MAI JANE ANSAH (TIPPEX) part1....

  Рет қаралды 33,316

LIKI-LIKI TELEVISION

LIKI-LIKI TELEVISION

26 күн бұрын

Пікірлер: 101
@PrinceThom-pe6ie
@PrinceThom-pe6ie 24 күн бұрын
Mcp machende mwanu nonse ndi galu chakwera
@user-vl5on2lj8b
@user-vl5on2lj8b 23 күн бұрын
Mulungu tilore akhale mulungu ndi amene akudziwa chilichonse amen
@SemuJali
@SemuJali 9 сағат бұрын
Amay ochenjera kwambili inu mabodza kumwamba kuri mulungu
@user-vh9uk1jy7w
@user-vh9uk1jy7w 22 күн бұрын
May Allah bless you we always love mom
@BizoSaka
@BizoSaka 19 күн бұрын
Ubwino wake wadziulula wekha zoti ndiwe wa DPP si mesa ukukaimila DPP pa u Mp
@MtisungeMandwe
@MtisungeMandwe 6 күн бұрын
Amai inuyo ndi mmai obheba kwambili ,pano tikuvutika zoziyamba tokha a malawi ,mum konda you
@CopNyasulu
@CopNyasulu 22 күн бұрын
Thanks mibawa for hosting mama Jane Ansah, well explained mama....
@EsnartGirivin
@EsnartGirivin 20 күн бұрын
Chilungamo akuchidziwa iwo ndi Mulungu wawo
@steriaphiri3478
@steriaphiri3478 23 күн бұрын
A Jane nenane zoona Yesu akubwera posachedwe munathawa. boza ndi ntchimo mukudziwatso zimenezo
@WhiteThamanga
@WhiteThamanga 23 күн бұрын
Ngati anathawa mulandu pano akulamulira ndindani?
@emmanuelmaluwa925
@emmanuelmaluwa925 11 күн бұрын
Ine ndlibe nanu mlandu nsaname
@georgesmart3791
@georgesmart3791 24 күн бұрын
Mmai Okonda dziko lake
@FaithKanzingeni
@FaithKanzingeni 18 күн бұрын
Big up my Lady
@Patrickgomani
@Patrickgomani 24 күн бұрын
May God continue to bless Jane Ansah ....
@user-gk6bf7xe9g
@user-gk6bf7xe9g 24 күн бұрын
ndikuyankhilen fuso may kunali km kuthawa😂😂😂😂😂😂
@user-lg2ws2ki3d
@user-lg2ws2ki3d 24 күн бұрын
Satana akomako ndithu
@LysonPagone
@LysonPagone 24 күн бұрын
My mama God be with u forever
@joemlelemba6572
@joemlelemba6572 23 күн бұрын
Mum you really loved malawi
@HassanElias-wy2du
@HassanElias-wy2du 16 күн бұрын
Mama you did your part
@RichardMatandala
@RichardMatandala 21 күн бұрын
Mai mbambande,mulungu nthaw yina amagwiritsa ntchito satana kut Zina zikhale bwino
@user-vl5on2lj8b
@user-vl5on2lj8b 23 күн бұрын
M'manjamo mwa mayi Jen kuti phwa phwa phwa ulemu wanu amayi .
@sakwatathom
@sakwatathom 21 күн бұрын
The woman who genuinely loves this country. Mum please forgive us for what we did . We were really crazy tinalozedwa
@AhmadumkomaTambala-lr9gp
@AhmadumkomaTambala-lr9gp 18 күн бұрын
Kod munthu akakhala paudindo sakuyenela kukhala mfulu wachipan
@SaidiMbawa-st6bj
@SaidiMbawa-st6bj 24 күн бұрын
Zisakho sizinayende bwino kuvomereza ndikwabwino
@user-yk1hw8kd5l
@user-yk1hw8kd5l 23 күн бұрын
Kapenatu name umagwira ku MEC
@FrancisTembenu
@FrancisTembenu 23 күн бұрын
The great Mama
@JayMilazi-fv6px
@JayMilazi-fv6px 23 күн бұрын
Mayi ankalifunira dziko zabwino uyu koma ife kusamva pano ndi izi ndikuona nyekhwe amalira ndipo tilira zeni zeni 😂😂😂😂😂😂sinditha
@shakajudahTV
@shakajudahTV 23 күн бұрын
The only best woman Malawi ever hard
@user-wm7vl4wp8v
@user-wm7vl4wp8v 23 күн бұрын
We did not know that we were making a big mistake by demonstrating over you.... But forgive us... forgive the entire Nation... We love u mum
@MadalitsoGama
@MadalitsoGama 23 күн бұрын
Salute
@princemlongoti4693
@princemlongoti4693 21 күн бұрын
Don't say we as if takutuma
@mwayimlambia5387
@mwayimlambia5387 18 күн бұрын
we you n who?,
@duncanchiyani3879
@duncanchiyani3879 21 күн бұрын
Koma Dziko la Malawi!
@aliedausi9733
@aliedausi9733 17 күн бұрын
Jane Ansah ngwabodza ndalama za deal saperekera pagulu
@NephtaliKumsenjere
@NephtaliKumsenjere 20 күн бұрын
Mai oipitstsa uyu .
@itumbagarments6989
@itumbagarments6989 8 күн бұрын
Inuo olungama
@ElinaMkandawire-hy1ct
@ElinaMkandawire-hy1ct 24 күн бұрын
Ananena za mwazi anali lazalo
@aliedausi9733
@aliedausi9733 17 күн бұрын
Mai wautsiru uyu
@ThandiBinali
@ThandiBinali 21 күн бұрын
Mulungu Akutsongoleni mama munagwira nchito ya bwino
@Patricia_Chisankha
@Patricia_Chisankha 20 күн бұрын
🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥
@successm-vt3dx
@successm-vt3dx 23 күн бұрын
kkk nde ati ndi chisakho choyamba kuyenda bwino kkk
@isaacpelani
@isaacpelani 21 күн бұрын
Definitely yes. It was the best ever. Kungotitu zonse zinachitika post 2019 polls zija inali kale plan. If you don't know mtambo was intercepted talking to a certain politician kuti APM akadzangoti wawina kudzakhala ziwawa zoti boma lidzakhale ungovernable mpaka boma lidzalandidwe and it was exactly what happened. Chitsankho chimene chija a UN auditors anali ntcheru kuonetsetsa kuti pasaberedwe. Majaji ajatu ankayenda chewu chewu mpaka ankayenda pa heavy military escort wokaweruza milandu. Zinyaeu nazo zinavuta mu LLs.
@successm-vt3dx
@successm-vt3dx 21 күн бұрын
@@isaacpelani andare amwene iiiii
@isaacpelani
@isaacpelani 20 күн бұрын
​@@successm-vt3dxndimamafia and anthu azithokoza kuti APM ndi munthu ofatsa and sanafune kutsatira nkhuli yautsogoleri inadzala mmitima mwa anthu analuza 2019 aja.
@isaacpelani
@isaacpelani 20 күн бұрын
​@@successm-vt3dxndimamafia and anthu azithokoza kuti APM ndi munthu ofatsa and sanafune kutsatira nkhuli yautsogoleri inadzala mmitima mwa anthu analuza 2019 aja.
@rodgersdamison2313
@rodgersdamison2313 21 күн бұрын
Koma nde aondatu
@4568553
@4568553 16 күн бұрын
I have bad memories about this woman
@MarthaSimon-nv1if
@MarthaSimon-nv1if 24 күн бұрын
You are a strong woman Jane
@GoodmanNzunda
@GoodmanNzunda 19 күн бұрын
We love you mum
@MphatsoAmos
@MphatsoAmos 14 күн бұрын
Satana anatinyenga , you were genuine mum
@NedsonBilly
@NedsonBilly 22 күн бұрын
Inde mdzko muno zinthu sizikuyenda bwino koma pachilungamo maiwa adalakwitsa ndthu,, ndpo yankho ndilakut adathawa mademo 😂😂😂
@user-cc4fm2mn4t
@user-cc4fm2mn4t 23 күн бұрын
Mayi madando mkukamba zabodza izi inu munathawa basi
@DonnieMaulidi-fd4td
@DonnieMaulidi-fd4td 24 күн бұрын
The great woman Malawi ever had🎉🎉
@EmercianahKasiku-en6hl
@EmercianahKasiku-en6hl 21 күн бұрын
Mai ndinu munthu oipa komaso wabodza nokha mukuti simunathawe koma munathawa momwe mwalakhulira apamu and simumkafuna kutsazika Kwa mabwana Anu...mukutiso mumanena kuti asagule tipex nde tipex anapezekapo pamenepo ngati judge simukuona kuti sizinayende bwino poti inuyo ngati munauza Anthu Anu kuti asagwiritse ntchito tipex monga zisakho zinazonse zimakhalira mbuyomu nde mumafuna kuti Anthu asadabwe mesa Inu njira imeneyo munaikana chifukwa ndi yomwe amabelera chisankho a DPP Mai wachabe osakonda dziko lino munapita ku UK kukakhomelera kuti IMF isapeleke zithandizo cholinga Tonse alliance government ioneke yolephera
@Jstanleybeatz
@Jstanleybeatz 20 күн бұрын
Tonse alliance ndiyolephera even chakwera ndi olephera....blame game za ziii.....chakwera muja amayendera kunja muja kukakambila NDA Zungu zimapindula zachi.... MCP inapita ndi mwina wake kamuzu
@beinhardkausiwa7107
@beinhardkausiwa7107 24 күн бұрын
Mai ambuye azikudalitsani kwambiri
@madalitsomakawa9708
@madalitsomakawa9708 24 күн бұрын
Tippex pa headline wabwera bwanji
@user-qc5hj1gy4s
@user-qc5hj1gy4s 19 күн бұрын
Mrs T ipex my good mum
@thiagosbotha2015
@thiagosbotha2015 24 күн бұрын
sattha kufusa mafus.
@user-mj3ms4jt3b
@user-mj3ms4jt3b 24 күн бұрын
Satana wamkulu galu ameneyu alibe chilunga ndipo asanyase Malawi sitimufunaso. Ndipo ndizodandaulitsa kuti imfa ikutenga anthu ofunikira kumasiya satana ngati ameneyu zodandaulitsa kwambiri
@PatrickPhiri-km3yt
@PatrickPhiri-km3yt 23 күн бұрын
Kuyankhura kopusa uku
@wizzyboychindamba8332
@wizzyboychindamba8332 23 күн бұрын
Back to Sender ungayambe kumwalira Ndi Iweyo Kapena Azibale Ako Galu iwe😠😠😠😠
@abdullahibrahimbacqri3628
@abdullahibrahimbacqri3628 23 күн бұрын
Satan mesa ndi chakwera wakoy
@user-mj3ms4jt3b
@user-mj3ms4jt3b 23 күн бұрын
Cod knows kuti Mai ameneyu ndi Mai oyipa nkhope ndi mtima omwe. Chilungamo tiyeni tizinena, anali ndi mtima oti anthu pafupifupi 20 million iyeyo akane zigawo zawo ndikuti atipangile chiganizo chopambanitsa DPP pamene anthu tinavotera ena. Zagalu wako usamapatse ine wamva? Iwe ukuchita kumva yekha akuti akuma polling center anawawuza kuti azingonkwatcha nzere, chinavuta ndichani kuwauzaso aku tally center kuwauzaso choncho poti onse amayendetsa chisankho chimodzi chomwecho? Ndi ugalu wakowo sungaone kuti panali chinyengo?
@user-wd9yd1bg9n
@user-wd9yd1bg9n 23 күн бұрын
Iwe ndiye mbuzu yamunthu , nyau yachabechabe
@rodgersdamison2313
@rodgersdamison2313 19 күн бұрын
Mai oipa inu
@asivenathilitye7268
@asivenathilitye7268 18 күн бұрын
🎉😊
@pushingpunisher6019
@pushingpunisher6019 17 күн бұрын
Pansana pako iwe
@BoniwelZimba-ki1dr
@BoniwelZimba-ki1dr 15 күн бұрын
Aaaaa she's was corrupt by using tipex as jugde
@emmanuelnavaya5703
@emmanuelnavaya5703 19 күн бұрын
BIG STORIES
@user-gt8nn5ic1v
@user-gt8nn5ic1v 23 күн бұрын
Kkkkkkkk anthu amajama za Mai uyu.Koma iyeyo ankafuna kuti sugar asafike pa K4,500
@JoyceGondwe-ve1zu
@JoyceGondwe-ve1zu 22 күн бұрын
Chiliichose chili ndinthawi. Kulibe wa muyaya. It's time for those ruling to rule. Nothing is wrong.. Ife mu nthawi ya Kamuzu sugar timagula K50. Accept change.
@JoyceGondwe-ve1zu
@JoyceGondwe-ve1zu 22 күн бұрын
Nthawi ya Kamuzu sugar timagula K50. What are you talking about. Accept change. 4500 yomweyo
@DeveriuosChitsime
@DeveriuosChitsime 18 күн бұрын
Galu uyu wabodza
@liki-likiladies---lilongwe6963
@liki-likiladies---lilongwe6963 24 күн бұрын
😂😂😂😂😂😂ma comment
@Midy265
@Midy265 23 күн бұрын
Forgive Malawi Mai Malawi...
@samusankhulani5423
@samusankhulani5423 21 күн бұрын
Mbava izi
@dysonmsamba5778
@dysonmsamba5778 23 күн бұрын
CHOMWE NDINGANENE MAI SIBWINO KUKAKAMILA PA MPNDO INE NDILI KUNONSO KU MANGALANDE TIKHOZA KUTENGAKO CHITSAZO KUCHOKELA KUNOKO
@FestonKapachika
@FestonKapachika 21 күн бұрын
Sorry my lady, you were right during your era
@user-eo2ol3ww8h
@user-eo2ol3ww8h 24 күн бұрын
chakuba icho
@YNOTGEORGE8
@YNOTGEORGE8 24 күн бұрын
Mastn sopano mukuwalatu
@user-lg2ws2ki3d
@user-lg2ws2ki3d 24 күн бұрын
Satana akomako ndithu
@bayanimponda8746
@bayanimponda8746 24 күн бұрын
Nkhani ndiyoti mumava bwanji kuti chisakho chomwe mumayendesa aku court nachikana? Ndipo ati chinalakwika chibwerere
@tamariahisrael6563
@tamariahisrael6563 24 күн бұрын
Amamva bwino chifukwa pano dziko likuyenda bwino ndipo aMalawi akusangalala😂😂😂😂
@josephphiri7161
@josephphiri7161 22 күн бұрын
Ndiye mwati amai awawa anali a judge ndithu mmhhh? Akuti tipex anatani? Mai uyu eeeee
@EvanceEdson-fz1vn
@EvanceEdson-fz1vn 20 күн бұрын
Atani kusakhala judge?
@Cittyboy363
@Cittyboy363 22 күн бұрын
I told them
@PrinceThom-pe6ie
@PrinceThom-pe6ie 24 күн бұрын
Amalawi kunzunzana wokha wokha.a immigration masende anu nonse
@AmosiSingano
@AmosiSingano 24 күн бұрын
Kkkkk
@user-nq9bg8zo4v
@user-nq9bg8zo4v 21 күн бұрын
I don't trust this one
@nellanzimba8181
@nellanzimba8181 24 күн бұрын
Kodi akutichan
@starneckkulemero7548
@starneckkulemero7548 11 күн бұрын
Amateur journalist
@simonkalambo1655
@simonkalambo1655 21 күн бұрын
The journalist lacks skill of questioning.sensitive questions:1.did you share tippex? 2.your successor used same resources and workforce but there was no tippex used,why? 3.why you didn't report to police for kukhetsa mwazi intimidation? If you go to bank to collect money,all the details and figures are correct but there is tippex, will they allow you to get money,why? There was no cheating at all at examination centre and police were there but a student used a red pen instead of a black pen.will Maneb mark that paper?4.As a referee,why did you attend swearing ceremony while your successor never attended the swearing in ceremony? 5.Do you that mp elections only affect one area.for example tippex used on mp vote in Luchenza will only affect that outcomes of Luchenza but not of Karonga Nyungwe or Migowi but tippex used on president vote in Mzimba for example can affect the outcomes of the whole country?
@mdakakachokammanja7510
@mdakakachokammanja7510 20 күн бұрын
So tippex used on MPs and councillors was ok cos only affected mma constituencies? Maganizidwe a chinyengotu awa 🤣 Thought the MPs were elected in the same manner as the president ? You don’t pick and choose when you talk about justice, that is a corrupt mindset, kufuna zofuna zako zokha zichitike
MAI JANE ANSAH (TIPPEX) part TWO-02
53:34
LIKI-LIKI TELEVISION
Рет қаралды 18 М.
La final estuvo difícil
00:34
Juan De Dios Pantoja
Рет қаралды 26 МЛН
The most impenetrable game in the world🐶?
00:13
LOL
Рет қаралды 16 МЛН
ANANDIKWATIRA NDILI NDI ANA ATATU KALE...true love
31:36
LIKI-LIKI TELEVISION
Рет қаралды 15 М.
MAI JANE  ANSAH ABWERA POYELA KUKAMBAPO ZA CHISANKHO CHA 2019!.🇲🇼
40:06
JB at Kanjuchi in Mzimba-1
9:34
Media Diary Consultants
Рет қаралды 8 М.
Times Exclusive featuring Bakili Muluzi - 11 May 2024
58:41
Times 360 Malawi
Рет қаралды 160 М.
JANE ANSAH PAC INQUIRY GOOFS
8:09
Davies Mofolo
Рет қаралды 1,7 М.
万多人SPM全科A是怎么回事? 27-5-2024@ahchungtalkshow8911
10:34
阿聪吹水堂 Ah Chung Talkshow
Рет қаралды 103 М.
MZIMAI WATHAWA CHITHUMWA KU MPOTO ....THE CITIZEN LIVE
31:56
MALIRO AKASIIDWA KU NTCHITO KWA MALEMU NDI akumtundu
16:16
LIKI-LIKI TELEVISION
Рет қаралды 31 М.
BRIAN BANDA LELO PA 6 MAY,  KWAGWANJI KUMUZUKUTA  DR CHILIMA 🙌
34:37
Village champion
Рет қаралды 29 М.
La final estuvo difícil
00:34
Juan De Dios Pantoja
Рет қаралды 26 МЛН