Пікірлер
@FarookYahaya
@FarookYahaya Минут бұрын
Bakili muluzi tv Ilibe mbali
@FarookYahaya
@FarookYahaya Минут бұрын
Bakili muluzi tv Ilibe mbali
@AlexKaunda-w7l
@AlexKaunda-w7l 5 минут бұрын
Tilibe ntchito ndi mcp akuchinda kwambili too much kupakula nyemba
@liliantamaona1669
@liliantamaona1669 9 минут бұрын
Wa MCP yu, musamuyankhe
@ChikupizgaKajawaMkandawire
@ChikupizgaKajawaMkandawire 10 минут бұрын
Ndiye ngati simmazitsa mmafunilanji kutinamiza
@WilsonNedi-s6t
@WilsonNedi-s6t 12 минут бұрын
Lero akambako za mzeru apule
@AlfredGanizani-v9f
@AlfredGanizani-v9f 17 минут бұрын
Muzatipase musaiware ikatuluka bwana timakunyadiran coz simumakamba zonyoza
@HarryChindiwo-p2i
@HarryChindiwo-p2i 19 минут бұрын
Nzake wake wa Kagame mbuzi iyi
@EmilyKanyika
@EmilyKanyika 22 минут бұрын
Zoovota kumalawi
@PhiriChiyambi
@PhiriChiyambi 23 минут бұрын
Wakambako za mzeru
@AlfredGanizani-v9f
@AlfredGanizani-v9f 25 минут бұрын
😅😅 tingodikira kut give zambili my vote to my chakwera is number one
@CharlesMukona
@CharlesMukona 29 минут бұрын
Mwazi wamunhu sizibwana mulumana
@FrancisStima-sc7zs
@FrancisStima-sc7zs 29 минут бұрын
Waachosa chifukwa alimbali ya kagame
@HusseinMofatt
@HusseinMofatt 30 минут бұрын
tímakunyàdílà àíse
@IbrahimWilliam-s8i
@IbrahimWilliam-s8i 32 минут бұрын
timakudalirani
@HusseinMofatt
@HusseinMofatt 37 минут бұрын
zikungofanana mosemuja
@AkimuKambalame
@AkimuKambalame 41 минут бұрын
Km chakwera akuona zmenez?
@FabianoKasonya
@FabianoKasonya 43 минут бұрын
MCP ikunama agogo amwewo basi
@JudithKatungwe
@JudithKatungwe 46 минут бұрын
Ameen🙏
@MphatsoChilangiza
@MphatsoChilangiza 47 минут бұрын
Iwe chakwera pamenepo pokha ndakukondako wachita bwino kwambili koma my vote ikapita ku dpp
@JUMAHSabiti
@JUMAHSabiti 48 минут бұрын
Palibe kunyoza kulikonse nkhaniyi ndiyoona ndipo pakufunika kuganiza bwino
@DONNEXKhama-bk1gy
@DONNEXKhama-bk1gy 48 минут бұрын
Zikuchitika ku malawi zomvesa chison kwambiri ngakhale andale akuba ndalama ndikulakwa chabe kma zafikapa ambiri atha kufa ndithu
@SostenPiyo-q8z
@SostenPiyo-q8z 51 минут бұрын
Mulungu amaona don't compete with God he is alone if he faces away from you know that you're gone,mukutaya nthawi yambani kulapa ndikuyamba kupemphera basi chifukwa MCP singawine am not politcian
@JohnWilliam-i9t
@JohnWilliam-i9t 54 минут бұрын
Achita bwino kulamula kuti achokeko
@TalumbaMsango
@TalumbaMsango 55 минут бұрын
Tiponyeren nyimbo imeneyo
@AtupeleMvula
@AtupeleMvula 55 минут бұрын
Ulibo mr Dj munyanane timawafila ma program anu😂😂😂😂😂 more fire 🔥
@ChikuMega
@ChikuMega 58 минут бұрын
Atitenga pokhapokha chakwela akachoka pa mpando
@HildaMbizi
@HildaMbizi 58 минут бұрын
MCP DPP nonse tinakuonani kale UTM my vote
@joempesi
@joempesi Сағат бұрын
Komanso azibusa inuyo mumapemphera mu chooona? Ndinudi atumuki a Mulungu? Koma mukudziwa kt Mukadzafa muzaweruzidwa? Oky ndi pemphere nanenso. Kwa ife ayi kwa ife ayi koma kwa zibusa onse amene asakufunira Malawi zabwino zabwino. Muwakathe azibusa amenewa ndi mabanja awo ndipo muwachotsere mwai wao. Achite manyazi pa September pano Amen
@George-zd5le
@George-zd5le Сағат бұрын
Kkkk koma Asa chakwera ayai
@ChristopherMwale-u7n
@ChristopherMwale-u7n Сағат бұрын
Monivoryeyaveh.
@eunicesaiti
@eunicesaiti Сағат бұрын
Ndipo Zikomo, Our soldiers must come back home and 🙏
@dumisanimoyo3152
@dumisanimoyo3152 Сағат бұрын
A a ameneyo si bakili tv shame
@joempesi
@joempesi Сағат бұрын
Mu mdzina la Yesu nkhristu Amen
@Lizzie-h1k
@Lizzie-h1k Сағат бұрын
Nkhani ndi DPP....I think even Chakwera is planning to join DPP , there is no question about that!
@LukaSamson-w5h
@LukaSamson-w5h Сағат бұрын
Chonde bola Malawi atengedwe abale
@BENSONRANGWANI
@BENSONRANGWANI Сағат бұрын
Achakwela munaphelanji chilima soka ndi thembelelo likhale pamu pako
@Lizzie-h1k
@Lizzie-h1k Сағат бұрын
Malawi trends ndaikonda....pena imabweretsa zinthu zoti ena saangadzipeze😅😅😅😅...awatu zawo zada...kkkkk...MP wanzeru apitiletu ku DPP...akapange nao ma primaries!
@DokisoKayuni-x6i
@DokisoKayuni-x6i Сағат бұрын
Ngati chilima anawononga nao zikoli nanga kambambe walakwa chani msiyeni kabambe ayesepo
@FrankBottoman-v4x
@FrankBottoman-v4x Сағат бұрын
Kwamuthu ozindikila ndimulandu
@NASP-g7h
@NASP-g7h Сағат бұрын
Kodi panoptu or pule bakili amatulutsa video pule number one to view
@NASP-g7h
@NASP-g7h Сағат бұрын
Bakili ndi one anabwera kuzailila zodiac pot pano inafooka...ndipo muluz wanena zoona kwambli ndipo bakili sangampange hack aja madala computer amaiyaza kwambli
@FrancisNyayi
@FrancisNyayi Сағат бұрын
Wabakili sabwera bwera pafupi ziiii
@FrancisNyayi
@FrancisNyayi Сағат бұрын
Who said ahhhh Like me here when listening
@Felista-m4q
@Felista-m4q Сағат бұрын
Tikunzunzika atitenge
@Enock-gu5ff
@Enock-gu5ff Сағат бұрын
Komatu akunena zoona zokha zokha ntumikiyu makosana
@MphatsoKakole
@MphatsoKakole Сағат бұрын
Atengedi Iiìiii tatopa
@MonicaThocco
@MonicaThocco Сағат бұрын
Komatu akufanana khopezi ngati ndi abale awo ,kkkkkk nde iwowa azitenga kuti ndi woyera ?
@ChinsinsiKantumba-p1u
@ChinsinsiKantumba-p1u 2 сағат бұрын
Mcp mukuchedwa inu
@MonicaThocco
@MonicaThocco 2 сағат бұрын
Mwina amafuna ndalama, pofuna kumamudyera ,pali zinsinsi zeni zeni ,zikadziwika ku khotiko