I like you guys but to have my comment on what you are saying. However all the mess we face today is our own making based on the choice that we made as citizens. It is not even fair to blame DPP as weaker opposition because by DPP opposing this government, it also means that DPP is opposing the choice that Malawians made through the votes. If Malawi has ever had decent party it is DPP because it gives respect to the wishes of Malawians. MCP is politics and Malawians chose politics and DPP is development and it's up to Malawians to choose development based on comparison between the two.
@BeatriceProfessor2 ай бұрын
Fantastic guys inuyo ndie ndi one respect 💪💪💪💪💪💪💪💪💪💪💪💪💪💪💪💪❤❤❤❤
@RonnMtafya2 ай бұрын
Continue being open.Musafoooke musagonje a Malawi.A new Malawi with new mindset needed.
@RonnMtafya2 ай бұрын
You guys mukunena zoona..Koma adzakutengere ku Chikangawa .Long live so that you continue civic educating us.
@wineskhaneni86692 ай бұрын
U guys are great, u can really guide
@SoldierWilison2 ай бұрын
Lelo ndi pamene mwalangula muopa mulungu please continue don't change
@paulpaseli63102 ай бұрын
Times mwezi umenewu mwayambapo ncito wabho love u
@Guttagaard2 ай бұрын
Wonder Msiska ndevu za mwanyi ali hard kwambili
@thulanimpphiri68732 ай бұрын
2025 kumalawi ngati tikufuna president wazeru achoke mu anthu awa 1 wonder musisya ndevu zamwayi 2 jona 3 Brian banda 4 chunga 6 bon kalindo 7 tanyiwa 8 bakili muluzi TV 9 kaliat 10 njawala Anthu amenewa mumozi atha kuyendesa bwino Malawi kusiyana ndi makape akulimbirana ku mcp.
@eliffagondewe82142 ай бұрын
🔥🔥🔥🔥
@JohnfosterNkusengwa2 ай бұрын
❤❤❤Guys all the way from cape Town PA boma PA Athlone zedidi l salute you guys and my vote and my ldea let's build Malawi and let's be not afraid 😊 utm more fire
@DominicNkosi-iq9fh2 ай бұрын
You guys you best tutors, only that people trust in regionalism.
@RonnMtafya2 ай бұрын
We need More fire ttv.
@DENSONZULU2 ай бұрын
Chaka chamawa tivote mwanzeru chonde.... Rest in peace SKC 💔🔥
@AbrahamTembo-z5k2 ай бұрын
MEC, pa nthawipo, 6AM to 4PM ndikuwona ngati nthawi yachepa. Bwanji itakhala 6AM to 6PM?
@user-ux3ed3ni1p2 ай бұрын
For me the lack of poor governance and the inability to deal with blatant corruption. 4% of development can not buy our vote.
@GiftCMlangeni2 ай бұрын
You people we love you and malawians are proud of you. Congratulations for all the times boad for this programme. Generation shall talk about this radio station and TV.
@RonnMtafya2 ай бұрын
Let us be patriotic and totally love our nation first.
@JaneBanda-ht4ve2 ай бұрын
Mafuta ayamba kubwera pa njanje after 21 years, ma mega farm ndi awo, zitukuko zochuluka mu zaka 4, ine vote yanga ndi MCP - Chakwera 🇲🇼✅🔥
@RedsonMasamba2 ай бұрын
hahahaa its your opinion
@SimenyeSimkondachirwa2 ай бұрын
Vote for Dpp thing will become better trust
@Cuddy-ol5wq2 ай бұрын
That's talking...but is it possible our mp to have two terms as maximum for serving the constituents rather than for life?
@paulmgombebanda-mr19sate2 ай бұрын
You have a point aise
@ziyamporoma3772 ай бұрын
Tisanamizanepo apa Chakwera yemweyu is a better option pa anthu amene alipowa #boma ndilomweli
@Creslevison-vj2sl2 ай бұрын
Kupusa
@famousphiri9442 ай бұрын
Mmm😢
@MakawaBenjamin2 ай бұрын
Big up guys mumatiimilira ❤❤❤❤
@AubreyWilson-j8w2 ай бұрын
Kkkk nde fisiyo ndindan😂😂😂
@JanuaryGwere2 ай бұрын
Yovotera chaunzika ndizopoyila akupangila aku Lilongwe okha kuno kulibe
@DENSONZULU2 ай бұрын
ACB tizangoithetsaso ntchito yake sidziwika
@RonnMtafya2 ай бұрын
Money Must not buy us.Ndalama zinapha Yesu.Akupereka ndalama ngoopsya ngakhale chipani lets avoid them.
@EvansNkumba-q7t2 ай бұрын
Me zikhale m'goma I want to imform the general public that we are closed this tv station tomorrow 😂😂😂
@eliffagondewe82142 ай бұрын
😂😂😂😂
@eliffagondewe82142 ай бұрын
Big up wonder and atsukuluzi mwayankhula mosaopa munthu chilungamo akumva amve anthu akuba mowononga zedi eesh....
Ma brother Aku t tv nthawi zina mumandilowa mmaganizotu mosakunyengelelani inuyo mumang`alula or thelele limandikomela mbamba
@BrightZionga2 ай бұрын
😂😂😂😂😂 wonder kodi tiana tumakuopsyzani love you guys ❤
@JanuaryGwere2 ай бұрын
From 2020 kufika lelo njala sikutha president wachikondi angapase bwanji mwanawake ma contraction aboma zinthu zingayende bwanji kwathu kuno chakwera sanafikeko kuno
@RonnMtafya2 ай бұрын
Anyanatanu muzigona kutali ndi ng'ona ngakhalenso mikango kuti mupitilize kutigawire
@DENSONZULU2 ай бұрын
1000% increase bwana 💔💔
@wisdomchilanga7232 ай бұрын
Guys apa mwang'alura😂😂😂❤❤
@SiphiweTonnyChidumayo2 ай бұрын
Kung'aluratu😂😂😂😂😅👐Kaliati,Njawala atimile u president we should see them.......Let's try out something new mbuzi zinazi ayi
@DENSONZULU2 ай бұрын
Zodiak ndinasiya kumvera ndimanvera times ndithu
@RobertLuka-wy9cl2 ай бұрын
Amcp inu olo inuyo zomwe zimachitika muulamulilo wa peter muthalika mungayelekeze ndi manyani tili nawowa a mcp wa inu muzikhala ndi manyazi dpp ilowa mboma mufune musafune
@EfeloYovita2 ай бұрын
mafuta akupezekawo akugulitsidwa ndalama zingati zopusa basi dpp imagulitsa 700kwacha za mcp zakozo kagwele 😅
@KennedyPhiri-c7g2 ай бұрын
Aford basi enawa atarephera kale
@MonicaSembo2 ай бұрын
Massive
@blessingsmandiwa48402 ай бұрын
Ati tchifiiiiii mubweraso why eeee anyamata inu😂😂😂😂
@AubreyWilson-j8w2 ай бұрын
Koma tikaika pa scale between chax and pix Bola pix😂😂😂
@JanuaryGwere2 ай бұрын
Moses anapha witika koma uyo akutukwana anthu dziko muno
I believe Usi is Malawi first, I have noticed Malawians are so stuck up to party politics that they can never appreciate anything, every day is politics day in Malawi, no political party will help you because they are from your region, as much as I hate chakwera for the way he was ready to betray chilima before he died, I don’t think there’s anyone better to run Malawi at this moment, unless it’s Bushiri the fake pastor but brilliant hustler.
@Andy202472 ай бұрын
Bravoooo
@StanleyChabwera2 ай бұрын
Boma ili kuganiza kukuvuta....
@OwenNyangu-nv1yt2 ай бұрын
Chakela ubwino ukuchuluka kuposa enawa
@JanuaryGwere2 ай бұрын
Palibe boma lalamula bwino
@vukanifracksonchinkonde73242 ай бұрын
Sindingaiwale ma black out a mbweeeeeee
@ShadreckMatenje2 ай бұрын
Guys apa nde tomati zisankho zayandikila kuswakuswa osaopa
@chiwaulaashraf46962 ай бұрын
Eeeeeeee
@Isaiahbotoman2 ай бұрын
Eeeeeee wonder 😂
@DonKapeniZagwah2 ай бұрын
Koma ndy kuswa kuswa di
@SababaHotel2 ай бұрын
chakwera sakufunika kukhalaso president
@ShaihSalaam2 ай бұрын
Boma Lili manja mwa Agalu
@StevieChilinde2 ай бұрын
Makape Inu;Poyamba mumayankhula Zanzelu koma pano mbola zenizeni dollar sizinthu zinakusinthani makape Inu.
@StevieChilinde2 ай бұрын
Kodi nkhani ya chikangawa ilipati?Naga Mr.B.Banda alikuti sizikubebaaaa olo pangono.
@UseniMailosi2 ай бұрын
Agalu wojoyina sipaniwa site chifukwa timavotela wina amalamulila wina
@JuvenileDebwe-bv8ow2 ай бұрын
zimenezo ndiye vuto lomwe tilinalo ma politicians athu ngooipa kwambiri amafuna tikhale owaonbera m'manja ndi 2000 mk
@ImediJames-b4u2 ай бұрын
Thanks you guys
@John-m6b4m2 ай бұрын
Lero ndye kwavuta osati masewera
@JamesFundi-zn7nk2 ай бұрын
Okay my friend
@Chisomo-h3c2 ай бұрын
Mwalankhulatu lelo takunyadilan
@MisheckAselo2 ай бұрын
Anthu atopa akung'alura🎉🎉🎉
@BornfaceMakamu2 ай бұрын
Thaw Zina mzachezepo za ku chikangawa
@SababaHotel2 ай бұрын
Kodi brain banda alikuti abale
@FelixGambiza-fp7tn2 ай бұрын
What's the point of this program bola izangotha
@SitiyaBatwell2 ай бұрын
Awa akungodzikilakola nawo mpira a aaa osabisapo apa
@MaggieBanda-ft5tu2 ай бұрын
Mukubowa times,mwakwela MCP inu
@VioletMbale2 ай бұрын
Nanuso pamene akwela mcp ndi Pati? Mziyamika these people alibe side
@francis12fombe542 ай бұрын
Shunga alikuti ma bwana
@LuciaOsman2 ай бұрын
Inde inu
@ChristMaunde2 ай бұрын
Yache madolo
@SheenahMwalabu-iz3pr2 ай бұрын
Sindimaliza Nanu mukuoneka kuti mukubowa zokamba zanu bola Chunga ndi Brian Banda apa inu phokoso too much aaa