Uyuyu ndi wabodza weniweni ine ndili kuno ku Mzuzu abale kunali mvula inayamba Sunday koma inagwa kwambiri tsiku la Monday komanso onse akuti ndege ku LL inanyamuka 9:17 am Ife tikulira nanu limodzi sogolo lowala lathu lapita koma mmm ma boza satithandiza kuno kunali chifunga
@ChikondiGlibert3 ай бұрын
Iwe ndiye chitsilu chothelatu udziwe. Komwe uliko
@JimmyIsaac-xd4ef3 ай бұрын
Zikomo m'bale chilungamo chidziwike, komaso a Mbuye akhale mbaliyanu
@harrispheleni22053 ай бұрын
Iwe ndi kape video ya momwe inanyakukira mpaka kugwa? Anakanika president Raisi kapusitse ana a utm azako
@sammyjonnes4 күн бұрын
ETI NDI ZOONA NSILIKALIYU ANAPEDWA ???
@KelvinJpchimphepo-sh6nc3 ай бұрын
Apa sipakuyenera kuwopa chifukwa zikatero mawa zizachitikira kwayena ndiye tizivomeleza zimenez mpaka liti apha anthu asogoro lawo angat pangani zomwezo bwana anthu ali pambuyo panu, tima dikira anthu ngat inu ndipo izi zowawa kwabasi, titeteze dziko osat kuphana tokha tokha ngat ndife anthu ndife obwera zoona
@YobuSatinphiri3 ай бұрын
WHY ANACHOSA BLACK BOX?
@GarkiThomАй бұрын
..nkhan za ndale..IZI
@PriscaChapsa2 ай бұрын
Iwe ndi opusa iwe ngat umaziwa chilunga umakeka kuulula chilima asanafe bwanji
@JoeMwandira-tq9rs3 ай бұрын
Mno mu Malawi ngatimli anthu ngati awawa bwedzi dzikolathu likanakhala lachilungamo tsangakuphe mdzanga amalawi ose akuimililani bwana opepela okha ndi amene adzvotera mbuziyi
Anthu for aja ndiAmene anapanga kokupha avice prsdnt
@ShelingtonMtemula3 ай бұрын
Ulemu wanu munthu wankulu apa ofunika audio muilengeze mu English kuti imveke ziko lonse lapansi
@ernesthkaunda79023 ай бұрын
This sounds fake to me. How could the crew members not notice that before starting off from Lilongwe. Tulutsani bodza lanulo .......kodi ngozi yayambira ku Malawi?
Mulungu Ali painu ndi kwa onse omenyera ufulu wa chilungamo
@murraykaliwo66383 ай бұрын
Nanga bwanji samauulula zisanachitike
@bostonbanda47743 ай бұрын
Zabodza izi unatani kunena zisanachitike
@BenPhillip-fw8hi3 ай бұрын
Eti eti
@Hellenistic1093 ай бұрын
Its Bwana Mumandinyasa ndisakubiseni 😂😂 for me
@mariajonasse97922 ай бұрын
😂😂😂
@ClementKamtedzaАй бұрын
God bless you bwana
@JudithAbinaele2 ай бұрын
U guys u are really taking us for granted..busy making up stories..bring the videos u iditots. Ma phone ama camera amapezeka even kwathu ku Tukombo ..osajambulako bwa? Akwa minyu biiii
@barnettbmphanda108Ай бұрын
Ndiye kunkhalangoko anachita kuyinyamula kukaponyako ndipo video imeneyo umajambula ndiwe? In your statement mwati ndege sinagwe tafotokozani bwino timve? Iweyo unali kuti?
@TWINKIDDMARSECOAL3 ай бұрын
Nde mwati mundege kuchotsamo mafuta??? APA mwanamatu and zambri seems bodza coz even galimoto imaonetsa level yamafuta so u mean ma pilot sankaona zamafuta??? Nde analolela kuyendetsa kuti afe???? And video mukuti yochoka ku airport mpaka kumene inagwa munkajambula munadziwa kuti zitere??? Bodza ili
@milanzichikondi73303 ай бұрын
Black board??, Benzene (this is just a small component in gasoline) how did they suck it? , Every pilot before flight makes a check list. We need real facts gents. We are with you but we need facts.
@koncyk71383 ай бұрын
Olo ngati driver amapanga check ma tyres, engine coolant, engine oil. Galimoto likalila amaonso all warning ⚠️ lights pa dash board and levels of fuel. Should we say gage ya fuel mu ndege inali yokufa. If at all they use a dip stick, sanapange zimenezo? Facts are really supposed to be laid osati trying to trigger unnecessary riots.