Mulungu amaona don't compete with God he is alone if he faces away from you know that you're gone,mukutaya nthawi yambani kulapa ndikuyamba kupemphera basi chifukwa MCP singawine am not politcian
@JohnWilliam-i9t54 минут бұрын
Achita bwino kulamula kuti achokeko
@TalumbaMsango55 минут бұрын
Tiponyeren nyimbo imeneyo
@AtupeleMvula55 минут бұрын
Ulibo mr Dj munyanane timawafila ma program anu😂😂😂😂😂 more fire 🔥
@ChikuMega58 минут бұрын
Atitenga pokhapokha chakwela akachoka pa mpando
@HildaMbizi58 минут бұрын
MCP DPP nonse tinakuonani kale UTM my vote
@joempesiСағат бұрын
Komanso azibusa inuyo mumapemphera mu chooona? Ndinudi atumuki a Mulungu? Koma mukudziwa kt Mukadzafa muzaweruzidwa? Oky ndi pemphere nanenso. Kwa ife ayi kwa ife ayi koma kwa zibusa onse amene asakufunira Malawi zabwino zabwino. Muwakathe azibusa amenewa ndi mabanja awo ndipo muwachotsere mwai wao. Achite manyazi pa September pano Amen
@George-zd5leСағат бұрын
Kkkk koma Asa chakwera ayai
@ChristopherMwale-u7nСағат бұрын
Monivoryeyaveh.
@eunicesaitiСағат бұрын
Ndipo Zikomo, Our soldiers must come back home and 🙏
@dumisanimoyo3152Сағат бұрын
A a ameneyo si bakili tv shame
@joempesiСағат бұрын
Mu mdzina la Yesu nkhristu Amen
@Lizzie-h1kСағат бұрын
Nkhani ndi DPP....I think even Chakwera is planning to join DPP , there is no question about that!
@LukaSamson-w5hСағат бұрын
Chonde bola Malawi atengedwe abale
@BENSONRANGWANIСағат бұрын
Achakwela munaphelanji chilima soka ndi thembelelo likhale pamu pako
@Lizzie-h1kСағат бұрын
Malawi trends ndaikonda....pena imabweretsa zinthu zoti ena saangadzipeze😅😅😅😅...awatu zawo zada...kkkkk...MP wanzeru apitiletu ku DPP...akapange nao ma primaries!
Kodi panoptu or pule bakili amatulutsa video pule number one to view
@NASP-g7hСағат бұрын
Bakili ndi one anabwera kuzailila zodiac pot pano inafooka...ndipo muluz wanena zoona kwambli ndipo bakili sangampange hack aja madala computer amaiyaza kwambli