Zilibwino akumudzi kwathu m' mbali mwa mtsinje wa Nathenje apo tinkadyerapo mbatata yosasenda kale ife tisakudziwa kuti pali ulaliki wathoo. Mwandisintha kwambiri ndi nyimbo maka maka yoyambayi. Andipatse mtima wopilira zonse zondipinga dziko lavuta ili. Masiku ano ndi gwira bango madzi angakutenge kikkkkkk Alleluya.
@GracePhirisakala-ml9vt4 ай бұрын
Amen and amen azimai
@chisonimponda36316 сағат бұрын
Amen azimai
@simbayihamaundu3552 Жыл бұрын
Watched this from Lundazi Zambia 🇿🇲
@rodankhoma5595 Жыл бұрын
Thats true we walk with God but we don't know him, Family of God let us walk in the right of God and we should know him
@agoranselema4974 ай бұрын
Very nice keep it up ladies
@CharlesChilinde-zm9xo Жыл бұрын
So nice do good keep it Nanthenje women choir thank you as lot