watsala pang'ono kuika chithunzi cha chilima mkulembapo kuti "Ntchito za manja anga kuikira umboni" kenako mkuzati " boma ndilomweli la chikangawali..........God you make them confess soon
@SamKaposa-i5c3 күн бұрын
😂😂😂😂😂
@JuvenileDebwe-bv8ow10 сағат бұрын
kkkkkk koma big eeee mwamulankhulatu kkk
@amoschataika74403 күн бұрын
Ntanyiwa akamakuwuzani kuti this is not 1964 this is 2024. Shame on you foolish Minister.
Achimwendo banda stop nonsense 😒 😑 🙄 😤 pls you most know this government 🙄 is going 2025 Apm is coming soon to be president of this country Malawi 🇲🇼 😉 🙄 😒 manyizi bwaaaaa dpp is my vote 🗳 boma 2025
@thulanimpphiri68733 күн бұрын
Koma nduna iyi imandibowa ndikamuona ndimaziwa kuti ndawona nduna yopanda zeru yozikweza yozitukumula or Chakwera ali pasi
@Eric-gb9msКүн бұрын
Muli ngati ine big azayambe kumanga iye
@AubreyMatress3 күн бұрын
Ng'ona party manjenje plus ziphwisi nde chomwe awona ndikumaba zinthu za ku India kumafuna kunamidza a malawi koma akuchepa,, malawi wa lero si omunamidza_ anthu awa akudziwa kuti coming 2025 sanunkha kanthu tsano angoganidza zomanamidza anthu😂😂 konseku kuyetsera kut asatulule m'boma koma achedwa atalawira,,, 2025 timanga timbava tonse ta emusipi_just wait and see Angels of God are busy sweeping off and restoring things for 2025
@actuarialscience22833 күн бұрын
Njanji inamangidwa ndi boma la Mozambique koma a Chakwera akuti amanga ndi iwowo. Bodza la MCP ndi loyipa kwambiri.
Mulungu pitilidzani kubweresa chilungamo poyela kuti tisukike maso
@IbrahimMatola-h4i2 күн бұрын
Mbuzi yamunthu chimwendo Banda
@GeophuliesHarry3 күн бұрын
Koma chimwendoyi makolo ake ndi abale alipo... Munthu wochitisa manyazi ndithu
@SanudiTchuma3 күн бұрын
Kalekale anthu ambir asakuziwa internet bodza ilili likanagwira km nowdayz mm apa ndye mwayaluka achi leg
@FelixAaron-jm3ui3 күн бұрын
Actually this guy is a really GOAT
@dalitsohealthchartcorner5498Күн бұрын
😂😂😂😂😂
@KingDavedNkhata3 күн бұрын
Boma la asatan okha okha okuba, kupha ndikunama Zitsirutso ndi zomwe zimazitembelera pomati boma ndilomweri Mulungu akuikani poyera ndipo mukuonanso ulamuliro uchititsa manyadzi Nanga izizi nzichani Malawi di wa 1964 uyu very shame
@FrankKambwani4 сағат бұрын
Chipani cha wanthu amagazi angapezeke bwanji ndi kunena zoona?
@ThomasMGamah3 күн бұрын
That's imeneyo ndikuti you are second Bakili muluzi tv look how explanation well understood listening from Capetown
@HanifiYaumu3 күн бұрын
Tikangositha boma mu September 2025 tikukandani madazio achina chimwendo musaza zomwe mwadyazo
@MathewKalinkhu2 күн бұрын
Zamanyazi, kuika zithunzi za ku India😂😂😂😂😂😂😂 Boma la bodza kuyambila President chakwera mpaka nduna zonse, eish! Malawi ili pa vuto kobasi.
@IsaiahMiSheck18 сағат бұрын
Basi boma loseli kumangoveka athu amoxi moxi achimwendo xikhale ng,oma basi
@AtupeleChitenjeСағат бұрын
Uuuuuuuuuu manyazi bwanji ndi chimutucho simunati munya
@IsaiahMiSheck18 сағат бұрын
Nduna zadyela basi kkkkkk km awa boma ndilomweli lachani lonamali inewo sixoti sanama km boma ili lawojexa
@FidesChandama7 сағат бұрын
Machende ake amenewo akuitenga Malawi ngati 1954
@DennisMdezq2 күн бұрын
Munthu osapangitsa manyaz uyu kapolo kobasi ukuona Ngati 1964 eti Ife ndi ama 1990
@hassanrasheed13792 күн бұрын
chimwendo iwe ndi galu mutu ngati chibazi savage iwe ukuwona ngati amalaei ndife wopepela Ndondotcha ya Achskwera iwe ''zoona'' shaaa 🤔 wadya manyi aise
@DigleDafter2 күн бұрын
Chimwendo uyu 2025 azangothawa bas chifkwa azafera mmanja mwawathu
Apm deserve to be the president of the republic of Malawi achimwendo shame on you
@hassanrasheed13792 күн бұрын
iwe chimwendo nzeru ulibe bolo yako aise iwe ndi muthu wopangitsa manyazi galu 😡 moti mukamapita mayiko enawa simumachita manyazi agalu
@FidesChandama7 сағат бұрын
ang'ona party mwationjeza kwambiri
@juliochiwalo2 күн бұрын
Dziko la malawi liribe utsogoleri nchifukwa kuli mavuto opsa
@FrytonKampira3 күн бұрын
Mcp ndiyaboza , a chakwela atinamiza za njanji ku nsanje a chimwendo banda kutinamiza za nsewu amalawi tinapanga mistake kuvotera mcp
@JuvenileDebwe-bv8ow10 сағат бұрын
Ndale za chitsiru zoona minister?
@ChifundoNinje2 күн бұрын
Minister ochitisa manyazi, muthu wakulukulu kufasa kumalemba zithu zimene akuziwa kt sizakumalawi shame on you
@MandalaChaona3 күн бұрын
Chimwendo Banda Chimodzi mwa Zitserekwete za Ku MCP. Ukulitenga ngati Dzikoli ndi lako. Changokula ichi koma ndichopanda mzeru. Nthawi mkachitsiru tidzakuonera ndi Nyansi zakozo.
@GEORGESITOLO3 күн бұрын
This is not propaganda I checked pa google it's true ndi nsewudi wa ku India 😂😂😂😂😂
@BillyKalambo-jx3vf2 күн бұрын
Vuto ndiloti ku mcp kuli agalu okhokha iyeyu chimwendo ndi mutu wakewo akuzimva udolo aziwanamiza anyau konko
@dumisanimoyo31522 күн бұрын
Kkkkkkkkk koma chimwendo wangokura chimutu chopanda manyazi
Koma mulungu amayika poyera nzisilu ngati chimwendo b galu wachabe chabe athu akufa kumabgonamabe
@JabilumatendewuКүн бұрын
Mutumidźile Dan lu
@juliussamson62123 күн бұрын
SAMALA CHIMWENDO NTHAWI ZINA KUDZACHE NGATI MMENE AMALAWIAN S AKUVERA NDIPO NTHAWI IDZAKHALA YAKO ANY CHIPANI UDZAROWE TIDZAKUTSA NDIKUPATSA MAKOFI OCHULUKA IWE CHIMWENDO BANDA TAKE CARE
@AubreyChiyaya-ty8ge2 күн бұрын
Achimwendo Banda ni mbuli nyani .... pamodzi ndi makolo ake
@HamanjaManyela2 күн бұрын
Ndizoba ameneyi
@AbdulNyambi2 күн бұрын
Nduna anasankha chakwera ndi mbuli zosaziwa chomwe akuchita
@MayesoBikefa3 күн бұрын
Shame on you Richard chimwendo banda
@phillipkazembe72813 күн бұрын
🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣 koma yaaaaaaa MCP muli pa ntchito never ever again
@HevenChiwaya3 күн бұрын
Umbuli wangokula chimutucho koma mulibemo kanthu komanso umbuli akuyesa a Malawi ndi osazindikila amalawi panopa amazisata za technology sungawapusise iweyo chimutu
@gmxplayboy65592 күн бұрын
Kodi a Malawi tidzadzuka liti? Kodi anthu amenewa azingotidoda mpaka liti? Can't we do something together to eliminate this nonsense before 2025 Election? Anthufe ndiye tikutoledwa kupusa ndithu. Vuto lomwe tiri nalo ku Malawi kuno ndi lakuti tiri ndi Opposition Parties yogona. Anyway, who knows? Maybe Otsutsawa akumawoneka kuti ndi otsutsa kumbaliko, but in actual sense they are together with these ruling party fooling poor Malawians