A DAY IS COMING. TAIMON TIPA WILL BECOME ONE OF MALAWI'S GREATEST MUSICIAINS
@marywyson80994 ай бұрын
Amen
@yankhomvahapule75084 ай бұрын
I'm praying for this🥺
@JaneMachemba4 ай бұрын
Ndipo live🥳🥳🥳🥳
@chifunirokachingwe37004 ай бұрын
Ndipo si kale😊
@Pozzijizzy4 ай бұрын
Biggies-wa ndi handsome plus alinkutchena🔥🙌 Anyways nice track keep it up✊🏻
@Ivymulumbe4 ай бұрын
Nyimbo zako zimandipasa chimwemwe pamoyo wanga,may God bless u dear🎉
@Stevengwalamba-pb5fe4 ай бұрын
If you believe that this is pure talent from God like my comment
@westonbanda23174 ай бұрын
My artist
@Andygoz214 ай бұрын
100%
@ShadreckKapangah3 ай бұрын
100%
@MossGass-g1k3 ай бұрын
Yes bro
@KarenBanda-o1z3 ай бұрын
Proud cheba here love this song
@kespor_Destiny4 ай бұрын
Aisee ndiwe Shasha u got talent anthu akuchedwa kuzindikira chimenechi this is great man
@FlorenceMambo-s3eАй бұрын
I like this song❤
@FlorenceMambo-s3eАй бұрын
Nyimbo imeneyi imandilimbikitsa muzambiri, big up 💪
@moffatzyambo31674 ай бұрын
Zambia is proud of you bro 🇿🇲🇿🇲🇿🇲🇲🇼🇲🇼🇲🇼❤❤ I will be liking my comment alone kaili no one will ever like it ❤😂
@ThayneTriq3 ай бұрын
This song made me shed tears 😭😭😭it reminded me of someone 💔I wish u wello dear wherever u r💔 Whenever someone likes this comment I will be coming to watch again and again
@PreciousMoir4 ай бұрын
" Ndiambiri okudalira ndipo akuchulukira ukazisiya adandaula" mawu awawa andilimbikitsa. Nice one iyiyi nyimbo mwakunga Bro🔥🔥🔥🔥💣
@prophetsamuel39474 ай бұрын
I love this song! Keep it up Taimon.
@ElizaMalimweАй бұрын
Kwambr inesot ndipomwe pandilimbikisa kwambr
@FeliMpishi4 ай бұрын
This song.......eeeh🙌 amene tikudutsa nyengo ya nyimboy like my comment❤
@OdettaChaomba4 күн бұрын
Nice song very powerful
@tiongekalaya-js9zk4 ай бұрын
I wish i could give million likes but am advertising it Song of the moment big up
@aungankadzinja4 ай бұрын
Yes Nyimbo zanu Big zimandiwaza havy palibe nyimbo yako yomwe unapala Big up prz Malawi Mulandilen Mu2yo kuno Watifilisa kwambiri
@emmanuelkaputula27334 ай бұрын
This Man is completely talented. I love your music ❤❤.. sending love to you from your die hard fan from Zambia 🇿🇲 ku Chalo 🌏
@DeveliousMasinja4 ай бұрын
Ndipaseni ma like ndipo nthawi yonse ndikabwera ndivera nyimboyi kutengera momwe achulukira ma like❤❤❤❤❤😂🎉
@pauljeanmoyo98704 ай бұрын
osadanda bro
@EdwardChibamboh3 ай бұрын
My favourite ....
@GiftJere-f7w2 ай бұрын
Amen
@BonnyLuhangaАй бұрын
I like this song please ago head❤❤❤
@DalitsoMantawa23 күн бұрын
God bless u bro good talent
@Clemegoldentuarick1014 ай бұрын
Nyimbo ili nd uthenga iyi Ndipo ngat ukufotokoza za ine 🙏🙏🙏 keep it up fadah
@ChifuniroMisiyasi4 ай бұрын
Ndipo mbali yakuno ngt wandiona ine
@Clemegoldentuarick1014 ай бұрын
@@ChifuniroMisiyasimaka apopo poti ukazisiya anthu Ena adandaula... Ndalimbikisika kwambiri 🔥🔥🙏🙏
@PriscillaTalabukhu4 ай бұрын
Nyimbo iyiyo olo kumaimvera daily singakutopese rather kukulimbikisa
@FelistusPhiri-u8x4 ай бұрын
To my own side he is the best so far from Malawi and I love this gentleman songs 🎉 I patiently waited for the full song my cousins from Malawi like my comment
@collenkaunda85794 ай бұрын
Ili ndi luso losakakamiza lija. ❤️ big up young man.
@almasinillanАй бұрын
Keep going Twin brother from another Land 🎶🎶👏🏽
@stanleyzimba81934 ай бұрын
Iwe ndi dolo kwambir Congratulations 🎉❤
@FrankMwaluka3 ай бұрын
Na nyimboyi mmmm repeat the whole day. Kuchita kumveka tseketseke
@AliJawabo-v2q27 күн бұрын
😂😂
@christophermkhize19914 ай бұрын
I love your songs my brother umatimvetsa kukoma osati zandale ndipo usasadzalole zachima Dan luh udzawononga tsogolo, umatiyika pa map nyimbo zako tikamawonela ndi anzathu osamva chilankhulo chakwathu amangovina nawo kamba ka ukhondo osati zojambulila pa phulusa
@HabrilMalaya4 күн бұрын
Ndipo zoona
@AtimaMkwapatira27 күн бұрын
Ndipo live .....okudalila ndi ambiri koma kungoti uzisiye mmmm adandaula nyimbo iyi yandipatsa chilimbikitso ndayikonda❤❤❤
@ChristopherMaxon4 ай бұрын
Kuswa kugwetsa basi , nice song
@JohnKalembo4 ай бұрын
Nyimbo iyiyi eeee muli uthenga wachilimbikitso ❤❤❤❤❤❤
@chifunironjolomole74984 ай бұрын
Your my favorite artist in Malawi your on high level dzina munapanga kale bro
@VioletChikopap4 ай бұрын
Nc song bg boss your number one music yachilimbikiso kwambiri 🎉🎉🎉🎉
@ZebronmaferaHara-p4f3 ай бұрын
Proud of your music big man I like it
@MuzzaishmaelАй бұрын
Iweyoo aseee nde pakufunikaa kukuomberaa bs cz nde eshiii ndili ndi nsanjee utipwetekaa ❤❤❤❤❤❤ God continue blessing u🎉🎉🎉🎉🎉
@rollnummnambala80304 ай бұрын
For example uli mu galimoto yako pamene paja 🔥🔥🔥ingamveke bwino
@ChiokoSarah4 ай бұрын
Ndipo chingakomeditu
@ErnestAllex4 ай бұрын
😂😂😂 ine tikuivela mu mgalimoto ya mmaganizo zanga phee apa ndili pa chingeni
@WiliamMussah14 күн бұрын
This music a very very good 💯 tipilila bas asaaaa you number one seriously ❤️❤️❤️❤️❤️
@norahkaunda21174 ай бұрын
Big up taimon tipa umayimba nyimbo zabwino kwabasi
@peterphiri2613 ай бұрын
Awawa ndi akatakwe pamaimbidwe ndipo nyimbo zawo ndizopatsa chilimbikitso.kudos Mr Meleka n keep it up big man ❤❤❤❤❤❤❤
@aaronchikalipo1014 ай бұрын
Apa ndapeza nyimbo ina ku playlist yanga. You're a blessing to Us ❤.
@LyfordPensulo3 ай бұрын
great message,yandigwira mtima,big up Taimon
@FatimanapawaChapinda4 ай бұрын
Keep fire burning 🔥
@ZerrahRodgers3 ай бұрын
Silidutsa tsiku osaonera nyimbo iyi🔥🔥🔥 keep it up 💃💃
@AnishaAnussah4 ай бұрын
Nyimbo iyi yawona nyengo zanga ndipo ndi ambiridi okhomererawo 🙏🥰
@kizitokambalame5814 ай бұрын
Almighty God, bless this lad for me. I have always enjoyed his music. Big up, day ndiyimozi nfanayi azafikapo pamene amafuna.
@HarrisonDaka-hv2rj4 ай бұрын
Viewing from Zambia 🇿🇲 it's my dedication from my family. But I promise this year I shud overcome my dreams
@johnchilima63514 ай бұрын
That's great 👌Well done and may the good Lord enrage your territory👏👏
@LucyLaiti4 ай бұрын
We got a talented one here in our country ❤❤❤❤❤
@frankgondwe85843 ай бұрын
This is nice Hit Bigman.. work hard. The message is Just too great
@JosephKumwenda-t6l4 ай бұрын
Powerful song brother
@GiftMlauzi-g8z27 күн бұрын
Amen nyimbo yoti ukamamvera kumangomwetulira wekha eeshii❤
@Stanalfred-v3h4 ай бұрын
Zambians let's gather here 🇿🇲🇿🇲🇿🇲 to support this man 🙏
@JohnTembo-z8p4 ай бұрын
❤❤ We're here 🇿🇲🇿🇲🤦👍💕🇲🇼 Zambia Malawi
@HildahDaka-s6s4 ай бұрын
Here
@MercyChirwa-m6kАй бұрын
We ae here❤
@beniyasmbewe52502 ай бұрын
Man ndavula chipewa coz it's mwang'alula 2 much. Congratulations go ahead .
@LovenessChauma3 ай бұрын
My favorite artist.chaka chake ndi chino.ishuta ndithu
@ClementinaIreenTsekaАй бұрын
Iweyo ndi one aise... Nyimbo zatanthauzo❤
@LouisLackson-f4c4 ай бұрын
Iweyo ndi dolo kambirimbiri. Luso ilili ndi mdalitso wako adah
@matiasbanda60124 ай бұрын
This song 🎵 ❤❤❤ achuluka okudelera Ena wokukhomelera kma tiyeee🎉🎉
@LloydBanda-t3k4 ай бұрын
Fadah uli luso kwambiri 🔥🔥🔥🔥
@dytonisaacmalenga35873 ай бұрын
A very powerful song. The message is just good and on time. Keep it up brother.
@FatimaYusuf-k7i4 ай бұрын
Nyamata woziwa kuyimba uyu🎉🎉🎉🎉🎉🎉 ulemu wanu
@GetrudeChione-tp6kx3 ай бұрын
Woow this song is nice Receive your flowers 💐💐💐 Can't wait for the day you will blow pipo will see your talent continue hoping in Jehovah❤
@Sharoshining2474 ай бұрын
Those who are coming from tiktok let's gather here and show some love❤❤❤❤❤🎉🎉
@EdwardMpungalume2 ай бұрын
Nyimbo iyiyi ndi mbambande!!! I like it❤
@tambalahaggebunaya4 ай бұрын
😢😢😢😢 nyimbo iyi waimbira ine pena ndikuti bola ndingozisiya😢😢😢😢😢😢 udindo wakula ndakanika
@patrickphiri33313 ай бұрын
Aisee you we become a legend very touching song🔥🔥🔥
@MoyendaBwanali4 ай бұрын
Komatu ukukamba zoona kungot nyimbo zako zose ndi zamathandauzo , koma iyi ngat ukundinena ine ayi zikomo wandimasuladi choona siine ndekhad
@HappinessBanda-h8w2 ай бұрын
Taimon Tipa will be great one day And may God Almighty keep his life safe always .....u give us hope ❤❤❤❤❤😂😂😂😂
@MonicaMbwera3 ай бұрын
❤❤❤❤❤Ndipo zoona
@ShaibKudzinja4 ай бұрын
Ndkaona anthu amene akumandidalira kumbuyo kwangaku, nyimbo iyi siingachoke pakamwa panga, big up taimo
@LucyThole-b1u4 ай бұрын
nyimbo zopatsa chilimbikitso ,🎉🎉
@EmilyMpira-ib5eg2 ай бұрын
You' re the best Taimon,I wonder why people don't recognize you,but it's my prayer that one day you'll become famous in Jesus name 🥰
@ChimwemweFilimoti4 ай бұрын
Matipatsa chilimbikitso God bless you all time
@manzy1964 ай бұрын
Kunena mwachirungamo ndima konda adh awa amamenya ma hit abwino hvy keep up good job bro 🙏
@ShaxyKalimbuka-ts1km4 ай бұрын
I like this guy ❤
@JaycieKaipa3 ай бұрын
I like you aisee ,,,,, continue nyimbo zako zimandiphunzitsa ndisaname
@GeoffreysVito4 ай бұрын
Ena nde akumati Video silibwino aaa Guyz this is the best video with this type of song. Mukachurkaso zochita mu video ngati iyi zimabisa uthenga wamunyimbo. Kudos Timon💯
@GeoffreyMsiska-h3e4 ай бұрын
Anthu ena anabadwa Ali afiti kale
@PrinceDickson-z5p4 ай бұрын
WOW congratulations all guys tiuzeni zokhuza oyimba a gospel
@TiongeDennisManeno4 ай бұрын
Powerful massage 🙏
@mervisphiri-d3l4 күн бұрын
Very powerful song..... God bless u Taimon
@FannuelNoah4 ай бұрын
Iyiyi nde mwapha akulu big up fada
@KaungaMustafa-x7tАй бұрын
Proud of you brother with best talent...... This is gifted from God Almighty..... Keep it up we are happy with you
@anniemasamba4 ай бұрын
Tiyeeeee iwe tiyeeeee🎉🎉🎉🎉🎉
@kenngondwe5698Ай бұрын
Landed his music today. He's full of life and hope. Thank you. From Zambia
@HusseinMofatt3 ай бұрын
Koma uyuyu nyimbozakezose ndi minyanga yokhayokha mmmm umathaaise
@TriciaHerbert-f2t3 ай бұрын
God bless you my blather❤
@RodrickBonongwe3 ай бұрын
Big up brother
@YotamuQoto-gv7xk3 ай бұрын
So educative song my brother,wandisangalasa ndi nyimboyi. Ndikumakufunira zonse za boo.