Mr Namiwa you our truly freedom fighter we as malawi you have our support
@chippakaribafox2865Ай бұрын
Opusa ndife amalawi...mbuzi za anthu We toralate nosense
@BeatriceProfessorАй бұрын
Mamawe now namiwa ukubwera ngati coming new Generation 😂😂😂kodi ku Malawi kuli anthu olimba mtima ngati chonchi aaaaa mumwa chani? Mr true leader I don’t believe this yooo am so proud of you namiwa i hope mwabwera ndi Mulungu angokusiyani kenako Mulungu apitaso kumwamba basi ✊✊✊✊✊💪💪💪💪💪🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥❤❤❤❤❤❤❤respect pati
@BiliatMzungudalaАй бұрын
Tili nanu limodzi dziko lamalawi silibwino😢
@AmosBandula-up4ybАй бұрын
That's true powerful message thank you my brother .
@ElliottBelon15 күн бұрын
Real freedom fighter...mr namiwa
@jamesjillan9687Ай бұрын
Anamiwa our hope now lies on you,mwina Malawi nkupulumuka kumavuto omwe tilinawo,big up sir.
@ernestphiri5507Ай бұрын
The president must step down to allow the commission of inquiry to investigate about the chikangawa accident freely
Agalu amenewa achoke atikwana a mcp. Awonjeza, kupha, katangare, tsankho, kuononga, komanso jealous ndi dzipani dzotsutsa.
@RonaldGama-gz9ugАй бұрын
Mr Namiwa You for one thing the Kunkuyu said that state got blackbox and its self .. pano akuti mu denge munalibemo blackbox anthuwa akudziwa chomwe chinachitika
@memoryziyaya2593Ай бұрын
i salute this papa..#SN💥no fear!!
@DysonGonthiАй бұрын
Keep the fire burning Mr namiwa🔥🔥🔥
@masterchitabwino898Ай бұрын
Following and straight to the points ena ali pa mpando chifukwa Biyeni anthu anamukonda ndikumvera kuti tisankhe izi
@chrisboyce2Ай бұрын
Thank you Comrade NAMIWA we need people like you woyipa pa Chilungamo nthawi Zonse Ndipo Osaopa, osafooka and Osatopa 💪 SKC 💔
@Halima-i4xАй бұрын
Namiwa kulimba m.tima uku ndikomwe timakufuna your are big ma chine
@EsetaGerateАй бұрын
❤❤❤ anapanga chiwembu chaumburi agaru amenewa
@LuskaMosesАй бұрын
Ambuye akudakitseni bwana mulungu akukuteni ine tsiku tsiku kulira abiyeni anapha Muthu wofunikira kuntundu wa anthu chakwera munalakwitsa koopsa😢
Exactly, how come vp osakhala ndi chitetedzo choyenera?? 😢😢
@MalonzoMazombweАй бұрын
Hon namiwa, chiyambireni kumenyera ufulu mulibe mbiri yoipa ngati activist enawa omangokhalira udzakwaye kwachakwera, inu mulibe dyera muli ndi ma bizness anu okuthandizani komanso simusankha munthu mukafuna kudzudzula.. pitilizani bwana, send number yanu.
@Happiness-p9zАй бұрын
Munthu wamkulu kulankhula mosapsatira big up
@SamuelMukhuraАй бұрын
should step down as president,and also the rest should be resign
@happychimwemwe-1805Ай бұрын
Boma latha ili palibe chazeru
@JanaJovianАй бұрын
Mr namwiwa mukuyesesa koma a mcp atinzuzakwambili
@DouglasDiminguАй бұрын
Wina azit chakwera boma🙄
@hopembendelaАй бұрын
Today you talk like seriously big up
@wendaemily3179Ай бұрын
Chifiti chi president ichi
@LewisFrancisco-o3bАй бұрын
Namiwa fire
@thomluciouss7360Ай бұрын
Let's put everything in God's hands he is the one who knows what has happened and one day the trueth will come out bisani matenda koma maliro akachitika tizamva
@mailos.laisoni7001Ай бұрын
Good work
@PatrickJames-m3wАй бұрын
Ma men you went school keep it up.
@KumbukaniKafatia-cd2hqАй бұрын
MUMAKHALA NDI NKHANI ZABWINO KOMA BACKGROUND MUSIC YANUYO IMANDINYASA KWAMBIRI. TIZASIYA KUKUPANANI FOLLOW
Ma phoneo alipo? I have the possibility to recover deleted files
@princedetbozsmallboy1749Ай бұрын
Mvuto la channel yi ma video ake kuyima yima each video please try to fix timakunyadilani pantchito yabwino
@WisikiBlack-gj4guАй бұрын
Apo mukamba chamuna big alephela awa,,zoona dziko paka ma passport kumavuta olo Zimbabwe 🇿🇼 inavuta koma ma passport sanavute , koma achakwela mmmm sikukudani koma chikondi mulibe ndidziko, kodi ngati mafika saizi yomupha chilima anakulowetsani boma, kodi ife amalawi wamba mutisunga??
@johnjoachim3820Ай бұрын
Komano osangokambirana zoti atule mpasi udindo bwanji, ma brief akambidwa but no solution. Mukakamiziine atule mpasi upesideti basi, president wannji omangoyenda even kuchiletsa osatheka aaaaa woke up guys
@Yohane-bg8bnАй бұрын
Ziko siliyedesedwa ndi ma little boy ikufunuka ma big boys peter ananana kale
Atsogoleri akamapita kwakugwa amapanga zoononga komanso kusanvera anthu akamawadzudzula. I hate chakwera the he run this government. Mcp is going to fall and shall never pass elections.
@billymhoni9527Ай бұрын
Nkhani ndipo isalekeleledwe otherwise tose sitili Safe mmalawi mono achakwera ali ndi mafunso oti ayankhe