KWAGWANJI - KUSANTHULA ZOMWE ZACHITIKA KU UTM 12 July 2024

  Рет қаралды 59,089

HOT 265

HOT 265

27 күн бұрын

Пікірлер: 252
@cassimyusuf6683
@cassimyusuf6683 25 күн бұрын
UTM have made a brilliant decision, simungakhale limodzi ndi anthu ankhaza, okhesa mwazi
@augustMag
@augustMag 25 күн бұрын
Kuganiza mwanzeru UTM palibe chokhalira mu gwirizano pamene mwini wake amene anasayinira kulibe ❤❤❤
@user-ty1vq9lq6w
@user-ty1vq9lq6w 25 күн бұрын
Achita bwino kutulukamo ngati ankaonetsa nkhanza chilima alipompo
@DinesiKafukiza
@DinesiKafukiza 20 күн бұрын
Mbambande zakhalabwinokwambili
@CathrineBizza
@CathrineBizza 25 күн бұрын
Zandikomela izi till pambuyo panu a utm osafooka
@StiveKantiki
@StiveKantiki 25 күн бұрын
Banja linali la amayi amagonesedwa nyumba yo dontha lelo amai amwalila mukagulile anawo nyumba adabwa anawo ndi ulemu ukubwelawo amai awo samaziona achitabwino kutuluka l ❤ utm more 🔥
@user-im7sc2my4w
@user-im7sc2my4w 25 күн бұрын
Tingopempha kuti amene atenge mpando wa chilima akhale munthu wokhwima nzeru ,kuti ma members asabalalike. Mr Usi ,ndi munthu wanzeru ,mumuwone zomwe apange ,musiyeni amalize term yoyambaonga mwa Mr malemu Chilima Mr Usi akhalabe wa UTM ,mudzandikhulupilila
@GeraldMandindi-ll1zq
@GeraldMandindi-ll1zq 25 күн бұрын
Mwina??
@user-fd6oh2vc1c
@user-fd6oh2vc1c 23 күн бұрын
You guys so massive.Wonder u r so wise dear brother….we are proud of you three Big boys.
@mkhulukinyata5198
@mkhulukinyata5198 24 күн бұрын
Well done UTM..You have made the good decision for being separate it yourself from the Killer's .. I'm from Zimbabwe but my fore-fathers are Malawian's.. So they've been telling us about how Harsh MCP was on that past years ago ..Mapanga bino kuchokha ku muwanthu wakuyipa yawa ..
@user-tf7yi9fp2u
@user-tf7yi9fp2u 25 күн бұрын
UTM is intact and is more united after the death and infact many people have joined UTM but don't just see the NEC only. We are set with votes in 2025. Whatever will come out as UTM we will cling to the principles no matter what come may. Viva UTM. If agreement was respected there would have been cordial working relationship. Why out of the full support, campaigning for you and you choose to ill treat him the whole of four years mmmmm not true of being a true Malawian and a Christian. So what is your conscious telling you today? Remember there is always tmrw. Be good to people as you will soon need them. Viva UTM
@JohnTchirati
@JohnTchirati 25 күн бұрын
MCP imapha kuyamba kare historically, komabe Chakwela is not involved but people around him.
@JohnTchirati
@JohnTchirati 25 күн бұрын
Just the remarks oti ndizaimanso? Pa alliance??????
@juliusnjerengo2610
@juliusnjerengo2610 24 күн бұрын
The combination of Brian, Jona and Wonder it is same as Aki, Paw Paw and Sam Loko. Very Entertaining.
@ThaboMoffia-j7p
@ThaboMoffia-j7p 24 күн бұрын
Big up UTM ndipo zamanganyazo ndizosagwiladi mtima zatha zatha osabwelela mbuyo
@JohnChiwaya-ym5me
@JohnChiwaya-ym5me 25 күн бұрын
Ma guys , you have scrutinised the politics well. Ndakunyadilani zeedi
@jacobstvn7995
@jacobstvn7995 25 күн бұрын
Malawi lost a visionary leader because MCP greedy behavior....UTM has moved out, let them enjoy the seats!! As Malawi we have not benefited from this alliance....we have been hurt even more!! So disappointing!!
@AustinChiyembekezo-cx4mz
@AustinChiyembekezo-cx4mz 25 күн бұрын
Very disappointed broz .
@user-zh9kb2sj2i
@user-zh9kb2sj2i 25 күн бұрын
Akanatuluka kalekale chilima sanakamwalila 😢
@ChimwemweBottomani-hc5ju
@ChimwemweBottomani-hc5ju 25 күн бұрын
This is brilliant Utm u made a right decision my advice is...dont let USI to join you hes evil like chakwera...congrats team
@VincentKatimba
@VincentKatimba 25 күн бұрын
That's a good distion wamkulu akakhala kuyipa sachita kumuuza amaonera mphepo tiripambuyo panu utm oyeee am I ❤🎉tikulira chilima ife timamukonda kwambiri 😂😂😂😂
@Christophermalema-o8t
@Christophermalema-o8t 25 күн бұрын
Thanks for your constructive decision UTM.You have made a right channel which will attract some people even to join you & vote for you in 2025 elections.May the almighty God paveway for you.
@user-wi8xw9qh7n
@user-wi8xw9qh7n 25 күн бұрын
Sitikuwaopa sitifooka mcp must goooo
@Lunnah-b1t
@Lunnah-b1t 25 күн бұрын
Mwayakhula bwino zedi ,wakumva wamva,mumatiyimilira guys love from cp,more fire
@FrankKambwani
@FrankKambwani 25 күн бұрын
Mtsikana wamzeru amati akafunsilidwa ndi mamuna panjira asanalore amapita kukawafotokozera abale ndi makolo ake cholinga onse adziyendera limodzi ndi mtsikanayo mumaganizo...Apapa vuto ndidaliwona ine pa Usi atasankhidwa kuti akhale vp sadapite kwamakolo(utm)kukakhala nao pansi adangoti ndatola banja dzotsatila dzake makolo akudzamuzimudziwa mamuna uja kuti ndi chimbalangondo it's too late ana akwatilana kale.Usi adzikhweza ndithu.😅😅
@user-ru5xg9qw4x
@user-ru5xg9qw4x 25 күн бұрын
😂😂😂😂
@user-pv9uk6sc3w
@user-pv9uk6sc3w 25 күн бұрын
Jona pankuku ukunena zoon, Usi si wa UTM, bwanji amakaimila u mp as independent pamene ali mu UTM. Manganya ndi wa MCP basi.
@ahmedwyson4865
@ahmedwyson4865 25 күн бұрын
Apapa nde ma team akumana Ndikamamvera nganizi chaaa ndimachita kumva kukhoma
@AlexKaunda-ny2eg
@AlexKaunda-ny2eg 25 күн бұрын
Achita bwino a UTM kusiyana nadzo dzigawenga dza MCP dzamagazi mmanja 😢😢
@JohnConar-kq4hi
@JohnConar-kq4hi 25 күн бұрын
That's what I was waiting utm be strong 💪
@WilsonMagongwa
@WilsonMagongwa 24 күн бұрын
Ngati pali kugawikana ku utm koma ochokawo apanga chiganizo chabwino ndale za a Michael Usi zitipwetekesa akufuna iwo okha ziziwayendela bwino kusiya 20 million people omwe akuvutika.
@BittonRashid
@BittonRashid 24 күн бұрын
Koma azibambo tikuyamikileni siyamika mukulowa mmanda mumatilankhulila odana nanu ndiodana ndichilungamo.ndakamba izi chifukwa mbalizonse mumagundako osanva asanve zikomo azibambo ❤
@SandforeKadzamira
@SandforeKadzamira 25 күн бұрын
Brian Banda,sitidzampezanso presenter ngati iwe
@MercyMwale-wc4lr
@MercyMwale-wc4lr 25 күн бұрын
Ndipo live....mmmhamatha owez on point
@JohnConar-kq4hi
@JohnConar-kq4hi 25 күн бұрын
Brian ndimachini
@user-ru5xg9qw4x
@user-ru5xg9qw4x 25 күн бұрын
Ndipo zoona
@user-lz4kc5ob1t
@user-lz4kc5ob1t 25 күн бұрын
Ndevu zamwayi munthu wanzeru kwambiri
@stanleymatolabanda5460
@stanleymatolabanda5460 25 күн бұрын
Ndangwirizana nazo zomwe chipani changa cha UTM chachita ndipo MCP iyiwale zotenga boma ndipo Chewa Muziwona kwanu kwatha akupha inu
@MayorMagombo
@MayorMagombo 25 күн бұрын
You are a liar , mcp is there to stay , you are just waste your time. DPP HAS MANIPULATED YOU SICK PEOPLE.
@lillynhlema9656
@lillynhlema9656 25 күн бұрын
Ndipo achita bwino kwabasi
@ChifundoNinje
@ChifundoNinje 25 күн бұрын
Mwaganiza mwa mzelu a utm km mubwerere kumeneko munachokela
@GospelSoldiers-sr7np
@GospelSoldiers-sr7np 25 күн бұрын
Ndipo chilungamo
@YOMALO.
@YOMALO. 25 күн бұрын
😂guys, you're making the show enjoyable
@batsong.chitseko5903
@batsong.chitseko5903 25 күн бұрын
Usi ngwa MCP. kuchoka mu mgwilizano a UTM achita bwino.
@user-oj2fy7vx1z
@user-oj2fy7vx1z 23 күн бұрын
Best analysis
@Aqiec09
@Aqiec09 19 күн бұрын
Can you pliz build your own better Malawi than criticizing others , I mean all those with meaningless coments , because I see no one Will ever be perfect on this
@mphatsosadiki4983
@mphatsosadiki4983 25 күн бұрын
Its not too late for UTM kubwelera Kwa make komwe anachokera.......🎉🎉🎉.I would love ma alliance akamachitika azinena zomwe agwilizana .
@InnocentEdasi
@InnocentEdasi 25 күн бұрын
UTM osafooka🔥🔥🔥. , mzimu wa Chilima wuse mumtendele
@RobertGoliat-gt2qh
@RobertGoliat-gt2qh 25 күн бұрын
Usi ndi wamzeru zakuya and tsiku lina azalankhulanso zamzeru kma UTM yachita bwino kutuluka mumgwirizano
@leonardgondwe1470
@leonardgondwe1470 25 күн бұрын
Zoonadi kuti Mr usi wabalalika chifukwa chakuti masapota a utm sakufuna mgwirizano pomwe a usi ndi a vice a boma😊😊😊
@user-ml2vw1dc9c
@user-ml2vw1dc9c 25 күн бұрын
Lef nthawi coach adachoka 😢😢😢
@LeviChakwira
@LeviChakwira 25 күн бұрын
This is a great move❤❤❤❤
@user-tl9xg4fg9x
@user-tl9xg4fg9x 25 күн бұрын
Zachitabwino mubwelele kumene munachoka kuti tichose chigawengachi
@AndersonChiponola
@AndersonChiponola 25 күн бұрын
Koma to be honest utm Ikuyenera kukhala pasi kusankha munthu wa nzeru otherwise chipani chawo chitha kudzakhala chopanda tsogoro because to be honest wisdom ya Chilima simugafanizira Anthu amene angoyankhulawa chifukwa foundation ya utm akudziwa bwino ndi Chilima koma vuto anafa Anthu asanawauze zithu. UDF ngati inatha tsogoreri alipo kuli bwanji UTM leader anamwalira kwa ine is no future ku UTM
@TonnyDyton
@TonnyDyton 25 күн бұрын
Likamatha banja or palafini wamunyali amapopedwamo
@user-oc8nj3or6y
@user-oc8nj3or6y 25 күн бұрын
We're not afraid anymore ndipo we're going to register with the aim of goin to vote ❤on a serious note,,,we cannot fail to survive that's because of Michel Utsi,,,nono let him do what he can
@BlessigsChabzola
@BlessigsChabzola 25 күн бұрын
Achita bwino kutuluka chakwera angakhale oyamba kupereka kalata ya upulezidenti kuchipani chawo, osakumbukira zosawakhuza zomwe anasayinira ndi malemu.
@SamuelAntone-mz6nq
@SamuelAntone-mz6nq 24 күн бұрын
Zakhala bwino tidakalila ife malilo wanthu panopa
@grantnantchito2919
@grantnantchito2919 25 күн бұрын
To us🎉we had no questions on the Statement made 😢 Don't put us words in our mouths. Decision well made on our behalf
@SlindileAyanda-sz4zw
@SlindileAyanda-sz4zw 24 күн бұрын
That's great idea utm
@user-du9qs4tb6u
@user-du9qs4tb6u 25 күн бұрын
I'm coming to malawi I want to meet you guys well done
@gracemkandawire8769
@gracemkandawire8769 25 күн бұрын
Palibe chokanila ,,iwe wonder,,,chipanichi chikulondoledwa ndi anthu ,,anachita bwino kukana mafuso
@user-co3wr3rn4h
@user-co3wr3rn4h 25 күн бұрын
Ife tilinganga pambuyo pa utm phee
@BlessingMkonda
@BlessingMkonda 23 күн бұрын
Sats true words
@samalanimacdonald9373
@samalanimacdonald9373 24 күн бұрын
Ndenvu zamwayi koma abanda akulakwila chiyan
@VanaKhama
@VanaKhama 25 күн бұрын
Amene anathawqpo a yufi ngati ine sangadabwe
@user-un6qv6sj3h
@user-un6qv6sj3h 25 күн бұрын
Achita bwino ndithu ❤❤❤
@ManninLongwe
@ManninLongwe 25 күн бұрын
Ngati mwatelemu mwathesa mugwilizano amene azayimila usogoleri kumbali yanu ya utm yomwe azakhala pa baluti ndindani?
@NosiphoMazwai
@NosiphoMazwai 25 күн бұрын
Live from capetown
@ziggympandakwaya3054
@ziggympandakwaya3054 25 күн бұрын
Keep the fire burning UTM
@user-nj5vu8cd5l
@user-nj5vu8cd5l 25 күн бұрын
Usi is good guy, he is not far behavior like Chilima. UTM members don't destroy party because of losing Chilima. Once you will start pointing figure someone in a party you will realize tomorrow when party is going to an end
@HarrisMathew-ve5ib
@HarrisMathew-ve5ib 25 күн бұрын
Bravo 👍
@veronicajana5225
@veronicajana5225 25 күн бұрын
🎉🎉🎉🎉🎉UTM bravo!!!!!
@user-cf9yz3ei5o
@user-cf9yz3ei5o 25 күн бұрын
Bravo Kalitta asiyeni
@Cathy-oc7vd
@Cathy-oc7vd 25 күн бұрын
Gwirizano sunathe pano ayi.. unatha 2 years ago, this is just formal panopo
@user-vm7iz6oz6r
@user-vm7iz6oz6r 25 күн бұрын
Zilibwino kwambilili mmm sha,,,wakwiya ndi fit😂😂
@omarmkwanda2184
@omarmkwanda2184 24 күн бұрын
Micheal usi ndi njoka mu udzu, alibe mtsogolo
@user-zh9kb2sj2i
@user-zh9kb2sj2i 25 күн бұрын
Inu musapusisike mcp ndiyomweinanenakuti zagwilizano sakuzidziwa
@BlessingMkonda
@BlessingMkonda 23 күн бұрын
Wakupha Sadyrra naye Segwaa imodzi
@LinlyNakombe
@LinlyNakombe 24 күн бұрын
Good decision
@MadaKanene
@MadaKanene 25 күн бұрын
Komatu band yagawana zida vinyo atantha kale 😮,,, I think is too late 🕐,,,, when justice delays become injustice
@brainsmkumbwa6267
@brainsmkumbwa6267 25 күн бұрын
Iam over the moon for the decision made by U.T.M,zaunetsa kuti Chilima wasiya anthu oganiza moyenelera
@sylviamsonthe
@sylviamsonthe 25 күн бұрын
Good move❤UTM
@gabrielchimangeni4376
@gabrielchimangeni4376 24 күн бұрын
Brain munthu wa bwino komaso opemphera mukayime nawo Ku coveshon bwana ngati presdent wa Utm bwana
@lillynhlema9656
@lillynhlema9656 25 күн бұрын
Koma decision ndaikondq That's part of kumulemekezq chilima after all the torture he went through with mcp
@RemaniBanda-u2n
@RemaniBanda-u2n 25 күн бұрын
achita bwino awonezina
@user-rp9wy6rd1q
@user-rp9wy6rd1q 25 күн бұрын
Achita bwino 🎉
@IssaJohn-cb8vn
@IssaJohn-cb8vn 25 күн бұрын
Amwene awa ali pakatiwa sindimawavesesa zokamba zawo serious
@SheenahMwalabu-iz3pr
@SheenahMwalabu-iz3pr 25 күн бұрын
Ndipo ngati ndinu nokha kkk amamuikilanji kaya. Apapa ikanabeba akanakhalapo a Chunga not Jonayo aaa. Amangodziwa kusokosa ndipo muli fundolesi 😂 mudzitimverako plz a times we love you but uyoyo wavala blueyo apume mu programyi. Ndinakupemphaninso to bring Mr Kapito John, Asowa and muli mutu mmenemuja 😂
@kotking-xg7pp
@kotking-xg7pp 25 күн бұрын
sanabwele bwino ndithu kkkkkkkk
@HappyKanyangala-oq1kk
@HappyKanyangala-oq1kk 25 күн бұрын
Amabodxa inu
@ProgloKazembe2-eu7hn
@ProgloKazembe2-eu7hn 25 күн бұрын
Zamphamvu Guys
@GreyMtungama
@GreyMtungama 25 күн бұрын
Umakwana wonder kikikik ma usher omweo
@PatrickMailos
@PatrickMailos 24 күн бұрын
Mungoti pheeeee muone
@user-le9su3mt7r
@user-le9su3mt7r 25 күн бұрын
Brian yomwe ni busa kkkkk
@LawrentNyasulu
@LawrentNyasulu 25 күн бұрын
Koma apamkuku banja latsopabo anthu amagona 4pm akuti usiku umafupika
@INNOCENTMOFOLO-io8tg
@INNOCENTMOFOLO-io8tg 25 күн бұрын
😂😂😂😂 banda banda akuopa kkkkk
@fumumdolo7341
@fumumdolo7341 25 күн бұрын
UTM has made the right political decision. Deputy President was supposed to lead to put the house in order. The guy lacks stamina to judge Malawians mind. USI can't afford to unite UTM it's lost opportunity, he could have demonstrated in presence of his boss. Very tricky situation to USI and MCP.
@ChimwemweBottomani-hc5ju
@ChimwemweBottomani-hc5ju 25 күн бұрын
Exactly
@user-du9qs4tb6u
@user-du9qs4tb6u 25 күн бұрын
A mcp ndi akupha Chakwela ndiwe munthu oipa machende ako
@PatrickMulangala-os4by
@PatrickMulangala-os4by 25 күн бұрын
Ndevu za mwayi wadya mbali yake
@user-xx4jb9se3z
@user-xx4jb9se3z 25 күн бұрын
Utm my vote
@madalitsochiumia755
@madalitsochiumia755 25 күн бұрын
That's great decision UTM
@SnogerSinclair
@SnogerSinclair 25 күн бұрын
Mwachidwule sakuyenera kukhala vp
@soulkanyinji982
@soulkanyinji982 25 күн бұрын
Congrats UTM
@jameskamanga628
@jameskamanga628 25 күн бұрын
Zovuta kwambiri
@georgengwira3152
@georgengwira3152 25 күн бұрын
Bravo UTM chipani chakupha ichi
@FrancisDominic-w1s
@FrancisDominic-w1s 25 күн бұрын
Ausi ngati sasamara azafera kusata
@user-px5tz4kb5s
@user-px5tz4kb5s 25 күн бұрын
Chawezi Banda ndidzanena Kuti chapita
@lukepeter8290
@lukepeter8290 23 күн бұрын
A banda mwati anatani 😅
@GodfreyWhayo-hh1dm
@GodfreyWhayo-hh1dm 24 күн бұрын
A MCP adakwera pachulu ndikulengeza kuti wina afune Kaya asafune iwowo adzapambana chisankho ndi 70% . Kodi kapena anaconda kale mwala ?
@dondamissonchdziwe3958
@dondamissonchdziwe3958 25 күн бұрын
Achoka mochedwa atawaphera Kale Chilima,kuimba chiminingo Njobvu zaononga zapita Kale
@lillynhlema9656
@lillynhlema9656 25 күн бұрын
Tasangalala ndithu.....
@lawrencekauwa8005
@lawrencekauwa8005 25 күн бұрын
Bliriant decision finally made
@user-uv5rf4zt5q
@user-uv5rf4zt5q 25 күн бұрын
It's a right decision if they moved out early chilima could be alive today.
@chrissyyendayenda4650
@chrissyyendayenda4650 25 күн бұрын
Good descions
FULL INTERVIEW: Donald Trump takes questions from NABJ panel
35:47
ABC News
Рет қаралды 1,2 МЛН
A little girl was shy at her first ballet lesson #shorts
00:35
Fabiosa Animated
Рет қаралды 17 МЛН
Smart Sigma Kid #funny #sigma #comedy
00:40
CRAZY GREAPA
Рет қаралды 33 МЛН
Mama vs Son vs Daddy 😭🤣
00:13
DADDYSON SHOW
Рет қаралды 51 МЛН
Doing This Instead Of Studying.. 😳
00:12
Jojo Sim
Рет қаралды 23 МЛН
GWEDE-GWEDE LERO PA 6 AUGUST 2024
21:08
HOT 265
Рет қаралды 11 М.
Let's Punish these XXX Website Scammers
19:54
Scammer Payback
Рет қаралды 20 МЛН
The Inside Story | USA Votes 2024
25:01
Voice of America
Рет қаралды 759
KU MCP KUSAMBWAZANA ZAMASEWERA AYI 🔥🔥🔥🔥
24:59
HOT 265
Рет қаралды 10 М.
12News Arizona Primary Coverage
1:44:21
12 News
Рет қаралды 1,5 М.
Americans Freed from Russia | Faith Nation - August 1, 2024
22:24
A little girl was shy at her first ballet lesson #shorts
00:35
Fabiosa Animated
Рет қаралды 17 МЛН