Ndkuuzen cholakhula chna mophweka auzen a Malawi msogolieli samasankha osauka bc alyese azwa cz enawa dollar akuiwonela m'boma ndye zngayende bwanj
@JulietMunthali-g9b5 сағат бұрын
😂😂😂😂😂😂😂 ndipo live akugwa chifufu
@IbuhIshma5 сағат бұрын
Ndipo tikaapeza ntanyiwa
@IbuhIshma5 сағат бұрын
Kod inu trump ali ndi zaka zingat inu inu
@ChristinaMdeza6 сағат бұрын
Mwandifusira bwino kwambiri comrade wathu kodi wakalamba , bwanji asayiwaletu, kuti Mulungu wathu, anasakha Mose ngati mene alili peter A dad koma bwanj mene anagwilira ntchito,Mose wathu leo ndi ADAD bas mu September mu DPP boma bas .Ambuye atipasa bas we love your comrade wathu.
@EdwardAlli-c6j6 сағат бұрын
Nkhani ndiyoti akuopa chipani cha DPP.kodi okalamba alive ufulu?
@MathewKalinkhu6 сағат бұрын
Yeah, yafika nthawi a Malawi, tinokole Chimwendo Banda one time, alliance yikufunika apa, DPP, AFORD, UTM, UDF ndi ena.
@thatgirrroskrr35706 сағат бұрын
Ayamba kale kunjenjemela heleu😊
@MathewKalinkhu6 сағат бұрын
Ndipo a Malawi tikuona kuchedwa zisankho, Chimwendo Banda ndi MCP yake adzamangidwe, useless government we've ever had in Malawi.
@MathewKalinkhu6 сағат бұрын
Aaaaaa Chimwendo Banda wasowa chonena, DPP yidasiya forex, koma a MCP yidawononga, mpakana kukondola 13 billion! Ah! Ndiye chitsilu ndani apa? Agalu awa akuchoka basi,