I commend this, this needs to be encouraged, please continue, with this kind of mentality Malawi will rise, God bless 🙏
@FloridaOssy192 ай бұрын
❤❤❤❤❤❤ mwayamb bwino a manganya
@DeborahHetekere2 ай бұрын
This is good development that's the spirit that we need as malawians,,,this is exactly what Late Dr Claus Chilima wanted
@mthawisakaunda2 ай бұрын
Zipatala za boma mavuto aakulunso ndomweo. Ogwra ntchto amafika nthaw yomwe akufuna and sayambanso ntchto nthaw yomwe afklayo amayamba wakhala kae akut kupumula then ayambe kugwra ntchto. Imafika mpaka 9 asanayambe ai. Chomwe amadziwa nkutukwana ma patient bas
@veronicamalisero26712 ай бұрын
A VP ndipo muyendele ma office onse aboma,,,....amakhala pa mtambasale anthu awa..keep it up, ,,,....
@GiftNgwira-e8l2 ай бұрын
Kkkkkkkkk koma vic wake kashoti
@masalinodovu17052 ай бұрын
Excellent Mr VP izi nde zofunikira kwambiri
@DinahNantchengwa2 ай бұрын
Proud of you Mr president, zikamatele dziko lathu liziyenda bwino, anthu muzipatsla amataililadi koma akamalombikitsidwa choncho ziziyenda
@giftsululu42742 ай бұрын
Ku utm''' '' mukuona koma... Mwataya gold
@vanalphamphaya35182 ай бұрын
Big up the VP continue the good work you started when you were there long time.
@nyasavoicebox2 ай бұрын
Good on the Right Honourable the Vice President for being positive. Especially when dealing with the young nurse. Samakalipa koma kulangiza kuti mavuto akunyumba aliyapo iyi ndi ntchito anthu amakudalilani muziyesesa ku bwela ku ntchito on time. Even when dealing with the DHO the conversation sinali yoti ine ndiwonke kuti ndine VP but after reprimanding her he made her feel safe to elaborate on the challenges their hospital and district are facing. Politics aside, this guy may actually care about improving Public Service Delivery in Malawi.
@robertkalima8742 ай бұрын
This is great. ife ogwira ntchito mboma tikugona kwambiri. Ngati sitifuna ntchito titsanzike