Zaululika zoti Chakwera Ndi anzake Ndi amene udamverana Chilima pamodzi ndi Wanthu wena aja Ndipo ada Chita kuwa wombera komanso Mowa maliza Ndi chikwanje, Utsi Ndi amene waphesa Chilima, Ndipo Utsi Ndi Yudasi, panopa nso osamati ndenge idagwa ayi,koma ndenge idagwesedwa Ndi magnet Ndipo m'maiko akunja aulusa Kale koma Ku Malawi ko sada lengeze Chifukwa chiyani? MCP and Chakwera Must go
@IbrahimUseni-p8f2 ай бұрын
No coment
@MphatsoMhoney-xn2ft2 ай бұрын
Koma a nsukuluzi muli mwara kwambili keep it up guys
@ChrissMatchadoeddie2 ай бұрын
❤
@JuliusNyirenda-ec1eo2 ай бұрын
Wonder and Jonah inu ndi machine
@BillyMhone-jp3kn2 ай бұрын
Amalawi ambirife sitikudziwa komwe tikupita honestly..kubwelera kwa pitala ndi corruption thooooo Chakwera ndi uyuuuu akugona nduna kumangoba ndalama ..we lost our directory
@petertaulo80142 ай бұрын
Anyamata aku times mwayamba ku kula mimbatu ngati Ken Zikhale ng'oma. Amenewa mapwevupwevu!
@MuyaoComedies2 ай бұрын
Am following
@AlexKamowa-u7m2 ай бұрын
Zamaudondo kubanja la chilima awasiye
@OmegaChingamuka2 ай бұрын
Inuyo mumatha 👏👏
@MissiPhiri-h3w2 ай бұрын
ndimati ndifuseko kodi ku America kuribe dothi ngati laku malawi ngati kuridothi ndekuti malawi ndi dziko rochititsa manyazi mulungu amati nseka kuti anthu aku malawi ndi dzinyama wosati athu
@KennedyPhiri-h9h2 ай бұрын
Ndikuwona amalawi tingokhala ndi DPP Bolani dppp kusiyana ndi izi manyi yeniyeni chakwela 😢
@GraceZumazuma2 ай бұрын
Utm ikamudalira usi ngat president chipani chifa chifukwa usi akuoneka kuti cholinga chake ndichosokoneza utm pofuna kusapota chakwera alibe vision ngati ya a chilima bola kabambe uja akhoza kuchimanga chipani
@AlexKamowa-u7m2 ай бұрын
Maradio akumalawi sanenachilungamo ndima TV omwe ndiamantha
@ChrisjuZiyaya2 ай бұрын
Takambani za nyasi zomwe zikuchitika m'boma osati kulimbana ndi utm Inu mwatani Kodi???
@steeziomfune66112 ай бұрын
Dr skc was UTM and he is gone...UTM is finished...ndanena ndanena
@DjshukulanGift2 ай бұрын
Uwusi ndi chipan cha thiko ,nden akaliyat ndi achipan cha achilima marem ,osat gwenembey
@CaristoMatimba2 ай бұрын
Koma Ngati olemekezeka ausiwo anapasidwa u vice President ndi a malemu a achilima.nde mumafuna a usi Akane udindowu or bwanji?