Iwe ndi chitsilu bwanji ukuona ngati sakukudziwa ndindani kuti ndiwe u Yudasi musatinyase ndife onyasidwa kale
@ChristianMalingamoyo2 сағат бұрын
Mr mthilakuwiri
@DavidPhiri-o6w2 сағат бұрын
My favorite Vice president USI Chilima anasankha usi anawonapo kanthi
@PollyLysonLutepoСағат бұрын
Nyenga yemweyo. a UTM tsamalani. Pa m'tsonkhano wa UTM ndi Chifukwa Chiani ama ntchura President kawilikawili? Akuonesa komwe Ali. Pempho.=Chonde Chonde Chonde UTM ya Chilima m'tsapite ku m'tsonkhano wa Usi. Ndipo pa Convention m'sayetse kukamulodza Chara kuti akhale nawo pa chisankho. Wakusina khutu ndi nasi.
@TecksonKaima-dr6er2 сағат бұрын
Umuwolotse chakwanayo akakutafune nawenso😅😅😅😅😅
@PempheroAlli-v8yСағат бұрын
Ulibe ntchto iwe thira kuwiri zikutsata thaw ikwana
A vp mudzakhumidwa atawina pano anthu anazindikilatu coz kabambe anthu anadziwa kale kt akufuna adzakhala vp wa Apm nde frim imene anakoza kt athetse utm coz ni chipan champhamvu ndeno ufunika kusamala kwambili osadzavotela kabambe ayi bola manganya omwewu Olo akwen ngat adzaime km wena wa ayi
@EthelKubalasaСағат бұрын
Yudasi uyu ndi spy wa Chakwera tisamukhulupilile, amachita zake osati za athu, ndipo sanali bali ya SKC, ndiye lero wavala SKC. kkk, koma drama sizithu
@gmxplayboy65592 сағат бұрын
Manganya ndi galu kwabasi, uyu ndamene adamugulitsa Chilima kwa adani uyu. Ndipo uyuyu kumupatsa mpata woti akhale President wa UTM mudziwiretu kuti UTM yathera pompo
@alexsumani682334 минут бұрын
Akukukamila ndani iwe iwe olo manyazi ulibe,ma quality a mtsogoleri ulibe usatitayise nthawi
Koditu munthu amangosankha koma samaziwa mtima was munthu, chimodzimoz mene anamuthandizira Chakwera kukhala president koma samamuziwa mtima wake kut ndi wa Chigawenga.
@MarcyKamagaСағат бұрын
zaboza tiye uko Satan's munthu woyipa iwe zowona kuyankhura nkhani yachirima iwe kupusa mkupusisa ndani ndare ya mcp yimeneyo tikukuziwa kare
@MATTHEWSANDREWMANDUTU47 минут бұрын
Kkkkkkk koma ziliko ku UTM awa ndikoyamba kuwava ine kkkkkkkk😂😂😂😂😂😂😂😂lero limenelo inu.
@munikabambe76252 сағат бұрын
Bwana olimbana ndi ma juniors ntchito yake imapakidwa mabi.....
@ElizabethMulinde2 сағат бұрын
Wachedwa manganya ndipo unya unya kupusitsa anthu kumeneko camping ya ku convection
@LongweLeya2 сағат бұрын
Kodi chilimayo anakusankha ali komwe unamuyika kuja ndiwe manyi eni eni ziwa muyeso omwe umamuyesela mzakoyo naweso uzayesedwela ndi omwewo
@FidesChandama2 сағат бұрын
Kodi muli mbali inuyo yathuyi kapena inayo komaso osaiwala izi mwatsala ndi miyezi kuchoka pamene wachiwili adamusankha kale izo zikutsalirani mmanja muzuona
@RAFICKRAHIMUMUSSAHСағат бұрын
Iwe dela lakwathu usazafike tizakugenda ife iwe wamanyi mkhos ngat chitete wava
@HacksonJereСағат бұрын
Koma akuluwapalibe chomwe amalakhumwazelu palibefundo apa
@RometcmaСағат бұрын
Mabatile amanganya chilima wa ambuyako munthu munamupha nde lero utm tsogolo la amako .
@NaomiMagoha-uw7rmСағат бұрын
Afuna akamusankhe ku convention, washera. Palibe kukusankha
@KondwaniBanda-ul8sj2 сағат бұрын
Ine uyu ndimamuwona ngati amaganiza bwino koma aaaaaaha umuthu mulibemo ndipo akuwonetselatu ndi muthu osanva zazake ndizayekha
@JafaliAjusa-zg2xi2 сағат бұрын
Mr usi don't take people like stupid with your chakwela.please you guys step down.Whether a leader should step down after failing to fulfill their promises depends on several factors. Here are some key considerations: 1. Reasons for Failing to Fulfill Promises Leader’s Incompetence: If the leader fails due to a lack of necessary skills, poor decision-making, or failure to manage plans properly, they might be seen as unfit to continue in their role. External Factors: If the failure is due to factors outside the leader's control, like global economic issues, natural disasters, or lack of support from others, it may not necessarily be the leader's fault. 2. Challenges Faced by the Leader Integrity and Effort: If the leader shows integrity, works hard, and is transparent about their challenges, many may still support them even if they haven’t fulfilled their promises. However, if the leader appears negligent or dismissive, trust can be lost. Impact of the Failures: If the unfulfilled promises significantly affect the lives of the people or the development of the organization or country, there is often more pressure for the leader to step down. 3. Opportunities for Correcting Mistakes Adjusting Strategy and Asking for Patience: The leader could introduce new strategies to fix the issues, asking for patience from their followers. If this plan is reasonable and shows potential for success, they may be given another chance. Internal Review or Public Decision: In some cases, there may be a process where the leader's performance is reviewed, either by their peers or through elections. The people can decide whether to give the leader more time or push for them to resign. 4. The Benefits of Resigning Maintaining Dignity: A leader may choose to resign voluntarily if they feel they cannot meet the demands of their role. This can preserve their personal dignity and honor. Restoring Public Trust: Resigning may also help ease public frustration or discontent, especially if the leader’s failures are causing widespread dissatisfaction. 5. Consequences of Resigning Operational Disruptions: A resignation can sometimes lead to instability or confusion within the organization or country, especially if there is no clear plan for a successor. Hope for a New Leader: If the public believes a new leader can perform better, resignation could bring positive change and restore hope. Conclusion: While it might seem reasonable for a leader who fails to deliver on promises to step down, not every failure requires resignation. It depends on the reasons for failure, the leader’s response, and what the public expects. Ultimately, the key issue is whether the leader is still capable of moving the people or organization forward effectively.
@LukiyaAlick32 минут бұрын
Iwe ndi chisilu bwanji pando mangas There manga
@PortiaMhlambi-y4g38 минут бұрын
Tikudikila mukapange masewero ndi amake sikono
@EsetaGerateСағат бұрын
Aaaa ndiwe Garu kwabasi chilima umkamkonda lwe machende ako
@charitykalulu2 сағат бұрын
Nsonkhano wa dziko kapena wachipani? Kambani za UTM zokha apa
@MosesDicostar49 минут бұрын
Chomwe chikupanga ada awa sindkuchiwona
@CarolineLiabunya-j8k56 минут бұрын
Usi ndinkankonda koma pano ndinamutuluka😔
@ernestphiri55072 сағат бұрын
Awanso ndi mabvuto ena palibe chabwino apapa
@WanangwaMfuneСағат бұрын
Lamuro lipotsadi mphamvu et kkkkkkk
@MsondaBanda2 сағат бұрын
Titemwanenge mwanyane tili wamoza pera
@ElizabethMulinde2 сағат бұрын
Ndipo tikaonana ku convection galu iwe
@MATTHEWSANDREWMANDUTU45 минут бұрын
Azimayi a mcp awa komanso aganyu
@MaryTchapo-py4hh4 минут бұрын
1mit awaphuzitsa APM
@MisheckKamwendo-w9nСағат бұрын
Zazi mulikuti athu akudya chiteze
@MandalaChaonaСағат бұрын
Michael Usi respect yourself . Chimuphereni Chilima,iweyo Usi unayankhulapo Kuti Chani. Uzapusa tsiku lako kukubwera, lero usamadzitenge ngati wochenjera. Ngati umamkonda Chilima bwanji isamukakamidza Lazalo yo Kuti Pakhale Commission Of Inquiry. Aaaaa iwe Usi Mapazi ako wa Ng'ona party 🐊🐊⚒️🔨🐊 iwe.
@chisomokapiseni18 минут бұрын
A chairman a NEEF😂😂😂
@MekeShonga28 минут бұрын
Uyu ndi ofoila aaaaa,
@ChikaikoBanda-v2d30 минут бұрын
Zabwino zonse bwana
@FavorChifisi20 минут бұрын
Yomweyo galu iwe
@felixjoseph8161Сағат бұрын
Manganya pa nyini pa mako
@MercyNkhoma-b6h2 сағат бұрын
Bambo a Sikono tsopano
@JoshuaNyirongo2 сағат бұрын
U are there by bad luck
@DixonChimanya27 минут бұрын
Machende ako maganya
@Chikulamayembe57Сағат бұрын
The truth will out!
@FaithGondwemaomba-bz6ntСағат бұрын
Koma ndale hmm
@NEBERTMVULAСағат бұрын
kubwebweta tu uku
@YellowmanMalawi-qe8zh32 минут бұрын
Mbuzi
@elliotchisalanga12Сағат бұрын
Mbwelera
@Edson-sj8vn2 сағат бұрын
Too late
@SanudiMcDonald48 минут бұрын
Ngati umamukonda chilima bwanji omuthandiza mkazi chilima pa zakafukufuku wandege yomwe idapha amuna ake ndi anthu ena aja izi sizoona umaganiza mwakuya osangoti mawu akoma mkazi chilima ali kulira ndi kafukufuku wa amuna wake ndipamene inu mukusangalala mulungu akuyendereni manganya
@SanudiMcDonald48 минут бұрын
Osamuthandinza
@Kiyamachilipa2 сағат бұрын
UTM YAMTHIKO
@IssahBannetСағат бұрын
Akulu inu u VP siukukukhalani bolani tikuf elanji yemeeuja mboloyako unamupereka biyeni galu
@jelsonmlowoka8611Сағат бұрын
Inu bwanji unakupetani 😢
@FredPondamwala2 сағат бұрын
Betrayal
@MicyThobveСағат бұрын
Mau
@FrancisNyayi2 сағат бұрын
😢
@LameckBanda-gk6ri2 сағат бұрын
Manganya akukamba za UTM nde ana akubanja kwa muntharika chikukhudzani ndichiyani zipangani za mkharamba yanu yopanda manoyo zoyakhura zosaveka,kumango bwebweta basi