NAYO DPP ISAZITENGE NGATI NDI ANGELO LERO ..Hot current 19/05/2024 a TTV's CONTENT.

  Рет қаралды 18,932

LIKI-LIKI TELEVISION

LIKI-LIKI TELEVISION

15 күн бұрын

Пікірлер: 72
@JustinPhiri-kq2bb
@JustinPhiri-kq2bb 14 күн бұрын
choti muziwe Chakwera sangazawine ampungu ndi amene azachuluke ngati sazapanga alliance
@user-bm5yg6zm3c
@user-bm5yg6zm3c 14 күн бұрын
😂😂Chilungamo chimawa pepani pepani
@user-yt2op5rl2q
@user-yt2op5rl2q 13 күн бұрын
Pagulupa wa mcp ndi wonder enawa amangosatila but no wonder this is kandodos TV but zoona chakwera ndiolephera ndipo whether you like it or not mcp ikupita thank you
@SheenahMwalabu-iz3pr
@SheenahMwalabu-iz3pr 14 күн бұрын
Olo mutayankhula bwanji, kulangiza bwanji, Chakwera sangasinthe ndi president wamwano ndioipa sinnaoneko eee. Ndinamukhulupilira koma ndinabetsa, bolanso tikanaika Chilima chifukwa amaoneka kuti zopusa safuna bwenzi zomamenyanazi anthu achipani cholamula kulibe 😢 ndezonse ndinthawi 2025 tiona chifukwa olo mulungu sakukondwa ndazo and l believe kuti malemu Sidik Mia bwenzi akusekelera izi
@user-ev6bi7jr7g
@user-ev6bi7jr7g 13 күн бұрын
Musavutike ndikuyankhula a Malawi akudziwa chabwino ndi choipa ndipo chomwe agwiracho ndi chomwecho DPP woyeeeeee
@marryphili5419
@marryphili5419 13 күн бұрын
Ine mutanena bwanji za zoipa za DPP Koma ine ndikuwona Kuti DPP yinali bwino chifukwa fertilize wunali wosika , makhwara muzipatara analimo chimanga chinali palipose mapassport timawapeza kwina kulikose mosavuta Koma kubwera Kwa MCP moyo wolimba okhaokha angomba ndarama mopanda chisoni ndipo I like DPP
@Abdul-xk8dq
@Abdul-xk8dq 14 күн бұрын
Koma inu simungathe kusiyanisa pa thawi ya dpp ndi ino tili ino?
@AleksaWilliams-qc6cn
@AleksaWilliams-qc6cn 14 күн бұрын
Mwadya banzitu iiiii koma ndalama anakonza
@ziyamporoma377
@ziyamporoma377 14 күн бұрын
Kodi anthu akanena zosakukomelani ndekuti adya banzi? Do you think 20 million tonsefe tingakhale ndi maganizo amodzi?
@AleksaWilliams-qc6cn
@AleksaWilliams-qc6cn 14 күн бұрын
@@ziyamporoma377 mwadya
@TarPoor-ye9jx
@TarPoor-ye9jx 14 күн бұрын
Yes Malawi izi sizingapitise chisogolo dzkoli chkufunika Inu maguys pakanemapa musamaope mukuona kwanga Inuyo madolo mukuopa mcp kut munene chilungamo mukubweza mau kwambiri and mcp ikusaka bakili muluzi tv chifukwa chachlungamo chimene iyeuja amalankhula Malawi yonse kuli Bakili muluzi tv and Bon kalindo saopa munthu and Inu zoona Malo mot boma likhale likuona mavto amalawi akulimbana ndkusaka bakili muluzi tv pali dzeru tonse yalepera pazonse bas we need new leadership chakwela ,chilima ,mutharika sakufunika boma and nankhumwa too we don't want them you should tell them please
@AhmadumkomaTambala-lr9gp
@AhmadumkomaTambala-lr9gp 13 күн бұрын
Inuyo azibambo atatunu mukudya ka 20 zidyan mudziwe kunjakuno kulimulungu komanso mulindiana muzaziona
@RobertLuka-wy9cl
@RobertLuka-wy9cl 13 күн бұрын
Olo mudye baziii mulungu akuona mmene akuvutikila anthu ake ku malawi azaweluza
@RamseyGuveya
@RamseyGuveya 13 күн бұрын
Dpp my vote olo mutanena bwanji
@llewellynkhungwa4712
@llewellynkhungwa4712 13 күн бұрын
Bwana ndevu zamwayi Diso laku right likuoneka lotupatu
@geraldtuwaga-iz6ll
@geraldtuwaga-iz6ll 14 күн бұрын
Bravo to you brilliant and breve gentlemen, you stand for us
@AllanMafelo
@AllanMafelo 14 күн бұрын
Aaa awasotu amakondela
@JIMMYWATHONJE
@JIMMYWATHONJE 14 күн бұрын
Anyamata a mcp ntchito mukuigwila
@SamukLungu-zg7fl
@SamukLungu-zg7fl 14 күн бұрын
Vuto ndarama anapanga chakwela amaziwakuti uku ndikayikako chuma asatira ineyo wose amene akuyankhurapa nawoso anadwakare zake
@KassimmwStevenetc
@KassimmwStevenetc 13 күн бұрын
Koma athu tiziganiza Chocho maka athu Ali aut Malawi
@paulkachulu
@paulkachulu 11 күн бұрын
Everyone knows that DPP has proven their worth, they are not perfect, yes..But they always deliver. You had been in Malawi, you have seen it yourself
@chifundocharles2348
@chifundocharles2348 13 күн бұрын
Title yanu ikusephana ndizomwe akuluakuluwa amakambilana🤣🤣
@user-hr2cg3ku1l
@user-hr2cg3ku1l 13 күн бұрын
Wel done ndevu zamwayi
@JamesMalango
@JamesMalango 14 күн бұрын
Mumaziona ngati anzeru ndinu nokha m'Malawi muno mukamati kut simmanyengerera popeza ndinu amanthanso
@AndrewSimakweli
@AndrewSimakweli 13 күн бұрын
🎉
@Mike-du7zt
@Mike-du7zt 9 күн бұрын
Mmmm awatu kubwera pa tv ndikusonyeza kulimba mtima
@user-fi2by2ui9o
@user-fi2by2ui9o 14 күн бұрын
Mukamatero za dpp zimandinyasa kwambiri sindimafuna kumamva Zina limeneli Peter olo bingu amandinyasanso ndi zimbava zowononga dziko chonde musamatchule zinthu zimenezi
@TarPoor-ye9jx
@TarPoor-ye9jx 14 күн бұрын
And we know kut zodiak, mbc and times media all zili pansi pa mcp does why you scared please try to tell people the Truth not just blaming dpp only what's about mcp
@JamesMalango
@JamesMalango 14 күн бұрын
Awanso ndi amantha asaname kuti samanyengerera mukuona ngati anzeru ndinu nokha
@user-nj5vu8cd5l
@user-nj5vu8cd5l 14 күн бұрын
Achakwera sogolo alibe, peter muthalika sogolo walibe ... Let find someone to lead us these two mubusa ndi professor tiwataye uko atinamiza chani Poti both of them akhala pa mpando wa upresident for 5yrs but nothing did for the nation Wonse Kuba, nepotism very excellent... Palibe wina wowapotsa
@WitnessMpakula-cs1so
@WitnessMpakula-cs1so 13 күн бұрын
Hot current idatha ndi Brian banda
@user-lw9su5om5z
@user-lw9su5om5z 13 күн бұрын
Munya muona bolan Dpp ili nd ma pictures abho ku mtundu wa amalawi
@WhiteRichard-cw2fo
@WhiteRichard-cw2fo 14 күн бұрын
Inu mwayamba kudya ndalama zachakwela iti
@user-un6qv6sj3h
@user-un6qv6sj3h 14 күн бұрын
Mulungu akudalitseni nonse chifukwa chowaunikira amalawi I love guys inudi simutenga mbali mumangonena chilungamo chokha basi
@user-fr4gb4bq6q
@user-fr4gb4bq6q 13 күн бұрын
Zipumi zanu mbuzi za anthu mukuzitenga ngati ndinu opambana
@uchizJoelMumba
@uchizJoelMumba 13 күн бұрын
Dpp sizabwelanso tiwaleko amene aja amapha anthu achialubino anthu oipa kwabasi
@ziyamporoma377
@ziyamporoma377 14 күн бұрын
Kodi andebvu zamwayi disolo akubulashani kapena Sakhalin bwanji?
@ziyamporoma377
@ziyamporoma377 14 күн бұрын
Koma abale look at Wonder & Jona kumasoko ndi mmasayamo kodi anthuwa amenyedwa or I’m I just drunk?
@user-hr2cg3ku1l
@user-hr2cg3ku1l 14 күн бұрын
Andevu zamwayi mumaseka monyodora mumativetsa kukoma kwambiri kkkk
@cosmaspeter3123
@cosmaspeter3123 14 күн бұрын
Dpp ndi moto
@user-nj5vu8cd5l
@user-nj5vu8cd5l 14 күн бұрын
Keep up ❤❤❤guys
@MisheckChinjala
@MisheckChinjala 14 күн бұрын
DPP 2025❤ from Cape Town South Africa Stellenbosch University
@EllenLuwanika-tl5ck
@EllenLuwanika-tl5ck 14 күн бұрын
Dpp 2025 Boma
@mphatsojuliostandy4918
@mphatsojuliostandy4918 14 күн бұрын
Mvuto la Malawi ndilimenelo saziwa chomwe akufuna ,DPP umakhala chete mukuti iyayi ikuyenera izuke MCP yatayirira chifukwa otsusa akhala chete ikati iyankhule mukuti inalikut isakhale angero lero
@MuhireDominic-rw4vf
@MuhireDominic-rw4vf 13 күн бұрын
Hot current 😂😂🔥🔥🔥❤❤❤
@user-nj5vu8cd5l
@user-nj5vu8cd5l 14 күн бұрын
Guys mwalunkhula chilungamo, we must never say DPP but Peter muthalika munalipo pamupanfo zinthu zinakukanikani ,,, MCP yilibe vuto, problem ndi Chakwera walephera kukoza dziko. These two people please Malawian don't worst our time to vote for them at least they must handover to another person to represent their parties
@CyprianoSandalamu
@CyprianoSandalamu 14 күн бұрын
Mcp my vote, during the time of DPP party,we have been killed by DPP party mainly the cost of dry maize,their cost was k60 per kg,but now we are going to admarc to sell dry maize at K650 per kg.But those they are not farming,they cry.Don't cry ,go to field and do farming you will not regret.
@husseinsangala3374
@husseinsangala3374 11 күн бұрын
You are selling that price bcoz of the devaluation your MCP brought but you can't see
@DennisDonework
@DennisDonework 14 күн бұрын
Charge mpaka 45,000. Ngati ndi thini la chimanga kapena izicharger. Or magesi kulibe
@samsonmtumbati4855
@samsonmtumbati4855 14 күн бұрын
Ndipo zoseketsa kwambiri
@AlickLayson
@AlickLayson 14 күн бұрын
Zooona xzake
@user-si7po9sd5i
@user-si7po9sd5i 14 күн бұрын
Kodi mumalimbana ndi dpp chifukwa chani,Kodi mwaiwala kuti mcp inapha anthu ambiri mu ulamuliro wao motsogozedwa ndi kamuzu Banda,timadziwatu kuti times ndi yakubanja kwa akamuzu,komaso timadziwa kuti ndinu anthu adyera komaso muli mkhwapa mwa mcp.
@mosespemba8822
@mosespemba8822 13 күн бұрын
Umbuli uli ndiinunso 😂😂. You will hate MCP up to when? Mbuzi ya munthu,,
@user-si7po9sd5i
@user-si7po9sd5i 12 күн бұрын
@@mosespemba8822 you have proven yourself of who you are,the nasty words always represent the real person.
@user-qp8kh2hj9o
@user-qp8kh2hj9o 14 күн бұрын
Ndipo ngati kuli chipani cha manyi nde ndi DPP anyamata inu
@AdenaGuest
@AdenaGuest 14 күн бұрын
Achabe
@JafaliAkimu-ll1bf
@JafaliAkimu-ll1bf 14 күн бұрын
vuto ku mcp kwachuluka mbutuma za anthu anyawu ndi mbuzi zosapita ku xool
@AlickLayson
@AlickLayson 14 күн бұрын
47:05
@PatrickLucius-bl3te
@PatrickLucius-bl3te 14 күн бұрын
Mufune musafune kaya ndinu a times kaya zodiac koma CHOTI muziwe ndichakuti nkhondo imeneyi Mulung aimenya ndiponso aimaliza yekha.kukanakhala kt peter anakakamila nthawi imene ija bwezi kuli nkhondo yoopsya .koma mulungu anamunong'oneza peter kt zisiye kaye lero anthu azindikila kt chakwela ndi chilima anatinamiza anthu ayambanso kumufuna peter Muthalika .Nkhondo iyi Mulungu aimaliza yekha
@alexmkolongo3089
@alexmkolongo3089 14 күн бұрын
Mau amphamvu
@ChiyembekezoPhiri-sv8nw
@ChiyembekezoPhiri-sv8nw 14 күн бұрын
Pankuku wayakhula bwino
@user-cs5ss4rj7g
@user-cs5ss4rj7g 14 күн бұрын
Zikulipana ndi dpp chifukwa mbuzi izi zikudya kwachakwela buli ndichakwela
@JafaliAkimu-ll1bf
@JafaliAkimu-ll1bf 14 күн бұрын
chakwera ndi mbuzi ya munthu democras samaiwa kuti ndi chani vuto lili pamenepo or kungoti mcp ndi anthu ankhaza ndizitsiru
@user-bm5yg6zm3c
@user-bm5yg6zm3c 14 күн бұрын
Izitu sizigwila ukamalemba utakwia umadumpha mau Ena 😂😂😂
@AdenaGuest
@AdenaGuest 14 күн бұрын
Anthioipamcp
@BiquitoniNsandamila
@BiquitoniNsandamila 14 күн бұрын
Sindikukaika kuti Nanunso mukudya nawo za chakwera
@tisuhmakhwah7085
@tisuhmakhwah7085 14 күн бұрын
mcp
@jemasmasimbi8109
@jemasmasimbi8109 14 күн бұрын
mmm kupusa bas,,, ngat mulinshunga makwanu
@user-nj5vu8cd5l
@user-nj5vu8cd5l 14 күн бұрын
Peter is musogolele wapha ma albinos ambiri, kuba ndi chisale, nepotism racist Peter galu. DPP yilibe vuto, problem ndi Peter muthalika ndi mudala woipa mutima kwambiri
@alexgweje8610
@alexgweje8610 14 күн бұрын
Inu muli ndi umboni Kuti Peter amapha ma komanso Kuba???bwinotu musamatamike ndi kuyankhula nanga anthu akuphedwawa ndi munthalikanso
Izindaba zesiZulu @19H00 | 02 June 2024
23:17
SABC Izindaba
Рет қаралды 17 М.
100❤️
00:19
Nonomen ノノメン
Рет қаралды 38 МЛН
Тяжелые будни жены
00:46
К-Media
Рет қаралды 5 МЛН
APM Sanaluze Zisankho Mu 2019 Ndi Mu 2020 - Innocent Mutholo
22:47
Nyasa VoiceBox
Рет қаралды 10 М.
MDYANGU COMEDY SERIES...24/02/2023
29:16
LIKI-LIKI TELEVISION
Рет қаралды 33 М.
USAUVER S05E02   NETWORK
11:52
Piksy TV
Рет қаралды 59 М.
[ICYMI] 'We won't work with ANC under Ramaphosa' - MK's Nhlamulo Ndhlela
21:22
2024 Elections : Cyril Ramaphosa First Speech After 2024 Elections Results
14:20
2024 Elections | 'I have accepted the results'| Maimane
15:40
SABC News
Рет қаралды 97 М.
MOSES KUNKUYU EXCLUSIVE INTERVIEW
56:13
Zodiak Malawi
Рет қаралды 24 М.
DPP ndi UTM alliance itha kukhala yamphamvu bwanji?..HOT CURRENT 26/05/2024.
1:30:35