TIMOTHY MTAMBO KUTHAMBITSIDWA NDIMAFUNSO UKU...

  Рет қаралды 55,019

LIKI-LIKI TELEVISION

LIKI-LIKI TELEVISION

24 күн бұрын

Пікірлер: 320
@GiftShugah
@GiftShugah 2 күн бұрын
Mtambo iweyo ndi machine and I support you
@GraciousMollys
@GraciousMollys 22 күн бұрын
Leyah ndi akatundu 😂😂😂😂😂😂 she born for journalism guyz kkkk
@user-rk4ch1ly3z
@user-rk4ch1ly3z 22 күн бұрын
A mtambo asaname kuti amamenyela ufulu wa dziko zaboza,amamenyela ufulu wake panopa ma demonstration adzipanga yekha.palibeso kukusatila.
@RobertDJambo
@RobertDJambo 22 күн бұрын
Mbuzi iyi akuvekaso ngat m'bulunditu
@KenChitete-pg3ws
@KenChitete-pg3ws 18 күн бұрын
Ended mutambo you went to school because your point is touching me in my heart.
@user-mr5yb4en2u
@user-mr5yb4en2u 22 күн бұрын
I don't see any reason why mtambo should apologise. Everyone was angry due to election ridging why should he apologise think properly as a real citizen of the country not as a puppet.
@coastersRob
@coastersRob 22 күн бұрын
Mtambo mutu wake wazaza zinyasi chifukwa sakuziwa kuti amalawi ndi okwiya naye mpaka pano ndiye kaya ngati anthu samupasa makofi ndikukayika ndipo aziyenda okozeka
@user-lv9vf6rf8r
@user-lv9vf6rf8r 16 күн бұрын
Leya ndakutayira kantengo. Keep it up.
@upfmalawi3859
@upfmalawi3859 17 күн бұрын
This is real frank talk. Thank you Commander in Chief.
@RobertLuka-wy9cl
@RobertLuka-wy9cl 22 күн бұрын
Inenso lero ndikutukwana iweyo machende ako ndi munthu opusa kwambiri
@lillianmwanza4218
@lillianmwanza4218 21 күн бұрын
Welcome bak wakukaya....nkhani njakuti when u are on top u bcome a topic
@mikemjuwen8025
@mikemjuwen8025 8 күн бұрын
Mau comrade wayankhulawo
@MCDONALDTHENGENDE
@MCDONALDTHENGENDE 6 күн бұрын
Uyuyu ndi mbuzi ,,,fisi wake ndiyemweyi sadasinthe mawanga........ Nyimbo zake ndizomwezija sitikuvinanao plz
@user-mr5yb4en2u
@user-mr5yb4en2u 22 күн бұрын
Mtambo helped us to know our voting rights some people who ridged the election and the courts ruled in favour of what mtambo was demonstrating for long live pagonachi mtambo!!!!!!
@georgechithumba530
@georgechithumba530 22 күн бұрын
😂😂😂😂
@juliusnjerengo2610
@juliusnjerengo2610 22 күн бұрын
You have a small knowledge
@user-mr5yb4en2u
@user-mr5yb4en2u 22 күн бұрын
People like Brian Banda and Jorge kasakula even now Nicholas dausi is saying they're the ones who helped this government but we don't put blames on them we only blame one man from the north why?
@innocentchisanga3334
@innocentchisanga3334 22 күн бұрын
Mzeru za Bakha
@AndrewChitani
@AndrewChitani 15 күн бұрын
Unatikhumudwisa mtambo
@KelvinWasuliya-yr1ct
@KelvinWasuliya-yr1ct 14 сағат бұрын
Kod iyeyo akulankhula ngat m mwenye ndi malawi iyeyo
@Creslevison-vj2sl
@Creslevison-vj2sl 22 күн бұрын
Kupusa uku isaaaa
@saadisadie3125
@saadisadie3125 7 күн бұрын
Mbava iwe
@YankhoGuza
@YankhoGuza 22 күн бұрын
I now believe that Mtambo ndi m'bulundi as it was said by Charles Ben Longwe it is really true ndipo galuyu Chichewa chake chikumvekeratu Kuti munthuyu ndi foreigner.
@johngrem2838
@johngrem2838 22 күн бұрын
M'Burundi weni-weni uyu guys ndipo ndi galu kwabasi
@allannthengu2239
@allannthengu2239 22 күн бұрын
Indeed Aford brought Democracy but you brought Distribution
@user-lu8px7td6p
@user-lu8px7td6p 22 күн бұрын
Uyuyu asatinamize uyu mtambo ndi mfiti wachabechabe garu
@user-zg9se4rw6v
@user-zg9se4rw6v 8 күн бұрын
Very clear Mtambo, not vakunyoza, but to build
@DymonSubiliLangboy
@DymonSubiliLangboy 15 күн бұрын
Rober
@user-tz4xw3bd1v
@user-tz4xw3bd1v 14 күн бұрын
Opoira uyu
@SamsonLynfordmpnda
@SamsonLynfordmpnda 22 күн бұрын
Asatinamize uyo ndiwausili aona kt anamuchotsa pa udindo bans mkulira kwatsalaku
@user-kj6qj1md5e
@user-kj6qj1md5e 22 күн бұрын
Aaaa akuphe kumene galu iwe okay udzanya one day aise
@AndrewLangwe
@AndrewLangwe 22 күн бұрын
Koma mtambo ndimbuzi kwabaaaasi
@user-kj6qj1md5e
@user-kj6qj1md5e 22 күн бұрын
Amalawi agalu awa asatipusitse ifeso tinakula ndipo sife opusa wava iwe awa akumenya kampeni agaluwa alilimodzi chenjelan amalawi dpp oyee awa asatinyase alilimodziose agalu awa
@yeletsanwilson9792
@yeletsanwilson9792 20 күн бұрын
🤣🤣🤣🤣
@WilsonWilsonZimba
@WilsonWilsonZimba 15 күн бұрын
Wabozayo manyanzi amenewo
@SaidNefitary
@SaidNefitary 22 күн бұрын
Koma ntamboyi ndi zikad WA kumarawi Chichewa chakechi guys
@LongiMtimabii
@LongiMtimabii 22 күн бұрын
Ndipo sungati pusisenso ubwelele kwanu ku congo
@user-qq1uj7ct6n
@user-qq1uj7ct6n 21 күн бұрын
Kkkkkkkkkkk ndiwakut Congo? 😂😂😂😂
@martinzicogaga5248
@martinzicogaga5248 22 күн бұрын
Bushiri is a funder of AFORD
@NgomaRaheem
@NgomaRaheem 22 күн бұрын
M'bale wake wa Coach wa noma uyu mbuzi m'bulundi awona nyenkhwe 2025 ino musiyenj
@user-mr5yb4en2u
@user-mr5yb4en2u 22 күн бұрын
So we have a lot of people here commenting for the sake of others eish kkkkkkk man up guys the guy Timothy made a history in Malawi and it was the first time in history for election to be nullified in Malawi
@MarkSambani
@MarkSambani 2 күн бұрын
😮
@user-iw4dg8lk8v
@user-iw4dg8lk8v 10 күн бұрын
Uyu azalira one day
@MarthaMalopa-kw9xw
@MarthaMalopa-kw9xw 22 күн бұрын
You can judge from the comments
@MosesKatelo-sb6fs
@MosesKatelo-sb6fs 21 күн бұрын
Mbuzi ya munthu
@johngrem2838
@johngrem2838 22 күн бұрын
Pa interview yonse palibe chanzeru chomwe wakambapo Timothy Ntambo.
@johngrem2838
@johngrem2838 22 күн бұрын
Inuuuuu!!! AMalawi anzanga, uyu siM'malawi ayi. M'malawi-tu weni-weni ndi uja Boma likum'manga pafupi-pafupi chifukwa chokamba chilungamo, ameneyu ndi Bon Kalindo. Ameneuja ndiye m'Malawi weni-weni, thats all🙅‍♂️🙅‍♂️🙅‍♂️🙅‍♂️🙅‍♂️🙅‍♂️
@johngrem2838
@johngrem2838 22 күн бұрын
Tchende lako m'Burundi iwe plus uzivayanso kwanu ku Burundi 🇧🇮 amalawi anakutulukira, ndipo anakutsika kale-kale. Olo utabwera ndi mfundo yanzeru yanji, but you'll never get a Malawian as your supporter anymore. 🙅‍♂️🙅‍♂️🙅‍♂️🙅‍♂️🙅‍♂️🙅‍♂️
@AdamMpalira
@AdamMpalira 22 күн бұрын
This guy soon you going to hear that EFF is supporting for his political party as his statement ineo ndikumva ngati chonch and his character same EFF wants 😮
@owenskabazanechiumia3543
@owenskabazanechiumia3543 22 күн бұрын
Musiyeni munthu atsate zimene akufuna ndiye Democrasy yo!! Musamusankhile zochita ai enafe tinawona kuti tingochoka kwathu tili kunja kwa Malawi ndizolinga, ndizofuna zanga, Atupele anasiya ndale, koma pano wabweleranso mu ndale.
@user-lu8sv8rk7e
@user-lu8sv8rk7e 22 күн бұрын
Chomwe akuyakhula sachiziwa ndiopusisisa m'malawi muno ameneyo Nanu a wayilesi muziona athu owapanga interview ahhh palibe point imene wakamba yomwe ingathandize dziko panopa analiononga basi asiye azake
@champianchampian2148
@champianchampian2148 22 күн бұрын
Yekha akuti sanakakamize munthu to come and join his hrdc demos to kick out DPP ,,akuti people did that for their own benefits yet now he is calling us again to support in his current course to bring down MCP ,,,, wapenga uyu kodi eti ? Why the contradiction ?
@SostenKalumo
@SostenKalumo 22 күн бұрын
Manyi amunthu uyu hiyaa
@user-kp8zh9qg2m
@user-kp8zh9qg2m 22 күн бұрын
Panopa akufuna kuukira Chakwera kamba koti akuchotsapo pa ndanda waovtiuze bishop kapena shelh amene anavalapo makala achipani chilichonse ku Malawi kuno
@user-bn3fg7sm2o
@user-bn3fg7sm2o 18 күн бұрын
Wabodza uyu sanatchulepo Enock
@GraciousMollys
@GraciousMollys 22 күн бұрын
😂😂😂😂😂 koma kumeneko oóooooo 😂😂😂😂, Leyah anabwera guys kkkkk
@champianchampian2148
@champianchampian2148 22 күн бұрын
Palibepo chanzeru chomwe walankhulapo on the whole interview kapeyu,,,, komanso he must learn to tame his tongue ,,he cant be calling anthu omwe sakumutsata mfundo zake kuti amisala ,,he must be the one maddest man in our country ,,too many contractions from his mouth ,,, akuti samafuna udindo ,yekhanso akuti for him contribute well amafunika udindo
@KereeditseMotsetse
@KereeditseMotsetse 2 күн бұрын
Ndizoona galuiwe unagwilisa ntchito amalawi namachendeiwe
@johngrem2838
@johngrem2838 22 күн бұрын
Kodi ku Malawi kulibe a Home Affairs?? Guys munthu ndi m'Foreigner-tu uyu. Mungomuyang'ana basi, agwidwe basi akakhale ku Dzaleka Refugee Camp or else Deportee him adzipita kwao ku Burundi
@NelsonBwanali-jx6yz
@NelsonBwanali-jx6yz 22 күн бұрын
mtambo ndi bulundi sure
@GraciousMollys
@GraciousMollys 22 күн бұрын
😂😂😂😂😂😂😂 ine sindkupanga nawo
@DennisDonework
@DennisDonework 22 күн бұрын
Machende ako ntambo akugwilisa ntchito a mcp kuti uphe afford galuiwe
@mphatsosadiki4983
@mphatsosadiki4983 22 күн бұрын
This guy is confused 😂😂😂😂...washota wabalalika
@MalakamMillie
@MalakamMillie 22 күн бұрын
Ndiwozikonda ameneyo wasawuka akufuna aizingowaphunsitsa athu Malawi aliyese azingopanga zake basi koma mcp suzakhalasopapando mpaka kalekale
@user-sc7uf5tn6r
@user-sc7uf5tn6r 18 күн бұрын
Alape ameneyu anatirakwira ife amalawi munthu oipa kwambiri
@user-mr5yb4en2u
@user-mr5yb4en2u 22 күн бұрын
Chilima anajoina MCP sakutukwanidwa koma mtambo? Malawi wake up there is no way you fight for rights and remain fighting even if the fight is over there is no way leave the guy to do what he likes. Northerners died a lot to fight for our rights what did they benefit?
@gearardphiri6904
@gearardphiri6904 19 күн бұрын
Thanks mutambo Good speck for Malawian
@evansjohn7766
@evansjohn7766 22 күн бұрын
Amalawi zikamawavuta musamangitamangira konyoza munthu kuti ndi Burundi ai,ndekuti atumbuka onse ndi mabulundi?aaaaaa........aise vomelezani kuti mtambo anawakanika ,Koma zoti ndi Burundi ndakaika chifukwa palibe amene ndamuona akupita ku court ndukukasuma kuti mtambo ndi burundi .nanga cawalephelesa kukamusumila ndichani?isapusisa wanthu musiye maboza anuo mwamva,zachamba zokazoka .tivomeleza mukasuma ku court kuti mtambo ndi Burundi that's it.
@user-bn3fg7sm2o
@user-bn3fg7sm2o 18 күн бұрын
Leya Keep it up
@AndrewChabadwa-xl3ff
@AndrewChabadwa-xl3ff 21 күн бұрын
Mbudzi yamunthu
@user-kp8zh9qg2m
@user-kp8zh9qg2m 22 күн бұрын
Kape ameneyo bwanji akukanika kuyankhula nchichewa bwanjinso akuyankhula chibwibwi galu mtumbuka iwe pita ukadye soya pieces ukoooo
@yassinjanna9564
@yassinjanna9564 19 күн бұрын
Ndiye ufulu ukamenyela ndani ukamenyela mimba yako chani
@Khosi-uy4yh
@Khosi-uy4yh 14 күн бұрын
Odamunaminza uyo
@KenChitete-pg3ws
@KenChitete-pg3ws 18 күн бұрын
Phavu mr mutambo God bless you mwana wapampoto
@champianchampian2148
@champianchampian2148 22 күн бұрын
Uyu nde alibe morale,,,,, mcp inamturuka,,,ifenso sitingamkhulupilire,,, kape uyu
@fortunatelykapeta1261
@fortunatelykapeta1261 22 күн бұрын
komano be honest iweo mtambo ndimfana wawusilu sungatipepelesenso us anymore, your time has passed sifee anako komanso ukamatulusa speech yoti anthu akuvutika that time mpano pomwe akuvutika anthu kwambili mpati mesa mpanopa
@user-vm7iz6oz6r
@user-vm7iz6oz6r 22 күн бұрын
Zomwe ukuyakhaxo sixikugwilixan ndi mafuso ,
@user-ez1kc7zp9m
@user-ez1kc7zp9m 20 күн бұрын
Mapwalako ntambo
@user-wn6xu4ir5l
@user-wn6xu4ir5l 22 күн бұрын
Andale nawoso amatimenyere ufulu atolankhani saziwa wina aliyetse akhoza kumenyere ufulu wwmunthu wina
@anthonysawa2039
@anthonysawa2039 21 күн бұрын
Bambowa sindikuwamvetsa bwino
@GeofferyKumwembe
@GeofferyKumwembe 6 күн бұрын
Leah 🙏🙏
@spargomw
@spargomw 22 күн бұрын
Timkapanga nawo ma Demo muja adali akuda kwambiri😂😂😂 pano adayerako. Wakamakama ku MCP pano akufuna kutipusitsaso ife a Malawi i think amatitenga a Malawi ngat ng'ombe zake
@RivinessiRivinessierick
@RivinessiRivinessierick 11 күн бұрын
Mwachidure gyz iyiyi nsimbamva wakaririro wachakwera kma wagwanayo osamvera garu ameneyi
@yohanebotso
@yohanebotso 12 күн бұрын
Mbava
@clintonhodda9830
@clintonhodda9830 22 күн бұрын
Mtambo ndi chitsilu anthu sangamutsatenso akungofuna kukhutitsa mimba yake
@KereeditseMotsetse
@KereeditseMotsetse 2 күн бұрын
Leyer umakwana wamukhaulisa galuyo
@user-qj3db4lu7c
@user-qj3db4lu7c 22 күн бұрын
Kodi foreigner ameneyi osamuchita deported bwanji
@user-kp8zh9qg2m
@user-kp8zh9qg2m 22 күн бұрын
Machendeko inuyo nthawi imene ija amati adzatani kupusa etiiiiiii pano ndi nthawi ya chakwera
@SemuJali
@SemuJali Күн бұрын
Uyu simarawi olo chichewa chake
@YamzyAmos
@YamzyAmos 22 күн бұрын
Galu ameney
@user-be3is8rc4r
@user-be3is8rc4r 22 күн бұрын
Usasokoneze amalawi mtAmbo
@jamesgama5489
@jamesgama5489 22 күн бұрын
Koma pagonachi uli mavuto kwambiri ndakumvera chisoni, unawonongesa katundu wa anthu millions of kwachas vuto umakula ntima kwambiri.
@bayanimponda8746
@bayanimponda8746 22 күн бұрын
I believe in Mtambo
@HarrisWipa
@HarrisWipa 22 күн бұрын
Sinner man judges the sinners for sinning differently
@GrecianWyson
@GrecianWyson 22 күн бұрын
Anatiyika pamoto opusa iwe fwetseke.sitingakukhulupilileso iwe opusa Ife tikulila coz you
@JabesiLaphion
@JabesiLaphion 22 күн бұрын
😂😂😂😂😂 ziliko2 km ukoooo ku mMmalawi
@AcksonNyirenda-we7ny
@AcksonNyirenda-we7ny 22 күн бұрын
Anatha awa
@YusuffuDaud-cs7yu
@YusuffuDaud-cs7yu 22 күн бұрын
Mtambo mbolo yako
@user-dc7qq9yz3v
@user-dc7qq9yz3v 22 күн бұрын
Aichosa😂😂😂😂 koma ndi malawi
@user-tn3ks8fw1z
@user-tn3ks8fw1z 20 күн бұрын
The first question should be, Kodi izizii akanalankhula akanakhalabe nduna? If the answer is YES, analankhulapo such comments against the government ali nduna? If the answer is NO, then I am not convinced an inch
@LongiMtimabii
@LongiMtimabii 22 күн бұрын
Usakane unagwilitsa ntchito amalawi kumene mtambo galu wachabe chabe
@RobertDJambo
@RobertDJambo 22 күн бұрын
Mtambo ndi chitsilu
@ChiefJustin-cl8jl
@ChiefJustin-cl8jl 21 күн бұрын
Basi mungolimbikila anthu anataya chikulupililo koma ayi ukuoneka kuti muli strong on the politics you are indeed a fighter
@FortuneKamowa
@FortuneKamowa 22 күн бұрын
Kukadakhala kuti sanamuchose ku mcp bwenzi akunena akunena zoti alayans ikulephela?
@CharlesMasautso
@CharlesMasautso 22 күн бұрын
Confused man
@JosephKabango-dp3ff
@JosephKabango-dp3ff 13 күн бұрын
Munthu oipitsitsa kwambiri
@kelfoodshatchery
@kelfoodshatchery 21 күн бұрын
Chisilu ichi
@SulaimanaEliyasi
@SulaimanaEliyasi 20 күн бұрын
Galu ameneyo musiyen
@samsonchidzani9533
@samsonchidzani9533 21 күн бұрын
I like your approach leah. You dont side with any party in your interview. Your are totally different unlike many human rights activits who gather good points to convince malawians for their own benefits.
BAKILI MULUZI KUCHEZA NDI BRIAN BANDA 11/05/2024.
58:38
LIKI-LIKI TELEVISION
Рет қаралды 23 М.
Giving 1000 Phones Away
00:18
MrBeast
Рет қаралды 21 МЛН
Como ela fez isso? 😲
00:12
Los Wagners
Рет қаралды 25 МЛН
ANANDIKWATIRA NDILI NDI ANA ATATU KALE...true love
31:36
LIKI-LIKI TELEVISION
Рет қаралды 15 М.
Times Exclusive featuring Bakili Muluzi - 11 May 2024
58:41
Times 360 Malawi
Рет қаралды 162 М.
Duduzile-Zuma Sambudla: The ANC party is not a progressive black party
3:23
EXCLUSIVE INTERVIEW WITH ULADI MUSSA
1:01:29
Zodiak Malawi
Рет қаралды 16 М.
Giving 1000 Phones Away
00:18
MrBeast
Рет қаралды 21 МЛН