Ma demo amenewo akufunika ku Malawi, zimagalimoto zodula zonse zigulitsudwe...
@JacobMsukwa-q6v3 ай бұрын
We're living in the world where the book of smouldering charcoal is still working.Chilima,,, John Phombe magufuri gone some few months/yeas ago NB:there legacies remained unshakable
@DavidPhiri-o6w3 ай бұрын
Su Chakwera ma constitution ndi abakili muluzi....koma we pray munthu wamulungu azabwera malamulo onsewo azawathese
@JafaliAkimu-ll1bf3 ай бұрын
kungoti kuyambira chakwera 'apolice' army ndi nduna zonse ndi zitsiru zokha zokha mbava zigawenga
@ChawasoMlotha-ys6bf3 ай бұрын
Under mcp government, chilungamo ku mzuzu mnthu kumtenga kupita ku lilongwe kuononga mafuta ma orders za ziiii.
@JafaliAkimu-ll1bf3 ай бұрын
boma ili lolamulila zigawenga zokha zokha zitsiru mbava chakwera ndi chitsiru chotheratu chigananga
@MirriamKambale3 ай бұрын
Ngati kuli mbatama za anthu mmalawi ndie a police ndipo ngati kuli anthu ophwanya komanso osaziwa malamulo ndie a police ndipo galu ameneyu mukuti president wamalawwiyu Kaya mukuti chakwera wapepelesa kwambiri a police amenewa
@thulanimpphiri68733 ай бұрын
Zimene mwanena stive banda ndizoona a police akupanga zopupuluma chikwa cha ndale ena.vuto boma ili ambiri zeru alibe chifukwa chopana cheru ndichifukwa amapupulumisa a police. And munthu walakwa ku mzuzu makhoti alikoko police ili koko basi bwerani naye kuno ku lilongwe kuli chani ku lilongwe.
@faroukakwah2913 ай бұрын
Chilungamo plus❤ twapukene amagwetu
@LemosBanda3 ай бұрын
Vuto Malawi Police inatha panopa ndi MCP Police.
@RobertLuka-wy9cl3 ай бұрын
Kuyambila chakwela ndi kabineti yonse apolice army zonse ndi zitsilu za kuba boma la mcp ndi la manyi
Cyber act will not yield anything, freedom of speech is enacted in our mother law( Constitution).
@BenjaminKamanga-p8w3 ай бұрын
Uchigawenga wachuluka kwambiri mmalawi.
@MatthewsJohn-kv8fj3 ай бұрын
Chadwell chinsiru kwambiri
@EliasKawuwa3 ай бұрын
Ngati wa Mpingoyo anapalamula nde asamangidwe,iyeyo ndi munthu, aaaaaaa ,munakangodzudzula zolakwikwazo,osati mpingo ,mpingo nde chiyani, Mesa mpingo ndi anthu,nde munthuyo ngati walakwitsa nde lamulo lisangwire Ntchito
@ThomasiSalijeni3 ай бұрын
Useless police of malawi
@MarvGerald3 ай бұрын
Kumibawa inu nokha ndiamene ndimakufilan mumanena chilungamo boma ili ndilofoira
@KayangeNicholas-vl6nu3 ай бұрын
Ine koma chomwe ndikuona chimalakwika mdziko muno ndichokuti:Civil servant akalakwila munthu/anthu,nkhuluza mulandu,chipepetso chimachoka ku boma.Monga a waterboard kumwetsa anthu madzi onyasa(uku ndikunyalanyaza chabe,just lack of seriousness) Anthu onyalanyazawa pa ntchito bwenzi akuwadula salary nkhupanga compensate ma victims.
@MirriamKambale3 ай бұрын
Chakwera nzeru alibe muzamuona chipumi bilubilu kaluka panga nawo participate pa function ya CCAP after all this ndikuti ndi galu ndithu
@NedsonKanjira-qj2ig3 ай бұрын
Onsewa mubomamo ndi zisiru za anthu panali azanu akamanga anthu , kupha anthu uzifuse kuti ali kuti
@MarcFelson3 ай бұрын
Umakhala uchitsilu wa boma pamodzi ndi umbuli wa apolisi Koma ka pay kang'onong'ono
@WillyMajiya3 ай бұрын
A police athu amalephera kugwira ntchito yawo mwa professional chifukwa cha ma politicians ena ake a nkhope ngati manyi
Nanga training ya ntchito umapanga 6 months and think you can get quality staff
@VictorAmos-my8ne3 ай бұрын
Mayi Aja mukuti wankula wapolice ndiwankhunyu
@MathewKalinkhu3 ай бұрын
Steve ndayamika pa nkhani yomaliza, President ndi nduna azidzipangila okha zonse osati zaulele m'mene zilili pano. Anthu akuvutika ku midzi. Ndicho chifukwa kudzikhala ma Demonstrations osonyeza kukwiya.
@RashdShalos3 ай бұрын
AMwene program ya gwede gwede musamayi phonye pilizi bulasa 🎉wanu
@lonjezompaso95123 ай бұрын
mukhoza kumaiona pa official page ya mibawa nthawi zonse
@DavidPhiri-o6w3 ай бұрын
You two God bless you speaking honest ❤❤❤❤
@marryphili54193 ай бұрын
Apolice akumalawi ndi mbamva chifukwa chake alowesa ndale pa ntchito yawo shame on you
Tikupempha program iiii achisili Achawezi asazalowelere
@MiddayDeleza3 ай бұрын
A police chitani manyazi mukulephera ntchito yanu
@CliffNankumba3 ай бұрын
Ndipo ife ana athu timalipira tokha fizi bwanji
@Pangolinimw3 ай бұрын
Kom iweyo umaganiza bwino bwino kobasi
@WysonBilly3 ай бұрын
Kondwani umayankhula. Bwino
@emmanuelchirwa34203 ай бұрын
Point take big man .komaso aziganiza kuti kunyumba kapena kulokecheni kulibe police officer,tisatenge malamuro pamanja azanja lathu. Ndi ye tiyeni tigwilentchi to kulingana ndimalamo , komaso Pali mwambe wakuti ukakhala pabwino lero usayiwale zamawa,chawonamuzakochapita mawa hilipayiwe..ndangoyimapamenepo, amoyo salekana,
@tamarajoycemalata3 ай бұрын
😊
@awardjafar29283 ай бұрын
JB uja sakumalakwisa akamatukwana msogoleri ndinduna zake