Oyimba Akugulidwa Ndi MCP

  Рет қаралды 30,864

Sam Malvitha

Sam Malvitha

Күн бұрын

#malawimusic #politics #mcp #Dpp

Пікірлер: 87
@GiftKananji
@GiftKananji Күн бұрын
Inetu ndigwirizana ndi zomwe dj munyanane wanena anthu sakungo lowa mwa kufuna kwawo koma mphavu za akumidima ndalama yomwe ikugawidwa ku mcp ili ndi chikoka chakumidima
@user-gp10.10
@user-gp10.10 Күн бұрын
Grace Chinga bwera udzawone kuno zijazi😢
@LomezyWhite-vq9bv
@LomezyWhite-vq9bv Күн бұрын
Ndipotu adaulula zija ndi zimenez
@HappyMunthari
@HappyMunthari Күн бұрын
Or onse oyimbawa atapita ku mcp ife ku mpoto sitikuopa chifukwa tikudziwa kuti chakwera sakudziwa kuyendesa dziko
@MosesDicostar
@MosesDicostar Күн бұрын
Athu akusatako ndalama koma ife MCP ayi taikana
@JohnGreen-v8f
@JohnGreen-v8f Күн бұрын
Ngati kwalembedwa kuti pita awine azawina
@CASSIMDinala-z7e
@CASSIMDinala-z7e Күн бұрын
komano boma ili kuli ndalama osati zochedZ
@AaronMsewezi
@AaronMsewezi Күн бұрын
Boma ndi lomweli, zoona, a Malawi chimene tikufuna si president wina koma chitukuko basi , let us work with Chakwera, wonani pa ground
@EsChinombo
@EsChinombo Күн бұрын
Boma ndi lomweli
@FidesChandama
@FidesChandama Күн бұрын
Ndi okha okha a illuminate awa pitani ku masamba awo antchezo mupeza kuti ndi apasi panyanja pompo
@PedroTomas-y9h
@PedroTomas-y9h Күн бұрын
Tamutulukabeeeeeeeeeee
@BilaliJafali-b9x
@BilaliJafali-b9x Күн бұрын
Kodi iwe zandale siziyeni uzingopanga za oyimba
@Chitani100
@Chitani100 Күн бұрын
Ine ndili pano kuvetsela mwa tchelu 😊
@JBMIKEBUNNAYAH
@JBMIKEBUNNAYAH Сағат бұрын
O imba omwe Ali bize kuimba zo yamikila chakwera ameneyo ndi kalu obanda uzimu ma udasi nonse ukuyamikira chakwera chikangawa busa unyenga sikaliyoti okuba anthu osalakwa nonse afiti
@KalongaWhy
@KalongaWhy Сағат бұрын
Koma dan lu iwe ndimuyawo ineso ndimuyawo petoga ryenu bwanawe wamvatu
@InnocentEdasi
@InnocentEdasi 16 сағат бұрын
Ku MCP kuli ndalamah zochuluka kadyeni km never MCP sikuwina,,, inukadyeni zabooka
@PeterChimbayo
@PeterChimbayo Күн бұрын
Just take this note.....OIMBA SANGAWINITSE CHIPANI.......🎉🎉
@PrinceBlessings-bv5bs
@PrinceBlessings-bv5bs 15 сағат бұрын
Onsewo akugulidwa ndi Mcp, zambia, Nigeria, south Africa and Malawi
@VitumbikoKaunga
@VitumbikoKaunga Күн бұрын
guys music industry Nd ya. Bushiri mkuziwa nose. Nde bushiriyo Ndi chikangawa alilimodzi msadabwe. Oyimba , amene salowa MCP Ndi ulendo
@GeorgeMoyo-w9m
@GeorgeMoyo-w9m Күн бұрын
Dziko la malawi ndi la democracy, chovuta ndi chiyani oimba kugwira ntchito ndi boma lolamula? Zaipa lero chifukwa anthuwa akutumikira boma, koma mmbuyo monsemu analipo oimba amene amayamikira DPP, PP, UTM vuto lanu ndi chiyani?
@LameckBanda-gk6ri
@LameckBanda-gk6ri Күн бұрын
Kodi oyimbawa mukufuna azilowa DPP poti ndichipani chakubanja kwanu,akalowa MCP aguridwa Mesa DPP yalamulirako dziko lino 14 years kusinthana pachibare ngati ufumu oyimba makuyimbirani aja mumagura nde mulibe ndalama zogurira ngati mumachikonda chipani chakubanja kwa muntharika athandizeni muwagurire oyimba akunja
@BlessingsmadalitsoShumba
@BlessingsmadalitsoShumba Күн бұрын
😂😂😅😅 oimba abalilalika , Mdyeleni chakwera 😂😂 azalila munthuyu kwabasi, Zachamba izi ma artist wose alowa mcp athela pompa .
@IbrahimPhiri-ky5jk
@IbrahimPhiri-ky5jk Күн бұрын
Paja osewatu anachulidwapo ndi mayi gres chinga ndiye ndi zosadabwisa anthuwa ndi satanic ndintu mosakaika chifukwa zonse zaonekela poyela
@WysonSadiki
@WysonSadiki Күн бұрын
Zikuthanthawuza kut Giboh adawuza Nkasa kuti ku Mcp ndalama yapweka ayi zikomo... basi ife tizidya chitezechi achuke iwowo😭
@AndrewChasweka
@AndrewChasweka Күн бұрын
Oimba alingati opanga sewerotu achina manganya umaona ngat muli limodzi kumapeto umazangomva odya zake alibe mulandu🤣🤣🤣🤣🤣
@NgalizeBanda
@NgalizeBanda Күн бұрын
Agulidwa poti ndi MCP ndi DPP adangolowa ndale zaku Malawi zimenezo mtima wajerasi okhaokha basi
@SimonBanda-b1f
@SimonBanda-b1f Күн бұрын
Oyimba ambiri pano alibe ndalama ndiye akufuna ndalama. Anthu ngati mukufuna kupitiriza kudya chitedze zanu zimenezo
@AminaAfink
@AminaAfink 2 сағат бұрын
Koma abare aziagura athuwo koma vot sazayiwona 2025
@KalongaWhy
@KalongaWhy Сағат бұрын
Koma ghibo ufuse anthu akutulukidwatu oooo wakura watha
@SammyChakwana
@SammyChakwana Күн бұрын
Ukunama aise legacy yavaya.azikufira ndi a mcp akowo aise watha basi in music industry in malawi believe you me.
@JaneHunga
@JaneHunga Күн бұрын
Or chakwera azawine or ayiii koma yemwe wawinayo azakhalabe Apure anthu basi mlungu tiyendereni😊
@chikamandala7436
@chikamandala7436 Күн бұрын
Ndie Pali vuto kod??, opposition ikulephera kuwagula bwanji
@AaronMsewezi
@AaronMsewezi Күн бұрын
Ndi bodza ilo kuti oyimba anagulidwa, nthawi ija Dan Lu anali ku DPP tinganene kuti dpp inamugula? , munthu ali ndi ufulu wolowa ndi kutuluka, ndikudabwa kuti anthu mumangoti a Malawi adabwa zoti mwakuti, aaaaa.
@MaxonKambazithe
@MaxonKambazithe Күн бұрын
Koma agalu oyiimba shaaaa satikonda ifeee amalawi tooonse ambiri oimba aiiiiiiiii niaagule zitsiru apite pamenepo oimba ambiri ukuopa kufa ni satanic money from galu bushiri
@EstherchavulankhomaNkhoma
@EstherchavulankhomaNkhoma Күн бұрын
Komaye mau kukhalangat ugalamule iweyo adzawineyo ndameneadzlamuletu bas
@PatricePhiri
@PatricePhiri Күн бұрын
Akagwele UKo amenewo akufuna angodya ndalama zaphweka ku mcp km zikatha abwelela
@ChrissWtness-e1z
@ChrissWtness-e1z Сағат бұрын
Giboh nyimbo xako timazisatila koma walowako ayi
@MCAnthonyNdau
@MCAnthonyNdau Күн бұрын
Akalowa ku dpp ndekuti sana gulidwe koma mcp agulidwa eti nanunso mukhoza kumagula palibe akukulesani
@SammyChakwana
@SammyChakwana Күн бұрын
Asikefa nde tataya kare muona mukatulusa nyimbozo ine pheeee kumastand
@EstherchavulankhomaNkhoma
@EstherchavulankhomaNkhoma Күн бұрын
Iweso wadziwabwanji kit wasataniki kod aliposo atsogoleri abwino aaaa iwe samala wava
@masterchitabwino898
@masterchitabwino898 23 сағат бұрын
Akuti unali mgwilizanotu ndi oimbawa ndiye ndi ndani safuna moyo kkkk
@NyangwaKoma
@NyangwaKoma Күн бұрын
Asiyeni oyimba akalowe ife sitikupitako popano tiwagwesela limozi
@BandahLemos
@BandahLemos Күн бұрын
Ndilamulo laku satanic onse oyimba akulambila chakwera ili ndi lamulo la bushiri
@WesleyKalimwayi
@WesleyKalimwayi Күн бұрын
Bwino lake ndi oyimba lokoni atatenga ose oyimba Malawi munu sangawine
@HalimaShafie-q9k
@HalimaShafie-q9k Күн бұрын
Dan lu mboloyanu or tinene kut phepwala lwenu mesa ndiwe wachiyao
@AlicksonMakata
@AlicksonMakata Күн бұрын
Mcp ikundigirigisha anthu akuthawa dpp chifukwa cha kalindo
@KentWilliam-r2v
@KentWilliam-r2v Күн бұрын
Mr chikangawa wagwa bsi or atagula oyimba sangawinise zisankho
@JohnmarkNazombe-hi9xd
@JohnmarkNazombe-hi9xd Күн бұрын
PETER MUNTHULIKA AKAWINA NEXT YEAR PLEASE STAY AT MCP ....
@esaMoha-dm4kj
@esaMoha-dm4kj Күн бұрын
Shinkangawaw satanic yinkuphangsa simeneso serious
@LovenessChanza-c5y
@LovenessChanza-c5y Күн бұрын
Inu oimba mwalowa Ku chipani chaku midi a dziwani kuti zanu zada basi
@IbulaMayikolo
@IbulaMayikolo Күн бұрын
Km kupatula banja lakwatu km kwache chisilu Dani luyo
@EsChinombo
@EsChinombo Күн бұрын
Iwetu ukufuna kuti anthu akutame😊 boma ndilomweli man
@AlexKaunda-ny2eg
@AlexKaunda-ny2eg Күн бұрын
Ntaba yakoyija. Uwabaye chijakeseni anawa akuziwe
@RodaLabana
@RodaLabana Күн бұрын
Ndiye nanga giboh akupezekamo bwanji
@LacksonLombwa-b6x
@LacksonLombwa-b6x Күн бұрын
Basi people are after money, leave them
@ChristopherChapeta
@ChristopherChapeta Күн бұрын
Oyimba ake adyelRa ko.a aziwona kapena a zigwira
@ShaneiJames-n1v
@ShaneiJames-n1v Күн бұрын
Kugulidwa sikhani ndiokavotayo😅
@ElishaMkandawire-j7o
@ElishaMkandawire-j7o Күн бұрын
Boma ndilomweli koma pd tkusitha
@MoosaSame
@MoosaSame Күн бұрын
Ndipo satanic yafikapo ku Malawi kkkkkkkkkkk
@GreyMwanyimbo
@GreyMwanyimbo Күн бұрын
Ali ndiufulu olowa chipani chilichonse
@AKAVIHENGOATHOSI
@AKAVIHENGOATHOSI Күн бұрын
Kkkkk koma ndalama ziphesa anthu
@chiletsobisweck5007
@chiletsobisweck5007 Күн бұрын
Ubwino wake sitimadya nyimbo
@AkoneyThomas
@AkoneyThomas Күн бұрын
Koma nanga amavota ndioimba kod 😂
@KondwaniNgoma-o5u
@KondwaniNgoma-o5u Күн бұрын
Asiyeni 2025 boma Dpp
@ElifalaThole
@ElifalaThole Күн бұрын
Nanuso zigulani anu oyimbawo
@SalomeManda-c1i
@SalomeManda-c1i Күн бұрын
Ma chendeyake Dan lu ndi gibo matumbi nose pa ntumbo panu
@SalomeManda-c1i
@SalomeManda-c1i Күн бұрын
Ma chendeyake Dan lu ndi gibo matumbi nose pa ntumbo panu
@thulambale2836
@thulambale2836 Күн бұрын
Dpp iiiiiii yilibe nkhalidwe
@etiennenyandwi058
@etiennenyandwi058 Күн бұрын
falling down of bab lone
@DaguDere
@DaguDere Күн бұрын
Iweso ndiwa mcp eeet
@WilliamChopika-u5b
@WilliamChopika-u5b 2 сағат бұрын
Eeee zilikotu
@starlonJames-qr4xl
@starlonJames-qr4xl Күн бұрын
zilibe ntchito zimenezi
@EstherchavulankhomaNkhoma
@EstherchavulankhomaNkhoma Күн бұрын
Ineyo wakupoto usamat Ifé kupoto ngat unatifusa ai iweyo ndiye wadpp.osat.kupoto ngat tonse ai pangazako
@mikeelmsukwa
@mikeelmsukwa Күн бұрын
Tamutukabe ameneyo
@VitumbikoKaunga
@VitumbikoKaunga Күн бұрын
Ndizaurura ananena
@SimenyeSimkondachirwa
@SimenyeSimkondachirwa Күн бұрын
Sitimadya nyimbo ife or yumba ose akhare ku mcp . Dpp 2025 boma
@SliviaJosephy
@SliviaJosephy Күн бұрын
Ndipo onse oyimba apite ku MCP ko athere komweko kung'onako aziwone ,,,, DPP boma basi
@Alexchikweza
@Alexchikweza Күн бұрын
Big up boys
@ErnestMkambwe-l2g
@ErnestMkambwe-l2g 4 сағат бұрын
MMAWA
@CathreenKadwala
@CathreenKadwala Күн бұрын
Rip Grace Chinga😢
@DaisonPiston
@DaisonPiston Күн бұрын
Zowona
@InnocentMsokera-h1t
@InnocentMsokera-h1t Күн бұрын
😂😂😂😂😂😂😂
@GiftMatiki-cb1tq
@GiftMatiki-cb1tq Күн бұрын
🤕🤕🤕
@NikolasNanawe
@NikolasNanawe Күн бұрын
❤❤❤❤❤
@VeronicaSekobi-is6dk
@VeronicaSekobi-is6dk Күн бұрын
🎉❤
@GiftMaolera-l1g
@GiftMaolera-l1g Күн бұрын
Ziko lapasa
@PaulokossimasiPaulo
@PaulokossimasiPaulo Күн бұрын
Takunvani madala
Oyimba Omwe Anabwera Awiri  Nkusiyana..panjira
9:09
Sam Malvitha
Рет қаралды 16 М.
А ВЫ ЛЮБИТЕ ШКОЛУ?? #shorts
00:20
Паша Осадчий
Рет қаралды 9 МЛН
Watermelon magic box! #shorts by Leisi Crazy
00:20
Leisi Crazy
Рет қаралды 8 МЛН
Oliver Kahn will never forget this humiliating performance by Ronaldinho
10:07
Top 9 Ya  Anthu Olemela Kwambiri Kumalawi
8:17
Sam Malvitha
Рет қаралды 75 М.
How to win a argument
9:28
ajaxkmr
Рет қаралды 570 М.
VOTO CERTO! Discurso de Venâncio Mondlane incomoda Frelimo
20:31
Hold On Angola
Рет қаралды 56 М.
TIKUDZIWENI - 25 FEBRUARY 2019
33:12
Times 360 Malawi
Рет қаралды 108 М.
CRUISE 5 WITH REV ALEXANDER KAMBIRI
46:48
Joab Frank Chakhaza
Рет қаралды 199 М.
А ВЫ ЛЮБИТЕ ШКОЛУ?? #shorts
00:20
Паша Осадчий
Рет қаралды 9 МЛН