ZIPANI ZIPHANA CHAKA CHINO😱🔥
5:20
14 сағат бұрын
NAYE NAMALOMBA WABWEZA MOTO DZULO
12:33
15 сағат бұрын
PAN’GONON’GONO AKANATUKWANA NDITHU ,
39:18
APA NDIPAMENE MCP YAONESERA KUT IKUOPA DPP
14:20
NAWO BAMBO A SIKONO SAKUGONJATU
5:03
2 сағат бұрын
ANTHU ADABWA NDIZOMWE WANG’ALURA GWAMBA
13:50
Пікірлер
@MchachaGoodson
@MchachaGoodson 38 минут бұрын
Yes tikufuna Amuna opanda mantha akangoyesela a MCP za age limit aza nong'oneza Bondo.
@PaulMBKathumba
@PaulMBKathumba 39 минут бұрын
Ndiye ine undimangitse ndiwebe wa satani
@PaulMBKathumba
@PaulMBKathumba 43 минут бұрын
Grace Chinga anafotokoza yekha usanamuphe ndiye apa usamakane apa muthu aliyese wachita choyipa amakana ndithu
@MchachaGoodson
@MchachaGoodson Сағат бұрын
Ngati alephela kuyendesa chuma pa zaka 5 ndiye akunena chani anthu opusawa.president wina aliyense amasitha zithu mu term yake koma zawavutilatu 0
@MarySinjirani
@MarySinjirani Сағат бұрын
APM Woyeeeeeeeeeeeee
@ThokozaniBondo-em9fr
@ThokozaniBondo-em9fr Сағат бұрын
Kodi chakwera akuwopa chani uyu zamuvuta chani age limit akapange kwao kukasiya
@RhodrickLion
@RhodrickLion Сағат бұрын
Koma bwana Bushiri sakunama gayezi mkuluyu anthu amalakwila kwambiri
@RhodrickLion
@RhodrickLion Сағат бұрын
Koma bwana Bushiri sakunama gayezi mkuluyu anthu amalakwila kwambiri
@CharlesJames-f1w
@CharlesJames-f1w 2 сағат бұрын
Nanga.sindio.ndi.akuba.akuopa.kumangidwa.
@RichardKataghala
@RichardKataghala 2 сағат бұрын
Sitikufuna ma gogo anu awo gogo APM😂 tapumani uko ndiye a gogo abuse
@waxy.A.k59
@waxy.A.k59 2 сағат бұрын
Munakhululuka nde ingopitirizani kukhululuka bwana ngatidi muli mneneri wamulungu owonadi pakuti kuweruza mkwake Mulungu
@SherifWhite
@SherifWhite 3 сағат бұрын
Ndili mbari yako use ur money anthu amaonjeza
@MarthaGama-q1o
@MarthaGama-q1o 3 сағат бұрын
APM my vote ❤
@MwinkhulanaLulu
@MwinkhulanaLulu 3 сағат бұрын
Ma M P amene angakavotele dzimenezo atitchulile maina taputhe adzikagona ndi Chakwera mpaka mavoti azavotedwe
@WasikaAlik
@WasikaAlik 3 сағат бұрын
Kkkkk koditu kabwilayotu ndihule kumenetu bro
@WasikaAlik
@WasikaAlik 3 сағат бұрын
A mcp akavotele ndi agule
@AubreyBanda-q4b
@AubreyBanda-q4b 3 сағат бұрын
Sinkhani yakumundatu asaiwale ,koma kukhala ndi dzelu za utsogoleli😊
@FrancisStima-sc7zs
@FrancisStima-sc7zs 3 сағат бұрын
Akumanga ukunjeza
@AubreyBanda-q4b
@AubreyBanda-q4b 3 сағат бұрын
Wathu ndi yomweyo
@AubreyBanda-q4b
@AubreyBanda-q4b 3 сағат бұрын
Tiyeni tilemekedze ufulu wa munthu
@AlexKaunda-w7l
@AlexKaunda-w7l 3 сағат бұрын
Koma mwati jessie kabwila amatha week asanadye mbolo amaoneka kuti ndi wanyele😂😂
@tingamasi106
@tingamasi106 4 сағат бұрын
Nde muziyendetsa dziko ndi nkabudulamo?
@GetrudeMakwinja-u4l
@GetrudeMakwinja-u4l 4 сағат бұрын
Asikana atani they were just celebrating their day 😂
@bashirsaizi2641
@bashirsaizi2641 4 сағат бұрын
Excellent
@BenjaminMakwinja
@BenjaminMakwinja 4 сағат бұрын
APM my vote
@KondwaniMsiska-l8n
@KondwaniMsiska-l8n 4 сағат бұрын
Mumaro mokoza Malawi mukupangazoputsa kumalimbana ndi bill ya age limits.Agalu Osaka inu mwapenga misara et.....Apm 2025 bomalllll
@JumahIssah-d2n
@JumahIssah-d2n 4 сағат бұрын
Bro machulutsa kuyankhura
@dreamsmediamw
@dreamsmediamw 4 сағат бұрын
Nde mudana ndikuyankhula kwanga chifukwa chani?
@supa4dupa
@supa4dupa 4 сағат бұрын
Ndi Democracy , ambiri amkamunena Peter Muntharika, Koma palibe amamangidwa, ndi 2025 osati 1974,nthawi ya Kamuzu Banda, pano kuli zipani zina ndiye pali ufulu woyankhula ngati zinthu sizilibwino.
@Mustapher-fb4qp
@Mustapher-fb4qp 4 сағат бұрын
Kuyaka moto marawi tiyenazoni chakwera chobibira chako
@JohnBamusi-o8l
@JohnBamusi-o8l 4 сағат бұрын
Pepani pepen
@luciabanda5589
@luciabanda5589 4 сағат бұрын
Mulungu salakwitsa
@ThomasBinali-t9f
@ThomasBinali-t9f 5 сағат бұрын
Nanga munthuyo ali osamva(deaf person) nde mwamugunda zitha bwanji?
@WarriorKB-l3i
@WarriorKB-l3i 5 сағат бұрын
Nde yake abusa tili limodzi 💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙caka cake ncino
@MathewKalinkhu
@MathewKalinkhu 5 сағат бұрын
APM akumuopa a MCP, ndiye Kabwira wledzela ndi tianyamata . Akubwebweta😂😂😂
@edwingondwe2860
@edwingondwe2860 5 сағат бұрын
APM my vote
@AllanChabwela
@AllanChabwela 5 сағат бұрын
Vote ndi mumtima , asiyeni apange msonkhano a mcp koma ovota ndiife
@ChancyKhonje
@ChancyKhonje 5 сағат бұрын
Muiafuna kuima muyambitse chipani chanu coz mukalowa ku mcp nkhanza sizizatha plz Bushiri nakuweya
@jameskachulu8141
@jameskachulu8141 5 сағат бұрын
Koma bwedzi akumativela chisoni
@KennedyEckison
@KennedyEckison 5 сағат бұрын
Ndkuuzen cholakhula chna mophweka auzen a Malawi msogolieli samasankha osauka bc alyese azwa cz enawa dollar akuiwonela m'boma ndye zngayende bwanj
@JulietMunthali-g9b
@JulietMunthali-g9b 5 сағат бұрын
😂😂😂😂😂😂😂 ndipo live akugwa chifufu
@IbuhIshma
@IbuhIshma 5 сағат бұрын
Ndipo tikaapeza ntanyiwa
@IbuhIshma
@IbuhIshma 5 сағат бұрын
Kod inu trump ali ndi zaka zingat inu inu
@ChristinaMdeza
@ChristinaMdeza 6 сағат бұрын
Mwandifusira bwino kwambiri comrade wathu kodi wakalamba , bwanji asayiwaletu, kuti Mulungu wathu, anasakha Mose ngati mene alili peter A dad koma bwanj mene anagwilira ntchito,Mose wathu leo ndi ADAD bas mu September mu DPP boma bas .Ambuye atipasa bas we love your comrade wathu.
@EdwardAlli-c6j
@EdwardAlli-c6j 6 сағат бұрын
Nkhani ndiyoti akuopa chipani cha DPP.kodi okalamba alive ufulu?
@MathewKalinkhu
@MathewKalinkhu 6 сағат бұрын
Yeah, yafika nthawi a Malawi, tinokole Chimwendo Banda one time, alliance yikufunika apa, DPP, AFORD, UTM, UDF ndi ena.
@thatgirrroskrr3570
@thatgirrroskrr3570 6 сағат бұрын
Ayamba kale kunjenjemela heleu😊
@MathewKalinkhu
@MathewKalinkhu 6 сағат бұрын
Ndipo a Malawi tikuona kuchedwa zisankho, Chimwendo Banda ndi MCP yake adzamangidwe, useless government we've ever had in Malawi.
@MathewKalinkhu
@MathewKalinkhu 6 сағат бұрын
Aaaaaa Chimwendo Banda wasowa chonena, DPP yidasiya forex, koma a MCP yidawononga, mpakana kukondola 13 billion! Ah! Ndiye chitsilu ndani apa? Agalu awa akuchoka basi,
@BunnahAdamh-n7s
@BunnahAdamh-n7s 6 сағат бұрын
❤ DPP
@GanizaniMaonga-z1g
@GanizaniMaonga-z1g 6 сағат бұрын
Kkkkkkkkk kkkk koma a Malawi eeeeee aiiiiiiii