Koma ine ndikufuna Kuti akabambe ndi mtumbuka modzi mwa inu kuluza modzi akhale Vice President zikhala bwino
@PatrickFicklem6 күн бұрын
Pk mwamutaya?
@abelkayange8666 күн бұрын
One ndikuganiza kuti akabambe atsogole Mtumbuka akhale vice
@DjshukulanGift6 күн бұрын
Ndipo ndizomwe ndimafuna ,even me
@clementmahoka62876 күн бұрын
My genuine advice to UTM: Don't make alliance with any party unless you are taking the leading role (presidential position) in that alliance. Otherwise, kaloweni nokha kuzisankho, and when you lose accept it and move ahead, you will win in 2030 with landslide because i don't see any leader who can change zinthu apart from leaders in UTM
@PetualCheyo6 күн бұрын
Exactly my thoughts
@modestamhango77375 күн бұрын
Zoona mwanenazi. 👏🏻👏🏻👏🏻👏🏻
@chifundomatumula16526 күн бұрын
Combination of Mathews mtumbuka and kabambe can take this nation to another level, Akweni pa mpando wa u SG ndiokwanila
@chesterphiri75236 күн бұрын
I think so too
@SimonJesimani6 күн бұрын
Koma guys achinyamatafe tikanagwirizana kuvotera UTM. Kuli ma candidate abwino kwambiri. Chakwera is a waste of time
@lightwellsilumbu6 күн бұрын
zoona
@justinchabwera53806 күн бұрын
Kwanu konko, congress ikunyenyani ndthu
@johnbullyohanittokasikizim71276 күн бұрын
@@justinchabwera5380yakuphayo😂
@rozertmbale95456 күн бұрын
@@johnbullyohanittokasikizim7127tiyavoterabe Congress
@AbsalomNkhoma5 күн бұрын
My vote 4 mathews Mtumbuka ,a leader of gud vision ,osati kwinaku
@actuarialscience22836 күн бұрын
Akulankhula Chichewa koma zamnzeru zokhazokha. You're very wise.
@SamukLungu-zg7fl6 күн бұрын
Amene azasankhidwe pa udindo wa u president arumbire kuti nkhope ya chirima asazachose paripose pamene yiri osati kungotenga ndikuchosa zose ayi
@BostonMalisawo6 күн бұрын
DR:KABAMBE :AZAWINA KOMANSO DR MTUMBUKA AZAKHALA VICE PRESDENT
@GeorgeMwale-ce8eb6 күн бұрын
Kabambe to vice opanfansi zokqmbilana
@actuarialscience22836 күн бұрын
God bless you Matthews Mtumbuka. You're the next president.
@AngelaMphinji6 күн бұрын
Mmmm. O mwa. Hundred. Mtumbuka😂
@MakhumboMbowe6 күн бұрын
a mr.mtumbuka tiri pambuyopanu mulunga akusogorereni ❤
Indeeeeeee awa ndi Nyamata uyu Bola azakhale President or VP oyeeee UTM Moto🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥
@BerthaMisanjo6 күн бұрын
Mfundo full more 🔥🔥🔥 mtumbuka
@JoycieMbaya6 күн бұрын
Mtumbuka president, vice Kabambe. I can't wait to vote!
@DeliaKaduya6 күн бұрын
Komatu anzanuso ankatero asanatenge boma, kungotenga ali buzy kumakakwera njinga ku Germany ife tikufa ndi njala, ntchito 1 million lija lasanduka kosaka chiteze kutchire 😢😢, Ambuye muoneni pomwe wafika Malawi tsopano, tisankhireni tsogoleri yemwe achose misonzi yathu, musalole tizisankhire tokha tsogoleri, Koma inuyo mutisankhire
@ussimasi24586 күн бұрын
😂😂😂😂kabaza
@user-nu3dq5hi7q4 күн бұрын
Pali kusiyana kwambiri pakati pa munthu wa xool ndi un educated. Enawo adanena ndithu kuti,one sindidziwa kanthu. Power mtumbuka akunenetsa Pano kuti Ali ndi upangiri wosiyanasiyana pa nkhani ya chitukuko
@samuzymkwanya84906 күн бұрын
He sounds like VP not President But Goodluck Mtumbuka ife a DPP tisankhileni munthu oti tagwile naye ntchito muchaka cha 2025 ADADI akazatenga usogoleri Plz ma delegeti a UTM munthu ndiameneyu
@GladesMhango3 күн бұрын
UTM oyeeh🥳🥳 waluka Continue waluta🔥🔥🔥
@PrescotMkhwema-gl4eq5 күн бұрын
I'm proud to have a youthful democracy in leadership in Malawi
@Biath-m4b6 күн бұрын
Zikumveka bwino koma vuto mumalonjeza tikavota simumatikumbukila ai ndye chonde mukunenazo zikhale zoona
@JeanfatsanJere6 күн бұрын
Mr mtumbuka ur president of Malawi ❤ UTM my vote
@MathaNamanja6 күн бұрын
Mmmmm hmmm Ambuye atithandizee
@khumbombale4965 күн бұрын
Atsogolreli a chipani cha UTM mutachita kuti kutenga A Mtumbuka ndi A Bambe onse kukhala kuyendesa U T M ndipo a Mayi athu okondedwa ndiposo olimba mtima a Kaliyati akhale pompo as SG ndipo musalowe mu alliance. Dzikoli lizaphulidwa.
Maganizo abwino big koma musalonjeze zambiri pakamodzi zingalowe bodza😮
@IshmaelAyami-l7s4 күн бұрын
Thandizen Mtumbuka zake Ku Mpotokoo😊
@user-iq5xk6ju7y5 күн бұрын
Me waiting the results after the Convention in November. Koma chomwe mudziwe Mtumbuka and Kabambe is more less than WIPON OF MASS DISTRACTION. Fredokiss will be the Minister of youth in the first place, but hope is there to be President in future. UTM ikadzangotenga boma ikubwera kudzakhala 🔥🔥🔥🔥 zinazi tayesa komanso zinazi tazibweleza koma manyaka okhaokha 🤮 a Malawi tikapusa ndithu dzikoli sitidzalinva kukoma mpaka Yesu adzabwera. Unless there is another Malawi after this life kumene mwina SKC anapita kukatikonzera 😭😭😭😭 REST WELL BIYENI 😭😭
@GeoffTchezan6 күн бұрын
Kodi nd za m'maboma? Kkkkk zikundivuta kunvetsetsa ine😅
@WillyNyirenda-l7h6 күн бұрын
Encouraging speech. Let's support him. Let's not look at his age but his ability to deliver. But should be careful not to promise people the moon.
@JoshuaNyirongo6 күн бұрын
Dr Mtumbuka ndi mtumbuka. Aphunzira kulankhula pompano asiya kuyowoya
@NolityKondowe6 күн бұрын
Vuto ndi wa ku mpoto.Ndale za mmalawi ndi za tsankho ndipo ndi za mzigawo.
@henrymwale89946 күн бұрын
Dziko linasintha chotsani kaganizidwe kameneko
@CatherineDesire4 күн бұрын
100 percent perfect said
@CatherineDesire4 күн бұрын
Kodi usi wadzima 🙄amajijilikila pakatipa 🙌
@ishmaelnkosi62286 күн бұрын
During Saulos iyeyi anali kuti and why saanamusankhe?
Malawi is lacking good leadership but these two leaders Mtumbuka and kabambe they must lead us ViVa UTM tsogolo lowala.
@elsa19736 күн бұрын
Chepesani kusisa voice pa intro makosana
@marthamwenelupembe11886 күн бұрын
Mulungu alowelelepo plz🙏 all the best
@SaidiMbawa-st6bj6 күн бұрын
Nthawi yonseyi adali kuti awa ndikudabwa kuti palibe akuluakulu ena palibe apa
@giftedmshan67796 күн бұрын
Mtumbuka hoyeeee
@SlindiryLoveness4 күн бұрын
Zaziii kungofuna kuzaba basi mungakhale prensident waziko inu kungofuna kuzawononga ziko basi bwanji panopa kulinjara osatuluka kuti kamene ulinako wapase anthu ovutika maboza basi
@paulbanda96386 күн бұрын
MCP Kuba kwambiri, tengani dzikoli a mtumbuka
@kensonmbewe66926 күн бұрын
Mudzaziwonanso m'mene adzazibere amenewa ndalama, these are politicians, nanji ma amateur
@EliasSupanela6 күн бұрын
True
@justinchabwera53806 күн бұрын
Kudzikonda chabe
@ishmaelnkosi62286 күн бұрын
Palibe zachilendo zikukambidwa apa
@NellieChikuse6 күн бұрын
There's future
@FatimaUmali-pc8sy6 күн бұрын
Atumbuka nawo ndiasakho amangofuna okhaokha maudindo wakhwituwakhwitu zanga eine mtumbbuka Bola kana be 😮😮😮
@jonathanmwanja39946 күн бұрын
Find another reason. That one is outdated.
@isaihmagani56976 күн бұрын
@@jonathanmwanja3994pita nazo kwina zimenezo ku UTM kulibe
@ephraimkadamika6 күн бұрын
Koma nanu pano sitikuyendera za ntundu koma yemwe awombole malawi
@MaryChavula-jz3di6 күн бұрын
Tadzilankhulani mukamaiza mupumule tilindi ntchito zomwe tinaziwona kale ndi dpp tikufuna zimenezo zongotinamizazi zatikwana
@GeoffreyMikondo6 күн бұрын
Pa mbuyo panu inu ndi kambabe kammbilani mugwile limodzi
@Veronica-o2d4 күн бұрын
UTM for sale now
@OmarManjawira-up3ns6 күн бұрын
A stitch intime indeed serves nine ,Utm as a problem of kuyang'anira zinthu ( kulekelera even the late SKC had a same problem so izizi we re not sure bwana ,,,,,, cos u have never been there before nde this time around Malawians wants anthu odziwa zintchito osati Ya class ,atleast "Kabambe , Atupele, Chihana and APM
@KettinesMunthali6 күн бұрын
Tiyeni tiyese atumbuka mwina angatithandize
@patrickmatabwa58286 күн бұрын
You are right its high time we should try the northerner and its my belief will do better as will be from minority may work for all regions to get the second term.....if we miss this opportunity mmmm kaya ..zakwathuzi sizikuthandiza chitukuko chadziko.....
@komanicomrademunyenyembe90966 күн бұрын
😢tione zina
@RowlandChimzimu6 күн бұрын
Mtumbuka wooooooyeeeeeeee
@MarthaGama-q1o6 күн бұрын
Mfundo ndiye zikuveka koma Poti a Malawi amadziwa kulonjeza koma kukwanilitsa kumavuta, akangowina amalephela kukwanilitsa zomwe amalonje ,chimene chimakula ndi kudzikundikila kusava zofuna zawanthu komanso kulephela Ku tsegula misika ya a dmaric , koma ngati mukunena zowona vote yanga ndiyanu
@JuniorSamalia6 күн бұрын
Lucky to you!
@actuarialscience22836 күн бұрын
There is no doubt he is intelligent. Ku MCP kulibe olo wa JCE. Chakwera alibe JC;
@rosebychikopa96606 күн бұрын
Hahahaha
@mishecksipolo71536 күн бұрын
Eti eti ,ali ndi PHD tu uyu
@KettinesMunthali6 күн бұрын
Za school anathana nazo pano alipa school yapa ground
@sashaphiri66626 күн бұрын
😂😂😂
@user-le9su3mt7r6 күн бұрын
Good bomaa
@jennyx69146 күн бұрын
amanganya kapena kuti a V P mr usi bwanji sanathamangileko kokadya chitedze abale inu? please mr. bon kalindo muuzeni mnzanu kuti akasye chitedze pomwe inu mr bon kalindo mukulankhulira anthu chilungamo our advocate amphawife
@mabvutomichaelpanagona19496 күн бұрын
Ineyo ndikusapota inuyo nose awiri Dr mtumbuka ,komaso Dr D,kabambe inuyo awirinu amene alephele adzakhale wa chiwiri kapena nditi vice president, mpando wa secretary ndikanakonda wini wa mpando umenewu asachoke akhale pomwepo mayi p, kaliati, mayi kaliati chonde sikukunyozani ayi mpando wanu ndi secretary general ndiye wanu mwachoka nawo kutali ndipo umakhalani,chonde chonde mai kaliati.uyu kazitapeyu mumati ndi Michael usi ameneyu akhale owona za achinyamata kapena nditi wa yufi chigawo cha kumwela adzinamiza anyamata akumeneko kuti adzipeza nthawi yopanga madirama ake akumudikira bon kalindo, nginde,mai asikono komaso achisi ndi enaotelo.
@JuniorSamalia6 күн бұрын
Kkk koma ase
@QueenMkandawire-sg4df5 күн бұрын
😂😂😂😂koma ada
@AlexiousMakondetsa-hl6dy6 күн бұрын
Mwauyu ndikuonamo utsogoleri
@EliaThomas-vp9jz6 күн бұрын
English v Mathematics Devaluation v Dama
@GodfreyWhayo-hh1dm6 күн бұрын
Kuyankhula kwa munthu oyembekezera kukhala mtsogoleri wa dziko koma kumeneku .
@MavutoLorry6 күн бұрын
Kulibe mapokoso
@ExcitedBreakingWaves-oh3zb6 күн бұрын
mtumbuka mukunama.
@charleskayerasky13426 күн бұрын
Ali ndi befutu koma azalimba during campaign time😅