Ulemu wako the DC iweyo sangakumange akuziwa kuti olo ukhale mundende Koma voice yako izamvekabe
@TamUs-u2h41 минут бұрын
Kalindo mzeru zamuthera kkkkk guys, Ben Longwe wamupepelesa
@bridgetmajor36462 сағат бұрын
Boma .....iliri Ayi ndinthu yatikwana .....the dc inuyo ndi 1😂😂😂
@TameeraInglis55 минут бұрын
Mr DC Winiko more faya
@BrianJoe-z7u25 минут бұрын
Boooon kalindo DC inuyo inuyo
@MarcyKamaga2 сағат бұрын
the dc ukunena zowona ukuwonera patari ndipo usazafe uzangosowa koma uyu chikangawa akuti pweteka mtima ukuwawa kwambiri m'mene anaphera skc mzimu wa sauros uwuse mwatendere
@calvinjamal711724 минут бұрын
Bonon Kalindo mwana oopsa kwambili iwe dolo
@TecksonKaima-dr6er2 сағат бұрын
Koma Mr born mwamva!!!,apuletu ayamba kufa ziwalo,moti pano mkono siukugwira ntchito.moti week yamawa timva afa mkabudula😅😅😅😅😅😅
@MosesMottah2 сағат бұрын
Akulu mukhaliketu
@chirwaellace10932 сағат бұрын
Eya nkono waku manzere wapanga paralyse😅😅😅😅😅
@VictoriaBakuliСағат бұрын
😂😂
@ShamimuBisaniСағат бұрын
Kalimdo sukunama nkhondo yafikapo panopa Iran Hezbroh Labanon ndi Palestine akuti akufuna kubwezera znse zomwe Israel yachita ku Gaza ndye kutha kwa Israel kwafika ndye anthu aja zoti Netanyahu angatumize anthu aja kunoko ndakaika mutu sukugwira Netanyahu panopa ndye zioneka
@ArchangelBandaСағат бұрын
Israel shall stand forever Let's talk about zinazo koma osati kutha kwa Israel
@IssahAluba59 минут бұрын
😂😂 wayitulukira Dc 🙌
@vittazomba23 минут бұрын
Hahahahaha koma ziliko
@FatiwelloKatemaСағат бұрын
Tirimbikire kugwirantchito yotithandiza zikorathu
@BlessingsChipetuka55 минут бұрын
Ulemu upite kwa my president the DC koma mlungu ashamed nanu
@BlessingsChipetuka49 минут бұрын
Mlungu akudalitseni the dc
@Andygoz212 сағат бұрын
Zikachitika timamvera Kwa iwe DC
@ThivadoartistDyson25 минут бұрын
Tiyen teyen kwacha pamsei
@frankiechasokoneza5802Сағат бұрын
Born Kalindo the DC
@OwenYobeСағат бұрын
KKkk koma DC Koma nde tiyamule ma truck awiri tikangulitse feetilizer tiwaone ngati avomele
@SostinMatchado-z2o2 сағат бұрын
Koma DC umaseka momukweza munthu BP ase power
@AlphaPoison-u3wМинут бұрын
Tchaya iweee 😂
@bridgetmajor36462 сағат бұрын
Koma The dc 🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥
@DavidKadewere3 сағат бұрын
Mr chakwela kkkkkkkk kom ayi zikom 😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂
@BoscoJosaya-u3r2 сағат бұрын
The DC ❤
@PulayaKalaka2 сағат бұрын
Proper Ganda
@JamesLongwe-qz9fdСағат бұрын
Ndiwe wa chikangawa 😂😂
@TecksonKaima-dr6er2 сағат бұрын
Mwamnyooooo auzeeee
@MosesDicostar2 сағат бұрын
😅😅😅😅😅 born kalindo ndlibe nawe mawu paka ukusaka ndende kkkkkkk😅
@Thewarrior70932 сағат бұрын
No wonder nkono wake wathyoka galu wa munthu
@MarcyKamaga2 сағат бұрын
ndipo akayiati mwatikhumudwitsa kwambiri ndipo murungu akuyendereni zowonadi mayi zukani mama chipani chathu chikutiwawa kwambiri koma chakwera murungu akurange koopya
Kalindo muuze Chakwerayo kuti dzulo lomweri Iran yayankhul pa Aljazeerah kuti yakonzeka 100% kuphulisa Israel ndye kutha kwa Benjamin Netanyahu kutha kwake kwafika panopa
@ArchangelBandaСағат бұрын
Kkkk maloto chabe amenewo Israel shall stand forever
@RoseThindwa3 сағат бұрын
Boma ili more tricks😂😂
@EvanceGilmonСағат бұрын
Zazii
@SelinaGamaliyere-q8v2 сағат бұрын
Boma la mamafia
@RebeccaFinias3 сағат бұрын
Bambo nyoooo tsopano
@WestonGawaza2 сағат бұрын
UTM ikalipo ndi mphavu chaka chino osasintha maudindo zinkhale mene zinaliri .MARRY chilima president Anenekuti tipange History malawi ziko lose lapasi