A ZIKHALE NG'OMA UKU NDIYE KWATENTHA🙌🙌🙌 TAMVANI MFUNDO ZOMWE ABWELA NAZO

  Рет қаралды 39,088

HOT 265

HOT 265

26 күн бұрын

Пікірлер: 540
@UseniMailosi
@UseniMailosi 24 күн бұрын
Malawi chikangawa party
@MaxWell-d7o
@MaxWell-d7o 24 күн бұрын
😂😂😂
@Allan-bk1
@Allan-bk1 23 күн бұрын
😂😂😂😂😂
@ackimchindimba9912
@ackimchindimba9912 24 күн бұрын
Mudyeleni apapa ndalama ziyamba kuphweka bas ndi kampeniyi tiyeni tiwadyele koma tonse ndikudziwa kuti ndife APM
@corretabanda7685
@corretabanda7685 24 күн бұрын
Nyama za mmanyumba mwanu. God is good and his eyes can see even in the heart of everyone. It will not work in the Name of Jesus
@user-wq3dh1ly2o
@user-wq3dh1ly2o 22 күн бұрын
Olo patavuta bwanji simungalamulileso dziko la malawi chifukwa munataya chipangano ambuye sangalole kuti mutilamulile anthu akupha inu
@anniedennis7127
@anniedennis7127 24 күн бұрын
Ng'ona zodya anthu zingalamulire anthu
@JumaGadaff
@JumaGadaff 16 күн бұрын
Bwana kuvota tidzavota koma dziwani kuti muli ndi mulandu ku chikangawa zikomo mulungu ankhale Nanu amen 🙏🙏🙏🙏
@spargomw
@spargomw 24 күн бұрын
Zikhale Ng'oma😂😂😂😂 tsitsi muzipesako tisamakugemuleni zonse😂😂
@PatriciaMbewe-xn7ke
@PatriciaMbewe-xn7ke 24 күн бұрын
😂😂😂😂😂
@MaryNyirenda-nq3mh
@MaryNyirenda-nq3mh 23 күн бұрын
Kukhwima afiti
@nadiahPhiri
@nadiahPhiri 23 күн бұрын
Umfiti sizinthu
@user-wu4tl2yn9e
@user-wu4tl2yn9e 24 күн бұрын
Before kuvota aliyense azizakumbuka kuchikangawa
@CatherineDesire
@CatherineDesire 24 күн бұрын
Eish ndipo 😭😭😭
@MeleckDennis-vg3bv
@MeleckDennis-vg3bv 24 күн бұрын
Zopusa zokhazokha mfiti za anthu,kwanu kwathapo agalu inu
@BrunoMbewe-xj1yy
@BrunoMbewe-xj1yy 22 күн бұрын
Ndangothokoza kuti mene mumampephelamo mu Mpephero lanu nonse simuna mutchulemo Yesu khristu.Zaoneka kuti inuyo mwazi wayesu simunauziwe mene munagwilira ntchito, pitilizani kugwira ntchito zakumidimazo.
@Sammy-vb1ed
@Sammy-vb1ed 23 күн бұрын
Mudzina la yesu krist ndikupemphera kut uone zowawawa zikhale
@Gmtmphats124gy
@Gmtmphats124gy 24 күн бұрын
Akanakhala kuti mulungu amalanga mpompo mpompo akanakuthilan moto pasokhano wanu omweo
@ChristopherKawilam
@ChristopherKawilam 23 күн бұрын
Ngat boza bro
@giftmaliwa2385
@giftmaliwa2385 24 күн бұрын
Za make Dzana this new generation
@user-eg8wx8oi5z
@user-eg8wx8oi5z 23 күн бұрын
Now it makes sense kod nkhumbai Nd mtumbuka eti😂😂
@user-cd4df3vg4y
@user-cd4df3vg4y 24 күн бұрын
Dzigawenga dzawanthu anthu akupha inuuu ng'ona zomwe mwachita pakupha abale athu asanu ndi anayi aja kuchikangawa dziko lonse lapansi ladziwa choonadi chifukwa ma German aja anenana zonse kuti black box inali ku palace.Ndipo anenaso kuti ndichiwembu chomwe munakonza.Pomwe inu muli pheee kufuna kutiuza bodza, ife tadziwa kale ndipo muyaluka
@AminaPhiri-pp9tw
@AminaPhiri-pp9tw 23 күн бұрын
Mukumbukeni chilima amene munamupha uja azikhale ng.oma ndipo zimu wake ukufinyeni ndipo khalira pomwe
@sanlakedickson6780
@sanlakedickson6780 24 күн бұрын
ana asatana awa Mzimu wa chilima ukuvutitsani
@lawrencekauwa8005
@lawrencekauwa8005 22 күн бұрын
Kkkkkkk,,,, to be a supporter 🙌
@ephraimmbiza9727
@ephraimmbiza9727 21 күн бұрын
Most important thing is that you know yourself that you will not come back in government
@RobertChisenga-ci2mq
@RobertChisenga-ci2mq 24 күн бұрын
Do you think karonga's ndizitsilu? Poti kukaronga kuliso mbudzi ndizomwe zilikumenekozo
@LindaNkwazi
@LindaNkwazi 20 күн бұрын
U r still remembering chikangawa
@georgemponda
@georgemponda 24 күн бұрын
Mbuli izi😂😂😂😂 Zikhalebg'oma nde panja penipeni
@user-sh1rj3ol3t
@user-sh1rj3ol3t 24 күн бұрын
But tu Laz has failed Malawians way more than APM
@ustintembo
@ustintembo 24 күн бұрын
Ndipo inu mmm..
@peterjoshua2595
@peterjoshua2595 22 күн бұрын
100% sure
@millionsenenje5010
@millionsenenje5010 23 күн бұрын
Mr Kamuyambeni ndiinu bambo wanga koma pena pake mhhhhhhh
@juntoiman
@juntoiman 24 күн бұрын
Pathako panu nonse Zikhale Ng'oma pantumbo pako wamva
@sharifujoe7633
@sharifujoe7633 23 күн бұрын
Uyu sikhale ngoma same like idi ameen
@TopoTopo-bm4vw
@TopoTopo-bm4vw 24 күн бұрын
😂😂😂😂 tango mdyelani ndalamazo azakhumudwa ameneyo
@FrancoKaunga-rq2ki
@FrancoKaunga-rq2ki 24 күн бұрын
Zikhale ngoma nkhope ngati kazizi mfwiti zawanthu! Kwacha kwacha 😂zakale kale. Kasi nkhumeta uli uko zikhale ngoma?
@FrankHaruni
@FrankHaruni 24 күн бұрын
😂😂😂😂 awande manyiwo😅😅😅😅
@EphraimNaveya-hz1du
@EphraimNaveya-hz1du 15 күн бұрын
Za ziiiiiii afiti simungazawine muli ndi magazi kale
@HassanMbalaka-gb5sv
@HassanMbalaka-gb5sv 23 күн бұрын
Palinyimbo inayake amat paulendooo paulendooo aaaayeee paulendoooo. Awakwao kwantha
@BittonRashid
@BittonRashid 22 күн бұрын
Aye aye paulendo tulinkwaula tulinkwaula kkkkkkk mfundo
@WilliamBandaWili
@WilliamBandaWili 24 күн бұрын
Mmmmm izo ndi ng'ona zikuruzikuru zikudyani
@alboxenzambabanda7230
@alboxenzambabanda7230 22 күн бұрын
Time to see chiterera
@ashikalam8616
@ashikalam8616 24 күн бұрын
😮 mbuzi za wanthu zonsezi
@MusaKazembe-b1d
@MusaKazembe-b1d 20 күн бұрын
They are not even ashamed 😮
@Extratremendouszeus
@Extratremendouszeus 23 күн бұрын
Dziko linaola...nduna yosapesa😅😅😅😅😅😅
@IssacMateyo
@IssacMateyo 24 күн бұрын
Amuna mutu wake ometa ngati chiboliwo Muthu osokonezayo zazi
@hopembendela
@hopembendela 23 күн бұрын
Kkkkkkkkkk manganya mukunva koma ati ndiwe mwana osapola panchombotu udziona
@GraceZumazuma
@GraceZumazuma 23 күн бұрын
Chikangawa party, okupha Inu muganiza asakudziwa ndani
@kinggasperagain
@kinggasperagain 23 күн бұрын
Kweni Malawi inasoka ivinthe kuwina waka nbwe chikurya waka ndalama
@PaulMwaona-kh1fj
@PaulMwaona-kh1fj 24 күн бұрын
Ubwino wake achinyamata alipo ambili kunjaku,apapa pachulukana makolo otamba
@WhiteRichard-cw2fo
@WhiteRichard-cw2fo 24 күн бұрын
Zikhale Ng'oma muti chani apaa tiyeni uko 😂😂😂
@user-oq5rg5mz7q
@user-oq5rg5mz7q 24 күн бұрын
Kusawa zoveselatu nanuso, agalu eni eni
@KhondanKhondan
@KhondanKhondan 24 күн бұрын
Aaaaaa chisili chamuthu zikhl
@Sammy-vb1ed
@Sammy-vb1ed 23 күн бұрын
Azikhaleo kwaona nkhopeyo ngati muru wamanyi afisi 😂😂😂😂😂😂.
@GanizaniKamvazaana
@GanizaniKamvazaana 20 күн бұрын
Aaaa dzitsiru dza athu kunamizana kukhwapa kwanu nonse
@user-fi7ko7bl6f
@user-fi7ko7bl6f 24 күн бұрын
Mukuzinamiza agalu Inu za kumachende, azimai nonse Nyini zanu zamanu,mugawane nonse phwala limodzi limodzi agalu okupha
@user-yp5cj2xb9y
@user-yp5cj2xb9y 24 күн бұрын
😂😂😂😂 koma 😂😂
@SphiweMalata
@SphiweMalata 23 күн бұрын
😂😂😂eeeh koma tikuyenda otopa kale
@PreciousBandah-l2r
@PreciousBandah-l2r 19 күн бұрын
Makape inu
@user-nu3zg6pr1l
@user-nu3zg6pr1l 23 күн бұрын
Koma please siku Lina Mulungu wanga nanu mudzayike comment please
@HopeMakoka
@HopeMakoka 24 күн бұрын
Akabwerstsa ndalamazo landirani guys Koma zodzalamuliranso awa mmmmmm Kumwamba kudzatsika pansi
@user-hl3st3cc4v
@user-hl3st3cc4v 24 күн бұрын
Kodi khope zimenezo zikuyakhula apazi pamodzi ndi zikhale ng,oma zamasana kapena zautsiku mmmmm anthu andalama olo kuwezuka
@user-hm9nc7lz6e
@user-hm9nc7lz6e 24 күн бұрын
Ndi zausiku mumuone or zikhameyo khope yace ngati chidzukwa
@innocentmakande5535
@innocentmakande5535 24 күн бұрын
Palibe popangira vn Kodi,? Ndimafuna nditukwana live
@user-mq2or1lz8h
@user-mq2or1lz8h 23 күн бұрын
Fundo yogwira mtima njakuti kuti ukhale mtsogoleli pakufunika ukhale nduna ,kupanda izizi ndiyekuti palibe chanzeru so funso nkumati? Tate wanu kuti akhale mtsogoleli anali ndani???😅😅😅😅
@JuniorHala-vf9ov
@JuniorHala-vf9ov 23 күн бұрын
Viskulu vinu kwacha ninkhuni mpakana kupemphela pamusonkhano apo naumo wanthu wakutambulila namwe kuzomelezganga kwacha chitima chikukolana kweni in fact Mose imwe mukukondwa na mcp Mavi yinu
@FrancisNyayi
@FrancisNyayi 23 күн бұрын
My pipo tiyenda bwanji 😢 koma able
@BashiruIbrahima-h6z
@BashiruIbrahima-h6z 24 күн бұрын
Kodi awa udindo wawo uja akuwuona kuchepa?? I'm feel sorry kwa manganya
@henryphiri6100
@henryphiri6100 24 күн бұрын
Manganya ndi mbuzi.amuthanso ngati saulos.nzeru za ma Rwanda amenewa nzoipa
@ChilangoNdalama
@ChilangoNdalama 23 күн бұрын
Suiona vote yanga Chaka chamawa ndangokudyera aise
@AleksaWilliams-qc6cn
@AleksaWilliams-qc6cn 23 күн бұрын
Adyeren vote ndimumtima bas
@StanleyChirwa-d6b
@StanleyChirwa-d6b 24 күн бұрын
😂😂😂 koma ndaseka kwacha kapena kwada
@BeliLikhola
@BeliLikhola 18 күн бұрын
muuzeni chilungamo ameneyo, chigawenga ameneyo
@user-tw2zf7bj3e
@user-tw2zf7bj3e 23 күн бұрын
Manganya waziwonera wekha kuti iweyo komanso utm sakufunani uziganizile
@user-mq2or1lz8h
@user-mq2or1lz8h 23 күн бұрын
😢😢😢😢oooh he has confirmed that this is serious business 😢😢😢rip SKS
@paulpaseli6310
@paulpaseli6310 24 күн бұрын
Kuika jingo apa mungaluphe akt ai chifukwa njala 😂😂😂
@PartsonMdeza
@PartsonMdeza 22 күн бұрын
Mmm kmaaa 🇲🇼🇲🇼🇲🇼
@CannyMpehla-d1s
@CannyMpehla-d1s 23 күн бұрын
koma malawi waoladi ng'omaso ikhale vp kkkkkkkk
@user-le9su3mt7r
@user-le9su3mt7r 23 күн бұрын
Chikangawa party mbuzi hiziiiii
@amosnyongo6565
@amosnyongo6565 23 күн бұрын
Pemphero lanu silingafike kumwamba afiti inu
@clintonhodda9830
@clintonhodda9830 24 күн бұрын
Kkkkk boma simuliona 2025
@Spaw-BTheGogoBoy
@Spaw-BTheGogoBoy 24 күн бұрын
Zikuchita kuonekeratu poyera kut izi ndi manyaka masewera enieni anthu akulu zimimba nzeru zimapita kutiko kod
@LawrenceNoson
@LawrenceNoson 24 күн бұрын
Masewela chani😅😅😅
@CatherineDesire
@CatherineDesire 24 күн бұрын
Bolansoni papa kwacha wakeyo or najere or Uja mbusa uja wa 6 milion wa 😇 uja 🤣🤣🤣🤣sidzinakukhareni simdzakharapo kamuzu mbuzi inu
@FrancisNyayi
@FrancisNyayi 23 күн бұрын
Mayo mayo chitumbuka sitikunva yankhurani chichewa
@ChimwemweJuwao
@ChimwemweJuwao 18 күн бұрын
Haha koma ndiye mukungooneka Mano okhatu kuli kuda Kwa athu kumeneko ndye kwati mukufuna u vice Muthu ukafuna kufa umankhotha makutu kaye
@IshumaliMakajunior
@IshumaliMakajunior 23 күн бұрын
Ndipo lnu mukanadziwa mene tikuvera
@InnocentnMbale-zq8pk
@InnocentnMbale-zq8pk 24 күн бұрын
Chikangawa forest
@rexphiri7242
@rexphiri7242 24 күн бұрын
Makape okha okha 😢
@jamesgama5489
@jamesgama5489 23 күн бұрын
Kwachaaa! Wachani mulibe manyazi eti!!.
@user-wx1jt5fd2j
@user-wx1jt5fd2j 23 күн бұрын
Mukamawanamiza anthuwo mumayesa kuti ndi Ana iwowo maso alibe samaganiza ndi alendo mumalawi muno amalawi anasukusula akakupasani mphatso landilani bvoti ili mumtima
@MisheckAselo
@MisheckAselo 23 күн бұрын
Ndimamva chisoni ndi anthu apanda nzeru ndikumanamiza anthu, mwaba zakwana azikhale ng'oma 😮
@BrightNyoni-yd4ip
@BrightNyoni-yd4ip 22 күн бұрын
Gulu iwe usamaseweletsa dzina la yesu nkhumba iwe
@AchinaKellz
@AchinaKellz 22 күн бұрын
Koma achina joza 😂😂
@ANDREWMATITI
@ANDREWMATITI 24 күн бұрын
Angodyelatu ndalama ameneyo nthawi yamuthela
@rabisonpias5131
@rabisonpias5131 24 күн бұрын
“Akuti kumabwera ndalama “ ndalama za misonkho yanu zomwe zija ndi zimenezo. M’malao momagura mankhwala mzipatalaa , akungotafuna ndi Ma families awo
@MarriamBakalie
@MarriamBakalie 24 күн бұрын
Manganya beware upita ngati chilima those r the same people who killed chilima with the same position they r nt happy with u take care
@mchotseniliwonde4182
@mchotseniliwonde4182 21 күн бұрын
Nyama zillkulu zikulu 😂
@ChrissySalimu
@ChrissySalimu 23 күн бұрын
Wooooooooooooooooooooo
@PatreckHija
@PatreckHija 24 күн бұрын
Iwe buzi kwabasi angakuvotele ndani iwe 😂😂😂😂
@alfrededwinmadziataika5869
@alfrededwinmadziataika5869 23 күн бұрын
Sapesa Adana ndimadzi..😮😮😮😮😮
@zondanitzulumusicfly.5202
@zondanitzulumusicfly.5202 24 күн бұрын
Adziwa kuti babiloni is falling.
@KennedyKanyama-ce8lb
@KennedyKanyama-ce8lb 24 күн бұрын
Mukutaya nthawi yanu dziko mwalitora eti kkkkkkkkkk
@BlessingsNyirenda-ru7ss
@BlessingsNyirenda-ru7ss 24 күн бұрын
Anthu awiri zaziii
@Felista-m4q
@Felista-m4q 23 күн бұрын
Simuyiwonanso vot yamalawi😊
@Zamwano
@Zamwano 24 күн бұрын
Ma suit ake amenewo chingawine ichoo 😅
@alexgweje8610
@alexgweje8610 23 күн бұрын
Mulibe manyanzi anthu okupha inu 😢
@MaxwellMulula-hj3rd
@MaxwellMulula-hj3rd 23 күн бұрын
😂😂🤣onse kuseka maso kupatula camera mn😅
@CharlesMongola-jw7sk
@CharlesMongola-jw7sk 22 күн бұрын
Pepani mfundo zanu zopusazo musaphenso Manganya,afiti inu
@LekkttarKhembo-or1tx
@LekkttarKhembo-or1tx 20 күн бұрын
Zitsiru za Malawi zikhale chakwera nonse ndinu osadura ndipo mumanukha kabudula mwanumo mukutinyasa tu
@lame8
@lame8 24 күн бұрын
Alandila ma 20 pin zikuchita kuonesa. Kuwatengela anthu ku Hotel kobisika angolowobela manja chifukwa cha ndalama😢
@TeciaKumpitah
@TeciaKumpitah 24 күн бұрын
Mnsonkhano osakapangira pa ground bwanji mukuopa chani? Afiti mukacita kuda ngt thako, majekete onyasawo mbuziiiii
@pacharokoloviko1694
@pacharokoloviko1694 21 күн бұрын
Mayankhulidwe ake amenewa anthu aphanako uku
@user-mq2or1lz8h
@user-mq2or1lz8h 23 күн бұрын
😢😢😢😢 mpakana kumutchula mulungu nyasi ngati?😢😢😢😢😢😢
@EviChio
@EviChio 24 күн бұрын
Mungodzinyenga ndichala bas
Викторина от МАМЫ 🆘 | WICSUR #shorts
00:58
Бискас
Рет қаралды 4,9 МЛН
I'm Excited To see If Kelly Can Meet This Challenge!
00:16
Mini Katana
Рет қаралды 28 МЛН
小宇宙竟然尿裤子!#小丑#家庭#搞笑
00:26
家庭搞笑日记
Рет қаралды 13 МЛН
لااا! هذه البرتقالة مزعجة جدًا #قصير
00:15
One More Arabic
Рет қаралды 8 МЛН
DR MICHAEL USI ZOMWE APEZA KU ROAD TRAFFIC🔥🔥🔥
16:50
OYIMBA A KU MALAWI AKUPEZA NDALAMA ZINGATI PA YOUTUBE? - TILI NDI TOP 10
14:10
kumalawi kuno ndani wandale angamake??
1:01:32
Malawian Cameras
Рет қаралды 94 М.
PRAYERS (with cut 5 min intro)
1:10:21
Temi Awolola
Рет қаралды 460
MWAMBO OYATSA MA KENDULO KU CHILIMBA.🙌🙌🔥🔥🔥
19:58
HOT CURRENT YA LERO PA 4 August 2024 🤔🤔🤔🙌🙌
38:50
Викторина от МАМЫ 🆘 | WICSUR #shorts
00:58
Бискас
Рет қаралды 4,9 МЛН