APM my vote izi mzochititsa manyazi kukakamiza zinthu
@MarthaBango10 сағат бұрын
Akuchita kuoneka kut akuchita manyazi😂😂😂
@aggogokina899210 сағат бұрын
Zamanyazi kwambiri
@MjombaMoosa10 сағат бұрын
Lozani nzanu nyimbo ya bhooo Peter oyeeeee 2025 bomaaaaaa
@mariamwandwanga303510 сағат бұрын
Manyazi adan .kusowa zochita .za ziiii .adad my vote
@austenbushiri-cx1kh9 сағат бұрын
Apm ❤🎉❤🎉 my vote
@JonesChingaya-yf4gg10 сағат бұрын
Once upon a time, there was Chilima and Mia, komabe zabwino zonse Dan Luu ife tidakali pambuyo pa APM.
@cynthiakamwana680910 сағат бұрын
Zuchita kuoneka kuti,nyimboyo yodyera pasi pamtima ukudziwa kuti zonse nzabodza munyimboyi. Lozani zunu wooyeeeee. APM my vote❤
@GeshoMwakitwile9 сағат бұрын
Ambiri akhamukila ku congeresi chifukwa nkhalamba ija ikukakamila pa mpando
@DeenesNurudMeke8 сағат бұрын
Dpp my vote muona 2025 inuyo
@giftmakuluni8 сағат бұрын
Dpp my votes❤❤🥰😍
@MlaziJames9 сағат бұрын
No vote zisiluinu a mcp
@hagayichiluwe10 сағат бұрын
Chakwela my vote
@CheManganda9 сағат бұрын
Mbuzi yamunthu
@BarnetMwanyula8 сағат бұрын
My vote dpp 💯/
@ShalomMtonda8 сағат бұрын
Apm my vote 2025❤❤❤❤❤
@PeterMsukwa-i1n8 сағат бұрын
APM my vote❤️
@kingsleydaud90949 сағат бұрын
Mzimu wa Chilima ukukwapulani ,,mukuwonekaso mwamanyazi zisiru za anthu
@heavisonjames12038 сағат бұрын
Komabe lozani zanu ija ndi number 1. 😂😂😂😂😂 Sine WA Dpp koma Utm
@MuhammadSamson-yz1kl9 сағат бұрын
Aaaa Danlu manyi okhaokha ine Munthu uyu kt wa chiyao ndimakaikira kuchiyao kulibe chitsiru ngati ichi
@mikesandali84257 сағат бұрын
Iwe ndi mbuzi sure
@WisikiBlack-gj4gu10 сағат бұрын
Dan Lu idyani ndalama yamisokho ya malawi 🇲🇼 yo ife dpp woyeee
@SherifaG.Mlelemba9 сағат бұрын
Koma ngati nkusaka chakwaza,anthu azungulira mitu...Shaa! Akuti n'chiyani!??? Popeza ndi ndale...Zikazavutanso,tizabweleranso.....🤔🤔🤔
@FebbieNjewa-g3k10 сағат бұрын
APM my vote
@ElizabethMajiga10 сағат бұрын
Mesa mumati mwasita kiyimba, munali kwa atelala kosokeke kasuli ka chikangawa ka etiiii !!!! Boni kalondo sananame Ku ti tiwona zithuuuu 😂😂😂😂😂😂😂
@johnjoachim38208 сағат бұрын
Dan Lu nyimbo zako ndikuchitsa mu 🖥 yanga ndimaona ngat ndi iwe solo koma mmmm paja pamuthu
@YasinSabili-dj9xe10 сағат бұрын
Apm my vote
@EsnartGirivin8 сағат бұрын
Ndimakumbukila chaka China ndinalandila msalu zachipani chilichomse Ndidzovalatu idzo sikuti akulandilawo kuti ndimavoti anu.mukunama atidye nawo amenewo Voti ili muntima mwawo
@ElizaSoko10 сағат бұрын
Akuloza iwe Dan lu 😤😤😤😤😤😤😤😤😤😤😤
@WisdomMwale-j9h9 сағат бұрын
Eeeh, Anthu awa ndi Amodzi Asiyeni!
@jamiajafali66199 сағат бұрын
Chimwendo Allah akakulange iweyo
@MpanjeHardware10 сағат бұрын
Apm may vote
@JOSEPHTAPSON10 сағат бұрын
Kkkkkkkkk ife ndi mcp basi chete chete
@mikesandali84257 сағат бұрын
Boma ndilomweli
@MaliGomani-z4k10 сағат бұрын
Anthu akuoneka kuti sakukondwa 😂😂😂😂😂
@DeenesNurudMeke8 сағат бұрын
Ndipo kwambiri
@WiliWili-y2d8 сағат бұрын
anthu akuopa chikangawa 😂😂😂😂
@mariamwandwanga303510 сағат бұрын
Akupha ndi inuyo a mcp😅
@NosiphoMazibuko-e9z8 сағат бұрын
Inu Dan lufani pangani kapeni nick chakwera mwana president chakwera akudya ndalama uko minister ndimwana wake nick chakwera chipani cha family ichi kd nick chakwera bwanji zamabwela kuzapanga kapeni iyeyu basi asigwira ntchito mu office inu muzivutika udindo ndimwana wake wachakwera ine chipani cha mcp ndidatuluka kuyambira pomwe adakhala mwana wake nduna yoyang'anila ku immigration ndidanziwa kuti chipa cha family komatu mwanawake zabwera kukapanga kapeni ya mcp km udindo amapatsa ife mamembera amcp ndikupanga kape yopangila nick chakwera kuti zapatse udindo kachikena amamayi kuvutika kwamalawi ozasindikira kodi tikufuna atuluke mwana wa president achakwera nick chakwera yemwe Ali nduna yoyang'anila ku immigration atandize abambo ake kapeni chifukwa chipani cha mcp ndicha family mawudindo akupanzana pachi family chipani choyipa icho mpaka mwana wa president kukhala nduna km amalawi kumangoyang'anila zotero
@SqueyaHosmane8 сағат бұрын
History is best teacher
@FungulanReuben9 сағат бұрын
APM my vote 😊
@bissankal7748 сағат бұрын
Wachiyao mukutamikatu ku mcp mpaka munthu wankulu 😂😂😂😅
@BlazioKamagwira9 сағат бұрын
kuseliku akuti safuna ndalama koma kufuna kudzasintha zinthu koma ndaseka kkkkkkkkk
@GeorgeChirwa-i8v8 сағат бұрын
Adyeleni ndalamazo koma nyimbo zanu zizingabebe ngat zomwe mumaimba mmbuyomo
@brainsmkumbwa62677 сағат бұрын
DPP my vote 2025❤❤❤❤
@thomasbotha979010 сағат бұрын
Mbuzi zekhazeka zili apo chakwera ni kawawa MCP nchipani cha ng'ona
@AndersonBishop-i2t8 сағат бұрын
Dan lu ndi wa ku balaka mangochi kmaso wa mcp uja ndi mwana wa kuzi osati kuti mcp izimenye pa mtima ai kwa m'baluku mcp kulibeko sumungqwineso anawina iye uja chifukwa choti ndi.mwana wa bwno muzimo tiyeni muimiseso wina muone pa central mangochi ngat mungazaphulepo kanthu muzawaziwe anyamata apa boma kuti amangomudyela munthu ndi kumusiya iwe chimwendo
@FunnyKatchenga8 сағат бұрын
Zosakoma anta, angotengana okhaokha kumalandilitsa nsalu,ati cholinga anthu aziti anthu akulowa Ku ng'ona party 😅😅😅😅 shame on you.
@doreenkaliati31668 сағат бұрын
Nkhondo ya pansi pansi ine Chilima kulibe mwayaluka inu Adani sory 🤣🤣🤣🤣🤣🤣
@LawrenceDickens-jk3zx8 сағат бұрын
Kamanjekete yomweyo😂😂😂 DPP my vote
@Samson-ve5rs9 сағат бұрын
Apm my vote awa alephera nduna zopanda nzeru
@DeliaKaduya8 сағат бұрын
Mwaiwala muja tinagwetsa ndede ku chikangawa chitsekoso atseka 😢
@NosiphoMazibuko-e9z8 сағат бұрын
Km amwene mcp yata basi inu zowoona okupangilani kapeni akhale Dan lufani km mcp nde basi yata vuto mcp palibe yemwe angakope anthu chifukwa chake akugula woyimba kusowa kwachipani inu amcp okupangilani kapeni yokopha anthu kuchipani Dan lufani
@EstherchavulankhomaNkhoma8 сағат бұрын
Inuyo Pagani zaddwanuzo dzuwa salozelana aliyese amalionakaye musiyeni dan lu
@PrinceThom-pe6ie9 сағат бұрын
MCP si political party koma music industry.
@wisdom20mkango499 сағат бұрын
Copy and paste 😂😂😂😂 learn to write your own comments
Chakwera ndiye satana, kwake nkupha, kuba ndi kuwononga, sangawine or pang'ono
@JamesChiphwanya-m4v10 сағат бұрын
Koma ineyo olo oyimba onse atatha kufa kumalawi koma dan lu sindingamunene kt ndioyimba komaso iweyo Dan lu kuti uziwe zoti ndi ofoila umati achiyawo saluza iwe apa siunaluze bolaso Sena
Chikangawa km kugwesa ndalama azuse kwacha cnanga akugwesa ndie chitukuko chake sakumukonda kumene ndipo okupha ndi chakwera ndi iweyo galu kaye kunyasa khope iwe mapwala iwe okupha chilima mesa munapha chilima munapha sadiki Mia munapha anthu 9 pa ndege ija chamba eti