AKUFUNA KUCHOTSA MPANDO WAU VICE PRESIDENT__ MALAWI WANUKHA🙌🙌

  Рет қаралды 32,580

HOT 265

HOT 265

22 күн бұрын

Пікірлер: 87
@homeremedys3748
@homeremedys3748 20 күн бұрын
Panopa akugwira ntchito za Vice president ndimwana wa president
@kondwanimunthali7401
@kondwanimunthali7401 20 күн бұрын
Osati kuthetsa u VP koma kukhale Deputy president nayenso azikhala ndi ntchito zake osati delegated powers
@user-is5dl7np9g
@user-is5dl7np9g 20 күн бұрын
I agree 💯 with this issue very much, VP amangowononga Chuma cha boma for nothing, a very good example is saulos chilima from time of DPP kufikila lero sindinaonepo chomwe anachita chopindulira dziko
@user-qm1qb2jp4s
@user-qm1qb2jp4s 16 күн бұрын
Mpando umenewo wa u vice president ulibe phindu
@user-sh6gi5uq3l
@user-sh6gi5uq3l 19 күн бұрын
I like this chipani chomwe chapeza mipando yambiri pambuyo pa owina kumeneko kuzichola vice president ndiye malamulonso asithe kuti uyu azikhala ndi macondition omuyenereza kusakhidwa komanso kuchosedwa like k in south Africa chipani cha anc
@AmusedDimSum-hd5yp
@AmusedDimSum-hd5yp 20 күн бұрын
wise spoken from Mr chingaipe big up Big man
@user-hq6dq7zr1e
@user-hq6dq7zr1e 18 күн бұрын
Am very agree of that conservation, ulemu wanu zipitilire malawi akhale ndi mphavu,nde kuti president azikhalaso ndi matha ngati pazikhala ma mistake olamula dziko
@saved1416
@saved1416 20 күн бұрын
I feel this can only work if we agree to review our constitution. The president has all the powers which makes it easy for him or her to abuse the vice president. The only problem is that our political scientists come out when they want to deal with an individual and not to correct things. I hope this is coming out because of milandu ikuthesedwa ija
@EmercianahKasiku-en6hl
@EmercianahKasiku-en6hl 18 күн бұрын
Yosagwira yoti president azichoka komwe mul ma mp ambirimbiri ndizosagwira chifukwa Malawi umakhala ndi mipikisano itatu pa masankho President kasala komaso mp nde vice president amasakhidwa pamodzi ndi president ngati udikilira kut atadwala kapena kumwalira dziko lisalowe chisawawa likhalebe ndi commander in chief koma bola zoti azikhala Deputy president not just president chifukwa vice amapatsidwa ntchito pomwe Deputy president amakhala kale ndi ntchito zoti agwire
@user-ux3ed3ni1p
@user-ux3ed3ni1p 20 күн бұрын
Very necessary discussion. We need to change ASAP.
@chipiliromalola6380
@chipiliromalola6380 20 күн бұрын
Good decisions ❤❤❤❤
@user-ez8zs1iq9k
@user-ez8zs1iq9k 19 күн бұрын
yes u vice president uthesedwe ndipo mumalo mwake tizikhala ndi prime Minister ndikuona kuti zitha kumayenda bwino
@CharlesPhiri-ds1rk
@CharlesPhiri-ds1rk 2 күн бұрын
In deep corgitate,, fundo ili bwino kwambir
@user-mj2te7vl6p
@user-mj2te7vl6p 20 күн бұрын
Koma president azikocha komwe kuli ma MP chipani chimenecho kuchoke president basi
@MarthaPhiri-nr7yb
@MarthaPhiri-nr7yb 4 күн бұрын
Tipange referendum za mpando umenewu. Osangopanga zanu mufunse ife aini ake ovota komanso olipila office imeneyi
@stellakaluluma8241
@stellakaluluma8241 18 күн бұрын
We also say that Head of state and government, my opinion is that the president must be the head of state and vice president be of government. What also Yuba James has said is very sensible and that should be the way to adopt
@douglaskamanga7679
@douglaskamanga7679 20 күн бұрын
Anthu amafa nde wina aka mwalira wachiwili wake azitenga position.Koma ngati zipani ndiza family,u vice usiyidwedi.
@HarrisonMwanga-xy4sc
@HarrisonMwanga-xy4sc 20 күн бұрын
Mmmm,inu mukudzidzwa,nangati,kuli anthu andale adyela ndiye,ku Malawi kuno.malawi,mpaka pano kulibe olo kukhala azitsogoleli alutha olo vision, chifukwa onse,ali ndi dyela.
@charleslimbani8590
@charleslimbani8590 17 күн бұрын
Osati Malawi wanunkha ichi nchichewa cholakwikaaa ......ngati Pali Malo ofuna kuti akonzedwetso mmalawi muno ufulu Otero ulipo.....osamakhazikika pa Malo amozi moxi ngati zinthu sizikuyenda bwino......sinthani zinthu.....
@LilianKachala-yz2xf
@LilianKachala-yz2xf 20 күн бұрын
Vice president amayamba kukulira mtima president that's why Vice president Aliyense amafuna naye akhalenso president.Ndichifukwa Chake Vice president Aliyense amayambitsa Chipani Chake Cholinga nayenso akhale president.Ndiyeno office ya U vice president.Komanso president amalephela kumuchotsa Vice wake
@MwizaChavula
@MwizaChavula 20 күн бұрын
Ndiye what if president aka mwalira hu will take the duties of president?
@user-yk9lx7xd1i
@user-yk9lx7xd1i 20 күн бұрын
Ndipo mwakambilana nthawi yabwino masankho ali patali chaka chamawa no vice president we will only vote the president
@user-xq6vp1tx7z
@user-xq6vp1tx7z 15 күн бұрын
Ndzowona vs asamankhalepho kumeneko diyeku4
@JohnFrank-cg1yh
@JohnFrank-cg1yh 20 күн бұрын
Zoona vice president akufunika azisakhidwa ngat nduna,
@AndersonInnocent
@AndersonInnocent 20 күн бұрын
Vice president kungotafuna misonkho yathu ku Malawi 🇲🇼 kukhale president yekha basi komanso Chakwela atule pansi udindo
@MarthaPhiri-nr7yb
@MarthaPhiri-nr7yb 4 күн бұрын
Kapena tinene kuti ifeyo tikhale oyamba kupanga kuti president azichoka chipani chowina,vice from opposition koma vice president akhale ndi duties derived from constitution 😊😊
@tawongamhango7335
@tawongamhango7335 18 күн бұрын
We don't need vice president position on ballot paper. I agree
@MpanjeHardware
@MpanjeHardware 20 күн бұрын
Nkhani imeneyi ndiyofunika kwambili kuno kuziko lamalawi nyumba yapekezidemti iyenela ithesedwe chifukwa ikungotha ndalama
@danielmsowoya9107
@danielmsowoya9107 20 күн бұрын
Izi zopanda nzeru izi, basi meeting ndi meeting kukakambirana zimenezi, bwanj osangoyambisa FEDERALISM?
@user-on3yu7wt9o
@user-on3yu7wt9o 19 күн бұрын
Inenso i think federal system ija can help
@MarkoMkundiza
@MarkoMkundiza 19 күн бұрын
Panopa ncto ya vice president sikuoneka coz akugwila ndimwana wake
@Johnybegood260
@Johnybegood260 20 күн бұрын
Tsopano a political science nu nthawi yoseyi munali kuti we needed thinkers like you iyi yokha iduse
@KnowxySainet
@KnowxySainet 20 күн бұрын
Fodya awa azindikila lit vuto amafuna chilima basi so zakanika
@thomluciouss7360
@thomluciouss7360 20 күн бұрын
This is a serious issue what we must do we need to put a right disition so that the president must no have a light disition to chance the vice president becoz its us we choose and vote for them
@EagerChicken-qj6xu
@EagerChicken-qj6xu 20 күн бұрын
Zimenezo sizingapangise kuti mzikolino anthu azingosankhana a chipani chimodzi modzi?
@cassimyusuf6683
@cassimyusuf6683 20 күн бұрын
Udindo umenewu umangotha ndalama za amalawi, atangochotsadi chifukwa phindu lake palibe
@MwizaChavula
@MwizaChavula 20 күн бұрын
Ndiye chisasawa mu govt
@danielmsowoya9107
@danielmsowoya9107 20 күн бұрын
Zaziiii, lero nde mwaona kut office ya Vice President imangoononga ndalama? Pali ma areas ambiri amene ndalama zimangoonongeka like AIP, bwanj tichotse Kaye zimenezi. There a Political smell behind this proposal.
@user-wx1jt5fd2j
@user-wx1jt5fd2j 20 күн бұрын
Zimangokhala zobvuta kusazichepesa chisanzo MCP kupanda fundo ndikufunikira kumene anthu anakuona kwa achilima chakwera zikanabvuta kukhala aprezident
@douglaskamanga7679
@douglaskamanga7679 20 күн бұрын
Fundo akunena Ayuba James,yingagwire muchipani ngati sicha family koma cha Public.Inu mwini chipani mungamuitane kumufunsa mafunso?Waku chalenjani APM kulibe zopita ku conversation aima ndiyeyo.Akususa ndani?.Mukuona bwa?
@user-wx1jt5fd2j
@user-wx1jt5fd2j 20 күн бұрын
And vice president amakhonza kukhala ndi maso mpenya kuposa president chifukwa nthawi zambiri vice amakhonza kukhala munthu amene akhonza kuthandiza
@thulanimpphiri6873
@thulanimpphiri6873 20 күн бұрын
Ndimaganizo abwino kuti vice asakhalepo and tizikhala ndi ma prime minister nduna zizichepa. Komaso vice President ngati akhalapo asakhale wachipani china
@ChicoBanda-kq7py
@ChicoBanda-kq7py 20 күн бұрын
Good discussion
@eliffagondewe8214
@eliffagondewe8214 20 күн бұрын
Iziii ndizoona ndinthu mwina anthu anga dza siye dyerali
@mphatsosadiki4983
@mphatsosadiki4983 20 күн бұрын
Best way kuzingokhala Prime Minister...
@mathewssimbi3052
@mathewssimbi3052 19 күн бұрын
Ndipo ndizoona mpando wa Vice President Uthe chifukwa palibe kufunikira kwina kulikose President wolamurayo ndiamene ammakula mphamvu kwambiri choncho Vice kwake mkumangoyembekezera
@user-pv9uk6sc3w
@user-pv9uk6sc3w 20 күн бұрын
Fundo apa pakungofunika kuchotsa office ya vice president, office yimenei yikungowononga ndalama.
@IbrahimWezely-qd4vj
@IbrahimWezely-qd4vj 20 күн бұрын
Apa ndiye mbambande
@user-yk9lx7xd1i
@user-yk9lx7xd1i 20 күн бұрын
I support Mr Auba kumeneko ndiyekunena
@HaroonSaidi-jv3ek
@HaroonSaidi-jv3ek 19 күн бұрын
Inenso zomwe wanena mkotakotayo ndagwirizana nazo
@MarthaPhiri-nr7yb
@MarthaPhiri-nr7yb 4 күн бұрын
Kapena tinene kuti ifeyo tikhale oyamba kupanga kuti president azichoka chipani chowina,vice from opposition koma vice president akhale ndi duties derived from constitution
@user-cl5pi4nb1e
@user-cl5pi4nb1e 19 күн бұрын
Ndizoonadi ithe palibe chanzeru chomwe imapanga ikumangotha ndalama zathu osauka muno mudziko libe ntchito imangoononga ndalama basi ma salary, allowances, utilities, fuels, workers, state rentals and etc
@user-pw2dq1yw4b
@user-pw2dq1yw4b 20 күн бұрын
Ndipo izii zichitike mwansanga tipange system yakuno Ku South Africa nsanga guys komanso parliament ndi imene izikhala ndi mphanvu yapadela.
@user-un6qv6sj3h
@user-un6qv6sj3h 20 күн бұрын
Please go on
@danielmsowoya9107
@danielmsowoya9107 20 күн бұрын
Ndale chabe izi
@lucymuhala2176
@lucymuhala2176 20 күн бұрын
The truth is all deputies whether ministry there useless position just worsting taxes pairs money
@user-yk9lx7xd1i
@user-yk9lx7xd1i 20 күн бұрын
Tiyeni tibwerere kuzokhoza zomwe zinakhala lamulo laosakhala ndi vice president mu 1965 no need for malawians to have a vice president
@user-le9su3mt7r
@user-le9su3mt7r 12 күн бұрын
Zazii vec president akufunika ziko lililose
@alphatosman3137
@alphatosman3137 20 күн бұрын
ine ndimaona ngati ntchito yake ndikudikira akamwalira winayo
@user-ub1mw7ce5p
@user-ub1mw7ce5p 20 күн бұрын
Good decision
@user-qi8xe7qh1e
@user-qi8xe7qh1e 20 күн бұрын
Pasakhaleso vp angotiwonongera zithu
@robertchitsulo8006
@robertchitsulo8006 20 күн бұрын
Agree with you
@FrynessMoyo-to2du
@FrynessMoyo-to2du 20 күн бұрын
Chakwera ndi mbuzi
@christopherchikankhen
@christopherchikankhen 20 күн бұрын
Nkhaniyo Ndiyoona Ndipo Ndaikonda.
@WysonMpatama-cv1mc
@WysonMpatama-cv1mc 19 күн бұрын
Chilimayo amuchotse akuvutitsa amalawi
@user-jk8sh7fh2d
@user-jk8sh7fh2d 19 күн бұрын
Ngati nkotheka achosedi , vice amangodya ndalama zaulele . Kunena zoona anthu awa samagwilizana kamba ka nsanje uwelesiki uwelesiki eeh zonse ndizipanga ndekha ndalama zizikhala zanga ndie ndi zovuta so kwa ine 100% ndikugwilizana nawo makosana amenewa ngati zingatheke kutelo . Olo mufufuze ma MP's ndi othandizana nawo aja mmizimu si ndikukhulupilira kuti amagwilizana kwenikweni why nkhani zake ndi zomwezi tikunena apazi , and osatila kwa ma MP's samafunikaso ai. Bwina nkhani yabwino ndi imenei yoti yowachepesela malo amene amalamulira why kupewa kusamvana .
@user-gq1lj6nc8h
@user-gq1lj6nc8h 20 күн бұрын
Koma iziz aaa ok
@user-vq9if2ep5q
@user-vq9if2ep5q 20 күн бұрын
Koma zilipo ku Malawi
@fanuelbinde
@fanuelbinde 19 күн бұрын
Vice presedent asakhaleponso
@EagerChicken-qj6xu
@EagerChicken-qj6xu 20 күн бұрын
africa Ndi dziko liti mu a frica muno limene lilibe vicepresident Ndi dziko liti mu a frika muno kulibe vice president?
@douglaskamanga7679
@douglaskamanga7679 20 күн бұрын
Nkhani yayi kuli ndiyakuti, zipani zambili mu Malawi muno ndiza banja pa chizungu timati family entities. Ndiye mwini wa chipani sangalole kusiila chipani vice president coz, ndekuti chuma chachoka mu banja LA mwini chipani. So nkhani iyi siyofunaso Political Scientist.Office ya vice president ndiyabwino ndithu koma zilinga zizakhala zotani?
@usumanidaudi
@usumanidaudi 20 күн бұрын
Osachosa chakwera aziba kwambiri
@user-xg2ks9nw5q
@user-xg2ks9nw5q 20 күн бұрын
Mukunama🎉 ku south Africa amasanga vice president amasanga ku corvetion ya chipani
@WakudaSawerenga-xu9xc
@WakudaSawerenga-xu9xc 20 күн бұрын
Exactly
@Chisomo-dh2gq
@Chisomo-dh2gq 20 күн бұрын
Which South Africa 🇿🇦..?
@HaroonSaidi-jv3ek
@HaroonSaidi-jv3ek 19 күн бұрын
Kodi vice president ndi deputy president kodi Tuttle ya mphamvu ndi iti
@goliathkujngo3262
@goliathkujngo3262 20 күн бұрын
Komaso ngati vice ali wanzeru ngati mene alili achilima muja ndekuti sangamukonde chifukwa amawona kuti sbwanawo kuposedwa choncho otsatira bwanayo amayamba kumunamiza bwanayo
@FosterChilumba
@FosterChilumba 20 күн бұрын
Who told u Chilima ndi wa nzeru?
@MwizaChavula
@MwizaChavula 20 күн бұрын
Bad idea
@paulmakaula4937
@paulmakaula4937 20 күн бұрын
ZOONA
@wilsonmmangeni9888
@wilsonmmangeni9888 20 күн бұрын
useless discussion ever. analedzela awa
@Felix-os3oq
@Felix-os3oq 20 күн бұрын
Ma scientists a fake.
@alexsumani6823
@alexsumani6823 20 күн бұрын
Olo utatha mpando opanda ntchito anthu ake sakondana 😮😮
@user-lc3sw8iz2g
@user-lc3sw8iz2g 20 күн бұрын
Akufuna kubweletsa u prime minister
@FosterChilumba
@FosterChilumba 20 күн бұрын
Good idea office of vice President is just wasting pples taxpayers money Koma nanga president yo passed on?
@JulianaNyerere
@JulianaNyerere 20 күн бұрын
Km ziliko ku bomako
@paulmakaula4937
@paulmakaula4937 20 күн бұрын
Guys nanuso you are piling too much to the already power intoxicated president! Create mmalo mwa "VICE PRESIDENT" to "PRIME MINISTER" like ku ZIM...mpatseni ntchito zake PRIME MINISTER" plus delegation from president pomwe zangakwanitse...koma Prime Minister go in all ministries to ensure ntchito ikugwirika...MULI BUSY PROTECTING PRESIDENCY ....Don't forget ma president ambiri amakhala clueless then with Prime Minister zitha kumayenda
Joven bailarín noquea a ladrón de un golpe #nmas #shorts
00:17
КАХА и Джин 2
00:36
К-Media
Рет қаралды 3,8 МЛН
HOT CURRENT/=ACHILIMA ALOWERA KUTI?
27:28
HOT 265
Рет қаралды 21 М.
SABC News Election Coverage | 29 May 2024
SABC News
Рет қаралды 1,2 М.
Iran President Raisi Killed in Helicopter Crash | Balance of Power
44:47
Bloomberg Television
Рет қаралды 6 М.
Labour’s Plan to Solve the Rental Crisis Explained
8:24
TLDR News
Рет қаралды 162 М.
Iran President Raisi Killed in Helicopter Crash | Bloomberg The Pulse 05/20/24
43:14
Expresso Show | 29 May 2024 | LIVE
Expresso Show
Рет қаралды 162
The Times Malawi Report: CCPF Impresses South African Officials
2:51
Elections 2024 |  IFP's Sizonqoba Final Rally
1:35:30
SABC News
Рет қаралды 4,5 М.
Joven bailarín noquea a ladrón de un golpe #nmas #shorts
00:17