Mangochi-Nyama ya Nkhumba scandal

  Рет қаралды 38,489

Enock Bwanali

7 жыл бұрын

When a business man is caught selling pork meat among the majority muslims who regards it as unclean. The fall out catch through a camera. 2013 production

Пікірлер: 77
@rhinowilliam8578
@rhinowilliam8578 4 жыл бұрын
Kodi anthu awa amadzikonda bwanji
@veronicanyanda7066
@veronicanyanda7066 7 жыл бұрын
kudzikonda koma kusetera manja aliyese Ali ndi ufulu wake ngat zimenezo mupeze dziko lanu
@ireenbwanali5456
@ireenbwanali5456 7 жыл бұрын
Veronica Nyanda Kkkkkkkk koma ndaseka
@Emmanuelsalifu-lc1rm
@Emmanuelsalifu-lc1rm 3 ай бұрын
Manyi ako ase
@victorbanda9039
@victorbanda9039 5 ай бұрын
Thats why akukuphwanyani ku gaza kuja asilamu anthu oipa kwambiri inu
@erickunkeani4726
@erickunkeani4726 5 жыл бұрын
Ndezafodyatu mulibe zochita eti... Kaye nkhumba kukoma... Asa makape inu..... Haramu ikhale nkhumba basi??
@fostetfostet900
@fostetfostet900 Жыл бұрын
Umbuli kodi asilamu mumalanda akazi a enaache kwa mulungu sinchimo kumapha anthu sinchimo dziko lapasi nkhondo zimachitika ndi asilamu kukangana ndi a christu mbuli zeni zeni Muhammad si mulungu kodi analenga nkhumba ndi mulungu not Muhammad
@josephineringstone7489
@josephineringstone7489 Жыл бұрын
Ndiye Kuti Mulungu analakwa kulenga nkhumba bvuto umbuli umene ukupangisa...akulimbana ndi namalenga chifukwa ndiamene analenga zonse zamoyo
@DanMhone-iw6xg
@DanMhone-iw6xg 5 ай бұрын
Yakula nd musanje
@yamiechikhola6705
@yamiechikhola6705 5 жыл бұрын
Asalamu asamaxitenge ngati kut dziko ndilawo aliyese alindimakondamakonda
@hassanjameskananjiekananji3736
@hassanjameskananjiekananji3736 3 жыл бұрын
Choka iwe
@Emmanuelsalifu-lc1rm
@Emmanuelsalifu-lc1rm 3 ай бұрын
Wawusilud ameneyo
@lewisbonongwe8518
@lewisbonongwe8518 Жыл бұрын
😂😂😂😂😂 mademo a mijomba anakaziwa kuti muli madyo mu ngumba
@YasiduPemba
@YasiduPemba 2 ай бұрын
Ndine khristu koma nkhumba kumpingo kwathu amaletsa kudya detronomo 14 vs 8
@ThumbikoChipofya-gq7sd
@ThumbikoChipofya-gq7sd 6 ай бұрын
Mowa ukugulitsidwa kumangochi si Haram? Nanga bwanji nkhumba ikuvuta alipo anakakamizidwa wa chisilamu kudyetsedwa ,Umbuli ndiye vuto APA.
@user-yi1cm6yl8i
@user-yi1cm6yl8i 6 ай бұрын
Asilam ndinu olakwa Kodi musikayambili tsamagulitsa nyama yakhumba metsa Muthu umasiya kugula mwaganidza bwanji Kodi mumene dzithu dzavutilamu kumalawi mubwedzeleni ndalama yakhe komatso kumangochiko kulibe ankhilititu?
@chimenyatvanganga8032
@chimenyatvanganga8032 Жыл бұрын
Mashaalah
@josephineringstone7489
@josephineringstone7489 Жыл бұрын
Ngakhale kuno Ku south Africa mashop ndiyambili ofuna amagula ngati sumadya umasiya koma zopusa zanuzo aaaaa chamba kwambiri
@Slyvia-uu3wc
@Slyvia-uu3wc 5 ай бұрын
Zisilu za anthu khumbayo mumadya kuno ku joni,, mbuli, chimidzi kwambili tayendani muwone agalu
@Emmanuelsalifu-lc1rm
@Emmanuelsalifu-lc1rm 3 ай бұрын
Iweso manyi ako
@lewisbonongwe8518
@lewisbonongwe8518 Жыл бұрын
Nkhumba ndi ntchimo koma chigololo ayi mmmm koma chipembezo ichi ndiye kaya Muhammad mwini wakeyo ankadya nkhumba
@Emmanuelsalifu-lc1rm
@Emmanuelsalifu-lc1rm 3 ай бұрын
Ase manyi ako
@fostetfostet900
@fostetfostet900 Жыл бұрын
Ine ndimakhala ku Newlands (JURBERG)pamalopo pali chisilamu wokha wokha koma za uchisuru zokhazokha achehe kumasintha azimayi anzizawo ankandifusa why you r eating pork? naneso ndimafusa bwanji iwe kumasintha azimayi komaso umanyenga akhazi a ena ache ? Abale zose akziwa mulungu no judgement pa dziko lapasi mu christu or musilamu tose ndife ana amulungu
@VeronicaGoliath-yg8vy
@VeronicaGoliath-yg8vy 6 ай бұрын
Sizoona kuletsana kupanga business Malawi ndi dziko la aliyense not asilamu okha be serious guys
@tingoalex6370
@tingoalex6370 Жыл бұрын
Ine singasiye mkhumba kudya ku mangochi kutitso
@twahayusuf2384
@twahayusuf2384 7 жыл бұрын
mashaallah
@enockbwanali9472
@enockbwanali9472 7 жыл бұрын
lets keep on watching these videos.
@lewisbonongwe8518
@lewisbonongwe8518 Жыл бұрын
Dziko ndi la aliyense ili palibe ulamuliro wa ntundu umozi
@patrickmchemo6804
@patrickmchemo6804 5 жыл бұрын
Inu ndi zitsilu za anthu Kodi mukumalitenga dziko la Malawi ngati ndi lanu.komatu zomwe mukupanga inu asilamu tsiku lina anthu Malawi tizanthamanga
@edisonnyasulu9568
@edisonnyasulu9568 5 жыл бұрын
Asilamu ndi zigewenga malingana ndi zikhulupilo chawo maiko ambiri anthu akuphedwa ndi asilamu mukawone boko halam shababu.
@macleanmachamo
@macleanmachamo 2 ай бұрын
I blame government
@erickunkeani4726
@erickunkeani4726 5 жыл бұрын
Mbuli inu
@alexanderkaunda9554
@alexanderkaunda9554 3 жыл бұрын
Pachichewa-kukwedza-mau-pachizungu-kuliziiiiiiii
@esmielaja2536
@esmielaja2536 7 жыл бұрын
kkkkk odiii ukooooooo!!!
@alexanderkaunda9554
@alexanderkaunda9554 3 жыл бұрын
Kkkkkk msilamu-samavachizungu
@mcmillanalexlmanda5051
@mcmillanalexlmanda5051 7 жыл бұрын
wawa
@ThumbikoChipofya-gq7sd
@ThumbikoChipofya-gq7sd 10 ай бұрын
Ndiye akut walakwa kugulitsa nkhumba? Wolakwitsa ndi otayawo chifukwa ogulitsayo sadawakakamize ,kodi kumaboma ena asilimu kulibe nanga nkhumba imadibwa bwanji?_Nanga amene amadya sakuwaphera ufulu? Vuto ndi umbuli by the way Malawi is a secular state kod Mangochi ndi state payokha
@daudlester1286
@daudlester1286 7 жыл бұрын
sukulu ndi chipembezo ndi zithu zoxiyana mbuli ndi iwe chifukwa ukutukwana bcz unapita m crass koma ulibe mtnchito usauka ngati ine
@hamiltondaved1522
@hamiltondaved1522 7 жыл бұрын
ayawo kusukulu ndikofunika !!.
@enockbwanali9472
@enockbwanali9472 7 жыл бұрын
eish but thanks for watching man
@user-gj8td8pc4d
@user-gj8td8pc4d 6 ай бұрын
Part of ignorance. Amaona ND anthu akeso
@aishakachewale8112
@aishakachewale8112 4 жыл бұрын
Umbuli ndi matenda asilamu ofunika kumangowakhulukila chifukwa apa palibe chifukwa chomuletsa munthu kugulitsa malonda ake munthu apo anaphera ufulu wake
@clivengwira9992
@clivengwira9992 5 жыл бұрын
if you don't it pork don't buy it!
@edisonnyasulu9568
@edisonnyasulu9568 5 жыл бұрын
Asilamu ndi mbuli vuto ndi limero sukulu ndi mbali yina Ku chisilamu
@happysteven4131
@happysteven4131 5 жыл бұрын
Akudya adye osadya asadye sizokhomerelana ayi sitipangilana zisankho
@randwellchisambi1231
@randwellchisambi1231 Жыл бұрын
Mburi za anthu odya nkhumbawo amadyera pakamwa panu
@osmanjere9516
@osmanjere9516 7 жыл бұрын
let anyone believe what he/she believe,let's respect ones belive
@veronicanyanda7066
@veronicanyanda7066 7 жыл бұрын
mupereke solid events why u r threatening some other religious he has de right inu mukasetera manja ndan amakuletsan ana anjoka inu
@IsaacKulongwe-ol5mx
@IsaacKulongwe-ol5mx 5 ай бұрын
Ignorance has no defence
@laurentvictor9387
@laurentvictor9387 5 жыл бұрын
Wina aliyense ali ndi ufulu ogula ndi kugulitsa chakudya chimene anthu akhonza kugula izi sakakamiza kt aslamu kagulani kma amene afuna kugula amagula ndiyeno inu achisilamu musatenge ngt Mangochi ndi yanu yokha ai kt mukhonza kumapanga control chirichose chimene mungafune zimenezo zosatheka ai chifukwa dziko la Malawi silasilamu
@ketrinanyalaya3049
@ketrinanyalaya3049 6 жыл бұрын
lts true malawi it's not anislamic country, &pork is allowed but ( resten very carefully ) NOT IN MANGOCHI.
@ThumbikoChipofya
@ThumbikoChipofya 22 күн бұрын
You don't know what you are talking about,think before talking
@softzandani1124
@softzandani1124 5 жыл бұрын
kodi kudya nkhumba kwa anthu ena inu zikunyasani bwanji aaaaaaaa chamba et
@esmielaja2536
@esmielaja2536 7 жыл бұрын
nkhumba woyeeeeee!!!
@noziphiwonzenze6935
@noziphiwonzenze6935 5 жыл бұрын
Woyeeee kukoma nganda woyeee
@peterbanda2473
@peterbanda2473 5 жыл бұрын
Zachamba bas my vote is nkhumba
@lukainnocent5380
@lukainnocent5380 Жыл бұрын
Vuto ndi umbuli ayawo kumangochi ndiye aliyese ndi musilamo basi Zausiru
@Emmanuelsalifu-lc1rm
@Emmanuelsalifu-lc1rm 3 ай бұрын
Iweso chisilu
@samuwilliam7478
@samuwilliam7478 Жыл бұрын
Iweyo ungangulise nyama yolesedwa malo ayo
@victorbanda9039
@victorbanda9039 5 ай бұрын
Mumachita machimo ambirimbiri kunyenga akazi a eni kupha azanu kusetera mmanja kumwa mowa nde mukamulange nzanu chifukwa chankhumba muphuzire kupita kusukulu
@EmmanuelGasiten-fo5dr
@EmmanuelGasiten-fo5dr 3 ай бұрын
Manga amagulitsira kunyumba kwako? Uchimo onse mumachita asilamu inj:1Nyanga,ufiti,dziwelewele,ndiye munenapo chani apa.
@stanleydamalekani7113
@stanleydamalekani7113 5 жыл бұрын
Kkkkkkkk
@wakalembhera2244
@wakalembhera2244 7 жыл бұрын
Nonsense
@rkumbangarokumbanga
@rkumbangarokumbanga 5 жыл бұрын
Where is the right in Malawi? Does it mean Mangochi is a state on it's own. Oh God help the people of Malawi.
@christophershuga5871
@christophershuga5871 7 жыл бұрын
nonsense.give them the place to sell pork.remember we are staying in the area of co-group of people,with different believes and religious.dont break others rights
@enockbwanali9472
@enockbwanali9472 7 жыл бұрын
keep on watching guys
@veronicanyanda7066
@veronicanyanda7066 7 жыл бұрын
mvuto lochuruka mbuli mu zikiti KO'd did u know wat human rights its all a bout kusukulu kwabwno achawa inu Ali ndi ufulu kukhara malo komanso kupanga business anywhere in Malawi
@RichmondLasma
@RichmondLasma 7 жыл бұрын
vuto osati 'mvuto' kkk okamba zasukulu akulephela spelling
@tammiejali1228
@tammiejali1228 7 жыл бұрын
when you are in Roman do what Romans do
@petrokamoza2090
@petrokamoza2090 5 жыл бұрын
uchisilu umeneo nde akufuna kutiuza kuti kumangochiko athu ongwila tnchito mu boma asamapezekeko nanga akakhala kuti ndi achi khilisitu asamaje khumba chifukwa ali malo olesedwa? zauchisilu zimenezo ngati akufuna apite azikakhala ku rebanoni komwe kuli asilamu anzao ziko la malawi ndiziko lamtendele and muli zipembezo zosiyana siyana ngaati akutelo naoso asamapite kumaboma omwe amaja khumba angaka desedwe ndi khumbazo
@Emmanuelsalifu-lc1rm
@Emmanuelsalifu-lc1rm 3 ай бұрын
Iweso ndi wawusilu
@lukinamunyavhi9642
@lukinamunyavhi9642 7 жыл бұрын
U are talking nonsense u must go to school because i can see ur brain there is lack of school
@osmanjere9516
@osmanjere9516 7 жыл бұрын
let anyone believe what he/she believe,let's respect ones belive
@tingoalex6370
@tingoalex6370 Жыл бұрын
Mukuti nkhumba harram nanga mitala imene mumakwatira si harram eti agalu
@rajahibrahim3873
@rajahibrahim3873 Жыл бұрын
Eyo mind ur mouth dude pls let's respect each other's bro
@osmanjere9516
@osmanjere9516 7 жыл бұрын
let anyone believe what he/she believe,let's respect ones belive