Kd or atamugula Danyo Daniyo ndi Mulungu ndamene atapangise kuti chakwela awineso chakwera akuchokatu pampando or atagula oyimba onse zikomo koma chakwera akumuchosa pampando ndi Mulungu osadera khawa
@JacksonSquare-us4bf2 сағат бұрын
MCP ndi ma vampire 👹👺🦀🦞🐦🔥🐞
@YoungsonmSimkonda3 сағат бұрын
Kalindo wazionesa kut ndwe wa dpp
@ALEXSUBME6723 минут бұрын
Iwe nde ndani what have you done for Malawiu
@MadalitsoIbrahim3 сағат бұрын
Dan Lu akukayimba zokupha chilima
@TecksonKaima-dr6er2 сағат бұрын
Komanso ndalama ndi tsatana basi.a dan lu mpaka kulowa mcp😢😢komano adzavotera adad mopandanso kukayikira
@AnaffSayamika-uh6vg3 сағат бұрын
The Dc 😊
@macksonmkandawire5718Сағат бұрын
Marry chilima abweleso ndi boza la mamuna wake
@macksonmkandawire5718Сағат бұрын
Winiko kkkk umphawi wavuta kwambiri
@andreakalambula7723Сағат бұрын
iiiiii mcp ndilibe nawo mau
@macksonmkandawire5718Сағат бұрын
Azilima Ku mpoto bwanji sitidya chitedze
@YoungsonmSimkonda3 сағат бұрын
Mkuchedwa ndzimenezo akalindo
@asiyatujuma5507Сағат бұрын
❤❤❤❤❤❤
@jacquelineboya952918 минут бұрын
Za mery chilimazo ukunama bon kalindo😅?mery mwini wake anakana kuti sakufuna ndale nde anthu achita kumumanga chingwe? Khalani pheee ku UTM kutuluka mtsogoleli mbambande akazawina mery chilima azamupasa ntchito not kukhala president
@Daniel-cf4tuСағат бұрын
Akalindo zilakhula zanu sizomanga or athu ena amakhalila kukuombelani m'manja koma zolakhula zanu ndizokhuza khondo wy?
@bysongeorge324320 минут бұрын
500 million kwacha kungoipeza all over sudden! Afufuzidwe and wapeleka ndalamayo ndani , waitenga kuti? Za Mai Chilima itayeni imeneyo. She is not the solution of Malawi issues.
@EusébioLucianoGaiondo33 минут бұрын
🔥
@lungisanishezi1023Сағат бұрын
Dan lu ndi ndani so mu ndale achoke kumene
@YoungsonmSimkonda3 сағат бұрын
Kod ndwe was dpp
@HalimaShafie-q9k52 минут бұрын
Kalindo alibe chipan palibe ku zionesa kuti ndi wa dpp galu iwe
@hantosidira872041 минут бұрын
Kalindo ndiwa DPP mukufuna mtinamize
@HerbartKaphamthengo2 сағат бұрын
Zipani zaku mabanja zimenezo ndiye mukuonakuti angachite chani Mary chilima angotaya nthu anamuvotera ndindani masewera eti utsogoleri sukusika Mbale pabanjatu ai Koma dziko.Ndiye mukamati Mary chilima mukuona Ngati bank mkhonde dzikoli
@GladysndilimbiraBonongwe-g6c3 сағат бұрын
Mcp ndalama zomwe Ali nazo ndi zogulira Anthu basi
@isaacchiwaula7312 сағат бұрын
Nthawi yonseyi ngat mumadziwa kut Dan lu anamugula, munkalekeranji kunena asanalengeze kut walowa MCP? Ndie chifukwa chakuti lero walengeza yekha kut walowa MCP ndie muzikati aaa ai amugula! Aaa ndinunachitsiru. Ndipo zomwe mukuyankhula apazi ndizopanda nzeru, mesa a DPP-wo ndiamene akumayambitsa nsankho kumanena kut MCP isadzapiteso ku kumwera, zomwe a DPP-wo amayankhula ku phalombe zija, bwanj osadzudzula zimenezijazi ukukanena za MCP? Kod basi umafuna kuyambanitsa anthu dziko muno chifukwa chot ndiwe mulomwe wakumwera? Activi wanji okhala ndi mbali chonsecho umati siwe wandale? Mmutu mopanda nzerumo, anakuuza kut Mery Chilima amafuna u president ndindani? Simupindula kanthu baba ndipo muphulika 😅😅😅😅😅😂😂😂
@ALEXSUBME6727 минут бұрын
Za usilu basi inu
@ChisomoNthukwa2 сағат бұрын
Koma zodabwitsa kut mukupanga izi ndinu alomwe okhaokha bwanji chikukuwawani ndichani asiyeni azani apange mbali yawo kupusa basi kuzikonda
@YoungsonmSimkonda3 сағат бұрын
Kod wabwino ndiuti
@YoungsonmSimkonda3 сағат бұрын
Zoona zake zit
@TemboHaswell2 сағат бұрын
Ngati ndichoncho zilibwinotu kt a mcp akachite manyazi akaone anthu mene akazazile ku nsonkhano wa dpp
@JackMvura-ik2tdСағат бұрын
Iwe ndiye wakamba iwe Malonda ndim'aso kumeneko MCP ingotumiza Wana chakwera sapita wakula ndipamene mudziwe Kuti MCP bomaaa ndilomweli gotani chimwendo oladi Musa akwana tambala Ali ndimoto pamutu wina akalira tiyeni konko tikakhomana DPP imadelera muona Ngati muliku mulanje kayiyambeni mudzadutsa Kuti simu Lilongwe tithana mukuchepela nyawu zathu konzekani tinyape alomwe pobwela kumeneko a police pumani tiombane Kaye apa