Antanyiwatu pena koma eti. Mumabebetsa timakunyadirani koma musamayerekeze za Yesu Kumwa mowa ayi ndithu. We are proud of u koma zinazi ayi mudzibweza moto.
Mmmmmm akunama amenewo mulungu simunthu ndichaka choti osakhulupilira mulungu akhulupirire chifukwa cha chodzizwa chimene mulungu achite dyeralo pangani koma achakwera achoka basi Kaya zikhala bwanji koma mulungu achita izi ingotini phee muone
@YahayaKondwan-mo8hu8 күн бұрын
Mulungu amukhuze mwa padela
@EirdLaher8 күн бұрын
Wapatsidwa chimanga ndindani
@MartinMwanjawanthu-dj3fw8 күн бұрын
Kalaiti
@HADIJAZAMBIA8 күн бұрын
km zovutat
@EsnartMkunda8 күн бұрын
Mr Ntanyiwa or mutanena bwanj km a opposition sangakumvelen aliyense akupanga zake mmmmm Ndipo a MCP akulowad boma anthu adzakhumudwa Tingopempha Ambuye kt akalowa a MCP zinthu zizakhale bwino