Inetu ndigwirizana ndi zomwe dj munyanane wanena anthu sakungo lowa mwa kufuna kwawo koma mphavu za akumidima ndalama yomwe ikugawidwa ku mcp ili ndi chikoka chakumidima
@user-gp10.10Күн бұрын
Grace Chinga bwera udzawone kuno zijazi😢
@LomezyWhite-vq9bvКүн бұрын
Ndipotu adaulula zija ndi zimenez
@HappyMunthariКүн бұрын
Or onse oyimbawa atapita ku mcp ife ku mpoto sitikuopa chifukwa tikudziwa kuti chakwera sakudziwa kuyendesa dziko
@MosesDicostarКүн бұрын
Athu akusatako ndalama koma ife MCP ayi taikana
@JohnGreen-v8fКүн бұрын
Ngati kwalembedwa kuti pita awine azawina
@CASSIMDinala-z7eКүн бұрын
komano boma ili kuli ndalama osati zochedZ
@AaronMseweziКүн бұрын
Boma ndi lomweli, zoona, a Malawi chimene tikufuna si president wina koma chitukuko basi , let us work with Chakwera, wonani pa ground
@EsChinomboКүн бұрын
Boma ndi lomweli
@FidesChandamaКүн бұрын
Ndi okha okha a illuminate awa pitani ku masamba awo antchezo mupeza kuti ndi apasi panyanja pompo
@PedroTomas-y9hКүн бұрын
Tamutulukabeeeeeeeeeee
@BilaliJafali-b9xКүн бұрын
Kodi iwe zandale siziyeni uzingopanga za oyimba
@Chitani100Күн бұрын
Ine ndili pano kuvetsela mwa tchelu 😊
@JBMIKEBUNNAYAHСағат бұрын
O imba omwe Ali bize kuimba zo yamikila chakwera ameneyo ndi kalu obanda uzimu ma udasi nonse ukuyamikira chakwera chikangawa busa unyenga sikaliyoti okuba anthu osalakwa nonse afiti
@KalongaWhyСағат бұрын
Koma dan lu iwe ndimuyawo ineso ndimuyawo petoga ryenu bwanawe wamvatu
@InnocentEdasi16 сағат бұрын
Ku MCP kuli ndalamah zochuluka kadyeni km never MCP sikuwina,,, inukadyeni zabooka
@PeterChimbayoКүн бұрын
Just take this note.....OIMBA SANGAWINITSE CHIPANI.......🎉🎉
@PrinceBlessings-bv5bs15 сағат бұрын
Onsewo akugulidwa ndi Mcp, zambia, Nigeria, south Africa and Malawi
@VitumbikoKaungaКүн бұрын
guys music industry Nd ya. Bushiri mkuziwa nose. Nde bushiriyo Ndi chikangawa alilimodzi msadabwe. Oyimba , amene salowa MCP Ndi ulendo
@GeorgeMoyo-w9mКүн бұрын
Dziko la malawi ndi la democracy, chovuta ndi chiyani oimba kugwira ntchito ndi boma lolamula? Zaipa lero chifukwa anthuwa akutumikira boma, koma mmbuyo monsemu analipo oimba amene amayamikira DPP, PP, UTM vuto lanu ndi chiyani?
@LameckBanda-gk6riКүн бұрын
Kodi oyimbawa mukufuna azilowa DPP poti ndichipani chakubanja kwanu,akalowa MCP aguridwa Mesa DPP yalamulirako dziko lino 14 years kusinthana pachibare ngati ufumu oyimba makuyimbirani aja mumagura nde mulibe ndalama zogurira ngati mumachikonda chipani chakubanja kwa muntharika athandizeni muwagurire oyimba akunja
@BlessingsmadalitsoShumbaКүн бұрын
😂😂😅😅 oimba abalilalika , Mdyeleni chakwera 😂😂 azalila munthuyu kwabasi, Zachamba izi ma artist wose alowa mcp athela pompa .
@IbrahimPhiri-ky5jkКүн бұрын
Paja osewatu anachulidwapo ndi mayi gres chinga ndiye ndi zosadabwisa anthuwa ndi satanic ndintu mosakaika chifukwa zonse zaonekela poyela
@WysonSadikiКүн бұрын
Zikuthanthawuza kut Giboh adawuza Nkasa kuti ku Mcp ndalama yapweka ayi zikomo... basi ife tizidya chitezechi achuke iwowo😭
Koma abare aziagura athuwo koma vot sazayiwona 2025
@KalongaWhyСағат бұрын
Koma ghibo ufuse anthu akutulukidwatu oooo wakura watha
@SammyChakwanaКүн бұрын
Ukunama aise legacy yavaya.azikufira ndi a mcp akowo aise watha basi in music industry in malawi believe you me.
@JaneHungaКүн бұрын
Or chakwera azawine or ayiii koma yemwe wawinayo azakhalabe Apure anthu basi mlungu tiyendereni😊
@chikamandala7436Күн бұрын
Ndie Pali vuto kod??, opposition ikulephera kuwagula bwanji
@AaronMseweziКүн бұрын
Ndi bodza ilo kuti oyimba anagulidwa, nthawi ija Dan Lu anali ku DPP tinganene kuti dpp inamugula? , munthu ali ndi ufulu wolowa ndi kutuluka, ndikudabwa kuti anthu mumangoti a Malawi adabwa zoti mwakuti, aaaaa.
@MaxonKambazitheКүн бұрын
Koma agalu oyiimba shaaaa satikonda ifeee amalawi tooonse ambiri oimba aiiiiiiiii niaagule zitsiru apite pamenepo oimba ambiri ukuopa kufa ni satanic money from galu bushiri
@EstherchavulankhomaNkhomaКүн бұрын
Komaye mau kukhalangat ugalamule iweyo adzawineyo ndameneadzlamuletu bas
@PatricePhiriКүн бұрын
Akagwele UKo amenewo akufuna angodya ndalama zaphweka ku mcp km zikatha abwelela
@ChrissWtness-e1zСағат бұрын
Giboh nyimbo xako timazisatila koma walowako ayi
@MCAnthonyNdauКүн бұрын
Akalowa ku dpp ndekuti sana gulidwe koma mcp agulidwa eti nanunso mukhoza kumagula palibe akukulesani
@SammyChakwanaКүн бұрын
Asikefa nde tataya kare muona mukatulusa nyimbozo ine pheeee kumastand
@EstherchavulankhomaNkhomaКүн бұрын
Iweso wadziwabwanji kit wasataniki kod aliposo atsogoleri abwino aaaa iwe samala wava
@masterchitabwino89823 сағат бұрын
Akuti unali mgwilizanotu ndi oimbawa ndiye ndi ndani safuna moyo kkkk