Ukumuyamikira umamuziwa bwino koma? How many kilometers from kasiya to South Africa? Anakupasa zambiri eti?
@jahiemmusa8796 Жыл бұрын
akunama iwowo akutitenga ngati ife ndiwana
@kariyobaker9617 Жыл бұрын
What language is this ? It sounds like some of the languages spoken in Uganda, Rwanda, Burundi and far north western Tanzania. It is a language I can learn easily and quickly.
@maxwellchibwe5956 Жыл бұрын
Chichewa language that's the local language in Malawi
@kariyobaker9617 Жыл бұрын
@@maxwellchibwe5956 Thank you. This proves that African peoples are one or have the same origin.
@yusufsadic2930 Жыл бұрын
Program ngat izi pls tamaperekan mpat ot anthu azimufunsa olankhulayo kups kt munth mmodz azingowanamiz anth wabodz uyu
@dumisanimoyo3152 Жыл бұрын
Iwe usatipusise mr dausi munthuyo anali waku ghana osati malawian
@dondamissonchdziwe3958 Жыл бұрын
Kamuzu Banda sanali wakuno kumalawi,koma anali wabwino woipa amapha wanthu anali osatira ake joni tembo, kazamira,kamwana,ndi amzawo ife tinali kusukulu tikuziziwa,uyunso dausiyu akubisa zina ine mwana wa pasapitwa pa Mulanje ndikuziziwa bwino ngakhale ndiku kalambira kunja
@yasitafuphiri-nw2he Жыл бұрын
Come in Malawi and explain better about Kamuzu Banda
@MrcharsCollen-cy6cr Жыл бұрын
@ dausi you are chamilion
@frezarphiri3480 Жыл бұрын
Kamuzu uyu anapha real kamuzu wakukasungu uyu analamula Malawi uyu kwake ndiku Ghana uyu not Malawi ayi anapha anthu amalawi ambiri azelu zawo ndikalingalira anthu awo ndimawawa mutima kwambiri ndi chipani chake cha mcp
@yasitafuphiri-nw2he Жыл бұрын
Inu mukudziwa zambiri za kamuzu Banda pitani ku Radio mudzatilankhule zoona ndinuyo ,osamawawata pa KZbin pano ai
@chrissygama8678 Жыл бұрын
Kod atanena chilungamo kut sadali waku malawi zingachtike
@chiyenangomba3330 Жыл бұрын
Kamuzu olephera kuyakhura chichewa, he was from Ghana
@MathewsChilota3 ай бұрын
The same as Kenneth Kaunda who was a Malawian ruling in Zambia
@MoosaSame Жыл бұрын
Nichoka Dausi bodza sanali mmalawi
@MitengoFrancis-sp9ox Жыл бұрын
Kodi mwafuna Kuti. Anthu amve Za kamuzu kapena Matamata amayankhulidwe?🎉🎉🎉
@PaulKwenda Жыл бұрын
Peter munthalika chichewa chimamukanika bwanji
@frezarphiri3480 Жыл бұрын
Dausi ayi osathawa fuso kamuzu ndiyo anati tikhale ndi chipani chimozo not aleke banda ayi
@daviekamanga1417 Жыл бұрын
Kaya anali wakugana kaya mumalawi zonse zilibe ntchito za dictator izo olo masiku ano ziliko mukumuona piter akufuna kuimaso ndiwo udictator woooo kusaona adzake kuti angayime
@johnman4619 Жыл бұрын
Zopusa munthu wanji osatha kuyankhula language yadziko lake ..inuyondamene mudaona dziko ATI kamuzu.osati chigawenga
@maggiekamphinda5699 Жыл бұрын
Hahaha anali dictator
@gilamwelekedwa4889 Жыл бұрын
Just google the Kamuzu Malawi history Wikipedia page tells it all .
@gamammwenye Жыл бұрын
who wrote the history if not people with biased minds....
@IsaacSombani Жыл бұрын
Koma akat alowenze maina 😂😂😂😂
@gilamwelekedwa4889 Жыл бұрын
Who was the first prime minister that time? You’re not saying the truth about the history Kamuzu was not the first prime minister after the federation you don’t know our history 😂😂😂 go back to our country’s politics history Mr Dausi
@frasernamaona-qs6ts Жыл бұрын
Mmalawi wosatha chichewa Komatu akuti anachoka kaya ali ndi dzaka 11. Ndan angayiwale chiyankhulo chake? Ghanaian uyu