A GEORGE ZULU A MCP ACHITITSIDWA MANYAZI NDI ANTHU AKU NTANDIRE PA MALIRO KUSAVUKILATU NDITHU

  Рет қаралды 24,454

Malawi Trends TV

Malawi Trends TV

Күн бұрын

Пікірлер: 182
@HappyAbyssinianCat-xt2bm
@HappyAbyssinianCat-xt2bm 7 күн бұрын
Ndie wina azikati boma ndilomweri akapezeka wachoncho ndi mbuli yamunthu ozindkira sangafune mcp ai, dpp woyeeeeee 💙💙
@ElizabethKachipeso-rl8fi
@ElizabethKachipeso-rl8fi 3 күн бұрын
Mudziwe kt athusakufunani Boma lolanda ukalanda sichako DPP oyeeeeee 🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥
@estherkalipinde7477
@estherkalipinde7477 8 күн бұрын
Hahahaha ndakomoka nkuseka ine. Anthu atopa😂😂😂😂
@PatricaTchuwa
@PatricaTchuwa 8 күн бұрын
Dpp yomweyo my vote ❤
@MarySinjirani
@MarySinjirani 8 күн бұрын
😂😂😂😂😂😂😂😂More fireeeee ntandile mwayitha ulemu wanu
@EsetaGerate
@EsetaGerate 8 күн бұрын
😂😂😂😂😂😂 MCP palibe akuyifuna 😂😂😂😂
@WarriorKB-l3i
@WarriorKB-l3i 6 күн бұрын
Awuze palibe akufuna chikangawa mmalawi muno 💙💙💙💙💙💙💙boma!
@FytonRichard-t3w
@FytonRichard-t3w 8 күн бұрын
😂😂😂😂 kkkkkk Malawi 🔥🔥🔥🔥 yayayaka Moyo 😂😂😂
@KalungamaBright
@KalungamaBright 8 күн бұрын
😅zamanyazi azionere basi😢 😊
@WarriorKB-l3i
@WarriorKB-l3i 6 күн бұрын
Komanso ndamva ena akukuwa akuti dpp oyee! Mumvesele bwino×2 mumumva basi mcp no chance mwatizunza kwakwana.
@DennisTobias-b4r
@DennisTobias-b4r 4 күн бұрын
Ine ndavanso
@isaaczuze
@isaaczuze 8 күн бұрын
Kkkkkkkkkkkkkk kugwa Kwa babulo ....anthu ngati sakukufunani bola kuvomeleza mcp anthu sakuyofunanso ayi .. .chipani choyendesedwa ndi zisilu
@MandalaChaona
@MandalaChaona 5 күн бұрын
Ndipo Zitsiru zake zokumwa Mwazi, mikodzo ndi Malobvu, opanda zimenezo mphamvu Chipani chilibe 🤣🤣
@LuwizaChika
@LuwizaChika 8 күн бұрын
😂😂😂😂😂😂😂😂 zochitisa manyazi Kwambili my vote Dpp oyeee 💙🔥🔥🔥
@eliffagondewe8214
@eliffagondewe8214 5 күн бұрын
Kkkkkkk koma pls eesh 🔥🔥🔥🔥
@JafarWiati
@JafarWiati 8 күн бұрын
Ayankhe kabwila 😂😂😂😂
@chrissyamanda5510
@chrissyamanda5510 8 күн бұрын
😂😂😂😂muchimva chikuyankha chikangotha kubwila fodya wa mphuno
@thokozanindalama
@thokozanindalama 8 күн бұрын
😮😮😮😮😮
@HappyAbyssinianCat-xt2bm
@HappyAbyssinianCat-xt2bm 7 күн бұрын
Ndpo hule limenelija liyankha manyazi alibe
@MandalaChaona
@MandalaChaona 5 күн бұрын
Even the Devil himself is angry with Chakwera and MCP Party 🤣🤣
@MemoryZiyaya
@MemoryZiyaya 5 күн бұрын
😂😂😂😂😂eeissh!​@@MandalaChaona
@ShukuraniTonex
@ShukuraniTonex 8 күн бұрын
😂😂😂😂😂😂kkkkkk
@YamikanBanda-z7z
@YamikanBanda-z7z 4 күн бұрын
Kma abale,eeee anthu akumasuka ndithu😊
@FytonRichard-t3w
@FytonRichard-t3w 8 күн бұрын
Kkkkk Dpp my vote 😅😅
@ChristopherJohn-z5z
@ChristopherJohn-z5z 8 күн бұрын
Timati zayang'ana ku thazi bomu 😂😂😂 soya wa chita mpapapa kkkk
@JohnWame-u3l
@JohnWame-u3l 8 күн бұрын
😂😂😂😂😂koma zina zikati zichitike😂
@DONNEXKhama-bk1gy
@DONNEXKhama-bk1gy 8 күн бұрын
Kukhala WA MCP ndi kulimba mtima 😂😂😂
@Amiduj
@Amiduj 5 күн бұрын
😂😂😂😂😂😂 moti mpaka pamenepo?
@TimothyKumwenda-z4m
@TimothyKumwenda-z4m 5 күн бұрын
Eya chifukwa ndimmene zinalili pamenepa mmm ine Bp kukwereratu
@OdettaLowrence
@OdettaLowrence 6 күн бұрын
Ndei zicsni ziiiiiiii 🤣🤣🤣🤣🤣🤣
@georgeaiwa8661
@georgeaiwa8661 8 күн бұрын
😂😂😂😂😂😂 iwe DJ umandiwaza koopsa ndimmene umatambasulira nkhani. Ndiwe wanga WA nambala one
@bridgetmajor3646
@bridgetmajor3646 8 күн бұрын
Apm my vote
@MillieMalakam
@MillieMalakam 5 күн бұрын
😂😂😂zamanyazi kwambili
@JJ-in-the-hut
@JJ-in-the-hut 4 күн бұрын
Koma mpaka DPP woyeee! Kuma Lacoste camp🐊🐊🐊?🤣🤣🤣🤣
@ReadsonChisaga
@ReadsonChisaga 8 күн бұрын
Apa zaoneseratu kuti anthu ku Lilongwe sankufuna Razaro ndi chipani chake cha mcp.
@KhadijaMsosa-d7z
@KhadijaMsosa-d7z 7 күн бұрын
Shaaaaa😂😂😂😂🙌
@phalysbanda2431
@phalysbanda2431 5 күн бұрын
Agalu amenewa adzipita 😂😂😂
@zimmekapachika6784
@zimmekapachika6784 8 күн бұрын
😅😅😅😅😅😅😅😂😂😂😂yomweyo Chikangawa party
@fannyzimba149
@fannyzimba149 8 күн бұрын
Akhaula a wachita bwino agalu amenewa
@Lizzie-h1k
@Lizzie-h1k 5 күн бұрын
Malawi trends ndaikonda....pena imabweretsa zinthu zoti ena saangadzipeze😅😅😅😅...awatu zawo zada...kkkkk...MP wanzeru apitiletu ku DPP...akapange nao ma primaries!
@rashidadan2533
@rashidadan2533 8 күн бұрын
No chance for the wicked
@BirzetScott
@BirzetScott 8 күн бұрын
😂😂😂😂😂 madzi apanga katondo.
@AlexKaunda-w7l
@AlexKaunda-w7l 5 күн бұрын
Tilibe ntchito ndi mcp akuchinda kwambili too much kupakula nyemba
@HenryKatopola
@HenryKatopola 7 күн бұрын
😂😂😂😂😂😂😂😂mcp yatha , chikangawa😂😂😂😂😂😂😂
@daviechikopa-r6w
@daviechikopa-r6w 8 күн бұрын
a geruge zulu kunoooo😅😅😅😅😅
@JamesALLi-m8i
@JamesALLi-m8i 5 күн бұрын
Yes chala mwambad Adad woyeeeeee dpp is my vote 🗳 😀 👍 2025 boma and Apm boma we love Malawi 🇲🇼 guys 🇲🇼 💙 🔥
@GiftBello-v1i
@GiftBello-v1i 8 күн бұрын
Esh chapanadi chitseko apa😮😮😮
@YounusWabullah
@YounusWabullah 8 күн бұрын
Ndie ena akukomenta kut dpp ku opposition mukhalitsako 😂😂😂😂😂😂😂 zikugwirizana manyazi bwanji muoneramu😂😂😂😂😂
@MathewKalinkhu
@MathewKalinkhu 8 күн бұрын
😂😂😂😂😂😂 zamanyazi , MP wa MCP, koma anthu akuti chala m'mwamba , meaning DPP! Eshi! Manyazi basi.😅😅
@MaxwellMangamba
@MaxwellMangamba 8 күн бұрын
zikutheka. APM my vote❤
@MayesoBikefa
@MayesoBikefa 5 күн бұрын
APM 💙 akubwera komweko
@jacquelinemphwere894
@jacquelinemphwere894 8 күн бұрын
Zaulendo uno😂😂😂
@JohnmjigoMalinda
@JohnmjigoMalinda 8 күн бұрын
Zovuta kwambiri kkķ
@SymonJowabe-y1q
@SymonJowabe-y1q 5 күн бұрын
Kkkkkkkk😂😂😂😂😂
@MarthaGama-q1o
@MarthaGama-q1o 8 күн бұрын
😂😂😂😂😂 komandiye apa yalimbadi nkandilo olo kuthila madzi sitheka , kukhala WA mcp nkulimba mtima
@LukaSamson-w5h
@LukaSamson-w5h 8 күн бұрын
Chipani cha mcp chantha chifukwa cha anthu awa, zikhaleng'oma, chimwendo Banda, Moses kumkuyu ndi Jessy kabwira ayipisa dzina la Chakwera
@HenryKasiyama
@HenryKasiyama 8 күн бұрын
Malawi Trends ndikukunyadirani mukuitha
@OwenJambo-g4m
@OwenJambo-g4m 5 күн бұрын
Kkkkkk koma Adah
@LeonardJere-h8s
@LeonardJere-h8s 8 күн бұрын
Kkkk anthu atopa ndikunamizidwa
@ChristinaMdeza
@ChristinaMdeza 8 күн бұрын
Pajatu Jesse akuti boma ndilomweli bas mzimu wa chilima wakwiya nawo bas chakwera munthu wakupha uja,Kuba, mkati, kumanga anthu osalakwa ddp boma bas mu September mu chakwera azipita bas ndi chipani chake cha mcp
@EstherChimombo
@EstherChimombo 8 күн бұрын
My Malawi 😂😂
@trifoniachilunda6263
@trifoniachilunda6263 8 күн бұрын
Yakwiya Mizimu ya chilima
@trifoniachilunda6263
@trifoniachilunda6263 8 күн бұрын
Chakwela paulendo pakilani
@MrArif-tc2cu
@MrArif-tc2cu 8 күн бұрын
Ine ndi mnyamata wa 31 yrs, bambo Anga amkandiuza Kuti mcp ndi yakupha, Kuba kuononga, But now l trust my dad, in our district, area, and my village we don't want mcp party
@spargomw
@spargomw 8 күн бұрын
Zavuta kumpanda, kuchipinda kwa MCP😂😂😂😂😂 Adachita mistake kupha Chilima coz ndie anali Joka wawo😂😂😂 Long live APM❤❤❤
@WisdomKapawo
@WisdomKapawo 8 күн бұрын
It's was big mistake brother ndipo awona zinthu
@ShamimuBisani
@ShamimuBisani 8 күн бұрын
Mwadzi wamunthu ndi wa nkhuku ndi osiyana
@FracksonMadani
@FracksonMadani 6 күн бұрын
E, pa infa ya Chilima yokhayo hmmmm anadzionongera heavy, kudzionongera kwamunthu wankulu kumavuta kukonza 😂😂😂😂anthu amangoseka basi lero siiziiii😅😅
@isaaczuze
@isaaczuze 8 күн бұрын
My vote is for Apm osati chisilu ichi akuti chakwera mbuzi yeniyeni ya munthu olephela .....sindingavotelenso chisilu ine ayi
@ELLENZAPS
@ELLENZAPS 8 күн бұрын
Simunati muziwona
@AlicePondani
@AlicePondani 5 күн бұрын
Bvutonso sitinaleembetse ambri😊
@UncleShopRite
@UncleShopRite 8 күн бұрын
Malawi trends woyeeee ❤❤❤❤❤
@MussaKachere
@MussaKachere 5 күн бұрын
😂😂😂 Yoo! Apa ungodziwa kuti yarakwa
@HildaMbizi
@HildaMbizi 5 күн бұрын
MCP DPP nonse tinakuonani kale UTM my vote
@FracksonMadani
@FracksonMadani 6 күн бұрын
Kodi kumtandire kunachulukanso anthu obwera ngati kwam'gona? Paja achina boma ndilomweri amati , kumene kuja ambiri ndi obweraaaaaa😂😂😂😂😂
@DeKelders
@DeKelders 8 күн бұрын
Kkkkk🤸👍
@CharlesJames-f1w
@CharlesJames-f1w 8 күн бұрын
Sanati.aona.
@LomosiKanzingeni
@LomosiKanzingeni 5 күн бұрын
Amenewo amamudziwitsa kuti akalowe chipani cha Dpp
@ShamimuBisani
@ShamimuBisani 8 күн бұрын
Malawi Trends aaaa ungabwerese nkhni yokoma chonchi apa moyo umenewu mawa ubwereses zina til pano koz iweyo
@jamessheki4293
@jamessheki4293 8 күн бұрын
MCP anthu akutopelani
@MussaAli-h4i
@MussaAli-h4i 8 күн бұрын
😂😂😂
@FracksonMadani
@FracksonMadani 6 күн бұрын
Gangata ndi Kabambe alikuti kodi?😂😂😂😂
@PaulMwachande
@PaulMwachande 8 күн бұрын
Kkkkkkkkkk koma anthu atopa eti mmmmmm mcp yathapo bassss mmmmmm manyadzi alibe koma
@Lizzie-h1k
@Lizzie-h1k 5 күн бұрын
Nkhani ndi DPP....I think even Chakwera is planning to join DPP , there is no question about that!
@WarriorKB-l3i
@WarriorKB-l3i 4 күн бұрын
@@Lizzie-h1k kkkkk ndi choncho kumene
@LookmanAdamu
@LookmanAdamu 8 күн бұрын
😂😂🎉😂😂😂
@PatrickChagaka
@PatrickChagaka 8 күн бұрын
Kkkkkkk koma zinthu zake zosayendatu
@LilianKachala-yz2xf
@LilianKachala-yz2xf 8 күн бұрын
MCP akunyozeka kwambili Chifukwa Cha njala ndi fertilizer sizinayende bwino.
@AlwayneH
@AlwayneH 8 күн бұрын
😂😂😂 komatu malawi trends
@AustinNangwale
@AustinNangwale 8 күн бұрын
😂😂😂 Ndimanena kale Kuti Chakwaela apangitsa chipani cha MCP kuthelatu ndipo palibe yemwe angakhaledo busy kumvesela boza la bwana chakwela😂😂😂
@VdbdbxDvv
@VdbdbxDvv 2 күн бұрын
Makape awa a mcp sadziwa chilichose koma kumba ungule basi
@WilsonNedi-s6t
@WilsonNedi-s6t 8 күн бұрын
Kkkkkkkkkkkkk zuchita kuwonekeratu
@TelezaManyera
@TelezaManyera 5 күн бұрын
Mkumanama kumati Lilongwe ndi chipinda cha MCP zamanyazi,chawo palibepo gangata kumeneko ndikwake basi.
@ChisomoSaiti
@ChisomoSaiti 8 күн бұрын
Chikangawa Chala mwamba
@WarriorKB-l3i
@WarriorKB-l3i 6 күн бұрын
Kkkkk chala mmwamba ndi dpp apapa anthu amayiwuza mbuzi ya mcp kuti kunoku sinu olandilidwa koma ndi kwa dpp dzosaowa kufunsa ichi ndichitsimikizo choti anthu chikangawa sitikumufuna, muwone olo a zimayi avala za mcp ali ndi manyazi 💙💙💙💙💙💙💙💙boma! Mcp ifune, isafune APM boma!
@AlieNkalapwagaNkalapwaga
@AlieNkalapwagaNkalapwaga 8 күн бұрын
Sanger konde and
@SherifaG.Mlelemba
@SherifaG.Mlelemba 8 күн бұрын
Iiiii! Aziona anzathu a boma ndilomweli😮
@hanifahmponda8711
@hanifahmponda8711 5 күн бұрын
Kkkkk a MCP anyanayo game DZIKO LATILUKA ANGOKAKAMIDZA ANTHU KOMA ANTHU ATHANA NAYO MCP MUDZINGODALIA MACHINE OBELA CHITSANKHO BASI OSATI VOTE YACHILUNGAMO SUMUNGAWINE NDINTHU
@ChifundoNinje
@ChifundoNinje 5 күн бұрын
Mmmmmmm😂😂😂😂😂
@ChriOffice
@ChriOffice 5 күн бұрын
Ndie one koma chala mwamba
@RosinaPatel
@RosinaPatel 7 күн бұрын
Chala mwambaaaaaaaaa
@chirwaellace1093
@chirwaellace1093 4 күн бұрын
😅😅😅😅😅
@VictorSiwale-e4v
@VictorSiwale-e4v 5 күн бұрын
Chakwela anabwela kupha a Malawi ndi Chipani cha mcp, ndeno mcp wake up rise against chakwela he has to resign otherwise no mp will win elections the whole country
@LeonardJere-h8s
@LeonardJere-h8s 8 күн бұрын
Anyway Dpp my vote
@AlexanderTraffick
@AlexanderTraffick 8 күн бұрын
Ntandile home ground yanga
@kaphika
@kaphika 5 күн бұрын
Akukuwa ndi anthu awiri basi, sinkhani
@AdamAhamad-g7u
@AdamAhamad-g7u Күн бұрын
Kumtumbo kwanu agalu a MCP anthu okupha
@PatsonmahoweNyirongo
@PatsonmahoweNyirongo 7 күн бұрын
Jesie akuti bwanji akawona apo
@josephalfred5138
@josephalfred5138 8 күн бұрын
Achoka agalu amenewa atikwana ndipo sakuyenelaso kupita Kwa amalawi atinzunza asatifune lelo
@SamLongwe-y9b
@SamLongwe-y9b 6 күн бұрын
Amakuwa ndiwa dpp osat zina
@SaidiMilaji-dk8sr
@SaidiMilaji-dk8sr 8 күн бұрын
Dpp iwina opanda campaign
@BensonJere-i9k
@BensonJere-i9k 7 күн бұрын
🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣
@MandalaChaona
@MandalaChaona 5 күн бұрын
Ndiye azinamizana Kuti adzabere Zisankho aaaaaa pa ground zochitika zikuchita kufotokoza zokha MCP MLUNGU wayikana ndipo musawakakamize Amalawi Chifukwa Ulamuliro wanu uzakhala opweteka
@chitanibenito1109
@chitanibenito1109 6 күн бұрын
Chipani chopasa manyazi very sorry!!!
@JonathanBonongwe-f3s
@JonathanBonongwe-f3s 8 күн бұрын
Angotula pansi dzawalaka akagwere uko
@ElizaSoko
@ElizaSoko 5 күн бұрын
🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣ndasekaaa🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤗🤗🤗🤗🤗
Mr Jokes Performing live at Mzuzu University, (Full Video)
33:43
Quilt Challenge, No Skills, Just Luck#Funnyfamily #Partygames #Funny
00:32
Family Games Media
Рет қаралды 55 МЛН
Что-что Мурсдей говорит? 💭 #симбочка #симба #мурсдей
00:19
VIP ACCESS
00:47
Natan por Aí
Рет қаралды 30 МЛН
The Best Band 😅 #toshleh #viralshort
00:11
Toshleh
Рет қаралды 22 МЛН
Quilt Challenge, No Skills, Just Luck#Funnyfamily #Partygames #Funny
00:32
Family Games Media
Рет қаралды 55 МЛН