MAFUNSO OVUTA OMWE ATOLANKHANI ANAWAPANIKIZA NAWO A BON KALINDO LERO PAMENE AMACHITITSA CONFERENCE

  Рет қаралды 90,801

Makosana

Makosana

Күн бұрын

Пікірлер: 358
@AiameAdamo-su1nt
@AiameAdamo-su1nt Ай бұрын
Kuyankha mafunso mosanyengelela munthu the DC😂😂😂.
@PropeeLucious
@PropeeLucious Ай бұрын
Mafunso ake ATI amalephera kuyankha o ha ha ha ha ha
@stevechikaonda3145
@stevechikaonda3145 Ай бұрын
Tinene kuti wopaanda nzeru nduyu walemba kuti atolankhani anapanikiza Kalindo, coz he has been consistent and confident in his responses to the posed or you just wanted to lure us and watch this
@edsongeorge8032
@edsongeorge8032 Ай бұрын
nkhaniyi ndiyoona malume opanda nzeru ndamene walemba izi.
@macrinenduna1024
@macrinenduna1024 Ай бұрын
Pamenepa mukati atolonkhani anapanikiza mafinso, ndifunso liti lajejemetse Malawi Fist?
@user-vt4zo7eo2s
@user-vt4zo7eo2s Ай бұрын
Ineso sindikupeza olo limodzi
@user-hm9nc7lz6e
@user-hm9nc7lz6e Ай бұрын
Palibe malawi first number one
@MarkJere-c2d
@MarkJere-c2d Ай бұрын
Njila imodzi yofuna kut muonele kaaaa kkkk
@user-zy1eh3pt8v
@user-zy1eh3pt8v Ай бұрын
I had the same question 😂😂😂😂
@edsongeorge8032
@edsongeorge8032 Ай бұрын
@@user-zy1eh3pt8v inenso I wanted to ask kuti ndipati pomwe Bon kalindo ?
@danielmurichi5673
@danielmurichi5673 Ай бұрын
Anyamata wa ali serious bwino kwambiri Keep it up osagonja ndipo boma limeneli lisamale osama one ngati malawi ndiiwowokhawo nafeso ndi malawi Pasafe olo mmodzi panewa kuteloko nkhondo idzayamboka chifukwa nthawi tiliyi ndiya democracy Tikufuna ufulu oyankhula osati kuopsezedwa
@user-sb2mw3xz4j
@user-sb2mw3xz4j Ай бұрын
😂😂😂Koma KALINDO eish big respect,
@KingfrahMachado
@KingfrahMachado Ай бұрын
Ndipo inu a bon mulungu aziwe pachilungamo chimene mukuonesa kwaife amalawi osauka❤
@TEACHTHEWORDMINISTRIESINTERNAT
@TEACHTHEWORDMINISTRIESINTERNAT Ай бұрын
In fact chilungamo chake anayenera kuti adzigula sticker ndi amene wagwidwa atazemba pa boarder. Wokhulupirika apatsidwe sticker yaulele, wozemba akapezeka agule sticker ngati mbali imodzi ya chindapusa.
@alexmakwangwala1615
@alexmakwangwala1615 Ай бұрын
Iwe nde Munthu 🔥🔥🔥
@lyiemanganjira9708
@lyiemanganjira9708 Ай бұрын
The DC woyeeeeee 🎉🎉🎉🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥
@KingfrahMachado
@KingfrahMachado Ай бұрын
Akapusa mwezi sivuto end President aziter kuyakha mopanda mantha💪💪💪🔥
@user-re7fo3be2z
@user-re7fo3be2z Ай бұрын
We love you Mr DC
@CharityGondwe-bw9gs
@CharityGondwe-bw9gs Ай бұрын
Mumatiimilira mr kalindo ndi azanuwo murandire ulemu❤❤❤❤❤❤❤
@InnocentMtafya
@InnocentMtafya Ай бұрын
Musaiwale atamupatsa u ambassador kupita kunja, anazasanduka munthu wina nkumati a Malawi sioafela koma makobidi nde dilu, mwaiwala, eti anapepesa...🤔🤔mmmhhh!(Ndalamaa eeeh!!!!)
@SteveniBanda
@SteveniBanda Ай бұрын
Kkkkk go ko nko sambe madzi achitedze basi 😂😂😂 😂😂😂 kalindo umakwana
@SteveniBanda
@SteveniBanda Ай бұрын
Osadanda tililimozi ati u ze 💪💪💪🔨🪓🗡️ bwino zatikwana
@user-ik5sz8hc6f
@user-ik5sz8hc6f Ай бұрын
Bon .you are very intelligent gentlemen. Iam behind you❤❤❤❤❤
@BenedictFriday-c2w
@BenedictFriday-c2w 24 күн бұрын
The DC keep it up the good work
@DollarChagamba
@DollarChagamba Ай бұрын
Palibe fuso lomwe lawakanika kuyankha
@user-bi5lg8mg9y
@user-bi5lg8mg9y Ай бұрын
Mr Bon kalindo z very strong weapon speech
@StanleyDama
@StanleyDama Ай бұрын
Do y know the meaning of weapon ?
@SteveniBanda
@SteveniBanda Ай бұрын
❤❤❤ 1277 kkkkkk
@SteveniBanda
@SteveniBanda Ай бұрын
Gwira chito kalindo 😂😂😂😂 kuswa kuswa kung'alura kung'alura😂😂 tiyenawo osawasiya😂😂
@ChipanganoPhiri
@ChipanganoPhiri 24 күн бұрын
Big boss
@user-rb7mp3rv7g
@user-rb7mp3rv7g Ай бұрын
Pamenepa mafunso ovuta alipati please ma topic anuwa tamaonani Kaye aaaa😂😂
@martinndawala8125
@martinndawala8125 Ай бұрын
Amangofuna anthu akhale ndi chidwi chowonera 😂😂
@HanishKenneth
@HanishKenneth Ай бұрын
Kutchaya kugwetsa we are united
@ChimwemweBottomani-hc5ju
@ChimwemweBottomani-hc5ju Ай бұрын
The DC🔥🔥🔥🔥🔥🔥MRA sikuganizira ife ochita malonga...in add off kubweretsa sticker ndi njira imodxi yofuna kusokoneza ife a business kuti tisamapindule ...Boma lionepo bwino apa....
@PetroGondwe
@PetroGondwe Ай бұрын
Kalindo is a true light to Malawian paths.youths wake up please,osamangovina amapiano fight for your nation and your future.
@aubreyvisuals2416
@aubreyvisuals2416 Ай бұрын
Kkkkkkk ati amapiano 😅
@daviebanda5098
@daviebanda5098 Ай бұрын
Kkk akut amathamanga ndimasuti😂😂😂😂 booom the DC🔥🔥🔥
@AronZayaweh
@AronZayaweh Ай бұрын
Masiku atha kale awaa chakwela abwelele kudambw
@UssenNjirinah
@UssenNjirinah Ай бұрын
Kkkkkk mpaka pele ajawuleje kudambwe Kwene chinyago changatama ku state house chijaule kwawo kwawo kudambwe
@user-dl4ud7mp4n
@user-dl4ud7mp4n Ай бұрын
😂😂😂😂😂
@user-fd1tu6ku1r
@user-fd1tu6ku1r Ай бұрын
Mr Chikangawa akutitola kwambiri
@PatYøna
@PatYøna Ай бұрын
Yesterday I saw achinyamata akulemba anthu a kwa tongole in area24, ndinafusa modzi wa Iwo anati atumidwa kuti alembe anthu osati obwera but amagazi ... Kuti adzilandira ntukula pakhomo every month and fertilizer. But onse ogula malo ayi asamulembe. Is this fair abale inuuuu 😢😢😢
@PastinaHope
@PastinaHope Ай бұрын
Tikuthoza kwambir a bon karindu pa zime mpatipangira ife osauka mulungu akhare ND Inu nose ❤❤🎉
@FrancisMbwana-z5l
@FrancisMbwana-z5l 29 күн бұрын
Very powerful from kalindo
@DysonChiumia
@DysonChiumia Ай бұрын
The DC🔥
@abdulsalammkwepu3321
@abdulsalammkwepu3321 Ай бұрын
The DC🔥🔥🔥🔥
@EffordKapichi
@EffordKapichi Ай бұрын
You are our weapon chief
@user-ee1ci2ku6o
@user-ee1ci2ku6o Ай бұрын
We are frant of you mr kalindo DC 💪💪💪💪
@KimuIbrahim
@KimuIbrahim Ай бұрын
Kalindo woye
@InnocentEdasi
@InnocentEdasi Ай бұрын
Kalindo ndinkamuna ogona kukhomo kosachinjika abro 🔥🔥🔥🔥 Yehova apilile kumusunga ndimoyo wautali
@YamikanipilatoPilato
@YamikanipilatoPilato Ай бұрын
Number one chi dc
@BlessingsNyirenda-ru7ss
@BlessingsNyirenda-ru7ss Ай бұрын
More fire born kalindo
@williammasiano1194
@williammasiano1194 Ай бұрын
Viva Malawi 1st ...eish anthu amafika potopa
@emmanuelmuyilaa
@emmanuelmuyilaa Ай бұрын
Koma kumeneko❤
@thulanimpphiri6873
@thulanimpphiri6873 Ай бұрын
Kumpoto kumwera tikuoneka ngati sindife amalawi. Koma achigawo chapakati ndi a Malawian. Kumupoto kulibe chilichose i love you Mr DC and your members mademo alhalepo tikufuna chilungamo si nkhondo koma kukoza ziko lathu
@JonathanHeadson
@JonathanHeadson Ай бұрын
Mafunso akeso ati ovutawo nanu
@thulanimpphiri6873
@thulanimpphiri6873 Ай бұрын
Kuchokera 2020 mupaka pano chimene tapidula ndibomali kukumangidwa boza kulankhula mozikona kulekerera muchitidwe wa katangale kulembana pamutundu ntchito kuononga immigration kuononga ACB kuononga admac kuononga apolice kuononga nkhalango ya chikangawo po gwesako ndege kuononga nrb kuononga chipani cha utm kusunga nduna zachiwewe muchipani zopanda phindu. Ndizina zambiri zaonongeka kumalawi ndichitukuko chimene talandila kumalawi for 4years mmmm
@kingsleyhopematchaya5184
@kingsleyhopematchaya5184 Ай бұрын
Stima yayamba kubweretsa mafuta sidaone
@isaacthawani5442
@isaacthawani5442 Ай бұрын
Ndie awa akut mafuso ovuta mene akuyakhiramo sukuona kt dola ndi kalindoyo mbuzi iwe
@FloridaMakwinja-eq2ek
@FloridaMakwinja-eq2ek Ай бұрын
The DC moto wokhawokha
@ClementKawinga-ik7wn
@ClementKawinga-ik7wn Ай бұрын
Chakwera bomaaaaaaaa palibenso amene ndikumuona basi ndi Lazarus
@DonPhiri-u2j
@DonPhiri-u2j Ай бұрын
Ife tikungodikira mulungu atithandize coz ulosi wa malemu grace chinga unanena kale kuli kuti kukubwera chipani cholimbana ndi mwazi komaso thukuta kma mukamaliza zonsezi muziwe kuti mulungu achitapo mbali yake ife tikuyembekeza pamulungu osati munthu amen
@PeturosiNyirenda
@PeturosiNyirenda Ай бұрын
😂 bon kalinda nd 1🎉
@PropeeLucious
@PropeeLucious Ай бұрын
Ndati ndikuuze I kuti bon kalindo akupusisani eye ndi ganyu imeneyi please please achinyamata musamangotenga ndizina zili zonse mtambo anakunamizan pano ndi bon kalindo please changamuka achinyamata mmalo mosaka ndalama kuti moyo wanu usithe muli busy kuchemelera munthu wina mmmmmmm
@SalaJawali
@SalaJawali Ай бұрын
Utiuza zopusa zo ife tilibe Maso owonela kuti dziko muno zinthu sizilibwino
@robenallie6985
@robenallie6985 Ай бұрын
Iwe ndi wa mcp
@SharonNdadza
@SharonNdadza Ай бұрын
Nawe akupasa a mcp ndrama? Chonsechonso azimbuyanu akuvutika mma midzi uko
@PropeeLucious
@PropeeLucious Ай бұрын
@@SharonNdadza ndye zoyankhula za kalindo zipangisa kuti ambuye asavutike mmmmmmm mbuli za kalindo muzafa chifukwa chosatilq zinthu zopusa ngt zimenezo
@PropeeLucious
@PropeeLucious Ай бұрын
@@SalaJawali iwe ndye kalindo ndi amene angasithe zinthu musanamizidwe kuti kape ngt amene uja palibe chimene angaphule
@ChifundoZimba-jh7dh
@ChifundoZimba-jh7dh Ай бұрын
Kalindo ndi wa DDP chonde a Malawi musapuse naye akudya ndalama za peter anapatsidwa target
@SharonNdadza
@SharonNdadza Ай бұрын
Muli ndi umboni?
@MadalitsoChipangula-i3z
@MadalitsoChipangula-i3z Ай бұрын
Mwana uvuta kwambiri the Dc zimenezi ndizo zofunika kwambiri kunokwanthu kumalawi
@stevenbanda6665
@stevenbanda6665 Ай бұрын
More fire bon
@jamessingini-fh1bz
@jamessingini-fh1bz Ай бұрын
I cant wait pa 8 August ,bravo team Dc❤
@JohnBanda-ux9fy
@JohnBanda-ux9fy Ай бұрын
The DC ❤❤
@ChikondiMaguza
@ChikondiMaguza Ай бұрын
Am coming to join u guyz❤
@TachikoMwanamanga
@TachikoMwanamanga Ай бұрын
The DC 🔥🔥❤️
@PeterChilombo-ou2cd
@PeterChilombo-ou2cd Ай бұрын
zoonadi atipeza kale kuno 25
@OMEXTWAIBU
@OMEXTWAIBU Ай бұрын
Chakwela my vote ❤
@HiAlvin
@HiAlvin Ай бұрын
DC awavula Ngati anadya ndalama akabweze alephera kufusa
@RasLuntha
@RasLuntha 28 күн бұрын
We must fight for our rebarty and freedom
@mkupabanda-nd2vb
@mkupabanda-nd2vb Ай бұрын
Mafunso onse ayankhidwa, what else do u want?
@TanazioUziyele
@TanazioUziyele Ай бұрын
Aaa akalindo ndale
@Atheeeefire
@Atheeeefire Ай бұрын
Respect the DC keep the fire burning
@user-eo2hl9ug1h
@user-eo2hl9ug1h Ай бұрын
Muyende..bwino...Isha. Allah
@COSMASSDAVITY
@COSMASSDAVITY Ай бұрын
D.C MWANA OVUTA NDIWE NYO😂❤
@MercyJohnsonkanchure
@MercyJohnsonkanchure Ай бұрын
Mr DC ulemu wanu kuti yimilira Amalawi
@evalisterphiri8435
@evalisterphiri8435 Ай бұрын
This is true, ma profit ndiochepa kale koma BOMA ili palipose utulutse ndalama and now this mmm.... Mademo akufunikadi
@user-ik5sz8hc6f
@user-ik5sz8hc6f Ай бұрын
Komano bon kalindo wawayankha bwino.Lopanda nzeru ndiboma ndiutsogoleri omwe ulipoli.Pa 8 go konko
@user-sm4vo2uo7g
@user-sm4vo2uo7g Ай бұрын
The dc mwana wachabe
@DanJohn-ws5gl
@DanJohn-ws5gl Ай бұрын
Mbambande the DC
@user-oe3dz7dy4j
@user-oe3dz7dy4j Ай бұрын
Zoona amacharger ndarama popereka chidindo,,, your true fighter kalindo
@BeckhamDavid-v6c
@BeckhamDavid-v6c Ай бұрын
Born kalindo respect big up
@KennedyPhiri-h9h
@KennedyPhiri-h9h Ай бұрын
Ife tikudikila pa 8 pano ✊💪✊
@serakillo8668
@serakillo8668 Ай бұрын
Born ❤❤❤ ndi one guys timakufirani abro❤❤❤
@MagunjeNewa
@MagunjeNewa Ай бұрын
Mr Born kalindo hoyeee
@user-ri8em6my2e
@user-ri8em6my2e Ай бұрын
Bon tiwomboleni asatana amenewa asatibere chonde 😭😭
@user-pe2tu1ip3v
@user-pe2tu1ip3v Ай бұрын
Good news ❤good work
@WillmotChiuimia-vr6ou
@WillmotChiuimia-vr6ou Ай бұрын
Yes , kuyankha kwabwino ndinthu mmm ndikanapanga nawo mademo amenewo yes yes
@user-dk6yc8pl2m
@user-dk6yc8pl2m Ай бұрын
The DC ❤❤❤❤❤
@user-eh1mg3ww6d
@user-eh1mg3ww6d Ай бұрын
Mulungu akusungeni ndi moyo gays wina aliyese ukumba zenje pa inuyo agwelemo yekha mudzina la yesu
@RobertChisenga-ci2mq
@RobertChisenga-ci2mq Ай бұрын
I wish bon kalindo azakhere minister of the land Kaya zikhare ng,oma mai yolam kukuyu Azakhara mwaufumu muno kaya.
@heartilygarven2624
@heartilygarven2624 Ай бұрын
Ulemu wanu Mr DC kuyankha mopanda nkhawa
@estherkachingwe3605
@estherkachingwe3605 Ай бұрын
God bless you Mr Bon kalindo
@PeterChuma-jr1vz
@PeterChuma-jr1vz Ай бұрын
Atolankhani agonja kunooo kkkk kuyankha mosaopa
@AgnessKavalo
@AgnessKavalo Ай бұрын
Kkkk komatu bon kalindo amathamanga ali mu suit 😂😂😂😂😂😂😂 koma mdaseka mokweza mau 😂😂😂
@KennedyPhiri-h9h
@KennedyPhiri-h9h Ай бұрын
The DC president wa anthu osawuka 💪✊ we always with you
@smartselemani2070
@smartselemani2070 Ай бұрын
Sweet talk with hidden agenda.
@InnocentMtafya
@InnocentMtafya Ай бұрын
Ambwiyee !!! Mafunso afunsidwa ndimayembekezela zachabe ,koma ambwiyeee!!!
@GiftSoko-w4h
@GiftSoko-w4h Ай бұрын
KATUNDU BOOOOOOOOON KALIIIIIIINDOOOOOOOOO LOVE YOU MY GUY
@GladsonBanda-m3e
@GladsonBanda-m3e Ай бұрын
Apresitent chamba chilitho nkumati tikuimira anthu kumangadi zingongo you should read as an example kalindo
@Littlefair7
@Littlefair7 Ай бұрын
Atolankhani aku malawi ndi mbola, amafunsa zopepera kwambiri. Utolankhani weni weni unapita ndi achina Eunice Chipangula osati izi zathovwa.
@Agin2pex-ms3di
@Agin2pex-ms3di Ай бұрын
Buka matevu 🎉
@IanAllstal
@IanAllstal Ай бұрын
Kodi kalindo umkachedwa ndi ma drama chifukwa chani? The D C 🔥🔥🔥
@macksonmkandawire5718
@macksonmkandawire5718 10 күн бұрын
Bon kalindo kkkk make ndi vice president sopano
@user-ii6lu1wy5f
@user-ii6lu1wy5f Ай бұрын
We are with you Mr DC
@GreenBadani
@GreenBadani Ай бұрын
💪👍💞
@innocentmusuli7380
@innocentmusuli7380 Ай бұрын
Mongo bwereza zomwe ndakhala ndikunena kuti any time, any day, any week, any month from now achinyamata azuka ndikuchosa nyasi zonse belive this
@MaloneBanda
@MaloneBanda Ай бұрын
Good work 💥💥💥💥
@ChifundoZimba-jh7dh
@ChifundoZimba-jh7dh Ай бұрын
Akalindo ayaluka mademowo kumwela Koko
@user-rk4ch1ly3z
@user-rk4ch1ly3z Ай бұрын
Achina kalindo ndiakamuna osati masewela.
@isaacharoon5652
@isaacharoon5652 Ай бұрын
Kalindo akuchita bwino,komano kwa anthu amene amaononga zinthu za anthu,inuyo a kalindo anthuo muzawalipila,chifukwa anthu akuba amalowelela.simutisaukisaaaaaa?
@ziyamporoma377
@ziyamporoma377 Ай бұрын
Chokani apa inu mulibe strategy iliyonse other than mademo. Don’t worry tikakufinyani konko
@MarthaBango
@MarthaBango Ай бұрын
😂😂😂😂😂iiIi ati masuti kothamanga😂😂
@DoulassSamuel
@DoulassSamuel Ай бұрын
Iweyo born ukungofuna udindo usatinyasepoapa
@LucyTatianahChikwekwe
@LucyTatianahChikwekwe Ай бұрын
More fire 🔥🔥🔥 the DC
@TANMBWANA
@TANMBWANA Ай бұрын
Mr chikangawa zawavuta
@PrinceBlessings-bv5bs
@PrinceBlessings-bv5bs Ай бұрын
Dc 🔥🔥🔥
@MarthaMalopa-kw9xw
@MarthaMalopa-kw9xw Ай бұрын
Pali funso lomwe lalepheredwa kuyankhidwa apa?
هذه الحلوى قد تقتلني 😱🍬
00:22
Cool Tool SHORTS Arabic
Рет қаралды 93 МЛН
王子原来是假正经#艾莎
00:39
在逃的公主
Рет қаралды 26 МЛН
Dad gives best memory keeper
01:00
Justin Flom
Рет қаралды 20 МЛН
KANDIMVELERE....KUFUKULA NKHANI  ZIKULUZIKULU .....TAMVANI NKHAN ZOMWEZAVUTA
30:49
ACHAKWERA KU DOWA PA MTENGO WANTHENGA 🤔🤔🤔
17:04
HOT 265
Рет қаралды 61 М.
EXCLUSIVE INTERVIEW WITH BON KALINDO
59:52
Zodiak Malawi
Рет қаралды 86 М.