Naam sheikh ma shaa Allah ndipo anthu amaopa kukhala kuqibula Allah awakhululukire zofooka zawo
@user-lf5qw7mk3h3 күн бұрын
Km this kind of lecturing sometimes zumandikhuxa bwanj Mmalo moti muzapephelera amzanu chikhululuko bas muli busy achibekete Panopat kumalawik kuli zambil zoti kalel sizimachitikai inuo ophuziran muthawi yanu samasephan pakhan ya eid km lero ikangofik mumangotukwanizana apa Be humble muziwapephera amzanu chikhululuk jaman kozan zomwe zilipoz pano a a jaman
@user-rl5zq1qr4d9 күн бұрын
Ulaliki wabwino ndithu koma kuchula mbiri ya munthu omwalira kuti anali wa shirik its very unfortunate mukanangokhonza zimene inu munaziwona kuti ndizolakwika in directily not directily nkutheka ena analowa chisalam kuchokera kuzimene iye amapangazo inde tiwalemekeze ndi amene anasunga deen inu ozindikiranu musanabwere choncho tiyeni tiwapemphere chikhululuko osati kuwapepusa MAY ALLAH SHOWERS US ALL WITH BLESSINGS FOR BEING MUSLIMS
@MoneyTiririMgwagwa8 күн бұрын
Zoonadi kuzuzula kwa bwino
@IsmaelBilal-lh1pi14 күн бұрын
Tiyeni tiwapangile ma duwah mwina kutheka amaizichita mu umbuli. Allah awakululukire chifukwa anatisungira Deen
@Qassimcedrick12 күн бұрын
Amee
@MoneyTiririMgwagwa8 күн бұрын
Munakakamba zoonadi koma osatchula muthu ngat inu mwazindikila muchoonadi munakalalikila pazomwe inu mwazindikila ndi mene mwaphuzilila
@JohnAsendi13 күн бұрын
Koma amwene ndi makusati mukulankhulana kwanu kwaonesa kuti wabwera kuzalimbana ndi anthu omwe anaphunzira kale kodi tizinena kuti muli PA chiwongoko ndiinu choti muziwe ndi chakuti dini ndi ntchito sizingagwilizane mupite Kwame e mukuwanyozawo samalandila ndalama kutha kwamwezi pomwe Ena inu mumalandila ndiye kumati uza zabwino zomwe akuchita ungokhala zonse ndizolakwika alibe zabwino zomwe akuchita
@Qassimcedrick12 күн бұрын
Sheikh kodi mitiuza mu Quran pomwe aletsa kulandira ndalama ukagwira ntchito ya Deen pakati panu ndi ife pali Quran ndi MA hadith atumiki basi palibe zokangana
@JohnAsendi12 күн бұрын
@@Qassimcedrick mumalandila ndiinu ingo ndiuzani lembalo mu qraan
@JohnAsendi12 күн бұрын
@@Qassimcedrick mumalandila ndiinu ingo ndi uza lemba mu quraan