One day is one day..... Komano mwapindulanji powatsogoza azanuwo.........😢😢😢😢😢😢
@geraldtuwaga-iz6ll15 сағат бұрын
Don't misslead people, that tv is national TV you must work without taking side, why you don't talk about black box
@chickob3859Күн бұрын
Guys hot current iyi mwamangika simukumasuka tidziti apule adakukozelani ka dongosoro kapadela dela? zikuonetsa ngati muli pachingwetu. Mukuti bwanji mr ndevu zamwai ndi anzanu.
@TywellShumba3 күн бұрын
Kodi ngt sanachite kuphedwa munawapeza anthuo ali ndi zovala mwachidule munatolako ma phone 📱 zinthu mkubisa koma mkuti mumalankhula chilungamo chabozacho😢😢
@dennisrobert46173 күн бұрын
Ngozi iyi ikanakhala yachilengedwe bwezi black box atapereka kale
@patriciajangaza6753 күн бұрын
Ngati ine mulungu anandiuza mmaso phenya kuti sinali ngozi
@jowiemhango50585 сағат бұрын
Ndipo ineso chimodzimodzi I dreamnt zimenezija zisanachitike ndipo ndimkalita anthu aja akuphedwa ndi anthu mmmhu
@lawrencedanielmandauka3 күн бұрын
Kupanga renew licence kungapangitse munthu amene Ali ndi experience ya 7 years kulephera kuyendetsa ndege zabodza izi zonse mukunena
@kennymwanyongo81653 күн бұрын
Why going round and round when information can be obtained from the BLACK BOX?
@ConfusedAstronaut-qv6wq3 сағат бұрын
Iwe Ryan uzitenge bwin timakupatsani ulemu kodi vuto chiyani kune kunena kuti ngozi ija ndiyochita kupanga
@ShalmoInvestmentsСағат бұрын
Ndipotu wandinyasa
@BlessingSikefa3 күн бұрын
Mulungu ndiamene akuziwa chilungamo
@BillyP0lly-x6n5 сағат бұрын
Good job azibambo
@ConduanieDicksonie12 сағат бұрын
Kod lincence ikapanga expire, for example ya galimoto, umakhala kuti waiwala kuika ma gear??? Koma2 guyz, kunjaku kuli mulungu
@HolmanDazah2 күн бұрын
Ife akubanja tikuti, we've learnt more kuti they are really maphias our hero has gone .
@AnthoniohMazengera14 сағат бұрын
Ma guys mwalandla ndalama simukusowa your speech all of you,mukufuna amange ndani guys muzalapa day one
@Ertyvhk3 күн бұрын
Why around the bush nkhani ya sikusinja ndi gwenembe iyi musaiwaretu panali kukanganira udindi wina 5 years wina 5 years ndiye ulendo usanafike wina akuti ine ndiimanso zivute zitani ndiye muzizungulira mutu wankhani mukuuziwa?
@JoelTchuma-g3s4 сағат бұрын
Ndili ku Matandani ku mpingo wa Thindi,ndidalika uthnga woti,"Tiuzane zoona."
@mabvutomichaelpanagona19493 күн бұрын
Koma mulungu yekha akudziwa zonse pangapite nthawi bwanji koma adzayankha zonse.
@ConfusedAstronaut-qv6wq3 сағат бұрын
😅😅😅😅😅 akulu akulu simukufunsa black box bwanj 😅😅😅 ,God knows.
They just described the outer description of the plane but they dont explain the technical fort of the plane. Kodi ndegeyo inagulidwa ilibe computer box? Why cant they get the information from the computer box and give us?
@HolmanDazah2 күн бұрын
Anthu maumboni ndiosayamba ndipo ogwirika koma MCP kuyambira kale ndiyakupha, anthutu akuopa kuphedwa. Inu mukidziwa kuti R. Kasambala anachita kuphedwa ndi kamajekete, after atamva zoti SKC ndi kasambala akambirana za withdrawn mu alliance? Did you know that? Ine am one of evident holder, I know every move they have made to kill SKC. Did you know kuti Army commander ndi pilot as well as asilikali analuza miyoyo together and SKC panali selective okhawo omwe amadana nao Verentino ndi amene anali involved pa infayi? Ife, kapena kuti ine sindingamve , ngati black box palibe thus it. Chakwera and his entire MCP government akufuna kuonwtsa ungweeu pa ise na Chiuta He must bring the black box pa open air, ndipo mitima ya a Malawi izausa!!
@dikenzthomo82843 күн бұрын
Vuto lake inuyo pamenepo mumadziva kuti mumakamba chilungamo,mukuti simunyengelera,kudziva kwambiri basi
@JaiLamu-dk8wd6 сағат бұрын
Tell dem
@jowiemhango50585 сағат бұрын
Ngat awawa akudzimva chilungamo why are they not talking about black box???? Useless pple
@andreabanda78382 сағат бұрын
Why are discussing the report when you don’t have it physically?
@charlesmuwanya784517 сағат бұрын
Mr Chunga abalalika zedi pa nkhani ya composition ya Commission of Inquiry ya aircraft crash. Akuti a kubanja sanayenele kukhala mu composition ya commission. Akunama. Akubanja ndi omwe akanaonesetsa kuti panalibe za chinyengo koma the whole truth.
@ConfusedAstronaut-qv6wq3 сағат бұрын
System yachani we all need black box,to stop all these things
@ConfusedAstronaut-qv6wq3 сағат бұрын
Wonder zanu ali mpakatiyi kitenge bwino
@MacxwellStuarts-h9r3 күн бұрын
Achakwera ndi chifukwa chani atauzidwa kuti ndege yasowa anayankha kuti azipasidwa lipoti after hours komanso chifukwa chani anauzidwa kuti ndege inafika ku mzuzu pomwe lipoti lakunja linati ngege sinafike ku mzuzu
@CCHANTHUNYA18 сағат бұрын
It is incredible and disgusting that we have so many of us who have seen an opportunity and are intent on making political capital out of this tragic death. These individuals will never accept the findings of any inquiry.
@charlesmuwanya784517 сағат бұрын
I hope nobody wants to get a political mileage from the tragic aircraft crash. People simply want to know the whole truth & nothing but the truth emineting from the findings of the commission of inquiry. No stone shouldn't have been left unturned like detailed reports on equipment like the transponder & the black box.
@khalidmakwinja256018 сағат бұрын
It's not about thinking but the fact of the matter is that. MCP is a killer
@IbulaMayikolo3 күн бұрын
Ngati mukufuna kuti muupeze umboni wen iweni tuluzani black box
@ShalmoInvestmentsСағат бұрын
Ndani angamasuke kupereka umboni wakufa kwamunthu....kodi uja ankava ndege ikumveka ngati chigayo munamfusa?
@HolmanDazah2 күн бұрын
Aaaaa Chikangawa anali atawerenga kale, kumeneko kunali kuwawiza lilibwino kanene Kwa a Malawi. Komano apapa akungounikira kuti anaphedwadi, tawonano, wait all will be on open air.
@ConfusedAstronaut-qv6wq3 сағат бұрын
Guys kodi hot current ikuti bwanji kodi,sitikuvetsani mukuopa chiyani
@MatchadoKalinda-h5z3 күн бұрын
Ko munthu liacense ukapanga expire ndiye kuti satha kuyendesa koma ndalama ndizoopsa ili ndiye silikunveka bolanso loyamba lija waoo but don't think we're all fools times be sincere with Malawians
@RaphaelWinford-t7u3 күн бұрын
Amanga ndani afiti amenewa😢😢😢😢
@noelmsiska36923 күн бұрын
Flying a plain like kekeke? Kumalawi tili pa mavuto Chilima anali ndi tsoka ndithu
@MartinNice-z9n2 күн бұрын
Chimene mungadziwe ndichakuti ufa ija ndiyokoza why? Vise president angagone ku tchire pamene asilikira alipo ndichifukwa chan amaresa kupita anthu pa nthaw yomwe ndege inangwa?
@JuniorJames-u8o12 сағат бұрын
Inuyo a hot current tangosiyani mukukhalangati mukukamba zanzeru koma palibepo mukunena ndinu mazoba
Adakhala kt chakwera akuyendetsa bwino kapena kt anthu sakumvutika sibwezi akuganizilidwa izi km chifukwa cha nkhaxa zawo anthu tili padzuwa chifukwa chake
@PatrickZinenanie3 күн бұрын
Where is a black box
@KimulaniImani-z4jКүн бұрын
Big up guys
@SamuelBhanda14 сағат бұрын
Awaso ndi amodzi mwaiwo paribe chikuvekapa
@ZimhungaEsther4 сағат бұрын
anachita kukonza inu mwatopa akupatsani ka desemmber
@MMK-p3y18 сағат бұрын
"i wish the dead could speak"
@JannahThomas-iw5xu2 күн бұрын
Anthu Olo ali ndi umboni kma mphawi ngt ine sangabwere poyera muboma lake ili Kod ma pilot ayamba liti awa ? Izi mkukamba za mapilot papers kambani zina , mapepala ndi experience nzosiya , sayemdetsa ndege ndimapepala km munthuyo ndi experience yake
@EvanceWame-v7v2 күн бұрын
Kaniso hot current ndi mbali imodzi ya mcp
@ZimhungaEsther4 сағат бұрын
Phone ikagwa umaziwa ikabedwa imaziiwika sinyengo bodza mwadya timamitazoo. Mawa ndi abale anu
@AlumakioChingaluКүн бұрын
wina asaname osakanena ku commission
@ConduanieDicksonie12 сағат бұрын
Inunso mukudziwa kuti MCP ndi yomwe ija. Chilungamo mukuchidziwa koma mukuopa kusowetsedwa. Shame on u guys
@andreabanda78383 сағат бұрын
Zonama zokhazokha. Apopo.
@WillyNyirenda-l7h3 күн бұрын
Working to please the president. Zizaululika zoona ze nizeniZeptember 2025.
Apa tiime pa chilungamo basi ngat a president sakuziwa kathu pa khani ya ifa coz iye ndi wa kulu wa asilikali police abwerese black box ndizomwe tikufuna kuti tiziwe choonadi cha ngozi kuti zinakhala bwanji ngati sipezeka black box akulu akulu ose amangidwe posatengela kut ali ndi udindo wanji
@AlexanderMbale3 күн бұрын
We are proud of you mr musiska
@HarrisonMatikiКүн бұрын
Lero mwadekhatu mafunso onse mumafunsa aja mwamwera burns
@MarthaMalopa-kw9xw16 сағат бұрын
To be frank, program yokhayi munayamba mwakumana ndi akuluakulu omwe akuthowetsani zikhatho
Angakhale inuyo ma presenter you know the truth chinavuta ndi fighting for u President pa 2025.kodi anthu samvetsa pati? this is why Malawi will remain unsuccessful country.Always run away from reality munthu anachita kuphedwa uyu.
@VelonikaMazengelaКүн бұрын
❤ cool
@RobertGovati-f8o9 сағат бұрын
MDF imadziva kuti they above everything and that they were born to be soldiers not applied for the jobs
@AndrewMachemba-j2u2 күн бұрын
Amalawi chilungamo simungachipeze coz tiyeni tiime papempelo basi itayeni basi
@EvansNaphazi6 сағат бұрын
Mwadya money
@patrickMakhumba-yc7rb3 күн бұрын
Only god knows
@JannahThomas-iw5xu2 күн бұрын
Kom kod manganene Kut anthu osewa mafoni awo amayenda bwnji?? Kod tiziti onsewo nalibe foni
@NoordeenBwanali-iw7me3 күн бұрын
Ndikuonangati zimene zinachitika kuchikangawakuja mwaiwala mufunamuthandizile oipayu kumuelesa ndege inagwa mamawa malo owonekela kuseu koma mumapepha chithandizoku maikoakutali kutiakuthandizeni kusaka ndege chosecho ukamadusamuseu imaoneka pamene yagwela chinavuta ndichani polephela kuuzatunduwa amalawi mofulumila ndikuthandizaso mwasang
@ChidaPhiri2 күн бұрын
Anthu amene aja anachita kuphedwa ndithu. Achakwera ndi gulu lawo anawapha anthu aja kuthetsa nkhani apolisi agwila Chakwera ndi Chimwendo anthu awa akaulura anzawo. Ndithu ndithu ma report onse onama oziteteza. Chonde gwirani Chakwera akaulura zonse
@JoshuaAamonКүн бұрын
Who was translating chichewa into English?
@MikeMsamalaphiri3 күн бұрын
Malume if these guys managed to kill the people who helped them to be in power, what more kadyagaga ongopelekela umboni?? Who can risk up his life to go and testify against these criminals? Only God knows them and He alone will sort them out. The true commission of enquiry will be seen on the judgement day
@ElizabethMulinde3 күн бұрын
Kod ndekut brain banda anasiya pg yimeneyi cox inuyo ndemandinyasa nsaname mabodza kwambili mukatero akupatsan ndalama zamagazi
@PatrickZinenanie3 күн бұрын
Mu black box ndimomwe mumapezeka information osati zamanyi zaozo
@RobertGovati-f8o9 сағат бұрын
what does your conscious say about this when sit around with your family is your integrity ok
@SamuelKhumbiwa3 күн бұрын
Kd Khan ya black box simukunena, kd mulichani m'box simo tatiuzan zoona.anthuwat sitingawakhulupilire chifkwa mbiri zao ndizakumpha basi,kutuluka Kwa enao ndiumbon kt chilungamo palibe,licesece simayendetsa galimoto
@paulmillion16523 күн бұрын
T y nyerenda anthawamo.chani. atiuze poyera ndinu m,busa tiuzeni
@TadalaBirsonkanjanga3 күн бұрын
Anari azibale awo
@sinoiajamu94843 күн бұрын
More questions than answers again it was better not to have this committee of inquiry did we ask if chakwera was aware of SKC been in the county or not ,hw came he as president did know where is deputy was,who are you trying to differed here MCP God is in heaven on day political power will end the truth will be know