Koma azimai chonde samalan popanga zithu kosekutu ndikususuka nda azimuna aweni aaa siii iziii sono mkuziika mmavuto ndithu aa mmalo moti mkapange za ntchito basi busy mukabudula wa bwana lero ndi izi mkulila apa aa mwana ndi mwana basi or atakhara wankazi ndi mwana iwe ukanene mwana ndiwangai mwamuna ngat nzako anabereka zidole iyaaaa wanya nayotu kulibe kugawa usampanse iyaaaa 😅😅😅
Mmmhu Mayi mugaireni zanu chuma mudavomereza mitala amuna Anu Ali moyo
@FrankNyoni-pm3jz6 ай бұрын
What was the final judgment ?
@McDonaldKanyinji6 ай бұрын
As long as the first wife accepted that they were on polygamy, the worth is suppose to be shared according to how many kids each wife has......... but not equal..... Court should observe this.❤
@PaulBambe-m3t5 ай бұрын
Where is the ruling. I need it pliz. Give me a link 😂
I like second wife she had a good question to first wife
@giftthexy6 ай бұрын
Next please
@dinnakabaghe42466 ай бұрын
Iyiyi imakhala Drama koma kuti tiphunzire mmene nkhani amaweluzira mma Court athu, moti muzionera pa MBC TV Monday 5:pm to 18:00. pamakhala nkhani zosiyanasiyana koma anthu ake otenga mbali ndi omwewa. Zikomo
@owenlingwa4 ай бұрын
Mau ngat kaz chiphwanya 🤣🤣🤣🤣🤣🤣
@glorynkhoma4 ай бұрын
Mwanayo athandizidwe bas kms amayi wo ndiopusa kangoona kuti pomwe ndkugwira ntchito pano pari chuma bas ndavomera banja zaziii ndpo musamupase kanthu azikhala konko kumipando yofubwako
@LovenessKathumba-d1mАй бұрын
I need to hear the judgement
@KelvinhenryMatopeАй бұрын
Kkkkkk
@RhodaKalumbi6 ай бұрын
Amen good wafunsa funso labwino mkazi wa mkulu mahule wa ndi anthu oyipa wake kunalibe
@MeltonMumba-rn9mf6 ай бұрын
Exactly
@patrisiobinalison84766 ай бұрын
Uyutu sihule ,mkazi wamkulu pomwe analakwila ndi kuvomeleza mitala
@GiftCMlangeni6 ай бұрын
Mind your tongue remember ngati pali hule ndi abambowo not mkaziyo. Am also aman how can idate wantchito wanga? Mesa amkagwirantchito nde amakapempha banja ngati? Wamkukuyo adavomeleza bwanji mitala nde chitavute nchani kungomugawirako kuti asathe nthawi yaboma? Kungoti ndikupatsa business imodzi or minibus imodzi basi nkhani yatha. Komaso akuiwalakuti chuma chimatha, dzina la abambowo lilindi wamwamunayo, enawo mawanja akakavuta adzamufuna nchimwene wawoyo?? Nanga mayiwa akadzakalamba akaziwa adzakwanitsa zonse zomwe zimafunika mamuna akhalepo?? Mmmmh kuipamtima kukuoneka apa
@nitafraphael23626 ай бұрын
Please part 2
@PamelaSumbuleta4 ай бұрын
Koma chigamulo ndie chikuchedwa bwanji kkkkk
@CeciliaPaulchidule4 ай бұрын
Km kuli zinthu😂😂😂....second wife is so courageous
@peterjoshua25956 ай бұрын
I just like the guy who’s sat behind the accused 😅
Kkkkkk kom tiphana😂 unatan kuwauza amunanuo kt akugawilen chomacho asanamwalile, mukufuna kuzumza munthu ot czikumukhudza
@TakondwaJeleman2 ай бұрын
😂😂😂😂ndikufuna andigayile chuma
@gracechingaresearch-b5v4 ай бұрын
Malemuwo asanamwalire anaenera kupangiratu kalikose pamwana wanuyo mesa mukuti anakugulirani kanyumba basi pangani za business sisi😂😂😂 muchedwa mukalilira chuma kubereka mtsikana sichifukwa iwe ungofuna chuma basi
@ChimwemweEddimael6 ай бұрын
Aah ine I think this is just acting why do I see the same faces on different cases or maybe it's only me 😂😂😂
@corretabanda76856 ай бұрын
Eyaka ndi acting. Akufuna kuti anthu adzipita ku khoti zikaavuta, komanso anthu tidzitengerapo phunziro.
@WAKISANJEGHENJE6 ай бұрын
😅😅😅😅😅🤣🤣🤣🤣🤣❤
@josephgondwe58296 ай бұрын
Nkhanizi ndi za kuMalawi konkuno, I like it kuti you are using Chichewa osati zokhala ndi interpreter.
@gremmerchris715 ай бұрын
Nkazi wachiwiri uziyamika kuti uyu woyambayu anakulola kulowa m'banja lawo komaso pokutenga kuti uzikamugwilila ntchito chokhacho uzimuyamika...usazitenge wapamwamba kwambili kuti wabeleka mwana wamamuna nzakoyo sikufuna koma zidangochitika.. Komaso iwe nkazi woyamba kuti ufike pomwe ulipo dzidatengela nzakoyo kukhetsa thukuta ndikudzichepetsa kwakwe kuti iweyo ukhale umoyo ofewawo muthokoze pomupatsa shop imodzi over time mudzapeza ina basi simple..mukutelo pokuti iye ndiyemwe wasunga nfunda wanu basi
@ShatterNinje5 ай бұрын
Mau omaliza akukhosi kkkk
@MaxwellMagowajmphiri2 ай бұрын
Mmmmmh zowopsa😢😢
@InnocentChisale-jv6ry2 ай бұрын
Good news
@LawrenceTambudzaiChidakwa5 ай бұрын
❤
@mackinlykabaghe36086 ай бұрын
Great!!
@marianyirenda5 ай бұрын
Komano walembedwa ntchito mphaka kumasukilana ndi a bwana wosachita mantha mphaka kuvomeleza kuti mukwatilana yikhale mitala ndi mkazi wa bwana mmmmm koma azimayi muzikhala ndi mantha please
@AgnessMaumbo5 ай бұрын
Akafukule amunache ankamuuza kuti amupatsa chuma adzamupatse,vuto la tsikana amasiya chomwe apitira maso muchanya kwa zimuna aeni ake kkkkk,akamaona nkazi akuoneka bwino amaona ngati akumusamala ndi mwamuna nde kumakhala kuti ndipite nane ndizikaoneka ngati amene aja,osadziwa kuti munthu wamayi amazilombikira yekha kkkkkkk,kuphunzitsa kwabwino amene akuonera atsikana aphunzirepo sure
Vuto lowakhira nkhani pali za uhule apa mesa akuti unali mgwirizano oti ayese zida abambowo amafuna mwana wa mwamuna ndye atafunsidwa amayi akuluwo anavomera kuti vuto palibe atha kukhala pa mitala mwayi uwo mimba mkubwera akabadwe mwana chimphongo ndye kuti mdala Ku khosi mbeeee kuti mission yatheka mwana wa mwamuna wapezeka. Ndye chomuchulira kt ndi hule mumakhala chili chani....?????
@AnnieBillyАй бұрын
Kkkkkk ziliko
@NaomiMagoha-uw7rm6 ай бұрын
Waiting for court ruling
@MilwardChanza-mr4yr5 ай бұрын
Mkazi wachiwiri anakakonda anamkagaila ma percentage angat?
@FrezarSolobala16 күн бұрын
Koma ya
@OviousSili-th5mk4 ай бұрын
Part 2 ilipo kod ?
@KondwaniGumba6 ай бұрын
Ngati adali mkazi wa malemu ndikumuberekera mwana , akufunika kukhara ndi gawo la chuma Cha mamuna wawe. Ndikukhulupirira kuti pakutha pa khaniyi ikomera odandaula.
@FloraGondwe-g9k2 ай бұрын
Amuna akewo anawona kuti zimene amamupangira zinali zomukwanira palibeso chifukwa choti azipitaso kwa mg1 kukafuna chuma chifukwa aliyense anali ndi nyumba yake anthuwa sikuti amakhala nyumba yimozi ayi
@SandikongoSulo2 ай бұрын
Next please
@MussaSwalleyi2 күн бұрын
How is the first wife
@KhalidYusufuАй бұрын
CHUMA cha masiye mkazi Ali ndi gawo lake komanso ana Ali ndi gawo lawo Mzimayi uyu she deserves to have her husband property komano timayang'ana chuma chomwe chomwe chapezeka during her time except mwanayo
@MwaleYankhoKatanga-k3e6 ай бұрын
The first daughter is coming with some juries and want to run away from this as solution
@HenryLaidon-pl9ly6 ай бұрын
1st born wa Dzanja from MG 1 uli ndi umunthu coz pa dziko pano uli ndi brother wako mmodzi from MG 2 komanso ndi mwana musamalire, komano zolinga ZENIZENI za MG 2 PA mlandu wu aaaaaa chabwino tiyeni tione kuti MALAMULO akuti chiyani
I think sanati akufuna chuma chonse, nkona akuti angowagayirako ka gawo chabe
@KelvinhenryMatopeАй бұрын
Maumboni wo akunama court ligamule agawe chumacho thandizopbuyo
@HenlyMusisi2 ай бұрын
Zosezi nkhani yakusatila pamphaso za YEHOVA, akanavomeleza ana akaziwo sibwezi ziliko izi; komaso asikana musamatengeke anayamba kukusalani munthuyu ali moyo; tiyeni tiphuzilepo pankhaniyi.
@AndrewSamuel-eo2mu6 ай бұрын
NdiNanchinditso ameneo 😂😂😂
@JoshuaNgosi4 ай бұрын
Ka nkazi ka ntchito aka ndikamisala.😂😂
@marthachapepa67294 ай бұрын
Share the properties, waiting for ruling
@KelitaMzikamanda5 ай бұрын
😂😂😂😂😂
@HevenChiwaya5 ай бұрын
Nkadzi wa chiwiliyo chuma akanapasidwa ndi mamunawakeyo chifukwa chumacho ndi cha kubanja lalikululo mamuna wanzeru satenga wa kwa Nkazi winabkupitisa kwina akanapanga zawo nthawi imene amunawo Ali ndi moyo😢
Yalakwatu apa kaya tidikile final episode kuti zitha bwanji
@mphatsokauta63876 ай бұрын
palibe kumugawila koma kugawana...100% ya assets yo then awona anthu oyenela kugawana ndangati then aliyense atenge percentage yake. community of property ijayo