M'manjamo mwa mayi Jen kuti phwa phwa phwa ulemu wanu amayi .
@sakwatathom21 күн бұрын
The woman who genuinely loves this country. Mum please forgive us for what we did . We were really crazy tinalozedwa
@AhmadumkomaTambala-lr9gp18 күн бұрын
Kod munthu akakhala paudindo sakuyenela kukhala mfulu wachipan
@SaidiMbawa-st6bj24 күн бұрын
Zisakho sizinayende bwino kuvomereza ndikwabwino
@user-yk1hw8kd5l23 күн бұрын
Kapenatu name umagwira ku MEC
@FrancisTembenu23 күн бұрын
The great Mama
@JayMilazi-fv6px23 күн бұрын
Mayi ankalifunira dziko zabwino uyu koma ife kusamva pano ndi izi ndikuona nyekhwe amalira ndipo tilira zeni zeni 😂😂😂😂😂😂sinditha
@shakajudahTV23 күн бұрын
The only best woman Malawi ever hard
@user-wm7vl4wp8v23 күн бұрын
We did not know that we were making a big mistake by demonstrating over you.... But forgive us... forgive the entire Nation... We love u mum
@MadalitsoGama23 күн бұрын
Salute
@princemlongoti469321 күн бұрын
Don't say we as if takutuma
@mwayimlambia538718 күн бұрын
we you n who?,
@duncanchiyani387921 күн бұрын
Koma Dziko la Malawi!
@aliedausi973317 күн бұрын
Jane Ansah ngwabodza ndalama za deal saperekera pagulu
@NephtaliKumsenjere20 күн бұрын
Mai oipitstsa uyu .
@itumbagarments69898 күн бұрын
Inuo olungama
@ElinaMkandawire-hy1ct24 күн бұрын
Ananena za mwazi anali lazalo
@aliedausi973317 күн бұрын
Mai wautsiru uyu
@ThandiBinali21 күн бұрын
Mulungu Akutsongoleni mama munagwira nchito ya bwino
@Patricia_Chisankha20 күн бұрын
🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥
@successm-vt3dx23 күн бұрын
kkk nde ati ndi chisakho choyamba kuyenda bwino kkk
@isaacpelani21 күн бұрын
Definitely yes. It was the best ever. Kungotitu zonse zinachitika post 2019 polls zija inali kale plan. If you don't know mtambo was intercepted talking to a certain politician kuti APM akadzangoti wawina kudzakhala ziwawa zoti boma lidzakhale ungovernable mpaka boma lidzalandidwe and it was exactly what happened. Chitsankho chimene chija a UN auditors anali ntcheru kuonetsetsa kuti pasaberedwe. Majaji ajatu ankayenda chewu chewu mpaka ankayenda pa heavy military escort wokaweruza milandu. Zinyaeu nazo zinavuta mu LLs.
@successm-vt3dx21 күн бұрын
@@isaacpelani andare amwene iiiii
@isaacpelani20 күн бұрын
@@successm-vt3dxndimamafia and anthu azithokoza kuti APM ndi munthu ofatsa and sanafune kutsatira nkhuli yautsogoleri inadzala mmitima mwa anthu analuza 2019 aja.
@isaacpelani20 күн бұрын
@@successm-vt3dxndimamafia and anthu azithokoza kuti APM ndi munthu ofatsa and sanafune kutsatira nkhuli yautsogoleri inadzala mmitima mwa anthu analuza 2019 aja.
@rodgersdamison231321 күн бұрын
Koma nde aondatu
@456855316 күн бұрын
I have bad memories about this woman
@MarthaSimon-nv1if24 күн бұрын
You are a strong woman Jane
@GoodmanNzunda19 күн бұрын
We love you mum
@MphatsoAmos14 күн бұрын
Satana anatinyenga , you were genuine mum
@NedsonBilly22 күн бұрын
Inde mdzko muno zinthu sizikuyenda bwino koma pachilungamo maiwa adalakwitsa ndthu,, ndpo yankho ndilakut adathawa mademo 😂😂😂
@user-cc4fm2mn4t23 күн бұрын
Mayi madando mkukamba zabodza izi inu munathawa basi
@DonnieMaulidi-fd4td24 күн бұрын
The great woman Malawi ever had🎉🎉
@EmercianahKasiku-en6hl21 күн бұрын
Mai ndinu munthu oipa komaso wabodza nokha mukuti simunathawe koma munathawa momwe mwalakhulira apamu and simumkafuna kutsazika Kwa mabwana Anu...mukutiso mumanena kuti asagule tipex nde tipex anapezekapo pamenepo ngati judge simukuona kuti sizinayende bwino poti inuyo ngati munauza Anthu Anu kuti asagwiritse ntchito tipex monga zisakho zinazonse zimakhalira mbuyomu nde mumafuna kuti Anthu asadabwe mesa Inu njira imeneyo munaikana chifukwa ndi yomwe amabelera chisankho a DPP Mai wachabe osakonda dziko lino munapita ku UK kukakhomelera kuti IMF isapeleke zithandizo cholinga Tonse alliance government ioneke yolephera
@Jstanleybeatz20 күн бұрын
Tonse alliance ndiyolephera even chakwera ndi olephera....blame game za ziii.....chakwera muja amayendera kunja muja kukakambila NDA Zungu zimapindula zachi.... MCP inapita ndi mwina wake kamuzu
Back to Sender ungayambe kumwalira Ndi Iweyo Kapena Azibale Ako Galu iwe😠😠😠😠
@abdullahibrahimbacqri362823 күн бұрын
Satan mesa ndi chakwera wakoy
@user-mj3ms4jt3b23 күн бұрын
Cod knows kuti Mai ameneyu ndi Mai oyipa nkhope ndi mtima omwe. Chilungamo tiyeni tizinena, anali ndi mtima oti anthu pafupifupi 20 million iyeyo akane zigawo zawo ndikuti atipangile chiganizo chopambanitsa DPP pamene anthu tinavotera ena. Zagalu wako usamapatse ine wamva? Iwe ukuchita kumva yekha akuti akuma polling center anawawuza kuti azingonkwatcha nzere, chinavuta ndichani kuwauzaso aku tally center kuwauzaso choncho poti onse amayendetsa chisankho chimodzi chomwecho? Ndi ugalu wakowo sungaone kuti panali chinyengo?
@user-wd9yd1bg9n23 күн бұрын
Iwe ndiye mbuzu yamunthu , nyau yachabechabe
@rodgersdamison231319 күн бұрын
Mai oipa inu
@asivenathilitye726818 күн бұрын
🎉😊
@pushingpunisher601917 күн бұрын
Pansana pako iwe
@BoniwelZimba-ki1dr15 күн бұрын
Aaaaa she's was corrupt by using tipex as jugde
@emmanuelnavaya570319 күн бұрын
BIG STORIES
@user-gt8nn5ic1v23 күн бұрын
Kkkkkkkk anthu amajama za Mai uyu.Koma iyeyo ankafuna kuti sugar asafike pa K4,500
@JoyceGondwe-ve1zu22 күн бұрын
Chiliichose chili ndinthawi. Kulibe wa muyaya. It's time for those ruling to rule. Nothing is wrong.. Ife mu nthawi ya Kamuzu sugar timagula K50. Accept change.
@JoyceGondwe-ve1zu22 күн бұрын
Nthawi ya Kamuzu sugar timagula K50. What are you talking about. Accept change. 4500 yomweyo
@DeveriuosChitsime18 күн бұрын
Galu uyu wabodza
@liki-likiladies---lilongwe696324 күн бұрын
😂😂😂😂😂😂ma comment
@Midy26523 күн бұрын
Forgive Malawi Mai Malawi...
@samusankhulani542321 күн бұрын
Mbava izi
@dysonmsamba577823 күн бұрын
CHOMWE NDINGANENE MAI SIBWINO KUKAKAMILA PA MPNDO INE NDILI KUNONSO KU MANGALANDE TIKHOZA KUTENGAKO CHITSAZO KUCHOKELA KUNOKO
@FestonKapachika21 күн бұрын
Sorry my lady, you were right during your era
@user-eo2ol3ww8h24 күн бұрын
chakuba icho
@YNOTGEORGE824 күн бұрын
Mastn sopano mukuwalatu
@user-lg2ws2ki3d24 күн бұрын
Satana akomako ndithu
@bayanimponda874624 күн бұрын
Nkhani ndiyoti mumava bwanji kuti chisakho chomwe mumayendesa aku court nachikana? Ndipo ati chinalakwika chibwerere
Ndiye mwati amai awawa anali a judge ndithu mmhhh? Akuti tipex anatani? Mai uyu eeeee
@EvanceEdson-fz1vn20 күн бұрын
Atani kusakhala judge?
@Cittyboy36322 күн бұрын
I told them
@PrinceThom-pe6ie24 күн бұрын
Amalawi kunzunzana wokha wokha.a immigration masende anu nonse
@AmosiSingano24 күн бұрын
Kkkkk
@user-nq9bg8zo4v21 күн бұрын
I don't trust this one
@nellanzimba818124 күн бұрын
Kodi akutichan
@starneckkulemero754811 күн бұрын
Amateur journalist
@simonkalambo165521 күн бұрын
The journalist lacks skill of questioning.sensitive questions:1.did you share tippex? 2.your successor used same resources and workforce but there was no tippex used,why? 3.why you didn't report to police for kukhetsa mwazi intimidation? If you go to bank to collect money,all the details and figures are correct but there is tippex, will they allow you to get money,why? There was no cheating at all at examination centre and police were there but a student used a red pen instead of a black pen.will Maneb mark that paper?4.As a referee,why did you attend swearing ceremony while your successor never attended the swearing in ceremony? 5.Do you that mp elections only affect one area.for example tippex used on mp vote in Luchenza will only affect that outcomes of Luchenza but not of Karonga Nyungwe or Migowi but tippex used on president vote in Mzimba for example can affect the outcomes of the whole country?
@mdakakachokammanja751020 күн бұрын
So tippex used on MPs and councillors was ok cos only affected mma constituencies? Maganizidwe a chinyengotu awa 🤣 Thought the MPs were elected in the same manner as the president ? You don’t pick and choose when you talk about justice, that is a corrupt mindset, kufuna zofuna zako zokha zichitike