Panopa akugwira ntchito za Vice president ndimwana wa president
@kondwanimunthali740120 күн бұрын
Osati kuthetsa u VP koma kukhale Deputy president nayenso azikhala ndi ntchito zake osati delegated powers
@user-is5dl7np9g20 күн бұрын
I agree 💯 with this issue very much, VP amangowononga Chuma cha boma for nothing, a very good example is saulos chilima from time of DPP kufikila lero sindinaonepo chomwe anachita chopindulira dziko
@user-qm1qb2jp4s16 күн бұрын
Mpando umenewo wa u vice president ulibe phindu
@user-sh6gi5uq3l19 күн бұрын
I like this chipani chomwe chapeza mipando yambiri pambuyo pa owina kumeneko kuzichola vice president ndiye malamulonso asithe kuti uyu azikhala ndi macondition omuyenereza kusakhidwa komanso kuchosedwa like k in south Africa chipani cha anc
@AmusedDimSum-hd5yp20 күн бұрын
wise spoken from Mr chingaipe big up Big man
@user-hq6dq7zr1e18 күн бұрын
Am very agree of that conservation, ulemu wanu zipitilire malawi akhale ndi mphavu,nde kuti president azikhalaso ndi matha ngati pazikhala ma mistake olamula dziko
@saved141620 күн бұрын
I feel this can only work if we agree to review our constitution. The president has all the powers which makes it easy for him or her to abuse the vice president. The only problem is that our political scientists come out when they want to deal with an individual and not to correct things. I hope this is coming out because of milandu ikuthesedwa ija
@EmercianahKasiku-en6hl18 күн бұрын
Yosagwira yoti president azichoka komwe mul ma mp ambirimbiri ndizosagwira chifukwa Malawi umakhala ndi mipikisano itatu pa masankho President kasala komaso mp nde vice president amasakhidwa pamodzi ndi president ngati udikilira kut atadwala kapena kumwalira dziko lisalowe chisawawa likhalebe ndi commander in chief koma bola zoti azikhala Deputy president not just president chifukwa vice amapatsidwa ntchito pomwe Deputy president amakhala kale ndi ntchito zoti agwire
@user-ux3ed3ni1p20 күн бұрын
Very necessary discussion. We need to change ASAP.
@chipiliromalola638020 күн бұрын
Good decisions ❤❤❤❤
@user-ez8zs1iq9k19 күн бұрын
yes u vice president uthesedwe ndipo mumalo mwake tizikhala ndi prime Minister ndikuona kuti zitha kumayenda bwino
@CharlesPhiri-ds1rk2 күн бұрын
In deep corgitate,, fundo ili bwino kwambir
@user-mj2te7vl6p20 күн бұрын
Koma president azikocha komwe kuli ma MP chipani chimenecho kuchoke president basi
We also say that Head of state and government, my opinion is that the president must be the head of state and vice president be of government. What also Yuba James has said is very sensible and that should be the way to adopt
@douglaskamanga767920 күн бұрын
Anthu amafa nde wina aka mwalira wachiwili wake azitenga position.Koma ngati zipani ndiza family,u vice usiyidwedi.
Osati Malawi wanunkha ichi nchichewa cholakwikaaa ......ngati Pali Malo ofuna kuti akonzedwetso mmalawi muno ufulu Otero ulipo.....osamakhazikika pa Malo amozi moxi ngati zinthu sizikuyenda bwino......sinthani zinthu.....
@LilianKachala-yz2xf20 күн бұрын
Vice president amayamba kukulira mtima president that's why Vice president Aliyense amafuna naye akhalenso president.Ndichifukwa Chake Vice president Aliyense amayambitsa Chipani Chake Cholinga nayenso akhale president.Ndiyeno office ya U vice president.Komanso president amalephela kumuchotsa Vice wake
@MwizaChavula20 күн бұрын
Ndiye what if president aka mwalira hu will take the duties of president?
@user-yk9lx7xd1i20 күн бұрын
Ndipo mwakambilana nthawi yabwino masankho ali patali chaka chamawa no vice president we will only vote the president
@user-xq6vp1tx7z15 күн бұрын
Ndzowona vs asamankhalepho kumeneko diyeku4
@JohnFrank-cg1yh20 күн бұрын
Zoona vice president akufunika azisakhidwa ngat nduna,
@AndersonInnocent20 күн бұрын
Vice president kungotafuna misonkho yathu ku Malawi 🇲🇼 kukhale president yekha basi komanso Chakwela atule pansi udindo
@MarthaPhiri-nr7yb4 күн бұрын
Kapena tinene kuti ifeyo tikhale oyamba kupanga kuti president azichoka chipani chowina,vice from opposition koma vice president akhale ndi duties derived from constitution 😊😊
@tawongamhango733518 күн бұрын
We don't need vice president position on ballot paper. I agree
Izi zopanda nzeru izi, basi meeting ndi meeting kukakambirana zimenezi, bwanj osangoyambisa FEDERALISM?
@user-on3yu7wt9o19 күн бұрын
Inenso i think federal system ija can help
@MarkoMkundiza19 күн бұрын
Panopa ncto ya vice president sikuoneka coz akugwila ndimwana wake
@Johnybegood26020 күн бұрын
Tsopano a political science nu nthawi yoseyi munali kuti we needed thinkers like you iyi yokha iduse
@KnowxySainet20 күн бұрын
Fodya awa azindikila lit vuto amafuna chilima basi so zakanika
@thomluciouss736020 күн бұрын
This is a serious issue what we must do we need to put a right disition so that the president must no have a light disition to chance the vice president becoz its us we choose and vote for them
@EagerChicken-qj6xu20 күн бұрын
Zimenezo sizingapangise kuti mzikolino anthu azingosankhana a chipani chimodzi modzi?
@cassimyusuf668320 күн бұрын
Udindo umenewu umangotha ndalama za amalawi, atangochotsadi chifukwa phindu lake palibe
@MwizaChavula20 күн бұрын
Ndiye chisasawa mu govt
@danielmsowoya910720 күн бұрын
Zaziiii, lero nde mwaona kut office ya Vice President imangoononga ndalama? Pali ma areas ambiri amene ndalama zimangoonongeka like AIP, bwanj tichotse Kaye zimenezi. There a Political smell behind this proposal.
Fundo akunena Ayuba James,yingagwire muchipani ngati sicha family koma cha Public.Inu mwini chipani mungamuitane kumufunsa mafunso?Waku chalenjani APM kulibe zopita ku conversation aima ndiyeyo.Akususa ndani?.Mukuona bwa?
@user-wx1jt5fd2j20 күн бұрын
And vice president amakhonza kukhala ndi maso mpenya kuposa president chifukwa nthawi zambiri vice amakhonza kukhala munthu amene akhonza kuthandiza
@thulanimpphiri687320 күн бұрын
Ndimaganizo abwino kuti vice asakhalepo and tizikhala ndi ma prime minister nduna zizichepa. Komaso vice President ngati akhalapo asakhale wachipani china
Ndipo ndizoona mpando wa Vice President Uthe chifukwa palibe kufunikira kwina kulikose President wolamurayo ndiamene ammakula mphamvu kwambiri choncho Vice kwake mkumangoyembekezera
@user-pv9uk6sc3w20 күн бұрын
Fundo apa pakungofunika kuchotsa office ya vice president, office yimenei yikungowononga ndalama.
@IbrahimWezely-qd4vj20 күн бұрын
Apa ndiye mbambande
@user-yk9lx7xd1i20 күн бұрын
I support Mr Auba kumeneko ndiyekunena
@HaroonSaidi-jv3ek19 күн бұрын
Inenso zomwe wanena mkotakotayo ndagwirizana nazo
@MarthaPhiri-nr7yb4 күн бұрын
Kapena tinene kuti ifeyo tikhale oyamba kupanga kuti president azichoka chipani chowina,vice from opposition koma vice president akhale ndi duties derived from constitution
@user-cl5pi4nb1e19 күн бұрын
Ndizoonadi ithe palibe chanzeru chomwe imapanga ikumangotha ndalama zathu osauka muno mudziko libe ntchito imangoononga ndalama basi ma salary, allowances, utilities, fuels, workers, state rentals and etc
@user-pw2dq1yw4b20 күн бұрын
Ndipo izii zichitike mwansanga tipange system yakuno Ku South Africa nsanga guys komanso parliament ndi imene izikhala ndi mphanvu yapadela.
@user-un6qv6sj3h20 күн бұрын
Please go on
@danielmsowoya910720 күн бұрын
Ndale chabe izi
@lucymuhala217620 күн бұрын
The truth is all deputies whether ministry there useless position just worsting taxes pairs money
@user-yk9lx7xd1i20 күн бұрын
Tiyeni tibwerere kuzokhoza zomwe zinakhala lamulo laosakhala ndi vice president mu 1965 no need for malawians to have a vice president
@user-le9su3mt7r12 күн бұрын
Zazii vec president akufunika ziko lililose
@alphatosman313720 күн бұрын
ine ndimaona ngati ntchito yake ndikudikira akamwalira winayo
@user-ub1mw7ce5p20 күн бұрын
Good decision
@user-qi8xe7qh1e20 күн бұрын
Pasakhaleso vp angotiwonongera zithu
@robertchitsulo800620 күн бұрын
Agree with you
@FrynessMoyo-to2du20 күн бұрын
Chakwera ndi mbuzi
@christopherchikankhen20 күн бұрын
Nkhaniyo Ndiyoona Ndipo Ndaikonda.
@WysonMpatama-cv1mc19 күн бұрын
Chilimayo amuchotse akuvutitsa amalawi
@user-jk8sh7fh2d19 күн бұрын
Ngati nkotheka achosedi , vice amangodya ndalama zaulele . Kunena zoona anthu awa samagwilizana kamba ka nsanje uwelesiki uwelesiki eeh zonse ndizipanga ndekha ndalama zizikhala zanga ndie ndi zovuta so kwa ine 100% ndikugwilizana nawo makosana amenewa ngati zingatheke kutelo . Olo mufufuze ma MP's ndi othandizana nawo aja mmizimu si ndikukhulupilira kuti amagwilizana kwenikweni why nkhani zake ndi zomwezi tikunena apazi , and osatila kwa ma MP's samafunikaso ai. Bwina nkhani yabwino ndi imenei yoti yowachepesela malo amene amalamulira why kupewa kusamvana .
@user-gq1lj6nc8h20 күн бұрын
Koma iziz aaa ok
@user-vq9if2ep5q20 күн бұрын
Koma zilipo ku Malawi
@fanuelbinde19 күн бұрын
Vice presedent asakhaleponso
@EagerChicken-qj6xu20 күн бұрын
africa Ndi dziko liti mu a frica muno limene lilibe vicepresident Ndi dziko liti mu a frika muno kulibe vice president?
@douglaskamanga767920 күн бұрын
Nkhani yayi kuli ndiyakuti, zipani zambili mu Malawi muno ndiza banja pa chizungu timati family entities. Ndiye mwini wa chipani sangalole kusiila chipani vice president coz, ndekuti chuma chachoka mu banja LA mwini chipani. So nkhani iyi siyofunaso Political Scientist.Office ya vice president ndiyabwino ndithu koma zilinga zizakhala zotani?
@usumanidaudi20 күн бұрын
Osachosa chakwera aziba kwambiri
@user-xg2ks9nw5q20 күн бұрын
Mukunama🎉 ku south Africa amasanga vice president amasanga ku corvetion ya chipani
@WakudaSawerenga-xu9xc20 күн бұрын
Exactly
@Chisomo-dh2gq20 күн бұрын
Which South Africa 🇿🇦..?
@HaroonSaidi-jv3ek19 күн бұрын
Kodi vice president ndi deputy president kodi Tuttle ya mphamvu ndi iti
Good idea office of vice President is just wasting pples taxpayers money Koma nanga president yo passed on?
@JulianaNyerere20 күн бұрын
Km ziliko ku bomako
@paulmakaula493720 күн бұрын
Guys nanuso you are piling too much to the already power intoxicated president! Create mmalo mwa "VICE PRESIDENT" to "PRIME MINISTER" like ku ZIM...mpatseni ntchito zake PRIME MINISTER" plus delegation from president pomwe zangakwanitse...koma Prime Minister go in all ministries to ensure ntchito ikugwirika...MULI BUSY PROTECTING PRESIDENCY ....Don't forget ma president ambiri amakhala clueless then with Prime Minister zitha kumayenda