Mulungu wathu kumwambapo chitani monga mukufunila pa dziko la Malawi ndipo chisomo ndi zifundo zanu zikhale pa dziko la Malawi chititsani manyazi asatanawa akudziweni kuti ndinu mulungu
@NgongireMwakasungulaКүн бұрын
Chakwera ananena kuti azakhesa mwazi asanalowe muboma pano si izi apha skc sidic mia kunamizila colona virus aphaso mavuto ife tikukuziwani a mcp
@LuciusMowaКүн бұрын
Pafunika kunkuyu kuzamumanga kupita naye ku maula chifukwa iye anapha witika koma nkhaniyi sakuyikoka kuona ngati ochenjeralero mawa aputsa ndithu
@xxxrepairКүн бұрын
Agwireni ndipo mufufuze osaiwala anaphedwa ndi mfuti yanu uja,komanso Ku chikangawa kuja osaiwala omenyedwa pa mbowe
@InacioCement-t7nКүн бұрын
True tikati tisamale tonse atipha
@bornface4786Күн бұрын
Kodi DPP ingaphe chimwanza? Tiyeni tiziganiza bwino a Malawi coz is the first time for to hear about chimwanza in political history of Malawi and for me I just see that people are following MC P bcz of money not good governing
@PabroKadams-q7yКүн бұрын
Ndi afiti wina akumetsere koma ndiiwowo
@MkwandaFaizКүн бұрын
Nonse amene mumasapota mcp machende anu
@NikolasNanaweКүн бұрын
ineso a DPP machede osandulao limozi ndi family yano yose
@TimeAbiluКүн бұрын
Mwana wamkaongo ndi mwana wamkaongo sangabale nkhosa apapa ifeyo Ana a pompano tadziwa kuti Mcp si chipani chabwino, koma agogo akanena koma makani
@MzikaPhiriКүн бұрын
Viva Dpp
@SpencerKadewere-cd5ok9 сағат бұрын
Even Ndege ija ndiomwewa a MCP adawapha ku chikangawa kuja
@Lazarus-qo1slКүн бұрын
MCP ndichipani chankhaza they're always abuse
@Randy-er2xoКүн бұрын
Mwaona akufuna a Mcp awononge dzina la dpp km akunama
@JonesChingaya-yf4ggКүн бұрын
Koma sizitheka kuyipisa mbiri ya DPP coz mau amati okumbira nzake dzenje amagweramo yekha.
@MaxwellKapalamulaКүн бұрын
MCP ,manyi party, chizalira chikachoka 2025
@JamesALLi-m8iКүн бұрын
That is true this government is killer 😳 🤣 😂 government and we don't need this government again Apm is coming soon to be president of this country 🙄 👏
@LerinaKatuli6 сағат бұрын
No secret underground
@ChimzyWesleyКүн бұрын
Mwayamba kumphanakotu ku MCP ko kkkkkk Old politics
Kumkuyu umandinyasa kwambiri, skc and Witika rest well
@MabasoMafaКүн бұрын
Namalomba,ndiwabodza
@MartinmkapangakapangaКүн бұрын
galu
@TauacalabduremaneAbdurem-cq3pfКүн бұрын
MCP mwapha nokha munthu musanamizile DPP mukumbukile ku chikangawa kuja
@DoncliffFrankKambwani-k4kКүн бұрын
kuyambila kale mcp imapha ma mp aku mmwera a mcp.
@BeckhamDavid-v6c9 сағат бұрын
Kunena zona mcp ndiyokupha zinangoona kuvuta kuika boma itivulazo
@Vincent-x6m5nКүн бұрын
Burea lure anaphedwa dpp Anthu 20 kuimbeledwa kumzuzu kuphelatu Dpp Albino kuzingidwa ngat nkhuku Wapolice anavulidwa Dpp Nanga banja linaphedwa Ku area 24 Lilongwe Nanga billy Mayaya kukunthidwa ndima cardet Adpp Dpp yapanga zonyasa kwambili no no Dpp isabweleso mu government bola ras chikomeni