Mafunso ake ATI amalephera kuyankha o ha ha ha ha ha
@stevechikaonda3145Ай бұрын
Tinene kuti wopaanda nzeru nduyu walemba kuti atolankhani anapanikiza Kalindo, coz he has been consistent and confident in his responses to the posed or you just wanted to lure us and watch this
In fact chilungamo chake anayenera kuti adzigula sticker ndi amene wagwidwa atazemba pa boarder. Wokhulupirika apatsidwe sticker yaulele, wozemba akapezeka agule sticker ngati mbali imodzi ya chindapusa.
@alexmakwangwala1615Ай бұрын
Iwe nde Munthu 🔥🔥🔥
@lyiemanganjira9708Ай бұрын
The DC woyeeeeee 🎉🎉🎉🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥
@KingfrahMachadoАй бұрын
Akapusa mwezi sivuto end President aziter kuyakha mopanda mantha💪💪💪🔥
@user-re7fo3be2zАй бұрын
We love you Mr DC
@CharityGondwe-bw9gsАй бұрын
Mumatiimilira mr kalindo ndi azanuwo murandire ulemu❤❤❤❤❤❤❤
@InnocentMtafyaАй бұрын
Musaiwale atamupatsa u ambassador kupita kunja, anazasanduka munthu wina nkumati a Malawi sioafela koma makobidi nde dilu, mwaiwala, eti anapepesa...🤔🤔mmmhhh!(Ndalamaa eeeh!!!!)
@SteveniBandaАй бұрын
Kkkkk go ko nko sambe madzi achitedze basi 😂😂😂 😂😂😂 kalindo umakwana
@SteveniBandaАй бұрын
Osadanda tililimozi ati u ze 💪💪💪🔨🪓🗡️ bwino zatikwana
@user-ik5sz8hc6fАй бұрын
Bon .you are very intelligent gentlemen. Iam behind you❤❤❤❤❤
The DC🔥🔥🔥🔥🔥🔥MRA sikuganizira ife ochita malonga...in add off kubweretsa sticker ndi njira imodxi yofuna kusokoneza ife a business kuti tisamapindule ...Boma lionepo bwino apa....
@PetroGondweАй бұрын
Kalindo is a true light to Malawian paths.youths wake up please,osamangovina amapiano fight for your nation and your future.
@aubreyvisuals2416Ай бұрын
Kkkkkkk ati amapiano 😅
@daviebanda5098Ай бұрын
Kkk akut amathamanga ndimasuti😂😂😂😂 booom the DC🔥🔥🔥
@AronZayawehАй бұрын
Masiku atha kale awaa chakwela abwelele kudambw
@UssenNjirinahАй бұрын
Kkkkkk mpaka pele ajawuleje kudambwe Kwene chinyago changatama ku state house chijaule kwawo kwawo kudambwe
@user-dl4ud7mp4nАй бұрын
😂😂😂😂😂
@user-fd1tu6ku1rАй бұрын
Mr Chikangawa akutitola kwambiri
@PatYønaАй бұрын
Yesterday I saw achinyamata akulemba anthu a kwa tongole in area24, ndinafusa modzi wa Iwo anati atumidwa kuti alembe anthu osati obwera but amagazi ... Kuti adzilandira ntukula pakhomo every month and fertilizer. But onse ogula malo ayi asamulembe. Is this fair abale inuuuu 😢😢😢
@PastinaHopeАй бұрын
Tikuthoza kwambir a bon karindu pa zime mpatipangira ife osauka mulungu akhare ND Inu nose ❤❤🎉
Kumpoto kumwera tikuoneka ngati sindife amalawi. Koma achigawo chapakati ndi a Malawian. Kumupoto kulibe chilichose i love you Mr DC and your members mademo alhalepo tikufuna chilungamo si nkhondo koma kukoza ziko lathu
@JonathanHeadsonАй бұрын
Mafunso akeso ati ovutawo nanu
@thulanimpphiri6873Ай бұрын
Kuchokera 2020 mupaka pano chimene tapidula ndibomali kukumangidwa boza kulankhula mozikona kulekerera muchitidwe wa katangale kulembana pamutundu ntchito kuononga immigration kuononga ACB kuononga admac kuononga apolice kuononga nkhalango ya chikangawo po gwesako ndege kuononga nrb kuononga chipani cha utm kusunga nduna zachiwewe muchipani zopanda phindu. Ndizina zambiri zaonongeka kumalawi ndichitukuko chimene talandila kumalawi for 4years mmmm
@kingsleyhopematchaya5184Ай бұрын
Stima yayamba kubweretsa mafuta sidaone
@isaacthawani5442Ай бұрын
Ndie awa akut mafuso ovuta mene akuyakhiramo sukuona kt dola ndi kalindoyo mbuzi iwe
@FloridaMakwinja-eq2ekАй бұрын
The DC moto wokhawokha
@ClementKawinga-ik7wnАй бұрын
Chakwera bomaaaaaaaa palibenso amene ndikumuona basi ndi Lazarus
@DonPhiri-u2jАй бұрын
Ife tikungodikira mulungu atithandize coz ulosi wa malemu grace chinga unanena kale kuli kuti kukubwera chipani cholimbana ndi mwazi komaso thukuta kma mukamaliza zonsezi muziwe kuti mulungu achitapo mbali yake ife tikuyembekeza pamulungu osati munthu amen