MUKAMVA KWAYAMBA MAPOKOSO KU UTM MUSADABWE NKHANI YAKE NDI YOMWE WAYANKHULA MATTHEWS MTUMBUKA LERO

  Рет қаралды 51,245

Makosana

Makosana

Күн бұрын

Пікірлер: 186
@muhamadizaidiphiri4449
@muhamadizaidiphiri4449 6 күн бұрын
Koma ine ndikufuna Kuti akabambe ndi mtumbuka modzi mwa inu kuluza modzi akhale Vice President zikhala bwino
@PatrickFicklem
@PatrickFicklem 6 күн бұрын
Pk mwamutaya?
@abelkayange866
@abelkayange866 6 күн бұрын
One ndikuganiza kuti akabambe atsogole Mtumbuka akhale vice
@DjshukulanGift
@DjshukulanGift 6 күн бұрын
Ndipo ndizomwe ndimafuna ,even me
@clementmahoka6287
@clementmahoka6287 6 күн бұрын
My genuine advice to UTM: Don't make alliance with any party unless you are taking the leading role (presidential position) in that alliance. Otherwise, kaloweni nokha kuzisankho, and when you lose accept it and move ahead, you will win in 2030 with landslide because i don't see any leader who can change zinthu apart from leaders in UTM
@PetualCheyo
@PetualCheyo 6 күн бұрын
Exactly my thoughts
@modestamhango7737
@modestamhango7737 5 күн бұрын
Zoona mwanenazi. 👏🏻👏🏻👏🏻👏🏻
@chifundomatumula1652
@chifundomatumula1652 6 күн бұрын
Combination of Mathews mtumbuka and kabambe can take this nation to another level, Akweni pa mpando wa u SG ndiokwanila
@chesterphiri7523
@chesterphiri7523 6 күн бұрын
I think so too
@SimonJesimani
@SimonJesimani 6 күн бұрын
Koma guys achinyamatafe tikanagwirizana kuvotera UTM. Kuli ma candidate abwino kwambiri. Chakwera is a waste of time
@lightwellsilumbu
@lightwellsilumbu 6 күн бұрын
zoona
@justinchabwera5380
@justinchabwera5380 6 күн бұрын
Kwanu konko, congress ikunyenyani ndthu
@johnbullyohanittokasikizim7127
@johnbullyohanittokasikizim7127 6 күн бұрын
@@justinchabwera5380yakuphayo😂
@rozertmbale9545
@rozertmbale9545 6 күн бұрын
​@@johnbullyohanittokasikizim7127tiyavoterabe Congress
@AbsalomNkhoma
@AbsalomNkhoma 5 күн бұрын
My vote 4 mathews Mtumbuka ,a leader of gud vision ,osati kwinaku
@actuarialscience2283
@actuarialscience2283 6 күн бұрын
Akulankhula Chichewa koma zamnzeru zokhazokha. You're very wise.
@SamukLungu-zg7fl
@SamukLungu-zg7fl 6 күн бұрын
Amene azasankhidwe pa udindo wa u president arumbire kuti nkhope ya chirima asazachose paripose pamene yiri osati kungotenga ndikuchosa zose ayi
@BostonMalisawo
@BostonMalisawo 6 күн бұрын
DR:KABAMBE :AZAWINA KOMANSO DR MTUMBUKA AZAKHALA VICE PRESDENT
@GeorgeMwale-ce8eb
@GeorgeMwale-ce8eb 6 күн бұрын
Kabambe to vice opanfansi zokqmbilana
@actuarialscience2283
@actuarialscience2283 6 күн бұрын
God bless you Matthews Mtumbuka. You're the next president.
@AngelaMphinji
@AngelaMphinji 6 күн бұрын
Mmmm. O mwa. Hundred. Mtumbuka😂
@MakhumboMbowe
@MakhumboMbowe 6 күн бұрын
a mr.mtumbuka tiri pambuyopanu mulunga akusogorereni ❤
@kumbukanikafwafwa
@kumbukanikafwafwa 6 күн бұрын
Mtumbuka yu ndendende Peter. ❤❤❤ Chichewa chovuta kma zipatso zautsogoleli zooneka
@doreenkaliati3166
@doreenkaliati3166 6 күн бұрын
Indeeeeeee awa ndi Nyamata uyu Bola azakhale President or VP oyeeee UTM Moto🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥
@BerthaMisanjo
@BerthaMisanjo 6 күн бұрын
Mfundo full more 🔥🔥🔥 mtumbuka
@JoycieMbaya
@JoycieMbaya 6 күн бұрын
Mtumbuka president, vice Kabambe. I can't wait to vote!
@DeliaKaduya
@DeliaKaduya 6 күн бұрын
Komatu anzanuso ankatero asanatenge boma, kungotenga ali buzy kumakakwera njinga ku Germany ife tikufa ndi njala, ntchito 1 million lija lasanduka kosaka chiteze kutchire 😢😢, Ambuye muoneni pomwe wafika Malawi tsopano, tisankhireni tsogoleri yemwe achose misonzi yathu, musalole tizisankhire tokha tsogoleri, Koma inuyo mutisankhire
@ussimasi2458
@ussimasi2458 6 күн бұрын
😂😂😂😂kabaza
@user-nu3dq5hi7q
@user-nu3dq5hi7q 4 күн бұрын
Pali kusiyana kwambiri pakati pa munthu wa xool ndi un educated. Enawo adanena ndithu kuti,one sindidziwa kanthu. Power mtumbuka akunenetsa Pano kuti Ali ndi upangiri wosiyanasiyana pa nkhani ya chitukuko
@samuzymkwanya8490
@samuzymkwanya8490 6 күн бұрын
He sounds like VP not President But Goodluck Mtumbuka ife a DPP tisankhileni munthu oti tagwile naye ntchito muchaka cha 2025 ADADI akazatenga usogoleri Plz ma delegeti a UTM munthu ndiameneyu
@GladesMhango
@GladesMhango 3 күн бұрын
UTM oyeeh🥳🥳 waluka Continue waluta🔥🔥🔥
@PrescotMkhwema-gl4eq
@PrescotMkhwema-gl4eq 5 күн бұрын
I'm proud to have a youthful democracy in leadership in Malawi
@Biath-m4b
@Biath-m4b 6 күн бұрын
Zikumveka bwino koma vuto mumalonjeza tikavota simumatikumbukila ai ndye chonde mukunenazo zikhale zoona
@JeanfatsanJere
@JeanfatsanJere 6 күн бұрын
Mr mtumbuka ur president of Malawi ❤ UTM my vote
@MathaNamanja
@MathaNamanja 6 күн бұрын
Mmmmm hmmm Ambuye atithandizee
@khumbombale496
@khumbombale496 5 күн бұрын
Atsogolreli a chipani cha UTM mutachita kuti kutenga A Mtumbuka ndi A Bambe onse kukhala kuyendesa U T M ndipo a Mayi athu okondedwa ndiposo olimba mtima a Kaliyati akhale pompo as SG ndipo musalowe mu alliance. Dzikoli lizaphulidwa.
@TitusGoba
@TitusGoba 6 күн бұрын
Akukhala ngat akuwelenga nkhani pa mbc, ngat Hassan Goba, eg, akumukuntha kwambiri mbomalooooo😂😂😂
@DjshukulanGift
@DjshukulanGift 6 күн бұрын
Dr kabambe akhare president inu vaic
@CelphaStephanSilungwe
@CelphaStephanSilungwe 5 күн бұрын
Never make alliance with other parties for utm to be successful
@LimbaniZimba
@LimbaniZimba 6 күн бұрын
My vote
@AndrewjemesJemes
@AndrewjemesJemes 6 күн бұрын
Ine sinima vota chifukwa snikhulupilira anthu andale koma uyu afuna aniyambise akanitenga bwino
@benitomtegha3788
@benitomtegha3788 6 күн бұрын
Welcome Mathews Mtumbuka. This is the rebirth of new Chilimas. Let's fulfill Chilimas ideas and beyond.
@MakeSunshine100
@MakeSunshine100 6 күн бұрын
Lets go!!!! Lets go!!!!
@emmaculatemenzeiwa
@emmaculatemenzeiwa 6 күн бұрын
Contesting doesn't mean division. Let the people's choice win.
@MpapiParadise
@MpapiParadise 6 күн бұрын
Utm ingotaya nthawi , kulibe wanzelu kumeneku ai . Utm inatha 2021
@PatrickFicklem
@PatrickFicklem 6 күн бұрын
Maganizo abwino big koma musalonjeze zambiri pakamodzi zingalowe bodza😮
@IshmaelAyami-l7s
@IshmaelAyami-l7s 4 күн бұрын
Thandizen Mtumbuka zake Ku Mpotokoo😊
@user-iq5xk6ju7y
@user-iq5xk6ju7y 5 күн бұрын
Me waiting the results after the Convention in November. Koma chomwe mudziwe Mtumbuka and Kabambe is more less than WIPON OF MASS DISTRACTION. Fredokiss will be the Minister of youth in the first place, but hope is there to be President in future. UTM ikadzangotenga boma ikubwera kudzakhala 🔥🔥🔥🔥 zinazi tayesa komanso zinazi tazibweleza koma manyaka okhaokha 🤮 a Malawi tikapusa ndithu dzikoli sitidzalinva kukoma mpaka Yesu adzabwera. Unless there is another Malawi after this life kumene mwina SKC anapita kukatikonzera 😭😭😭😭 REST WELL BIYENI 😭😭
@GeoffTchezan
@GeoffTchezan 6 күн бұрын
Kodi nd za m'maboma? Kkkkk zikundivuta kunvetsetsa ine😅
@WillyNyirenda-l7h
@WillyNyirenda-l7h 6 күн бұрын
Encouraging speech. Let's support him. Let's not look at his age but his ability to deliver. But should be careful not to promise people the moon.
@JoshuaNyirongo
@JoshuaNyirongo 6 күн бұрын
Dr Mtumbuka ndi mtumbuka. Aphunzira kulankhula pompano asiya kuyowoya
@NolityKondowe
@NolityKondowe 6 күн бұрын
Vuto ndi wa ku mpoto.Ndale za mmalawi ndi za tsankho ndipo ndi za mzigawo.
@henrymwale8994
@henrymwale8994 6 күн бұрын
Dziko linasintha chotsani kaganizidwe kameneko
@CatherineDesire
@CatherineDesire 4 күн бұрын
100 percent perfect said
@CatherineDesire
@CatherineDesire 4 күн бұрын
Kodi usi wadzima 🙄amajijilikila pakatipa 🙌
@ishmaelnkosi6228
@ishmaelnkosi6228 6 күн бұрын
During Saulos iyeyi anali kuti and why saanamusankhe?
@JaporAhmed-e2j
@JaporAhmed-e2j 6 күн бұрын
Pomwe pagona khani ndiposekula makapanipo boma lamalawi tikumvutika kamba kopanda makapan chifukwa tilindizambili zotiyenereza modzikoli dzikomo Dr Matthews
@henryphiri6100
@henryphiri6100 6 күн бұрын
Tikadzaluza tidzavomereze zotsatirazo chifukwa sitikufuna kuti chipani chife.
@jonathanshonga4742
@jonathanshonga4742 5 күн бұрын
mulibe utsogoleri umu, zikatha anona ndi aswiswiri dithu
@jimmykanjere5877
@jimmykanjere5877 5 күн бұрын
Akulu awa ndithu zadzawina,mark my words
@ChristianMalingamoyo
@ChristianMalingamoyo 6 күн бұрын
Pakati pa iwe ndi kabambe please ,mulungu atipase
@MzikaPhiri
@MzikaPhiri 6 күн бұрын
Ine ndamukonda Mtumbuka
@lucianogeoffrey4275
@lucianogeoffrey4275 6 күн бұрын
Kambalame koulukitsa kamaphonya chisa bwana mukuyenera kukhazika mtima pandi phuma lachuluka. Otherwise you’re a good leader 🎉
@AubreyWilson-j8w
@AubreyWilson-j8w 6 күн бұрын
Zikomo bwana Bola nanunso mukazawina musazayambe kunena kuti (wakhwitu wakhwitu)
@user-db3mh9wr9v
@user-db3mh9wr9v 6 күн бұрын
Mtumbuka ndi Kabambe ndiomwe agathandize dziko lino
@user-ro3yw2zv5b
@user-ro3yw2zv5b 6 күн бұрын
Where were you Mr mtumbuka?UTM may God see you through
@AbelNyirenda-lu1qy
@AbelNyirenda-lu1qy 6 күн бұрын
I love you Mr mtumbuka /
@TreverDominic
@TreverDominic 6 күн бұрын
Zaziiii bas ina ankatelo
@MadalitsoBokosi-j3u
@MadalitsoBokosi-j3u 6 күн бұрын
Bola izi sizokhalira kunja nsima misika mumuuze usi apite akajambule tikuferanji komwe akuja chiteze
@AustinMhone-r3s
@AustinMhone-r3s 6 күн бұрын
Malawi is lacking good leadership but these two leaders Mtumbuka and kabambe they must lead us ViVa UTM tsogolo lowala.
@elsa1973
@elsa1973 6 күн бұрын
Chepesani kusisa voice pa intro makosana
@marthamwenelupembe1188
@marthamwenelupembe1188 6 күн бұрын
Mulungu alowelelepo plz🙏 all the best
@SaidiMbawa-st6bj
@SaidiMbawa-st6bj 6 күн бұрын
Nthawi yonseyi adali kuti awa ndikudabwa kuti palibe akuluakulu ena palibe apa
@giftedmshan6779
@giftedmshan6779 6 күн бұрын
Mtumbuka hoyeeee
@SlindiryLoveness
@SlindiryLoveness 4 күн бұрын
Zaziii kungofuna kuzaba basi mungakhale prensident waziko inu kungofuna kuzawononga ziko basi bwanji panopa kulinjara osatuluka kuti kamene ulinako wapase anthu ovutika maboza basi
@paulbanda9638
@paulbanda9638 6 күн бұрын
MCP Kuba kwambiri, tengani dzikoli a mtumbuka
@kensonmbewe6692
@kensonmbewe6692 6 күн бұрын
Mudzaziwonanso m'mene adzazibere amenewa ndalama, these are politicians, nanji ma amateur
@EliasSupanela
@EliasSupanela 6 күн бұрын
True
@justinchabwera5380
@justinchabwera5380 6 күн бұрын
Kudzikonda chabe
@ishmaelnkosi6228
@ishmaelnkosi6228 6 күн бұрын
Palibe zachilendo zikukambidwa apa
@NellieChikuse
@NellieChikuse 6 күн бұрын
There's future
@FatimaUmali-pc8sy
@FatimaUmali-pc8sy 6 күн бұрын
Atumbuka nawo ndiasakho amangofuna okhaokha maudindo wakhwituwakhwitu zanga eine mtumbbuka Bola kana be 😮😮😮
@jonathanmwanja3994
@jonathanmwanja3994 6 күн бұрын
Find another reason. That one is outdated.
@isaihmagani5697
@isaihmagani5697 6 күн бұрын
​@@jonathanmwanja3994pita nazo kwina zimenezo ku UTM kulibe
@ephraimkadamika
@ephraimkadamika 6 күн бұрын
Koma nanu pano sitikuyendera za ntundu koma yemwe awombole malawi
@MaryChavula-jz3di
@MaryChavula-jz3di 6 күн бұрын
Tadzilankhulani mukamaiza mupumule tilindi ntchito zomwe tinaziwona kale ndi dpp tikufuna zimenezo zongotinamizazi zatikwana
@GeoffreyMikondo
@GeoffreyMikondo 6 күн бұрын
Pa mbuyo panu inu ndi kambabe kammbilani mugwile limodzi
@Veronica-o2d
@Veronica-o2d 4 күн бұрын
UTM for sale now
@OmarManjawira-up3ns
@OmarManjawira-up3ns 6 күн бұрын
A stitch intime indeed serves nine ,Utm as a problem of kuyang'anira zinthu ( kulekelera even the late SKC had a same problem so izizi we re not sure bwana ,,,,,, cos u have never been there before nde this time around Malawians wants anthu odziwa zintchito osati Ya class ,atleast "Kabambe , Atupele, Chihana and APM
@KettinesMunthali
@KettinesMunthali 6 күн бұрын
Tiyeni tiyese atumbuka mwina angatithandize
@patrickmatabwa5828
@patrickmatabwa5828 6 күн бұрын
You are right its high time we should try the northerner and its my belief will do better as will be from minority may work for all regions to get the second term.....if we miss this opportunity mmmm kaya ..zakwathuzi sizikuthandiza chitukuko chadziko.....
@komanicomrademunyenyembe9096
@komanicomrademunyenyembe9096 6 күн бұрын
😢tione zina
@RowlandChimzimu
@RowlandChimzimu 6 күн бұрын
Mtumbuka wooooooyeeeeeeee
@MarthaGama-q1o
@MarthaGama-q1o 6 күн бұрын
Mfundo ndiye zikuveka koma Poti a Malawi amadziwa kulonjeza koma kukwanilitsa kumavuta, akangowina amalephela kukwanilitsa zomwe amalonje ,chimene chimakula ndi kudzikundikila kusava zofuna zawanthu komanso kulephela Ku tsegula misika ya a dmaric , koma ngati mukunena zowona vote yanga ndiyanu
@JuniorSamalia
@JuniorSamalia 6 күн бұрын
Lucky to you!
@actuarialscience2283
@actuarialscience2283 6 күн бұрын
There is no doubt he is intelligent. Ku MCP kulibe olo wa JCE. Chakwera alibe JC;
@rosebychikopa9660
@rosebychikopa9660 6 күн бұрын
Hahahaha
@mishecksipolo7153
@mishecksipolo7153 6 күн бұрын
Eti eti ,ali ndi PHD tu uyu
@KettinesMunthali
@KettinesMunthali 6 күн бұрын
Za school anathana nazo pano alipa school yapa ground
@sashaphiri6662
@sashaphiri6662 6 күн бұрын
😂😂😂
@user-le9su3mt7r
@user-le9su3mt7r 6 күн бұрын
Good bomaa
@jennyx6914
@jennyx6914 6 күн бұрын
amanganya kapena kuti a V P mr usi bwanji sanathamangileko kokadya chitedze abale inu? please mr. bon kalindo muuzeni mnzanu kuti akasye chitedze pomwe inu mr bon kalindo mukulankhulira anthu chilungamo our advocate amphawife
@mabvutomichaelpanagona1949
@mabvutomichaelpanagona1949 6 күн бұрын
Ineyo ndikusapota inuyo nose awiri Dr mtumbuka ,komaso Dr D,kabambe inuyo awirinu amene alephele adzakhale wa chiwiri kapena nditi vice president, mpando wa secretary ndikanakonda wini wa mpando umenewu asachoke akhale pomwepo mayi p, kaliati, mayi kaliati chonde sikukunyozani ayi mpando wanu ndi secretary general ndiye wanu mwachoka nawo kutali ndipo umakhalani,chonde chonde mai kaliati.uyu kazitapeyu mumati ndi Michael usi ameneyu akhale owona za achinyamata kapena nditi wa yufi chigawo cha kumwela adzinamiza anyamata akumeneko kuti adzipeza nthawi yopanga madirama ake akumudikira bon kalindo, nginde,mai asikono komaso achisi ndi enaotelo.
@JuniorSamalia
@JuniorSamalia 6 күн бұрын
Kkk koma ase
@QueenMkandawire-sg4df
@QueenMkandawire-sg4df 5 күн бұрын
😂😂😂😂koma ada
@AlexiousMakondetsa-hl6dy
@AlexiousMakondetsa-hl6dy 6 күн бұрын
Mwauyu ndikuonamo utsogoleri
@EliaThomas-vp9jz
@EliaThomas-vp9jz 6 күн бұрын
English v Mathematics Devaluation v Dama
@GodfreyWhayo-hh1dm
@GodfreyWhayo-hh1dm 6 күн бұрын
Kuyankhula kwa munthu oyembekezera kukhala mtsogoleri wa dziko koma kumeneku .
@MavutoLorry
@MavutoLorry 6 күн бұрын
Kulibe mapokoso
@ExcitedBreakingWaves-oh3zb
@ExcitedBreakingWaves-oh3zb 6 күн бұрын
mtumbuka mukunama.
@charleskayerasky1342
@charleskayerasky1342 6 күн бұрын
Ali ndi befutu koma azalimba during campaign time😅
@andofullkay8404
@andofullkay8404 6 күн бұрын
Fire
@user-gd2kl1fx1q
@user-gd2kl1fx1q 6 күн бұрын
Utm forever
@juliussamson6212
@juliussamson6212 6 күн бұрын
CHITSILU CHSKWRRA ANTHU AKUDYA ZOSADZIWIKA CHITSILU MUTU WAMAKO CHITSILU OSAGANIZA IWE CHAKWERA
@TopoTopo-bm4vw
@TopoTopo-bm4vw 6 күн бұрын
Amtumbuka aku achita kuphedwa ndimabugwe ,,,zikakhala bwino chikanakhala chiganizochake ndekuti azakhala ngati achakwela sakuziwa chomwe akuchita asongoleni ngati awa aziza yendela maganizo anthu
@henrymwale8994
@henrymwale8994 6 күн бұрын
Wandale aliyese amatero inu Mesa imakhala njira yofuna kupanga anthu kuti adziwe kuti ndiofunikira
@user-mv6tn3qv8v
@user-mv6tn3qv8v 6 күн бұрын
Mfundo zabwino kwambiri komaso zogwira mtima koma ofunika anthu kuwachotsa maganizo akuti atumbuka amachita tsankho MMA office kuti azikhala okha okha pachibale Pao
@rosechapita3434
@rosechapita3434 6 күн бұрын
Inu mukumunyozani pitanitu mukayimile muli phwii
@FredKanyerere
@FredKanyerere 6 күн бұрын
Good speach.
@ConlardNkhoma
@ConlardNkhoma 6 күн бұрын
Kkkkkk kusowa msogoleni ndiinu nomwe
@OnexAliMwale
@OnexAliMwale 6 күн бұрын
Kulankhula ndikuchita ndi zinthu zosiyana..ndipo palibe chachilendo apa
@GraceZumazuma
@GraceZumazuma 6 күн бұрын
Inutu mwinadi kuphula Malawi pa mavuto
@JoelCHIHANA-y6p
@JoelCHIHANA-y6p 6 күн бұрын
Wooooooooo
@KestonNGUBO
@KestonNGUBO 6 күн бұрын
Kuyakhul bho bho t Mr
@omarlux3434
@omarlux3434 6 күн бұрын
Wandale amana muti athu andiphepha mmm izi ine ayi
@GeorgeMwale-ce8eb
@GeorgeMwale-ce8eb 6 күн бұрын
Palibe mapokoso apa. Manganya ndiamene wazi hitsa yekha
@juliussamson6212
@juliussamson6212 6 күн бұрын
CHAKWERA AKUFUNIKA ADXAKHALE LIFE NDENDE MTSOGOLELI OYAMBA KUTI ENA ADZATENGEREPO PHUZILO
@mishecksipolo7153
@mishecksipolo7153 6 күн бұрын
Kudzangomunyonga bwanji ?
@Veronica-o2d
@Veronica-o2d 4 күн бұрын
Kamageni kaye Peter uja
@AndreaBotoman
@AndreaBotoman 6 күн бұрын
🔥🔥🔥🔥🔥🔥
Amazing Parenting Hacks! 👶✨ #ParentingTips #LifeHacks
00:18
Snack Chat
Рет қаралды 15 МЛН
У ГОРДЕЯ ПОЖАР в ОФИСЕ!
01:01
Дима Гордей
Рет қаралды 8 МЛН
Je peux le faire
00:13
Daniil le Russe
Рет қаралды 19 МЛН
Men Vs Women Survive The Wilderness For $500,000
31:48
MrBeast
Рет қаралды 94 МЛН
Ramaphosa to attend UN General Assembly in New York
6:30
SABC News
Рет қаралды 1,6 М.
KUFA NDI NJALA UTAPHODA // DENIS MAHATA
29:56
MALAWI TODAY
Рет қаралды 16 М.
Amazing Parenting Hacks! 👶✨ #ParentingTips #LifeHacks
00:18
Snack Chat
Рет қаралды 15 МЛН