NTHAWI YA UMBULI KUIMBIRA MFITI MMANJA SH.ABOU SUFIAN KHATWEEB DAWOOD

  Рет қаралды 1,269

Qassim cedrick

Qassim cedrick

23 күн бұрын

Пікірлер: 14
@user-gk6bf7xe9g
@user-gk6bf7xe9g 14 күн бұрын
❤❤❤❤
@UseniMailosi
@UseniMailosi 13 күн бұрын
Ameen inshaah Allah
@Musa-cz1nm
@Musa-cz1nm 12 күн бұрын
Ma shaallah ma shaallah ma shaallah
@MariamJaffali
@MariamJaffali 12 күн бұрын
Naam sheikh ma shaa Allah ndipo anthu amaopa kukhala kuqibula Allah awakhululukire zofooka zawo
@user-lf5qw7mk3h
@user-lf5qw7mk3h 3 күн бұрын
Km this kind of lecturing sometimes zumandikhuxa bwanj Mmalo moti muzapephelera amzanu chikhululuko bas muli busy achibekete Panopat kumalawik kuli zambil zoti kalel sizimachitikai inuo ophuziran muthawi yanu samasephan pakhan ya eid km lero ikangofik mumangotukwanizana apa Be humble muziwapephera amzanu chikhululuk jaman kozan zomwe zilipoz pano a a jaman
@user-rl5zq1qr4d
@user-rl5zq1qr4d 9 күн бұрын
Ulaliki wabwino ndithu koma kuchula mbiri ya munthu omwalira kuti anali wa shirik its very unfortunate mukanangokhonza zimene inu munaziwona kuti ndizolakwika in directily not directily nkutheka ena analowa chisalam kuchokera kuzimene iye amapangazo inde tiwalemekeze ndi amene anasunga deen inu ozindikiranu musanabwere choncho tiyeni tiwapemphere chikhululuko osati kuwapepusa MAY ALLAH SHOWERS US ALL WITH BLESSINGS FOR BEING MUSLIMS
@MoneyTiririMgwagwa
@MoneyTiririMgwagwa 8 күн бұрын
Zoonadi kuzuzula kwa bwino
@IsmaelBilal-lh1pi
@IsmaelBilal-lh1pi 14 күн бұрын
Tiyeni tiwapangile ma duwah mwina kutheka amaizichita mu umbuli. Allah awakululukire chifukwa anatisungira Deen
@Qassimcedrick
@Qassimcedrick 12 күн бұрын
Amee
@MoneyTiririMgwagwa
@MoneyTiririMgwagwa 8 күн бұрын
Munakakamba zoonadi koma osatchula muthu ngat inu mwazindikila muchoonadi munakalalikila pazomwe inu mwazindikila ndi mene mwaphuzilila
@JohnAsendi
@JohnAsendi 13 күн бұрын
Koma amwene ndi makusati mukulankhulana kwanu kwaonesa kuti wabwera kuzalimbana ndi anthu omwe anaphunzira kale kodi tizinena kuti muli PA chiwongoko ndiinu choti muziwe ndi chakuti dini ndi ntchito sizingagwilizane mupite Kwame e mukuwanyozawo samalandila ndalama kutha kwamwezi pomwe Ena inu mumalandila ndiye kumati uza zabwino zomwe akuchita ungokhala zonse ndizolakwika alibe zabwino zomwe akuchita
@Qassimcedrick
@Qassimcedrick 12 күн бұрын
Sheikh kodi mitiuza mu Quran pomwe aletsa kulandira ndalama ukagwira ntchito ya Deen pakati panu ndi ife pali Quran ndi MA hadith atumiki basi palibe zokangana
@JohnAsendi
@JohnAsendi 12 күн бұрын
@@Qassimcedrick mumalandila ndiinu ingo ndiuzani lembalo mu qraan
@JohnAsendi
@JohnAsendi 12 күн бұрын
@@Qassimcedrick mumalandila ndiinu ingo ndi uza lemba mu quraan
KUWACHEPETSA MACHIMO OMWE ALLAH ANAWAKUZA  SH ABOU SUFIAN KHATWEEB DAWOOD
36:36
SHEIKH ABOU SUFIAN KHATWEEBU DAWOOD
Рет қаралды 4,8 М.
ОСКАР vs БАДАБУМЧИК БОЙ!  УВЕЗЛИ на СКОРОЙ!
13:45
Бадабумчик
Рет қаралды 6 МЛН
Sigma girl and soap bubbles by Secret Vlog
00:37
Secret Vlog
Рет қаралды 6 МЛН
Heartwarming moment as priest rescues ceremony with kindness #shorts
00:33
Fabiosa Best Lifehacks
Рет қаралды 38 МЛН
EP 2 KODI SINAKWANE NTHAWI
14:20
SHEIKH ABOU SUFIAN KHATWEEBU DAWOOD
Рет қаралды 1,6 М.
Professor Said Hassan Zambia
3:17
CheNaNaNaH Visuals(Poet Kinanah Jannah)
Рет қаралды 548
PEWANI KUWADA ABWENZI A ALLAH SHEIKH ABOU SUFIAN KHATWEEB DAWOOD
11:59
kumalawi kuno ndani wandale angamake??
1:01:32
Malawian Cameras
Рет қаралды 89 М.
Friday sermon by Sheikeh Fakebba Ceesay havezahullah
42:07
FOCUS AHL SUNNAH IN GAMBIA
Рет қаралды 9 М.