THE COURT..(Malawi )🤔

  Рет қаралды 391,006

Malawi News Update

Malawi News Update

Күн бұрын

Пікірлер: 541
@aaronbanda4494
@aaronbanda4494 3 ай бұрын
So interesting! I need to hear the judgement 😅😅
@MussaSwalleyi
@MussaSwalleyi 2 күн бұрын
Uhure umenewo Amati w tchito sakuyenera mugawo ameneyo 😅😅
@STEVENPHAMBALA-o5l
@STEVENPHAMBALA-o5l 5 күн бұрын
Here waiting for judgement
@GetrudeGama-gu5rb
@GetrudeGama-gu5rb Ай бұрын
kkkkkk anakazi alibe tchito atenge dzina ndiwangayu wa mmuna ndikufuna andipatse gawo langa kkk😂😂😂😂😂
@ChristopherKasonya
@ChristopherKasonya 27 күн бұрын
Koma azimai chonde samalan popanga zithu kosekutu ndikususuka nda azimuna aweni aaa siii iziii sono mkuziika mmavuto ndithu aa mmalo moti mkapange za ntchito basi busy mukabudula wa bwana lero ndi izi mkulila apa aa mwana ndi mwana basi or atakhara wankazi ndi mwana iwe ukanene mwana ndiwangai mwamuna ngat nzako anabereka zidole iyaaaa wanya nayotu kulibe kugawa usampanse iyaaaa 😅😅😅
@MwaleYankhoKatanga-k3e
@MwaleYankhoKatanga-k3e 6 ай бұрын
She knows how to explain,this marriage issue
@ishmaelimani3779
@ishmaelimani3779 6 ай бұрын
Apatsidwe gawo lawo mayiwo ,komaso ndasangalala mwayamba kuzenga mulandi mchichewa osati kufuna otathauzila tonse ndachewa 😅😅😅
@aminamussa9835
@aminamussa9835 6 ай бұрын
Point of correction, tose ndamalawi
@marianamwanje8968
@marianamwanje8968 6 ай бұрын
​@@aminamussa9835ndiposo yonse ndachewa ndiye kuti chani eti
@EvelynDamiano-zg9kn
@EvelynDamiano-zg9kn 6 ай бұрын
M'bambo akakhala pa mitala amayenera mkazi aliyense azimupangira zotsogolo payekha ndi ana ake..momwe zilili apapa palibe chifukwa chomwe mkazi wamkulu atengere chuma kugawira mkazi wamng'onoyi..angoyamikanso kut ntsungwana uja wanena kut azimusamala brother wakeyo
@JamesMalemba-tx4uh
@JamesMalemba-tx4uh 6 ай бұрын
Very beautiful I need kumva chigamulo
@ChikhuJustin
@ChikhuJustin 5 күн бұрын
Nice eli njuchi
@Lameckbwanali-l3v
@Lameckbwanali-l3v 6 ай бұрын
To the world ❤
@tiyanjanemazinga2002
@tiyanjanemazinga2002 2 ай бұрын
Kodi chuma apanga wonse in wht way?? Mesa anali watchito n amalandila pakutha pa mwezi?? Khani ndichithandizo pamwanayoo
@ChrispoGawani
@ChrispoGawani 6 ай бұрын
Mwanayu ndi wa m'ng'ono akuyenera kusamalidwa aphunzire school yabwino azigona pabwino chuma adzapanga yekha msogolo m'mayi wa mkuluyi wavuta sapereka gawo la chuma komanso bamboyu analakwitsa osalemba will iyeyo ndiyemwe anayenera kugawa chuma adakali ndi moyo azibambo anzanga tiphunzirepo apa nkhani izi always zimavuta kwambiri
@wishesdominion
@wishesdominion 15 күн бұрын
The daughter is wise and the second wife is wise as well
@MadalitsoBokosi-j3u
@MadalitsoBokosi-j3u 6 ай бұрын
Na ngati wakulu adavomera kt ndi mitala ali mwana wa bambo chuma amupase komaso amupase 25% yamwa make 10%nkhani yatha
@sharifujoe7633
@sharifujoe7633 6 ай бұрын
Camera man is 🏃‍♂️ runner
@ganizanizuze7104
@ganizanizuze7104 4 ай бұрын
The second wife is very genius
@AshleyMbewe-k5z
@AshleyMbewe-k5z 5 ай бұрын
I second with you bro,the rulling is very important
@TabithahLloyd-z4t
@TabithahLloyd-z4t 5 ай бұрын
I don't think kubeleka mwana wammuna chikhale chitonzo pa anzawo , iwo adakangopempha thandizo la mwana osati mpaka chuma chifukwa mkazi wankulu kuvomeleza mitala sindiye kuti chilichose chomwe ali nacho ndye kuti nkazi wango'ono akhale nazo
@KafelaMwale
@KafelaMwale 2 ай бұрын
🤣🤣🤣🤣🤣🤣kutengeka.... mg 2 ndiwe galu.
@kesterkaunda
@kesterkaunda 6 ай бұрын
This is true story or movie?
@JeanBanda-zy6wu
@JeanBanda-zy6wu 6 ай бұрын
Chonde tibweleseleni nkhaniyi timve kuti anagamula bwanji so interesting 😂😂😂 Komabe mwanayo akuyenela kumugawilako chifukwa amayiwa anavomeleza mitala linali banja ndithu akanafuna akanakana kuti mitala sakuifuna kangachepe ampaseko mwanayo
@AnnieChaonekera
@AnnieChaonekera 4 ай бұрын
Mesa nkazi aliyense amakhala kwao Kodi and abambowo aliyense amamupangira zomwe anakwanitsa? Wantchitoto deserves mpando ophotchoka omweo iyaaa
@GetrudeGama-gu5rb
@GetrudeGama-gu5rb Ай бұрын
kkkkkk tizigulila ma toy sizodula zimenezo😂😂😂😂😂
@MakhumboNyasulu
@MakhumboNyasulu 2 ай бұрын
Shaaaaa
@PstriciaGoston
@PstriciaGoston 3 күн бұрын
Mmmhu Mayi mugaireni zanu chuma mudavomereza mitala amuna Anu Ali moyo
@FrankNyoni-pm3jz
@FrankNyoni-pm3jz 6 ай бұрын
What was the final judgment ?
@McDonaldKanyinji
@McDonaldKanyinji 6 ай бұрын
As long as the first wife accepted that they were on polygamy, the worth is suppose to be shared according to how many kids each wife has......... but not equal..... Court should observe this.❤
@PaulBambe-m3t
@PaulBambe-m3t 5 ай бұрын
Where is the ruling. I need it pliz. Give me a link 😂
@pridebihalie
@pridebihalie 4 ай бұрын
Palb chifukwa chogawana katundun( kd munthu wakalimbusidwa nsima Pali chifukwa Choti uzilamulila nsima ya ainake?) Mutayen ameneyo wangotopa nd umphawi aaah 😂😂
@MwaleYankhoKatanga-k3e
@MwaleYankhoKatanga-k3e 6 ай бұрын
The second wife is fully genius,
@gracioussinoya2850
@gracioussinoya2850 6 ай бұрын
Dont forget that she's from ndirande
@ShamilKumwembe
@ShamilKumwembe 4 ай бұрын
Mahuleee kkkk
@hajikasaku6054
@hajikasaku6054 4 ай бұрын
I like second wife she had a good question to first wife
@giftthexy
@giftthexy 6 ай бұрын
Next please
@dinnakabaghe4246
@dinnakabaghe4246 6 ай бұрын
Iyiyi imakhala Drama koma kuti tiphunzire mmene nkhani amaweluzira mma Court athu, moti muzionera pa MBC TV Monday 5:pm to 18:00. pamakhala nkhani zosiyanasiyana koma anthu ake otenga mbali ndi omwewa. Zikomo
@owenlingwa
@owenlingwa 4 ай бұрын
Mau ngat kaz chiphwanya 🤣🤣🤣🤣🤣🤣
@glorynkhoma
@glorynkhoma 4 ай бұрын
Mwanayo athandizidwe bas kms amayi wo ndiopusa kangoona kuti pomwe ndkugwira ntchito pano pari chuma bas ndavomera banja zaziii ndpo musamupase kanthu azikhala konko kumipando yofubwako
@LovenessKathumba-d1m
@LovenessKathumba-d1m Ай бұрын
I need to hear the judgement
@KelvinhenryMatope
@KelvinhenryMatope Ай бұрын
Kkkkkk
@RhodaKalumbi
@RhodaKalumbi 6 ай бұрын
Amen good wafunsa funso labwino mkazi wa mkulu mahule wa ndi anthu oyipa wake kunalibe
@MeltonMumba-rn9mf
@MeltonMumba-rn9mf 6 ай бұрын
Exactly
@patrisiobinalison8476
@patrisiobinalison8476 6 ай бұрын
Uyutu sihule ,mkazi wamkulu pomwe analakwila ndi kuvomeleza mitala
@GiftCMlangeni
@GiftCMlangeni 6 ай бұрын
Mind your tongue remember ngati pali hule ndi abambowo not mkaziyo. Am also aman how can idate wantchito wanga? Mesa amkagwirantchito nde amakapempha banja ngati? Wamkukuyo adavomeleza bwanji mitala nde chitavute nchani kungomugawirako kuti asathe nthawi yaboma? Kungoti ndikupatsa business imodzi or minibus imodzi basi nkhani yatha. Komaso akuiwalakuti chuma chimatha, dzina la abambowo lilindi wamwamunayo, enawo mawanja akakavuta adzamufuna nchimwene wawoyo?? Nanga mayiwa akadzakalamba akaziwa adzakwanitsa zonse zomwe zimafunika mamuna akhalepo?? Mmmmh kuipamtima kukuoneka apa
@nitafraphael2362
@nitafraphael2362 6 ай бұрын
Please part 2
@PamelaSumbuleta
@PamelaSumbuleta 4 ай бұрын
Koma chigamulo ndie chikuchedwa bwanji kkkkk
@CeciliaPaulchidule
@CeciliaPaulchidule 4 ай бұрын
Km kuli zinthu😂😂😂....second wife is so courageous
@peterjoshua2595
@peterjoshua2595 6 ай бұрын
I just like the guy who’s sat behind the accused 😅
@BrightSilumbu-h5n
@BrightSilumbu-h5n 3 күн бұрын
Tiponyele nkhaniyo tiyimalize chonde tione kumene inatela please
@TabiahWisick
@TabiahWisick 4 ай бұрын
Fusolanga kod mayi akut chumachili mmanja mwa anaawo akuyendetsandi ana ngat chuma chawo,tsopano nanga bwanji mboniyoikutiso chuma chili mmanja mwamayi awo sangathe kugawa ?
@NedsonKennedy
@NedsonKennedy 6 ай бұрын
The best way is, write willo b4 pass away 😂
@WilsonPhiri-vl1di
@WilsonPhiri-vl1di 6 ай бұрын
Exactly
@JemayPinto
@JemayPinto 4 ай бұрын
😂😂😂😂😂😂😂
@IsumailaSalanje
@IsumailaSalanje 6 ай бұрын
Kumupatsa gawo lachuma kukhoza kulimbikitsa antchito kumagwa muchikondi ndimabwana.Mngosokoneza mabanja amenewa
@jameswajumpha6790
@jameswajumpha6790 6 ай бұрын
Waiting for next part
@ShaibuMbwana-h2i
@ShaibuMbwana-h2i 3 ай бұрын
Shaibu mbwana 😂😂😂😂😂
@Idrissa-r2h
@Idrissa-r2h 4 ай бұрын
Ndimadikila chigamulo abale please aaaa ndangoononapo bundle sinzaonelaso izi
@StellahChisale
@StellahChisale 6 ай бұрын
Kkkkkk kom tiphana😂 unatan kuwauza amunanuo kt akugawilen chomacho asanamwalile, mukufuna kuzumza munthu ot czikumukhudza
@TakondwaJeleman
@TakondwaJeleman 2 ай бұрын
😂😂😂😂ndikufuna andigayile chuma
@gracechingaresearch-b5v
@gracechingaresearch-b5v 4 ай бұрын
Malemuwo asanamwalire anaenera kupangiratu kalikose pamwana wanuyo mesa mukuti anakugulirani kanyumba basi pangani za business sisi😂😂😂 muchedwa mukalilira chuma kubereka mtsikana sichifukwa iwe ungofuna chuma basi
@ChimwemweEddimael
@ChimwemweEddimael 6 ай бұрын
Aah ine I think this is just acting why do I see the same faces on different cases or maybe it's only me 😂😂😂
@corretabanda7685
@corretabanda7685 6 ай бұрын
Eyaka ndi acting. Akufuna kuti anthu adzipita ku khoti zikaavuta, komanso anthu tidzitengerapo phunziro.
@WAKISANJEGHENJE
@WAKISANJEGHENJE 6 ай бұрын
😅😅😅😅😅🤣🤣🤣🤣🤣❤
@josephgondwe5829
@josephgondwe5829 6 ай бұрын
Nkhanizi ndi za kuMalawi konkuno, I like it kuti you are using Chichewa osati zokhala ndi interpreter.
@gremmerchris71
@gremmerchris71 5 ай бұрын
Nkazi wachiwiri uziyamika kuti uyu woyambayu anakulola kulowa m'banja lawo komaso pokutenga kuti uzikamugwilila ntchito chokhacho uzimuyamika...usazitenge wapamwamba kwambili kuti wabeleka mwana wamamuna nzakoyo sikufuna koma zidangochitika.. Komaso iwe nkazi woyamba kuti ufike pomwe ulipo dzidatengela nzakoyo kukhetsa thukuta ndikudzichepetsa kwakwe kuti iweyo ukhale umoyo ofewawo muthokoze pomupatsa shop imodzi over time mudzapeza ina basi simple..mukutelo pokuti iye ndiyemwe wasunga nfunda wanu basi
@ShatterNinje
@ShatterNinje 5 ай бұрын
Mau omaliza akukhosi kkkk
@MaxwellMagowajmphiri
@MaxwellMagowajmphiri 2 ай бұрын
Mmmmmh zowopsa😢😢
@InnocentChisale-jv6ry
@InnocentChisale-jv6ry 2 ай бұрын
Good news
@LawrenceTambudzaiChidakwa
@LawrenceTambudzaiChidakwa 5 ай бұрын
@mackinlykabaghe3608
@mackinlykabaghe3608 6 ай бұрын
Great!!
@marianyirenda
@marianyirenda 5 ай бұрын
Komano walembedwa ntchito mphaka kumasukilana ndi a bwana wosachita mantha mphaka kuvomeleza kuti mukwatilana yikhale mitala ndi mkazi wa bwana mmmmm koma azimayi muzikhala ndi mantha please
@AgnessMaumbo
@AgnessMaumbo 5 ай бұрын
Akafukule amunache ankamuuza kuti amupatsa chuma adzamupatse,vuto la tsikana amasiya chomwe apitira maso muchanya kwa zimuna aeni ake kkkkk,akamaona nkazi akuoneka bwino amaona ngati akumusamala ndi mwamuna nde kumakhala kuti ndipite nane ndizikaoneka ngati amene aja,osadziwa kuti munthu wamayi amazilombikira yekha kkkkkkk,kuphunzitsa kwabwino amene akuonera atsikana aphunzirepo sure
@FloraMweza-u7y
@FloraMweza-u7y 6 ай бұрын
Next plz
@DesireMphatsogama
@DesireMphatsogama 6 ай бұрын
Apatsidwe chuma chifkwa kuli mwana komanso akaz akuluwo anavomeleza
@JamesMsowoya-cp3lf
@JamesMsowoya-cp3lf 4 ай бұрын
Mxiiiii ndimmene yathera ? No chigamulo kupereka fotseki
@vestarmkandawire6138
@vestarmkandawire6138 6 ай бұрын
Mkazi wa chigololo ameneyo ndi mbuzi,, banja ndi ndalama ndi zinthu ziwiri zosiyana. Mkazi woyamba ayankha bwino kuti adavomereza mwamunayi akhale awose osati chuma. Ndiye huleyo chuma chake ndimwana wamwamunayo. 1 Akumbukire kuti anali wa ntchito wa mayi wamkuluyo 2 wamulakwira kumulanda mwamuna wamwini. Apapa kunena zoona chuma asamugawire ndi wakuba mayiyu. Zikuonesa kuti wapha mwamuna ndiye kufuna chumacho.
@AwufWaria
@AwufWaria 6 ай бұрын
Wolakwisa ndi mayi oyambayo povomereza mitala,chuma chiyenera kugawidwa basi
@FatimaAyami
@FatimaAyami 6 ай бұрын
Mwanvetsa koma inu kapena ndinu achibale a MG1
@macdonaldkorea2928
@macdonaldkorea2928 6 ай бұрын
Inutu ndiodwala, munkhaniyi mwakambidwa zoti wina ndihule? Iwe momwe umkabadwa makolo akowo anakwatirana mwadongosolo? Kumasata nkhani osati mopusa.....
@macdonaldkorea2928
@macdonaldkorea2928 6 ай бұрын
@@AwufWaria nkhani koma imeneyi ndithu.....
@johnssanamah1408
@johnssanamah1408 6 ай бұрын
Vuto lowakhira nkhani pali za uhule apa mesa akuti unali mgwirizano oti ayese zida abambowo amafuna mwana wa mwamuna ndye atafunsidwa amayi akuluwo anavomera kuti vuto palibe atha kukhala pa mitala mwayi uwo mimba mkubwera akabadwe mwana chimphongo ndye kuti mdala Ku khosi mbeeee kuti mission yatheka mwana wa mwamuna wapezeka. Ndye chomuchulira kt ndi hule mumakhala chili chani....?????
@AnnieBilly
@AnnieBilly Ай бұрын
Kkkkkk ziliko
@NaomiMagoha-uw7rm
@NaomiMagoha-uw7rm 6 ай бұрын
Waiting for court ruling
@MilwardChanza-mr4yr
@MilwardChanza-mr4yr 5 ай бұрын
Mkazi wachiwiri anakakonda anamkagaila ma percentage angat?
@FrezarSolobala
@FrezarSolobala 16 күн бұрын
Koma ya
@OviousSili-th5mk
@OviousSili-th5mk 4 ай бұрын
Part 2 ilipo kod ?
@KondwaniGumba
@KondwaniGumba 6 ай бұрын
Ngati adali mkazi wa malemu ndikumuberekera mwana , akufunika kukhara ndi gawo la chuma Cha mamuna wawe. Ndikukhulupirira kuti pakutha pa khaniyi ikomera odandaula.
@FloraGondwe-g9k
@FloraGondwe-g9k 2 ай бұрын
Amuna akewo anawona kuti zimene amamupangira zinali zomukwanira palibeso chifukwa choti azipitaso kwa mg1 kukafuna chuma chifukwa aliyense anali ndi nyumba yake anthuwa sikuti amakhala nyumba yimozi ayi
@SandikongoSulo
@SandikongoSulo 2 ай бұрын
Next please
@MussaSwalleyi
@MussaSwalleyi 2 күн бұрын
How is the first wife
@KhalidYusufu
@KhalidYusufu Ай бұрын
CHUMA cha masiye mkazi Ali ndi gawo lake komanso ana Ali ndi gawo lawo Mzimayi uyu she deserves to have her husband property komano timayang'ana chuma chomwe chomwe chapezeka during her time except mwanayo
@MwaleYankhoKatanga-k3e
@MwaleYankhoKatanga-k3e 6 ай бұрын
The first daughter is coming with some juries and want to run away from this as solution
@HenryLaidon-pl9ly
@HenryLaidon-pl9ly 6 ай бұрын
1st born wa Dzanja from MG 1 uli ndi umunthu coz pa dziko pano uli ndi brother wako mmodzi from MG 2 komanso ndi mwana musamalire, komano zolinga ZENIZENI za MG 2 PA mlandu wu aaaaaa chabwino tiyeni tione kuti MALAMULO akuti chiyani
@zimmekapachika6784
@zimmekapachika6784 6 ай бұрын
Kwakoma ndikuno😅😅😂😂😂😅😅
@kanyengamatress6130
@kanyengamatress6130 4 ай бұрын
Akazi achiwiri skut muzit mutenge chuma chose aiii nkhan ndiyot akugairen gawo lanu basiii awoso akuyener kuperek ndinth
@WillardPatrick-h9s
@WillardPatrick-h9s 4 ай бұрын
I think sanati akufuna chuma chonse, nkona akuti angowagayirako ka gawo chabe
@KelvinhenryMatope
@KelvinhenryMatope Ай бұрын
Maumboni wo akunama court ligamule agawe chumacho thandizopbuyo
@HenlyMusisi
@HenlyMusisi 2 ай бұрын
Zosezi nkhani yakusatila pamphaso za YEHOVA, akanavomeleza ana akaziwo sibwezi ziliko izi; komaso asikana musamatengeke anayamba kukusalani munthuyu ali moyo; tiyeni tiphuzilepo pankhaniyi.
@AndrewSamuel-eo2mu
@AndrewSamuel-eo2mu 6 ай бұрын
NdiNanchinditso ameneo 😂😂😂
@JoshuaNgosi
@JoshuaNgosi 4 ай бұрын
Ka nkazi ka ntchito aka ndikamisala.😂😂
@marthachapepa6729
@marthachapepa6729 4 ай бұрын
Share the properties, waiting for ruling
@KelitaMzikamanda
@KelitaMzikamanda 5 ай бұрын
😂😂😂😂😂
@HevenChiwaya
@HevenChiwaya 5 ай бұрын
Nkadzi wa chiwiliyo chuma akanapasidwa ndi mamunawakeyo chifukwa chumacho ndi cha kubanja lalikululo mamuna wanzeru satenga wa kwa Nkazi winabkupitisa kwina akanapanga zawo nthawi imene amunawo Ali ndi moyo😢
@ShamirahMakungwa
@ShamirahMakungwa 6 ай бұрын
Munthu utha kuvomera mitala malingana ndinyengo mmene iliri...vuto ndimalemuo coz sitikuziwa kuti ankagwirizana chani ndiwantchito wawo akakhala awiri.kmanso ngati inali mitala mamuna amapanga equal popanga zithu.iwowo kod sanasiye will...
@aminamussa9835
@aminamussa9835 6 ай бұрын
tikudabwa nanu enanu ma comment anu mmalo moyakhula zinthu zomanga zadzelu, muli busy kumunyoza nkazi wachiwiliyu anthu mukuzimvela nokha kuti anavomelezana mbali zose ziwili khani yamitala sono wasanduka bwanji kukhala hule! Chomwe mukumunyozela munthuyo ndichani? munthu pozindikila kuti zapadziko ndazakutha chovuta ndichani kumugawilako gawo lililoselo kuti naye asangalale ngati njila imodzi yoyifunila zabwino business kuti ikhale ndimadalitso pokana zokokanakokana
@ashadokhomzy
@ashadokhomzy 6 ай бұрын
Yalakwatu apa kaya tidikile final episode kuti zitha bwanji
@mphatsokauta6387
@mphatsokauta6387 6 ай бұрын
palibe kumugawila koma kugawana...100% ya assets yo then awona anthu oyenela kugawana ndangati then aliyense atenge percentage yake. community of property ijayo
@mustazahra8398
@mustazahra8398 6 ай бұрын
Part 2 please
@MalawiNewsUpdate
@MalawiNewsUpdate 6 ай бұрын
@@mustazahra8398 kzbin.info/www/bejne/rpW8cqWufsh_isksi=RBymCehao5Kz1SCU
@DavidChapalala-i2g
@DavidChapalala-i2g 6 ай бұрын
Nkhan yabwino kwambiri 😂😂😂😂😂😂 Chumacho ndi cha onse ndipo akuyenera kugawa bas
@FrankKambwani
@FrankKambwani 6 ай бұрын
Comedy iyi
@gracejere452
@gracejere452 6 ай бұрын
Mboni yufanana ndi step mom😂😂😂
@apollochikoza5737
@apollochikoza5737 6 ай бұрын
Ndipo ndendende ndi dzala zomwe😂😂
@PhyllisJiva
@PhyllisJiva 6 ай бұрын
😂😂😂😂😂😂
@SebastiaoErnesto-mh6ec
@SebastiaoErnesto-mh6ec 6 ай бұрын
😢😢😢😢😢😢
@MikePetros-e7m
@MikePetros-e7m 6 ай бұрын
❤ Mai awa sakuyakhura mwanzeru'!!
@MustafaAmeen-tb6wd
@MustafaAmeen-tb6wd 6 ай бұрын
Ngat nkazi anavomeleza mitala akuyenela amugawileko nzakeyo chumacho, congratulations ku mboni athandizedi mlongo wakeyo kuti naye azafike ngati pomwe ali iyepo
@TakondwaJeleman
@TakondwaJeleman 2 ай бұрын
Abale Kodi ndisewelo kapena chan
@PeterJafari
@PeterJafari 5 ай бұрын
Kodi anagamula bwanji guys ine ndikusaka koma sikupezeka koma mkadzi wang,onoyi akuyenera amupase ngawo lake ndithu
Prophet Uyu Walosera Zoopsa Pa Zisankho Zikubwerazi ... Tanvani
27:34
Sam Malvitha
Рет қаралды 103 М.
REVIVAL CRUSADE
7:49
Katondo C.C.A.P Church-Dzenza Presbytery
Рет қаралды 43
New Colour Match Puzzle Challenge - Incredibox Sprunki
00:23
Music Playground
Рет қаралды 44 МЛН
Горы Бесплатной пиццы
00:56
Тимур Сидельников
Рет қаралды 8 МЛН
Last Person Hanging Wins $10,000
00:43
MrBeast
Рет қаралды 151 МЛН
Main Street UMC 250209
55:54
Main St UMC Kokomo
Рет қаралды 1
Usauver S09E02   AKAZANU ASOWA
16:28
Piksy TV
Рет қаралды 255 М.
NDATAYA - Episode 174
10:28
CHE MANDOTA COMEDIES
Рет қаралды 118 М.
THE COURT (Malawi)
24:46
Malawi News Update
Рет қаралды 112 М.
Chifukwa Chimene Anthu Amamudera Miracle Chinga
11:55
Sam Malvitha
Рет қаралды 323 М.