Manganya is good at this koma ku ndaleku aaaaa ndimaona kuti sakumasuka bhobho 😊
@AniyaChapola-gy3td27 күн бұрын
Mkazi samalawidwa kkkkk,Manganya mwaphunzitsatu
@user-ly6eg7zk1s28 күн бұрын
Kajambuleni kawiri we want the real tikuferanji not politics
@KasanjeManess28 күн бұрын
Kkkkk 😂 so ❤ zakwathu more nice 🇲🇼👊🤞
@PrescotMwafulirwa21 күн бұрын
Bravo manganya utumbuka sungathe🎉🎉
@SimoniChimpeni27 күн бұрын
DR MANGA MY VP MUMAKANA
@user-qq1uj7ct6n28 күн бұрын
watching from Capricorn Cape town
@user-ux8bc6wy1i28 күн бұрын
Manganya sewero labwn bwn wayamba kulowesa ndale
@AndsonMaundha28 күн бұрын
You're coming old manganya just because muli m'boma
@Ritta-cj2jw15 күн бұрын
Watching after he been made Vice President
@PrinceBlessings-bv5bs10 күн бұрын
😂😂😂😂 Ndaone mochedwa atakhala kale pa vice president. Anyway u perform well
@kastenyokonia953824 күн бұрын
Watching from Johannesburg olifantsfontein
@yonawillardgreyciam624127 күн бұрын
😂😂😂😂 manganya anakonza nthawi Zina zimamveka zongosekesa chabe koma ayi ndithu zili ndi thandauzo
@AndrewMaloya-wf7lo28 күн бұрын
A Namalawa 😅😅😅 great piece of advice
@AngelaTebulo15 күн бұрын
Komano ndiye muzitipangirabe sewelo Dr Manga
@damianojbanda419628 күн бұрын
Kuganiza mwakuya Maso anga adali kwa a Chitsi sindimadziwa kuti angapange Khomani!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!! Kunena zoona nthawi yatha tisamachedwe ndi kukokana
@GraceLefiat15 күн бұрын
Mumakwana a vp😂
@user-ux9ik4zr5x13 күн бұрын
Mlelemba akukwatanitsa Nkhwasala😂😂😂
@rosekumbangarose353528 күн бұрын
Manganya those were the days kale lathu 😂🎉
@MisheckNamagowa27 күн бұрын
My best ever My home boy
@SparrowBanda28 күн бұрын
Kkkķkkk mmakwana madolo inuyo more respect
@jonathanchirwa329727 күн бұрын
Live Long sir usi
@vitumbikocobysinyiza-511628 күн бұрын
Ndale zoli apo manganya amatha kuyambila kale koma uwu unali msonkhano wa ndale
@user-ly6eg7zk1s28 күн бұрын
Paja nae alikomweko akudya nawo
@MosesSolomoni28 күн бұрын
Tinkawakonda amanganya km pano kkkkkkkkkk anatha analowa ndare opusa iwe manganya
@OjesjGande27 күн бұрын
Manganya
@AlliUsuman-mj1mr27 күн бұрын
Ulemu wanu avep
@FaithSinyangwe-jw6cm28 күн бұрын
😂😂😂Manganya ndigalu kwabasi
@EmmyYafete11 күн бұрын
Palibe ndatola ky ndikuuma mutukwanga ky😂😂
@Martha143628 күн бұрын
Achisi ndimangoti alankhula zosanveka.
@GiiiKatekesa28 күн бұрын
Kkkkkkkkkk mmmmm manganya wadiwonjeza mpaka akapa iwe tikumana tikalowesa zoma lathu ndilinawe ntchito
@user-zy8xo2nb8d28 күн бұрын
Mumakwana inuyo ❤❤❤❤
@user-od9wh3iu9w26 күн бұрын
Km manganya mmmm iwe anakoza
@user-el3yo9sf2s27 күн бұрын
Manga you're one
@SamukLungu-zg7fl28 күн бұрын
Zopusa basi ndare pa sewero
@gidyonmshani525928 күн бұрын
Manganya ipatseni moto
@inessmsiyambiri851728 күн бұрын
Kakakakakakak ndaswekaa koma manganya kkkkkkk
@ForsterThawan28 күн бұрын
Manganya iweyo umakwana
@AcksonBanda-zr7fh16 күн бұрын
Panotu akuti vp koma kkkkkkk
@user-wm7db8zx6g28 күн бұрын
Kkkkk❤❤❤❤ more
@yaledigondwe-lz5yg28 күн бұрын
Salute
@immaculatechitsakamile25228 күн бұрын
Manganya kumtima mbee...😂
@AlexMaganga-ul3vq28 күн бұрын
Anamalawaaaaaaaa!!!!!!!!!
@nevabikinosi619719 күн бұрын
😂😂😂😂 ndiye mwati knomani?😅😅😅😅😅
@ElizaDema-ce5jh27 күн бұрын
Zopusa izi ndale pasewelo
@haroldchirombo791828 күн бұрын
Yomweyoooo 🎉
@Allieshaibu861228 күн бұрын
Ayambitsa nyimbo asa kudabwa2 ine
@user-bl4mr4tu3l28 күн бұрын
Kdi ndye paulo atulukira liti😊
@jameschibisa143328 күн бұрын
Inuyo zoti ndi a honourable sizimadziwika munthu odzichepetsa koopsa I 👍 you Dr manga
@mranzeru28 күн бұрын
Bring back ma sikono
@hassammaulana452928 күн бұрын
Ai zikomo
@NgomaRaheem27 күн бұрын
Zopusa zeni zeni
@chiletsobisweck50078 күн бұрын
Riiiiiiih khomani😂😂😂😂
@asiyatujuma550727 күн бұрын
Eeeeeee ziliko
@patrickmoffat960928 күн бұрын
timakusatani mwalowesa ndale😊
@AcksonBanda-zr7fh16 күн бұрын
Mfumu kadzi ndawonatu ananyoni
@ZdjamalikarimAbdul-im6px26 күн бұрын
Abale Nyoo Ali kuti???
@AcksonBanda-zr7fh16 күн бұрын
Ruth similar AKA make sikono
@Allieshaibu861228 күн бұрын
Akuluwo kd saima kuvuna nao aaaaa
@aminajalabuni284528 күн бұрын
🎉🎉
@patrickmoffat960928 күн бұрын
kapeni for tonse
@madalitsoonale533828 күн бұрын
Munalowetsa ndale akulu inu
@tomthompson442928 күн бұрын
🔥
@JosephChitseko-ro9fv28 күн бұрын
Waikamo zandale basi ingotsiyani amaganya
@llewellynkhungwa471228 күн бұрын
"Munthawi yosiliza" 🤔
@FaraiMatandika27 күн бұрын
Ili sisewele la tikufelnji koma kuteteza udindo wanu nkulu mukuononga drama group ndi ma politics anuwo moya
@user-eo9pt5oc9v28 күн бұрын
😂😂😂😂😂😂 koma
@morganchisama74646 күн бұрын
Come on Mr VP we proud of u not chakwera
@user-fy6fs9uq1w28 күн бұрын
Mmmm zalowa ndale
@chiletsobisweck50078 күн бұрын
Kutsegula comment box kufuna kutitapa mkamwa😏🙄
@user-if3pe9mp4l28 күн бұрын
Anali kale awa
@sharrifgwape716928 күн бұрын
😂😂😂😂😂 tikuferanji kapena nsonkhano wa ndale
@user-ly6eg7zk1s28 күн бұрын
Ndimaganiza ngat nduwona ndekha
@LuundoJohnkabage28 күн бұрын
Msonkhano ndipo azathuwa sakuona vto poti akudya musavutikila ngat ife ife timagobola basi
@HashimMussa-ms4nq28 күн бұрын
Ndale
@RobertGoliat-gt2qh27 күн бұрын
Bamboo a sikono ajaa
@user-xp9zd1wk8g28 күн бұрын
Mwazilowesa ndale
@user-ly6eg7zk1s28 күн бұрын
Ndipo kwabas ya week ino yalowa ndale zedi
@user-xp9zd1wk8g28 күн бұрын
@@user-ly6eg7zk1s ndipo sizinabebe taaa
@user-xj2yg7hb1n28 күн бұрын
Mbola
@YusuffuDaud-cs7yu28 күн бұрын
Where is Mr nyo
@yamikanifischer28 күн бұрын
Mukuononga mbili yanu chifukwa chandalama
@user-qs2tx7wt6g28 күн бұрын
Gindee
@alexpetros402127 күн бұрын
Tikufelanji anasiya kubeba ndale too much
@alishahid-rc1ru28 күн бұрын
😂😂😂
@Lloyd-gd6pu28 күн бұрын
Mimba nkagunde chigololo salawa
@alexsumani682328 күн бұрын
Koma Honourable Manganya
@JosophineKavute28 күн бұрын
Ipatse motooooo
@llewellynkhungwa471228 күн бұрын
Alinse Ali ndi mutu wachewache achinyamata musamale
@prayer-room3528 күн бұрын
Boma losaopa Mulungu, zitheka bwanji kuti Ampingo alowererepo, kodi akanena chilungamo mungakhonze kuchimvera ? Atanena kuti Mulungu akuti president aime , chakwerayo angaime? Kumbukilani Mfumu Ahabu ... Adauzidwa ndi mneneri Mikaya zooona zake zomwe Mulungu wanena koma adasankha kusamvera , ndiye mundiuze inuyo kuti chidamuchitikira Mfumu Ahabu ndichiyani ! Adafa chifukwa chonyoza mau a Mulungu! Momwemo the current government will surely die 😢
Mu dziko lino lapansi tili ndi soka lalikulu! We will surely die in the way zamasiku otsiliza... Ndilibe kanthu ndi munthu , ndili ndi kanthu ndi moyo wanga ndi onse akumvera chenjezo la Mulungu ndi kuyenda m'menemo! How would you say inu ndi Mulungu! Just worried of asking this such question
@patrickmoffat960928 күн бұрын
mangqdyq and mulemba don't talk nonsense musazitenge Malawi ndioupusa
@LuundoJohnkabage28 күн бұрын
Akudya bwino akalephele kusangalala😢
@promisemakawa155628 күн бұрын
This is tikuferanji or politics??? Stop talking abt politics plz, sewero munaliyamba bwino koma mwalowetsanso ndale
@user-qq1uj7ct6n28 күн бұрын
Koma mikuluwiko ili umu eishií bwana Michael usi ndi group yanu ai ai mumatha. ❤️❤️❤️❤️ watching from Capricorn Cape town
@SmartNoxy28 күн бұрын
I think it's better to stop acting tikuferanji not boring like this.we don't need ndale tikufuna tikuferanji yachikale yokamba Za HIV and AIDS
@MadalitsoDindi-ir6vj28 күн бұрын
You have just wasted my bundle with your boring drama. A drama full of politics asah
@Thembokatuli28 күн бұрын
Why u open
@trindersausa152628 күн бұрын
My question
@user-ly6eg7zk1s28 күн бұрын
100 percent
@MadalitsoDindi-ir6vj28 күн бұрын
I thought ndi Tikuferanji without knowing Kuti ndi Tonse alliance
@Midy26527 күн бұрын
I don't know why I always think of entertainment other than politics...I found it fun.😂