Nkhani si imene awamangirayo ayi mumva kuti takupezani ndi mulandu wa kulankhula mofuna kudzetsa chisokonezo dziko and kumangidwaku kukuchoka pa speech ya pa nsonkhano wa atola nkhani anapanga zipani zingapo uja nkhani ndi commission of enquiry ikuwabaya.kmso manganya za ku convention.
@SylessKamangaСағат бұрын
Chakwera sakufuna chipani Cha utm koma wayiwara kuti chipanda utm sakanakhala president,ukakwera pamusana wa njovu usamati kulibe mame chakwera chikangawa akunama
@BeardKamuwombaHarawa-d6vСағат бұрын
Ngati sanalakwe Ambuye akuyima naye
@alickziba67562 сағат бұрын
Chilima anayamba ndikumamangidwa kenako kuphedwa. Apa kaliati wamangidwa. Pakuyeneka kukhala maso pamenepo.
@Andrew-nz9shСағат бұрын
If I was to choose politicians the first person I'd choose mama kaliyat and where ever you are mama am surely behind you it's my prayer you will be fine and strong in Jesus name 🙏🙏
@Fanie-i7z2 сағат бұрын
Please musavotere usi ndichifukwa anaphesela SKC.
@patrickmwenibanda45652 сағат бұрын
Praying for you mama akweni
@shayrafernandeslatif95563 сағат бұрын
Praying for you madam Kaliyati,ambuye alowelele ameen Akweni President
@RabeccaMkandawire-i9jСағат бұрын
We are praying for mama
@RhodrickChauluka2 сағат бұрын
Zonsezi ndi manganya akufuna kusokoneza kuti kaliyati a kweni kuti asakapezeke ku conversation galu wachabe chabe Michael Usi
Akanakhala kuti wamangidwa ndi mai ako sukanayankhula za manyi zakozo
@yobesaikonde61662 сағат бұрын
Kkkkkkkkkk let's pray, Mai Kaliat ndi munthu. Akhoza kulakwitsa komanso kupekeredwa nkhani , zonsezi mzotheka. Choona akuchodziwa ndi omanga ndi Mai Kaliat. Koma Mulungu ndi wankulu.