bushiri nde bodza the guy is bad luck kungobwera zinthu kuzsiiratu kuyenda kumalawi kuno. I dont like this guy
@victormsika1538
@victormsika1538 9 ай бұрын
Nchifukwa chake this country can’t go further because of sick and twisted people like you. If you don’t like him very good but don’t shit on whatever good thing he’s doing. And he didn’t ask you to like him or not. Tabakhalabe pa umphawi wakowo mfiti iwe
@FacekidofficialmozMoz
@FacekidofficialmozMoz Жыл бұрын
🇲🇿Hi
@user-vo4yj7vz2r
@user-vo4yj7vz2r 7 ай бұрын
Wabodza iwe
@mustafailanga5010
@mustafailanga5010 2 жыл бұрын
Sanje amalawi
@masiyekalisitusidayton9210
@masiyekalisitusidayton9210 2 жыл бұрын
Apanga bwino nd2
@jonathandube9422
@jonathandube9422 Жыл бұрын
Bushili is a hill
@bryanfuimaono709
@bryanfuimaono709 Жыл бұрын
you need to speak in English
@AminaPhiri-pp9tw
@AminaPhiri-pp9tw 6 ай бұрын
😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂
@patchipanga8445
@patchipanga8445 2 жыл бұрын
Amange Malawi basi
@fridayngungadaud731
@fridayngungadaud731 2 жыл бұрын
Channel ichi sindichikhulupirila anta
@yamikanijames6915
@yamikanijames6915 11 ай бұрын
Amaphatikiza choonadi ndi bodza vuto lake ndilimenelo
@KAIPAAA3211
@KAIPAAA3211 2 жыл бұрын
Wakuba wabela anthu ambiri ku south aafrica, amawanamiza anthu ambiri aike ndalama ku acount yake miez itatu apeza ndalama zambili ku ma count ao, ambiri akulila
@jomonor4915
@jomonor4915 2 жыл бұрын
Dziko likufunika kukhala ndi munthu ngati uyu,uyutu amadzigwilila ntchito pa yekha wosati zomaba misonkho ya anthu.papa yr great wishing yu best mwatimasula amalawife
@saudamwanyali8700
@saudamwanyali8700 2 жыл бұрын
Do you hv a proof for wat u a sayin
@ronaldchirwa253
@ronaldchirwa253 Жыл бұрын
Tazingogwirani ntchito apa... wakuberanipo chan chanu kapena cha makolo anu?
@yamikanijames6915
@yamikanijames6915 11 ай бұрын
Then akuba bwinotu coz he is stealing to help others
Times Exclusive featuring Shepherd Bushiri - 13 January 2024
1:12:31
Times 360 Malawi
Рет қаралды 409 М.
The Giant sleep in the town 👹🛏️🏡
00:24
Construction Site
Рет қаралды 20 МЛН
Bony Just Wants To Take A Shower #animation
00:10
GREEN MAX
Рет қаралды 7 МЛН
SPILLED CHOCKY MILK PRANK ON BROTHER 😂 #shorts
00:12
Savage Vlogs
Рет қаралды 49 МЛН
لااا! هذه البرتقالة مزعجة جدًا #قصير
00:15
One More Arabic
Рет қаралды 52 МЛН
Mbiri ya Moyo Wanga with Napoleon Dzombe
29:26
Fletcher Matandika
Рет қаралды 136 М.
BON KALINDO LERO PA 27 AUGUST 2024 |
17:02
DZIWE TV
Рет қаралды 10 М.
Report La Chilima Labwela - Ntanyiwa Kufotokoza
31:53
Mw Xtra
Рет қаралды 7 М.
Napoleon Dzombe speaks on Standard Bank Africa China Agent Proposition
2:35
Standard Bank Malawi
Рет қаралды 25 М.
EXCLUSIVE INTERVIEW WITH BON KALINDO
59:52
Zodiak Malawi
Рет қаралды 81 М.
Times Exclusive with Prophet David Mbewe - 8 October 2022
50:07
Times 360 Malawi
Рет қаралды 76 М.
Top 10 Richest People in Malawi 2023 - 2024
3:03
Acb King TV
Рет қаралды 83 М.
Msika Wa Ziwalo part 2...
53:20
Malawi Lovers 🇲🇼
Рет қаралды 59 М.
JB asambwaza Tygrin, poulula zinsisi Zina za ku America
43:12
Sam Malvitha
Рет қаралды 25 М.
The Giant sleep in the town 👹🛏️🏡
00:24
Construction Site
Рет қаралды 20 МЛН