Mbiri ya mpingo wa Seventh Day Adventist.

  Рет қаралды 53,857

Bakili Muluzi TV

Bakili Muluzi TV

3 жыл бұрын

Iyi ndi mbiri ya mpingo wa Seventh Day Adventist padziko lonse lapansi.

Пікірлер: 75
@user-sh5wq4uf6r
@user-sh5wq4uf6r 2 күн бұрын
Good history keep it up
@bkelly3053
@bkelly3053 3 жыл бұрын
keep it up boss tikuziwa zambili kamba ka inu ulemu wanu💪
@bakhtullah5154
@bakhtullah5154 3 жыл бұрын
Thanks for the best video.
@ishmaelbilali574
@ishmaelbilali574 2 жыл бұрын
Wow brother still following, keep it up
@mukatitchulebrand9244
@mukatitchulebrand9244 3 жыл бұрын
Good jod done mr ,,,,,continue doing it
@djsishimanemunena6785
@djsishimanemunena6785 Жыл бұрын
Big up bwana mumandivetsa kukoma in Munena sandram.
@bestonjoseph2193
@bestonjoseph2193 3 жыл бұрын
Good job Mr 🙏🙏
@cephasnkhoma2301
@cephasnkhoma2301 Жыл бұрын
Now did you have the books of those history's? .because this is my food to study those things.
@basiliojeremias6200
@basiliojeremias6200 2 жыл бұрын
Ambuye apitilize ku peleka Nzelu ndi Mavumbulutso. koma ndimati ndipemphe kuti pa Chito yanuyi ikufunika mutenge Yesu akhale mbuye ndi pulumusi wanu chifukwa amagelasi ndi ambili pakufunika chitetezo chochokela kumwamba
@chinsinsikundiya1171
@chinsinsikundiya1171 5 ай бұрын
Great history 🎉
@lusayomkumbwa211
@lusayomkumbwa211 3 жыл бұрын
Good stuff, keep the good work
@user-zc9wb4dj4q
@user-zc9wb4dj4q 4 ай бұрын
Man of God,let me talk with you,I have so many questions
@dorikakamwendo6970
@dorikakamwendo6970 3 жыл бұрын
Nice church
@umaliisah6920
@umaliisah6920 3 жыл бұрын
Thanx man
@viktak.d.o2835
@viktak.d.o2835 3 жыл бұрын
please do mbiri ya william marrion branham
@blessingchirwa8683
@blessingchirwa8683 2 жыл бұрын
God bless our sda
@patrickmacky6315
@patrickmacky6315 3 жыл бұрын
Amen
@andreaphiri4760
@andreaphiri4760 3 жыл бұрын
Ambuye adzikudaritsani timava zambiri kwayinu zosiyana siyana
@franciskhundi9335
@franciskhundi9335 3 жыл бұрын
Ambuye akutsogoleri pantchito yomwe mukugwira
@user-dy4xi2wk6w
@user-dy4xi2wk6w 8 ай бұрын
Nice
@demobreyngwira4440
@demobreyngwira4440 2 жыл бұрын
Thanks
@gracechiwaya667
@gracechiwaya667 2 жыл бұрын
For God so loved the world , that he gave his only begotten son, that whoever believes in him should not perish but have eternal life (John 3v16)Let not your hearts be troubled , Believe in God believe also in me ,in my father's house are many rooms ,if it were not so,l would have told you that l go to prepare a place for you.And if I go and prepare a place for you,l will come again and will take you to myself , that where l a'm you may be also.(John 14v1)"l a'm the way ,and the truth ,and Life,No one comes to the father except through me"(John 14v6)
@gabrielatanasiopessulane1279
@gabrielatanasiopessulane1279 2 жыл бұрын
Mwalankhula zoona...coz nkhaniyi ndikuidziwa
@cephasnkhoma2301
@cephasnkhoma2301 Жыл бұрын
Koma inuyo muli ndi zida ndithu, mulugu akutsungeni. ndi inutso mumu kuluphilire.
@spiwejafal7268
@spiwejafal7268 3 жыл бұрын
Kodi aulutsi a program imeneyi ya kafukufuku wa mbiri za maiko Muli mpingo wanji
@johnstonumali5881
@johnstonumali5881 Жыл бұрын
Aah koma adha mumatha ulemu wanu
@ezakidalitso6523
@ezakidalitso6523 2 жыл бұрын
Bola muzikamba zowona kamba anthu sakhulupilaka
@prosskaymw9953
@prosskaymw9953 3 жыл бұрын
Nkhan yabwino ndithu
@chippiephiri4505
@chippiephiri4505 Жыл бұрын
To God be all the glory
@ThokiseWiriyam-ws1ec
@ThokiseWiriyam-ws1ec 11 ай бұрын
Ame
@sanlakedickson6780
@sanlakedickson6780 3 жыл бұрын
Tipangileni mbiri ya charlies chaplin
@user-pg4pt9bl6n
@user-pg4pt9bl6n Жыл бұрын
Amen 🙏🙏🙏 to God be the glory 🙏🙏
@johnbauya1794
@johnbauya1794 3 жыл бұрын
Nkhani yopatsa chidwi
@osmank.milanzi8836
@osmank.milanzi8836 Жыл бұрын
Man inuyo mumatha
@husseinsamuson5173
@husseinsamuson5173 3 жыл бұрын
Mumakwani tikudzindikila zambili kuchokelakwainu
@kholwanigondwe9086
@kholwanigondwe9086 Жыл бұрын
Kufotokoza kwabwino
@kuziririzaisabatosiitegeko7088
@kuziririzaisabatosiitegeko7088 Жыл бұрын
😆😆😆😆😆
@nditumenichagunda4192
@nditumenichagunda4192 Жыл бұрын
Anthu a sda amazitenga ngati oyera mtima namanyoza anzao chikhalirecho background ya mpingo wao it's from fake prophet komanso ziphunzitso za mpingo wao zikuchokela munthu wachabechabe otchedwa Ellen g white osatinso mulungu
@memorylipenga2069
@memorylipenga2069 7 ай бұрын
Ine ndi mmodzi wa seventh-day adventist koma sindinamveke akunyoza mpingo wa munthu aliyense amangolalikira kuti yemwe alinalo khutu amvee chifukwa chipulumuso aliyense ndi chayekha ndipo momwe amayakhula apa sananyozepo seventh-day adventist wangonena za mbiri ndi chiyambi chake
@thembaphiri4523
@thembaphiri4523 3 жыл бұрын
Welcome to muslim truth religion in the world mark 13:21 quran 3:19 from blantyre
@truthtellerlastonk.m.p4985
@truthtellerlastonk.m.p4985 3 жыл бұрын
Zoona mzoti kulibeso munthu otchedwa Jesus amene adzabwere kuchoka kwamwamba,,,,, I was Jehovah's witness Christian,,, but I quit it,,,, please next time tell us about history of Jehovah's witness
@truthtellerlastonk.m.p4985
@truthtellerlastonk.m.p4985 3 жыл бұрын
@hope saiden zabodza izo
@truthtellerlastonk.m.p4985
@truthtellerlastonk.m.p4985 3 жыл бұрын
@hope saiden don't waste my time with your Jesus,,, he's nothing for me 🤷🤷,,, and the story of Jesus it's not real so I don't want to talk about it
@truthtellerlastonk.m.p4985
@truthtellerlastonk.m.p4985 3 жыл бұрын
@hope saiden mapeto achani inuso zongotaisana nthaw I was one of those people they preach this so called good news,, but it's just waste of time,, ndinali mkhristu wa mbon za yehova, not just a witness ai I was minestrial servant ( Mtumiki othandiza) ndalalikira kwambiri, koma am telling you mzachabechabe zongotaisana nthaw,,, open your mind brother and see the truth,,, now am just regretting for the time I wasted when I was Christian,,,,, but am happy coz I know the truth now,, and it was not too late,, even for you it's not too late
@truthtellerlastonk.m.p4985
@truthtellerlastonk.m.p4985 3 жыл бұрын
@hope saiden thanks for understanding don't waste your time for nonsese thing,,,,,,,
@truthtellerlastonk.m.p4985
@truthtellerlastonk.m.p4985 3 жыл бұрын
@hope saiden all of Christianity issue
@andrewmaluwa2713
@andrewmaluwa2713 Жыл бұрын
Ine always ndimanena kuti chimphuzitso cha seventh day Adventist, sicholongosoka coz anthu omwe adayambitsa mpingowu amatsogoleledwa ndi munthu wabodza fake prophet, mpovuta kuti omutsatila ake adzikamba zoona
@yamikansintala4178
@yamikansintala4178 Жыл бұрын
Exactly ndithu
@patelaysha7752
@patelaysha7752 Жыл бұрын
yese amene akuti kulibe Jesus amene adzabwere uli ndi tsoka chifukwa iwe otchedwaso kristu koma osadziwa Yesu, uwelenge chivumbulutso 1 vest 7 komaso machitidwe 1 vest 11, khalani nchocho mumuona posachedwa akubwela
@olivechikwindi9126
@olivechikwindi9126 Жыл бұрын
Asaaaaaa kuyankhula kwabwanji uku?
@francisevalleygama2984
@francisevalleygama2984 Жыл бұрын
U shall know the truth and the truth will set u free. There were others who were spoken like u but today they are members of SDA Church after knowing the truth. May good LORD help u
@johnsoko7098
@johnsoko7098 3 жыл бұрын
Amen
@patelaysha7752
@patelaysha7752 Жыл бұрын
ndikutanthauza mpingo owona ndiuti
@patelaysha7752
@patelaysha7752 Жыл бұрын
kapena ungandiuze iwe khristu zanga malamulo a mulungu Ten anja lilipo or limodzi lomwe linatha mphamvu koti tisaligwiritseso ntchito nde ngati ukuti ai ,nanga ndichifukwa chani la mulo number 4 sumalitsata? akuti uzikumbukila tsiku lasabata,motani,ungandiuze?
Kutha kwa dziko kwafika? Mtsinje wa m'baibulo wayamba kuuma.
14:50
Bakili Muluzi TV
Рет қаралды 46 М.
Backstage 🤫 tutorial #elsarca #tiktok
00:13
Elsa Arca
Рет қаралды 11 МЛН
Эффект Карбонаро и бесконечное пиво
01:00
История одного вокалиста
Рет қаралды 6 МЛН
Would you like a delicious big mooncake? #shorts#Mooncake #China #Chinesefood
00:30
Заметили?
00:11
Double Bubble
Рет қаралды 3,4 МЛН
Kodi ufiti ulipodi? Amene anayambitsa ndani
10:08
Bakili Muluzi TV
Рет қаралды 52 М.
The History of Anglican Church
14:22
Bakili Muluzi TV
Рет қаралды 19 М.
Rev Alexander Kambiri preaching at the funeral service in Malomo Ntchisi
30:23
Rev. Alexander Kambiri
Рет қаралды 31 М.
CRUISE 5  WITH ESAU BANDA - PENTECOST INTERNATIONAL CHRISTIAN CENTRE
48:56
Joab Frank Chakhaza
Рет қаралды 21 М.
CRUISE 5 WITH ARCHBISHOP TARCIZIUS GERVAZIO ZIYAYE
1:04:44
Joab Frank Chakhaza
Рет қаралды 33 М.
IZEKI NDI JAKOBO MALAWI GREAT COMEDIANS
1:41:46
Friends Connect Malawi tv
Рет қаралды 98 М.
Why Prophet TB Joshua died.
13:37
Bakili Muluzi TV
Рет қаралды 96 М.
Gwanda's Funeral - Last Sermon
25:21
Edson Gunsalu
Рет қаралды 147 М.
Backstage 🤫 tutorial #elsarca #tiktok
00:13
Elsa Arca
Рет қаралды 11 МЛН