Ndipo chakwera adalankhula yekha pa campaign kuti akadzalephela kusintha dziko adzatula pansi udindo, koma akulephela.
@BrightPhiri-bt6ev3 ай бұрын
Koma iweyo i think anakakupasa u vice president chifukwa zikuwoneka kuti u gardener waku state house siunakusangalase.pamene umadya nawo unali zii siumatisokosela panopa munanyelana uko wayamba kutisokosela kuzimva inu kumakuvutani.lwara unasuzgo yambula kwamba uwongenge kuti uli kugwilapo ntchito ku state house bcoz of chakwela not chilima.
@damianokachingwe35313 ай бұрын
Tamuuzen amvetse ameneyu chidebe chopanda madzi mmesa adakaona ku state chifukwa cha Chakwera not chilima, komanso adakhoza kumulemba as gardener adaona kt mulibe umunthu weniwen
@NthambiInvestment3 ай бұрын
Chakwela mbuzi yeni yeni kupanda chilima bwenzi Ali ndani ,,lero anaiwala mpaka kumuphanso timuona kuti kampeni yaulendo uno aziti chani
Nawenso openga kwambr ukuona ngt voice ya Lwara ingasinthe support ya Chakwera? Support weniwen sasunthika ngakhale Lwara atachezera kulankhula akungovutika chabe siziphula kantha zimenezo
@HalisonSolomon3 ай бұрын
AAAAAA IWE AMENE UKUTI MULUNGU ANAPANGA IMFA NDIPO IMFA IMABWERA NDI CHOLONGA UKUTANTHAUZA CHANI? IMFA YAKE NDIYE SI YACHILIMA IYI IMFAYI MUSAIKEPO MULUNGU UTENGEREPO TCHIMO NDIWEYO IMFA IYI SIYOCHOKA KWA MULUNGU INACHIKA KWA CHAKWERA NDI NDUNAZAKE IWE UNAONAPO NGOZI YA CHITIKA ANTHU NKUPEZEKA MALISECHE OLO NSAPATO KUPHAZI NGOZI YAKE YOTANI , MPAKA MA FONI KUSOWA TIZITI NDENGE NDI YOMWE INATENGA MA FONI AWANTHU AJA ? MUSAKWIITSE ANTHU NANU
@dumisanimoyo31523 ай бұрын
Arwala atifumbireniko ku boma uko ka minda ya press wakuguriska ninja and uyo wakuguriska iyo wakagura kwanja? Fukwa ine pa mayano yano yane nge minda ya press walekere wanthu awo kamuzu wakapokako malo iye wakagura cha wakapoka wawezgereso kuwanthu
@sanuhabdullah59983 ай бұрын
Talk n dont fear only fear God
@MikeManyamba3 ай бұрын
Akunena zoona
@eliffagondewe82143 ай бұрын
Keep on talking Lwara wina achire Kaya a mwa panadol
@YassinAssima3 ай бұрын
Kuimbila ufiti mmanja phuno salota
@HendrickBanda3 ай бұрын
🔥🔥🔥💪
@BlessingsMakalani3 ай бұрын
16:33 💪💪💪
@jamesgama54893 ай бұрын
We need people like you more fire rwala
@JackMvura-ik2td3 ай бұрын
Kuchikamwa uku kudzachita manyazi one day mulibe ndiumunthu maliro tinaika Koma andedwa ndiye mwawazuza ukanati kunena zayesu bolani Koma akulu ndale Mwai pa maliro Pola Moto peza Ina nkhani adaaa usaonekele utsilu wako