That's a very greatful speech we need such type of people who can't fear but they stand for the right thing keep it up pastor/bishop
@AlexManuelMisomali-sv1vn3 ай бұрын
You have spoken wisely and positively to all the audience that's true kuti this government of Chakwera and his tonse alliance have totally failed and destroyed Malawian economy and it will be difficult for the next government to restore it
@brunobonkainga3 ай бұрын
I LIKE YOU FATHER AWUZIDWE ZOONA NGAKHALE ALI OSAMVA KOMA TIDZAWONANA PA 2025
@RabeccaMkandawire-i9j3 ай бұрын
A Malawi kususuka zithu zoti sizitithandiza kukopeke nditu k500
@WilliamBandaWili3 ай бұрын
Boma anachita kulilira ili that's y vamunyera chakwera pls anthu apa central region musamuvoterenso uyuyu atipha
@stanleymollen72733 ай бұрын
A patriot.....kuphunzitsa economics momveka bwino...economics 101
@PrinceKachimanga2 ай бұрын
i can vote for this pastor in 2025!..if he joins politics.Chakwera has failed this country..
@MphatsoMvula-k6e3 ай бұрын
Udatani umuwuza peter wakoyo mbuli ya mbusa iwelenge yohane 10 mbusa wakuba iwe
@ChimwemweMuhelliwah2 ай бұрын
Kkkkkk mwina tiyese kutenga anthu oti Ali mkanthu kalewa bwanji...anthu ngati Mpinganjira aja ndi amchina Simbi ,,,osaukawa akuwonjeza kuzilemeletsa kaye okhatu.....😂😂😂
@JeanKambala-gm1zr3 ай бұрын
Kodi abishop mawuwo basi antha siinu mikuyankhula ndimulungu wakutumani. Tikudikila titsegulenni maso ndi chilungamo
@OFG-th3st2 ай бұрын
Iyiyi atiwonelele😂😂
@martinmoyo42113 ай бұрын
Kudzudzula kulipamenepo koma inunso atsogoleri athu achikatolika mulindivuto. Timakonda kuloza chala anzathu koma ndichani timapangapo polithandiza bomalo. Tikati tiyang'anitsitse kumpingo kwathu inuyo atsogoleri a ntchito anunso simumawasala molongosoka mumalipiro. Mwachitsanzo a Gulupa samapatsidwa malipiro abwino komanso a ntchito ena. Ifenso tikonze gawo lanthu mpamene tidzizuzula enawa. You should also set good example in leadership. Zisakomere mbuzi kugunda galu.
@VictorKachulu-y3n3 ай бұрын
Popeza mwati ndi munthu wa Mulungu bola tamva koma sanafike kukhala mwana wa Mulungu popeza nayeso ndi wochimwa koma ndi wa bodza uyu Ngati kumpingo kwawo walephera ndiye alonze chala wina angoyesetsa nayeso kutukula dzikolino ndizofunika kugwilana manja koma mukalowetsa ndale ndi mu mpingo momwe ndiye Kuti tigwa tonse ndi nkhosa zomwe or iye sungayendetse dziko ife a DPP zinatikanika kale 😅😅😅
@DEXSTALLONEKAWAMA-s4g3 ай бұрын
Oro muthalika a lowe mudzavutika chimodzimodzi musaone kuti akalowa Mutalika ndiye zinthu zisintha ayi mukuzinamiza kwambiri tiyeni tiziwelenga mau aMulungu atiuza zoona awatu ndi masiku otsiliza Buku lopatulika linanana kale kuti masikuotsiliza mudzaona nkhondo kukangana mu maiko osiyanasiya and munthu afzakonda ndalama not munthu nzake ndipo zinthu zambiri zidzakhala zokwera mtengo kwambiri ine ndakambako zokomo abale mwabuye
Church silimakhala ndi anthu a opposition okha, mliso a m boma, ukulalika mosasamala utha kuyambanitsa anthu m MPINGO. Maka nthawi ya campaign tilimoyi.
@DouglasDazuKamwendo3 ай бұрын
Kodi umafuna anene kuti zithu zilibwino zisali bwino? Taganizani kae bwinobwino amwene osathamanga poyakhula taonani kwa nthawi yoyamba anthu a Mulungu kuyankhulapo m'mene dziko likuyendera ndipo ndi ambiri zedi moti mukwanitsa kuwaletsa onsewo? Tadekhani inuyo ngati simukuona manvutowa khala phee muzingodyelera apa sakunena za campaign ayi koma kutsegula maso anthu amene akunvutika, ndipo idakakhala campaign in church bwezi pakunveka ena kumutsutsa pompo koma ngati akumuombera m'manja choncho ndekuti anthuwo akunvomerezana nazo zomwe munthu wa nzeruyu akuyankhula ku mpingo wa Mulungu. Dziwani kuti mudziko Mulungu adalenga anthu anzeru kuposa azitsogoleri anthuwa koma kuzichepetsa kokha kumapambanitsa so you better watch your mouth.
@kingsleymsampha22603 ай бұрын
Chilungamo chilibe zoti wochimwa ali momwemo ayi. Truth will remain and the wise will choose the right way to go. The foolish will blame the advice.
That's true i do respect your massage father keep it up i like the ward's you taling as
@ChristopherJohn-z5z3 ай бұрын
Ku bandura osaopa osafooka kkkk
@LETUSCHIPHUPHU3 ай бұрын
Muli nzeru umu this audio shud reach to the state 🏠
@YasinThomuVakhaniMilanzi3 ай бұрын
Zikumveka bwino ndithu kuchokera pa mawu amenewa boma la abusa a Chakwera lalepheradi. Zikufunika kusankha moyenera.
@SymonPaul-s8h3 ай бұрын
It's true that they failed
@AndrewMukhwapa-qj4vo3 ай бұрын
Thanks very much God bless you. Your talking the truth
@giftnyirongo-ey3qy3 ай бұрын
What an intelligent gentleman
@marryphili54193 ай бұрын
That's true pastor we need to use the brain life now is expensive
@kingsleymsampha22603 ай бұрын
Samuel told Saul kuti umfumu wanu wakanidwa. Ndiye abusa azingoti zakumwamba?? Kulowa kumwamba ndi umphawi aaaaah
@BressingsMahele3 ай бұрын
Powerful
@clalesschisale37923 ай бұрын
Our next Bishop of blantyre archdiocese
@AndrewMukhwapa-qj4vo3 ай бұрын
Your talking the truth God bless you thanks very muh
@TamandaniMaseya3 ай бұрын
🙏🙏🙏🙏🙏
@DEXSTALLONEKAWAMA-s4g3 ай бұрын
Uyu ndi wabodza anthu malo poti awauze anthuwa mau achipulumutso akupanga kampeni yandani inu mungafanizile dziko lamalawi la Mozambique or zambiya zambia ndi dzikolimene limagulitsa miyala ya mtengo wapatali komanso muli Ma boulder ambili amatolera ndalama zochuluka komanso kumalawi timabalana kwambiri sizigwiliza ndikuchepa kwadzikolo Mozambique kuli ma madoko awili amene ama bweletsa ndalama plus mogodi anthu amulungu ngati awa ndi amene amapangitsa kuti dziko lisamayende bwino chifukwa amaiwala mau aMulungu amayamba kulalikira ndale mudziko simungakhale m'dalitso ayi toyeni tizipemphera kuti mulungu afalitse Malawi zikomo
@BrightZionga3 ай бұрын
Akunenatu chipulumutso kupulumutsa miyoyo ya anthu apulumuke kunjala kuumphawi kukukwera mitengo ya zinthu Kodi mau oti kupulumukawa amakamba zakumwamba kokha pepani ngati ndakulakwirani koma sitingamakambe zaulemelero ukudzawo pamene apapa anthu tikuvutika
@WinerdShadreck3 ай бұрын
Thank you man of God
@PrinceKachimanga2 ай бұрын
inu a busa awa akulankhula chilungamo...MCP HAS brought misery in this country.and we are tired of mbuzi zimenezi
@gabrielmulowe84813 ай бұрын
Anthu Ngati awa ndi amene timawacuna
@victormasambuka83663 ай бұрын
Mu church mumakhala anthu azipani zasiyasyana sibwino kukamba za ndale mufzagawanittsa church as a pastor keep your opinion to yourself
@EmanuelMuotcha2 ай бұрын
zoona father imani pachilungamo zikoli silili bwino anthu akubvutika+++
@hamiltonsolomon37563 ай бұрын
Well said......👏👏👏👏👏👏👏👏
@paulbanda96383 ай бұрын
Patakhala kuvota mau anu ndavotera kale,u r a good preacher
@LilianKachala-yz2xf3 ай бұрын
Takumvani Abusa
@mayesojameskatete3 ай бұрын
Good speech ❤❤❤❤
@DONNEXKhama-bk1gy3 ай бұрын
Zochezatu😂😂😂😂😂 chilungamo
@TopoTopo-bm4vw3 ай бұрын
Good advice thanks
@beakab23783 ай бұрын
Well said
@AchinaKellz3 ай бұрын
Kukhala ngati kachilungamo
@KennethMchenga-j9c3 ай бұрын
Very true man of God
@IsaacMusa-py2jm3 ай бұрын
Zamphanvu 🙏
@MarcosDjussa3 ай бұрын
Mumakwanila fr 😂😂
@NdalamaCharse3 ай бұрын
🙏🙏🙏🙏
@EdsonKamwendo3 ай бұрын
Mbambande Father
@RonicSouza-sk5ux3 ай бұрын
Mau
@HedgensChisale3 ай бұрын
Ine ndinauza koma sakuva
@ConradccjSokoSoko3 ай бұрын
Sizocheza
@SaidiMbawa-st6bj3 ай бұрын
Alomwe awa tazilarikilani za ufumu wa Mulungu
@PeterBendeka2 ай бұрын
Akanene kumene atikwana amenewa
@DEXSTALLONEKAWAMA-s4g3 ай бұрын
Uyu ndiwabodza zambia nayo ili pamavuto azachuma munthu wa mulunguyu ndiwabodza kwambiri
@LamekiSamson3 ай бұрын
Wabodxa ndi iweyo
@AliJack-e6r3 ай бұрын
Akumanganitu
@Creslevison-vj2sl3 ай бұрын
Dont fear everything akulu
@Patricia_Chisankha3 ай бұрын
Unenesko uli papa
@JosephAMoses-ne8ji3 ай бұрын
It is very true that they have failed
@ConradccjSokoSoko3 ай бұрын
Iweso ukulalika zopusa, economics yakuti unaphunzira iwe, you do not compare zinthu zosiyana,, Mozambique ukuchita compare ndi Malawi, kapena Tanzania .... Just chinthu chimodzi like DOOKO,LA PA NYANJA ..... what it earns cannot compare ndi Malawi.Ukawauzenso nawe omwe akutumawo.
@marryphili54193 ай бұрын
Ngati ndiwe wa MCP wuzipase wulemu amalawi tilipa moto sitimasekesekerere ndi mbamva zimenezi
@ClementinaKapanga3 ай бұрын
Ndiwe opusa kwambiri ndi MCP yakoyo
@simeonbanda42403 ай бұрын
Umva pheni wa MCP ulendo uno
@johnchrispine39493 ай бұрын
Point ndiyonena kuti, zinthu zochepa zomwe tili nazo tizigwirisa ntchito bwino.