ali biz kuba ndalama dza boma ndi mcp iweso masu mutu wako sugwila ncthito iwe ungamayamikile galuyu
@ArexBrightКүн бұрын
Sorry wapita mwachangu coz timadikila kt ayibe nyimbo mubo lilipoli koma ay zidko limatha bas kulimbanila nkazi kaya zichani tilibe nazo ntchito koma ife tingoti abuye wayakha bas RIP BINGU MUTHALIKA
@lingstonenagoli77294 ай бұрын
That's why Lucious Banda panopa sakuyimba nyimbo zolongosoka,, mmbuyomu album yonse imakhala nyimbo zonena Bingu yekhayekha
@loidchikoti93383 ай бұрын
Abodza inu munene kuti inuyo mzanu ndi bingu osati bandayo
@RuthChilobwe22 сағат бұрын
The woman probably was Calista as all these were parliamentarians. Not so ?
@user-kh4wy6ze9b4 ай бұрын
Ndy Pano akuti chani agalu okonda ku dyesa mimba zawo😢
@user-zv9zk2wr6u4 ай бұрын
Okay ndakumvani auncle Sam
@nysonzeperiana98694 ай бұрын
Munthu oipa uyu ndiokonda ndalama nthaw amadana bdi bingu chifukwa samaonapo cholowa...ngati ali munthu osaopa why now ogokhala or nyimbo kuimba ..sakuona anthu kuti akuzuzika
@JanetJamesMachila4 ай бұрын
Lucius banda dyera amafuna bazi koma anaona kuti bingu anali dolo sanamupatse 😂😂palibenso president angazafanane ndi bingu 😢😢alucius nanga lero muli kuti dziko lili pa moto ili
@user-lq2zj1vy5e3 ай бұрын
Mumatiuza zomwe sitimaziwa bwana mupitilize
@SurprisedDrumKit-ql7rj4 ай бұрын
Boss apa ndie meatinamiza zoti Lucius dagulidwazo mmm
@davidwakhokamoto11244 ай бұрын
I hate Lucius Banda ndipo ndiwadyera kwambiri amkagofuna kumamudyera bingu nde ataona kut bingu simuthu oti akhoza kumupusisa ayi
@franciskameko25864 ай бұрын
Si wabwino Lucius Banda
@chisalebeston4 ай бұрын
I like you Sam a historian
@user-ux1gc7qo3i16 сағат бұрын
Sir Paul banda is alive
@hendsonmaganizoofficial17584 ай бұрын
Taphunzilapo kanthu brother 🤝🙏🙏
@NzeruDesign-ut1go4 ай бұрын
Mot uzingofotokoza apa ndye ukuopa zchan?
@mosesharoldngolombe4 ай бұрын
Pano zinthu nde zikuyenda bwino? Ali kuti nanga bwanawa 😂😂😂
@lingstonenagoli77294 ай бұрын
Achitsiru aja
@WisdomKmsiska3 күн бұрын
Anapangitsa kuti mnyenyembe afe si uyu mkumutama apayi?
@user-vt9cw1dw1d15 сағат бұрын
Sam mavita kapenso
@user-zu2cc6qs9r4 ай бұрын
Amanena bingu emweyo
@user-vq7rs7zj2r4 ай бұрын
Uyu ndigalu wadyela
@chiefjusticie4 ай бұрын
Lucia's Banda anayesesa mokwanila kutimenyela khondo ndipo oyimba ambiliwa akutchuka chifukwa cha iye he is bg boss
@BornMandala-rz1dk4 ай бұрын
Ndisiyileni kanga nyimbo ija imanena Bingu😊
@user-pj7rl5fq6p4 ай бұрын
Amanena bingu kuti watani?
@user-kl5fo1rb5z4 ай бұрын
Komanso ngat kumalawi kuli andale osadziwa chomwe akupanga one of them ndi Lucius
@raymondchautsi62824 ай бұрын
Nde Pano sakuyankhula ndizopusa zomwe akupanga achakwelazi??🙄
@alexnyirenda12322 күн бұрын
Imfa ya Munyenyembe imandiwawa
@ClementKampaka4 ай бұрын
Kudali Billy kaunda yemwe adalimbana ndi bakili kapena mudali muli ana
@jamessaiti4 ай бұрын
Pano anampasa bazi ameneyo
@user-ux1gc7qo3i16 сағат бұрын
Paul banda alipo
@olobodokatwaha59474 ай бұрын
Ok chabwino tamvani man
@user-ci5cu1eq4e4 ай бұрын
Ine zambiri ai guys ngati mukuidziwa kanyimbo kameveka kumapeto koo ndiuzeni kuti anayimba ndindani chonde
@sammalvitha4 ай бұрын
Search nyimbo ya Sam Malvitha youtube chanel... muipedza ...pa youtube pomwepa boss Anaomba ndi Yb Africa ndi Kikey Malawi
Soja wa mphawi , speaking on behalf of the poor masses
@madalitsochabwera59034 ай бұрын
Ndisiyireni ena amati amanena Mulli kaya kkkk
@mosesharoldngolombe4 ай бұрын
Ineso namva chomcho
@maggiekamphinda56994 ай бұрын
Muli ankayenda ndi ndani Mlaka ndi bernadetter?
@patricgama47884 ай бұрын
bingu anapotsa kamuzu muzochitika pa 7eyes yake ndiye mungama fanidze ndi galu yo lus
@user-lz8do1or9l4 ай бұрын
Good ,could you please do more
@websterkausiwa89194 ай бұрын
Nawesotu nyimbo zachamwiniyoo usamangochaputaa ndiza Tygrin zoo
@robertmakupe28634 ай бұрын
Ase iwe ukumutama galu uyu alikuti luciac freedom fighter wakunyumba kwako tu
@VeronicaSekobi-is6dk4 ай бұрын
🔥
@mariamhassan40894 ай бұрын
Tadziwa nao
@EvalistoMilanzi3 ай бұрын
Like it
@user-dg8qx5eq5y3 ай бұрын
Am interesting
@ConfusedAtv-bs4gc4 ай бұрын
Mmmmmm lusius wakupha uyu anapha oyimba azake ambiri ATI asachuke kuposela iye
@chiefjusticie4 ай бұрын
No mukulakwisa mukatelo kod mayiko enawa anthu samafa nakha anthu ena osayimba ndipo sanatchuke komwe anthu akumuzi samafa ndi infa za m'zizizi munganene kuti ndi bwana Lucia's Banda. No come on guys let's us learn to respect our favorite artist from our country because if we could no palibe Munthu yemwe angawalemekeze
@zionekanjoka75754 ай бұрын
Mmmmmm
@user-cd8ke5pm4v4 ай бұрын
Amati yimilira wulemu wawo
@franciskameko25864 ай бұрын
Lucius Banda munthu woipa kwambri but he's a pretender ngat ndwa bhobho
@user-kh4wy6ze9b4 ай бұрын
Zowona zake waononga anthu ambiri galu ameneyi🤔😢
@user-ok9bb3de5m3 ай бұрын
Mumatha amwene
@patricgama47884 ай бұрын
amadana ndi chilungamo wautsilu ananga pano akuti chani ku mcp chifukwa ampasa mpando kumalawi balibe amene angaipitse bungu
@Mickeykasambula2654 ай бұрын
Ndepano lucius banda wanuyo sanagudwe ndi ndalama?
Liciusa Banda ndi hero anamuuzaso Bingu akuopsa kuti ndinamenyana ndi Mkango kunena Kamuzu nde sindingaope IWE Kambuku, Osafanizora zomwe amapanga Bingu ndi Kamuzu Bingu zitukuko zake zinachiitikira mu mseu umodzi opita ku state house 1 chiliza Cha Kamuzu 2 parliament 3 Bicc 4 Presidential villa basi, And dziwani kuti zitukuko za term yoyamba za president timakhala za emwe wamusiyila emwe Ali Dr Bakili muluzi mu 2 years yakeyake Bingu palibe Chomww anapanga kuposaposa Kwa nthawi yoyamba mu mbiri ya dziko lathu mafuta a GALIMOTO sugar soap bread zinkasowa komaso magetsi ndi ndalama za kunja mdziko muno munalibe ndi motsogozedwa ndi Mwakadungula timapanga ma demo komaso ampingo anampatsa 90 days kuti asiye pansi udindo because malawi was worse Bingu mzimu wake usamause mumtendere anaphetsa abale Anthu muzipatala kaba kokana kutsitsa mphavu ya ndalama yathu yomwe idali itathelatu Emwe sangayamikire za soldier Lucius' Banda ndi mfiti anayamba kulimbana ndi Kamuzu, Bakili muluzi kenakoso Chitsiru Bing
@ChimwemwePhiri.14 ай бұрын
I don't agree with you... Bingu did alot...you hated him i can see.
@user-kl5fo1rb5z4 ай бұрын
Nkulu uyu akunyoza Binguyu kaya ngwakuti kaya koma nzeru mmutu umu zilimo zochepa kwambiri ine nthaw yakamudzu kunalibe koma na Bingu palibenso president ndaona ineyo oposa iyeyu
@chiefjusticie4 ай бұрын
Respect brother pitilizani
@yamikanifischer4 ай бұрын
If he is strong why now
@christopherphiri84764 ай бұрын
I like your job go ahead some navitar
@chinyongakaole-qz5mh4 ай бұрын
0
@EvelynWilliams-ec5fxАй бұрын
😅😅😅😅😅 osamasakaniza zopusa ndi za nzeru bingu ndi ophunzira komaso anali wazeru sopano winayu mmmmm mumchimwisa ngat ali apongoz ako sorry
@dreamsneverdie-24211 күн бұрын
Chisiru ichi panopa akukanika kupanga za nzeru panopa
Liciusa Banda ndi hero anamuuzaso Bingu akuopsa kuti ndinamenyana ndi Mkango kunena Kamuzu nde sindingaope IWE Kambuku, Osafanizora zomwe amapanga Bingu ndi Kamuzu Bingu zitukuko zake zinachiitikira mu mseu umodzi opita ku state house 1 chiliza Cha Kamuzu 2 parliament 3 Bicc 4 Presidential villa basi, And dziwani kuti zitukuko za term yoyamba za president timakhala za emwe wamusiyila emwe Ali Dr Bakili muluzi mu 2 years yakeyake Bingu palibe Chomww anapanga kuposaposa Kwa nthawi yoyamba mu mbiri ya dziko lathu mafuta a GALIMOTO sugar soap bread zinkasowa komaso magetsi ndi ndalama za kunja mdziko muno munalibe ndi motsogozedwa ndi Mwakadungula timapanga ma demo komaso ampingo anampatsa 90 days kuti asiye pansi udindo because malawi was worse Bingu mzimu wake usamause mumtendere anaphetsa abale Anthu muzipatala kaba kokana kutsitsa mphavu ya ndalama yathu yomwe idali itathelatu Emwe sangayamikire za soldier Lucius' Banda ndi mfiti anayamba kulimbana ndi Kamuzu, Bakili muluzi kenakoso Chitsiru Bingu
@FerecidadedeshilaShilaКүн бұрын
Basi ose akumana komweko apezana azikamenyana komweko