A TIMOTHY NTAMBO KU NSOKHANO WA AFORD KU DOWA 19 May 2024

  Рет қаралды 38,714

HOT 265

HOT 265

25 күн бұрын

Пікірлер: 102
@user-lu8px7td6p
@user-lu8px7td6p 22 күн бұрын
Apm my vote
@user-hk1lp2ho9w
@user-hk1lp2ho9w 23 күн бұрын
ANTAMBO ACHIHANA MWAYANKHULA BWINO KWAMBIRI GOD BLESS YOU
@stevenfrancism3638
@stevenfrancism3638 22 күн бұрын
Wachita bwino kupepesa malangizo a the DC ❤❤❤❤
@user-rd2td7bg4c
@user-rd2td7bg4c 23 күн бұрын
❤❤❤ kuli wa mcp ko akhoza kuzikozelatu😂😂😂
@user-nf3ik3ff6y
@user-nf3ik3ff6y 22 күн бұрын
Moto buu Good message ❤
@AlexManuelMisomali-sv1vn
@AlexManuelMisomali-sv1vn 21 күн бұрын
Mbuzi yamunthu yomwe inapeleka miyoyo ya anthu kwa mimbulu
@PrinceKachimanga
@PrinceKachimanga 23 күн бұрын
koma MTAMBO ukatichotsela a Chakwera.IWEYO UKHALADI HERO.CUZ TATOPA NDI CHAKWERA
@GulliverTower
@GulliverTower 21 күн бұрын
Ubalira Ase . MCP 2025 Bomaaaaa , DPP is just useless.
@jemasmasimbi8109
@jemasmasimbi8109 23 күн бұрын
nice speech....
@stevenfrancism3638
@stevenfrancism3638 22 күн бұрын
🎉wachitabwino kupepesa mtambo.❤❤❤❤
@NgomaRaheem
@NgomaRaheem 22 күн бұрын
Apa Mtambo nde wayankhulano kupepesa ndegwelo logonjalo big up
@DONNEXKhama-bk1gy
@DONNEXKhama-bk1gy 22 күн бұрын
Ukapepesa umapeza mtendere thanks 🙏
@jamesgama5489
@jamesgama5489 22 күн бұрын
Comrade kumeneko nde kukhala zinthu zikavuta kumapepesa akhwana heavy.
@amoschataika7440
@amoschataika7440 22 күн бұрын
Big up Brother Ntambo pena umaganiza boo penaso umayitaya Game.
@Rose-tr6pn
@Rose-tr6pn 22 күн бұрын
Aford sidzawinaso muja anayambila ndiliti limenelija ndiye akawine pano 😂😂😂
@Blessings-td4cr
@Blessings-td4cr 23 күн бұрын
Eya zimafunika choncho,muthu azimva malangizo kwa ena mwapepesabe,bolaniko.
@user-jm8kw9gw2d
@user-jm8kw9gw2d 19 күн бұрын
There's hope, afford party is going to rule this country
@YellowmanMalawi-qe8zh
@YellowmanMalawi-qe8zh 22 күн бұрын
Mwa inu nokha simungawine,pangani alliance
@ManganiStanley
@ManganiStanley 22 күн бұрын
Onsewa ndi akuba
@user-nf3ik3ff6y
@user-nf3ik3ff6y 22 күн бұрын
❤❤❤ number one moto buu
@user-nf3ik3ff6y
@user-nf3ik3ff6y 22 күн бұрын
Good message
@princessyvonnesinoya6571
@princessyvonnesinoya6571 22 күн бұрын
Chilungamo chiyende ngatu madzi chihana
@stalickkafera3454
@stalickkafera3454 23 күн бұрын
Kusowa zo sapoter
@KassimmwStevenetc
@KassimmwStevenetc 21 күн бұрын
Sitingataye thawi kuba 'fundo za ntambo Tambo ndiwa boza owukira amakamba zithu akawina kut wavutika korowera Bora komawonera TV osat zakhutu kuve iyi
@stanleykaludzu-bm4pm
@stanleykaludzu-bm4pm 23 күн бұрын
More fire Aford
@AndrewChimwaza-rf7hw
@AndrewChimwaza-rf7hw 23 күн бұрын
Timothy ntambo ndinu opepela munaononga kale ziko la malawi ndipo tikudziwa kt mwatumidwa ndi chakwera musokoneze DPP nkhanga zaona. APM my vote
@user-fl7br3dw4h
@user-fl7br3dw4h 23 күн бұрын
What ever koma walakhula za dzelu antambo tiyeni nadzo tilimbane nawo mpaka tikafike
@GeeGuu-zy4oi
@GeeGuu-zy4oi 23 күн бұрын
@@user-fl7br3dw4h u r right
@user-jn9tz3li3v
@user-jn9tz3li3v 23 күн бұрын
​@@user-fl7br3dw4hThe devil 👿 also knows the bible, do not be blinded
@Kasawalah
@Kasawalah 22 күн бұрын
Yes it's true make alliance kuti muphe chakwela mbava
@ibrahmdoka7486
@ibrahmdoka7486 23 күн бұрын
Apology received We take neither side in receiving Still we feel pain because of those whom you put in power
@user-he4jv1sb1m
@user-he4jv1sb1m 23 күн бұрын
Kuzaononga chipani
@JonesChingaya-yf4gg
@JonesChingaya-yf4gg 23 күн бұрын
Mtambo ndiwe oseketsa kwabasi, posachedwapa pa zodiak unanenetsa kut sungapepese chifukwa palibe chifukwa chopepesera, ndie lero uzikat ndikukupepesani amalawi zoona????? Koma anthu mukamafuna ma votii, ayi zikomo.
@AUSTENBUSHIRI
@AUSTENBUSHIRI 22 күн бұрын
Amtambo azindikila liti kuti amalakwisa kkkk my malawi
@OwenMajoni-qv3eg
@OwenMajoni-qv3eg 22 күн бұрын
Sindi sapota zipani zotsogozedwa ndi banja limodzi.
@user-vw7tj2ss3l
@user-vw7tj2ss3l 21 күн бұрын
Nonse ndin mbala
@KanyozaMatope
@KanyozaMatope 23 күн бұрын
Ndinkafuna ndigale ndichidwe.. koma chifukwa Cha Mtambo... Aaaaaaa.. bsi
@user-oc9vl9xz8e
@user-oc9vl9xz8e 22 күн бұрын
Freedom fighter
@mcsellahntv6896
@mcsellahntv6896 23 күн бұрын
Popanda nfundo, tingonva za akamuzu apa.
@user-dp7bc7yy6s
@user-dp7bc7yy6s 23 күн бұрын
Or mutabwaza bwanji km chikhulupiliro chikataika zimakhala povuta kut uchibwezeletse
@jameshuwanzulu
@jameshuwanzulu 23 күн бұрын
Ayi man peter munthalika anthu anataya naye chikhulupirilo lero bwanji anthu abwezeletsaso chikhulupiro mwa iye
@user-vl5on2lj8b
@user-vl5on2lj8b 22 күн бұрын
Chikapanda kukuthamangisa ku m c p ukanakapepesera kutu ? Tikudziwa kuti ukupepesa chifukwa anakuthamangisa ku m c p
@AllanChabwela
@AllanChabwela 22 күн бұрын
Mtambo,wabudula nmemo wagulu
@vytwistthelion98
@vytwistthelion98 22 күн бұрын
A Ntambo kutha ma plani kanamizeni ena
@josephykapichi3647
@josephykapichi3647 23 күн бұрын
Following
@giftbanda7690
@giftbanda7690 23 күн бұрын
Or pa chikondi mukhale mwasiyana ndee muzbwerelaneso mmmh Love imasiyana amwene than the past nde awawa asatipepeleseso😅😅
@eliffagondewe8214
@eliffagondewe8214 23 күн бұрын
🔥🔥🔥🔥🔥
@user-dv6rt6vb6e
@user-dv6rt6vb6e 23 күн бұрын
After kuchotsedwa unduna
@user-zv3cy2xj5p
@user-zv3cy2xj5p 22 күн бұрын
Mwana wathu wathu, osaopa
@GraceLimani-zw7dx
@GraceLimani-zw7dx 22 күн бұрын
Wa hit a bwino kupepesa mtambo ku mtundu wa Malawi unazitenga for granted kuli konse ukupita uwapepesedi a Malawi inawononga Malawi ndi iweyo kuwaphuzitsa ma demo achimata amaononga katundu wa anthu ndiye mupepesedi amtambo
@chekiamaabdul5083
@chekiamaabdul5083 22 күн бұрын
Chiphwala cosadulacho GaLu
@ManzyNgoleka
@ManzyNgoleka 23 күн бұрын
Mwadziwa liti kuti ndinu adolo inu 😂😂😂😂 abusa aja osadzawaphwekesa anasefa zisilu zadyera zonse
@GodfreyKampezeni
@GodfreyKampezeni 22 күн бұрын
Pa mtumbo pako mtambo ndi mzakoyo
@EnockChibwilo-kv8oq
@EnockChibwilo-kv8oq 22 күн бұрын
Iwe ndiwe garu kwabs chifkwa anakuchosa garu zakouja
@petermsamariamapira8933
@petermsamariamapira8933 23 күн бұрын
Mtsing,anga ndi meneri saona za kutsogoro ayi ,never apo ayi ,only Mulungu amaona za tsogoro
@PatriciaTikhiwa
@PatriciaTikhiwa 22 күн бұрын
Koma mulungu amasadamuzadi zithu. Ndaonera Timothy
@user-zk7jw9up6m
@user-zk7jw9up6m 23 күн бұрын
Mwayankhula bwino lelo silut mtambo
@MaryTchapo-py4hh
@MaryTchapo-py4hh 22 күн бұрын
Chitsiru iwe ndi mcp yako ndi lazaro wako wakuba ngat bambo ako omwe
@user-nx7yz4qo8f
@user-nx7yz4qo8f 23 күн бұрын
Zikomo kamba kopepesa Mr mtambo,coz eeee tipseleratu PANO tasala thako limodz,Lina ladyeka ndi njala
@user-mv1er5zr7e
@user-mv1er5zr7e 22 күн бұрын
Kkkkkk
@user-wx5fq7gg7d
@user-wx5fq7gg7d 20 күн бұрын
😂😂😂😂😂😂 kma abale
@petermsamariamapira8933
@petermsamariamapira8933 23 күн бұрын
Mavuto alipo ,ndipo ndale nkanyama nkofutadi kkkk
@francisvisage2705
@francisvisage2705 23 күн бұрын
Camera man is not doing his job...
@antonioaugustochikopa8146
@antonioaugustochikopa8146 22 күн бұрын
Moto moto
@innocentkandulu2825
@innocentkandulu2825 23 күн бұрын
apa afod basi siyingawineso
@MussaMhango-ep9bt
@MussaMhango-ep9bt 23 күн бұрын
Masanje eni eni
@user-bw9sr7dm9h
@user-bw9sr7dm9h 23 күн бұрын
Khakhakha kkkkk
@PrinceKachimanga
@PrinceKachimanga 23 күн бұрын
AFORD......😂😂😂😂😂😂😂
@salimmkumakumakitombi-yc7pw
@salimmkumakumakitombi-yc7pw 23 күн бұрын
Mpunga uja wathulidwa Tchenga bansi
@tisuhmakhwah7085
@tisuhmakhwah7085 23 күн бұрын
I feel ka fungo ka mcp umumu
@Chiso2019
@Chiso2019 23 күн бұрын
Zachibwana zenizeni
@user-yq1mc3nm1f
@user-yq1mc3nm1f 22 күн бұрын
Kuyenda ndi chisekwete chimenechi zachiziwikire kuti ma mp olo atatu sazawapezanso kkkkk
@user-vl5on2lj8b
@user-vl5on2lj8b 22 күн бұрын
Chakwera iweyo nkhati ukudziwa kuti udzawina ,2025 usiye kutuma zigawenga zinzako kukhapa anthu pansonkhano anthu tikufuna machitidwe osati uchigawenga wakowo komanso usiyiretu kusaka B K
@oskidooscar7468
@oskidooscar7468 22 күн бұрын
Palibe president amakwanisa kuyamkhula chichewa Ndinu makape kobas
@JayMilazi-fv6px
@JayMilazi-fv6px 22 күн бұрын
Takambani mfundo apa history ya kamuzu ndi chani nthawi ino ndiyoti muzitiuza mfundo zogwira mtima osati zama history
@beatricekamwendo-ow1ok
@beatricekamwendo-ow1ok 22 күн бұрын
Aford boma kale wina afune asafune
@francisvisage2705
@francisvisage2705 23 күн бұрын
Media people??! Voice and capturing is so poor
@user-nw6ie3xx8b
@user-nw6ie3xx8b 22 күн бұрын
U can't even thanks chakwera iwe pakati pano mulindindalama coz of chakwera
@AmosBurnet-te4rg
@AmosBurnet-te4rg 22 күн бұрын
Mafakitale ake mubuwerse muwatenga kut palibe chachilendo chomwe mungatiuze
@Trancy-xt4py
@Trancy-xt4py 23 күн бұрын
Mcp yayamba kale kunjenjemera
@MussaMhango-ep9bt
@MussaMhango-ep9bt 23 күн бұрын
Wafuntha uyu
@GraceLimani-zw7dx
@GraceLimani-zw7dx 22 күн бұрын
Ndiye lero ukupepesa ku mtundu wa Malawi lero mesa pa zodiak unka kana kupepesa ku mtundu wa Malawi lero wapepesa bwa?
@user-zk7jw9up6m
@user-zk7jw9up6m 23 күн бұрын
Komaso mwachita bwino kupepesa zikomo
@PrinceKachimanga
@PrinceKachimanga 23 күн бұрын
iwe...ife tikufuna ADADIE.....APM
@spargomw
@spargomw 22 күн бұрын
Nganganga kumbuyo kwa Adad❤❤❤
@ChikondiChauma-ib9pg
@ChikondiChauma-ib9pg 22 күн бұрын
Asilikali or a security 🤔 😅
@user-ln3zx6wo4w
@user-ln3zx6wo4w 23 күн бұрын
Chakachamawa ikupita mcp
@BlessingsTembenu
@BlessingsTembenu 22 күн бұрын
Nsilikali amakhumata? Aaaa
@user-vl8uw8mc3u
@user-vl8uw8mc3u 22 күн бұрын
Dpp boma Apm boma basi
@ashadokhomzy5781
@ashadokhomzy5781 23 күн бұрын
A Ntambo sopano tinamizeninso tilipano kumvesela
@petermsamariamapira8933
@petermsamariamapira8933 23 күн бұрын
Kodi atinamize kkkkkk
@JonesChingaya-yf4gg
@JonesChingaya-yf4gg 23 күн бұрын
Kkkkkkkkkk
@assankamwendo852
@assankamwendo852 22 күн бұрын
Mr Mtambo Thanks for help Malawian to remove APM anatikwana makamaka ndi Chisale wake uja Thanks for giving us good government ever. Better you stop here otherwise you can't manage to remove our almighty Dr Lazarus MacCathy Chakwela. Viva MCP,Viva Malawi MCP Upto 2050 wooooh
@dondamissonchdziwe3958
@dondamissonchdziwe3958 23 күн бұрын
Koma Enoch,ndiwe waukali pitiriza Chakwera Ndi khakhakha mzake wa katumbu amangonya nkhanu zokhazokha, Koma heee zirrikoooo
@user-ux9ik4zr5x
@user-ux9ik4zr5x 22 күн бұрын
Can't support this nonsense,he's doing this because of his dismissal from Cabinet,he's just greedy & selfish trying to take Malawians for granted.
@GulliverTower
@GulliverTower 21 күн бұрын
Afford is just useless . T. Mtambo is a desperate man ,hz no direction 😂
@RobertDJambo
@RobertDJambo 21 күн бұрын
Mtambo nd opepera uyu
@SamsonMokowa
@SamsonMokowa 22 күн бұрын
This guy has no interest to human being
@PatriciaTikhiwa
@PatriciaTikhiwa 22 күн бұрын
Koma mulungu amasadamuzadi zithu. Ndaonera Timothy
Iindaba zesiXhosa @19H00 | 11 June 2024
20:45
SABC Iindaba
Рет қаралды 10 М.
KUMALO KOMWE NDEGE IDAGWELA😭😭 RIP
20:44
HOT 265
Рет қаралды 61 М.
Climbing to 18M Subscribers 🎉
00:32
Matt Larose
Рет қаралды 14 МЛН
I Built a Shelter House For myself and Сat🐱📦🏠
00:35
TooTool
Рет қаралды 28 МЛН
СНЕЖКИ ЛЕТОМ?? #shorts
00:30
Паша Осадчий
Рет қаралды 2,7 МЛН
A Malawi Mulimbe Mtima - Bon Kalindo
10:30
Nyasa VoiceBox
Рет қаралды 27 М.
EXCLUSIVE INTERVIEW WITH ENOCK CHIHANA
56:27
Zodiak Malawi
Рет қаралды 51 М.
ZOMWE WAYANKHULA WANKULU WA ASILIKALI
13:35
HOT 265
Рет қаралды 60 М.
TIMOTHY MTAMBO KUTHAMBITSIDWA NDIMAFUNSO UKU...
59:42
LIKI-LIKI TELEVISION
Рет қаралды 61 М.
WATCH THIS IF YOU WANT A ONE ON ONE PROPHETIC MOMENT WITH PROPHET KAKANDE.
43:15
The Kakande Ministries
Рет қаралды 89 М.
Times Exclusive featuring Enoch Chihana - 20 May 2023
1:00:04
Times 360 Malawi
Рет қаралды 24 М.
BON KALINDO 10 JUNE 2024
13:59
HOT 265
Рет қаралды 16 М.
Cruise 5 with Prophet Habakkuk Stanford Sinyangwe
1:06:02
Joab Frank Chakhaza
Рет қаралды 91 М.
Climbing to 18M Subscribers 🎉
00:32
Matt Larose
Рет қаралды 14 МЛН