HOT CURRENT/=ACHILIMA ALOWERA KUTI?

  Рет қаралды 30,373

HOT 265

HOT 265

23 күн бұрын

Пікірлер: 62
@JosephLemani-qq1is
@JosephLemani-qq1is 21 күн бұрын
Chilima akuyenela kubwelela ku dpp ndipo akhoza kukhala ndi ubale wabwino ndi amalawi komanso azakhala president otsatila pambuyo pa a Peter muthalika kusiyana ndikupitilila ndi mcp palibe angapange chanzeru koma hot current iyi ma guys mukukamba chilungamo zedi from durban south africa
@stevenbanda2409
@stevenbanda2409 19 күн бұрын
Mbavayo, lkhale konko ku alliance, UDF and DPP, Musa lore ku joiner ndi UTM leader.
@danielmsowoya9107
@danielmsowoya9107 21 күн бұрын
UTM ikasiyana ndi MCP, MCP should forget that it can win on her own. It's better to stick to their initial agreement failure which they are out of power come 2025!!!
@user-jd9yz5hp7y
@user-jd9yz5hp7y 21 күн бұрын
Zikhoza kukhala bwino kwambiri kuti asadzalamulile chifukwa onsewa ndi osandalilika osakonda dziko lawo atipatsa umphawi kwambiri anthu awiriwa
@FatimaUmali-pc8sy
@FatimaUmali-pc8sy 21 күн бұрын
Chili a abwerere ku dpp ngati akufuna kukhala piece of mind
@SolokingChimzy-yt7dj
@SolokingChimzy-yt7dj 17 күн бұрын
Zoona che Fatima...that's only the truth koma akabwelelaso akhala peace of mind komabe mtendele wake ukhala osakoma
@mozykavalo7352
@mozykavalo7352 18 күн бұрын
Amalawi aaaa tizingokhalila mcp utm dpp dzikoli anzelu ndi okhawo lets allow God to choose magufuli for us as nation not za dpp analephela kale amenewo ine nduona kuti its God who can giv us a leader like magufuli
@PrinceKachimanga
@PrinceKachimanga 20 күн бұрын
without UTM...MCP should forget kulowa m'boma...one a chakwera saadziwa kuyankhula😂😂😂😂😂😂😂😂
@JoshuaNyirongo
@JoshuaNyirongo 21 күн бұрын
Noise vs news
@DysonMuwata
@DysonMuwata 21 күн бұрын
These gentleman are mabomba. Amaganiza. Bravo wonder , Chunga and Pankuku
@goodbossmw2468
@goodbossmw2468 20 күн бұрын
bushit ,onse aturuke(utm&mcp)
@DanielChikoti
@DanielChikoti 14 күн бұрын
Chilima my Vote whatever. He changed the mindset of many people. Chilima Chilima Chilima!!!!!
@user-dl1dg4yz1j
@user-dl1dg4yz1j 21 күн бұрын
Anyapapi mwadya za MCP akatero. Bring back Brian Banda
@FrancisStima-sc7zs
@FrancisStima-sc7zs 21 күн бұрын
UTM ndi MCP isatayane Ngati akufuna ipitilile kulamula kupandaapo ai DP P ndibwanawao osewa
@greysondymon890
@greysondymon890 15 күн бұрын
Forget about winning . Their unity will remain a casualty.
@HarrisonHara
@HarrisonHara 21 күн бұрын
Amukhomelera chilima koma paja sataya Mtima nkatundu ameneyu😂😂
@chitanibenito1109
@chitanibenito1109 21 күн бұрын
A chilima ali ngati wa khungu yemwe ndiwongosatira kuli konse komwe owona akupita, this tym also he will b used koma zoti akhale ndichiyembekezo choti mikango ya mcp ingampase mpata ayiwale izo ndiye ayiwale.
@StivinMabandi
@StivinMabandi 21 күн бұрын
❤dpp piter oyeee
@OsmanOsher-sh6gp
@OsmanOsher-sh6gp 21 күн бұрын
Popanda UTM ku MCP , tiyiwale kuti MCP ikudzalowanso m Boma believe me
@africahasani-gl2nq
@africahasani-gl2nq 20 күн бұрын
Chilima ndi munthu modzi ozakonetsa kwambili dziko la malawi
@user-nj5vu8cd5l
@user-nj5vu8cd5l 21 күн бұрын
Utm my future my vote
@isaacmsumba127
@isaacmsumba127 21 күн бұрын
UTM 🔥
@godfreykhungwa8316
@godfreykhungwa8316 19 күн бұрын
SKC is the Main character that's why he is always on people's mind en thought,,,,,,come rain or sunshine SKC & UTM is the next president MALAWI....!!!!!!!
@kondwanichiwanda
@kondwanichiwanda 22 күн бұрын
UTM my vote
@shaddaimaonga5832
@shaddaimaonga5832 21 күн бұрын
Brian banda & kasakula miss you guyz pa show imeneyi
@UmarAjussu
@UmarAjussu 20 күн бұрын
UDF AND DPP ❤
@user-qg4it7my9n
@user-qg4it7my9n 21 күн бұрын
hot hot mumakwana watching from cape town malawi waora ndi mbuzi za atsogolerizi
@SamuelMukhura
@SamuelMukhura 20 күн бұрын
you are right my vote is for Chilima
@RobertLuka-wy9cl
@RobertLuka-wy9cl 21 күн бұрын
Mcp utm palibe angauze amalawi alephela basi
@samdiverson9733
@samdiverson9733 19 күн бұрын
Apm only hope for Malawians chilima ummmm sanazipeleke Nsembe ku mtundu wa amalawi
@NumbDee
@NumbDee 21 күн бұрын
Ndamva kukoma kwabasi
@wanangwamwafulirwa8839
@wanangwamwafulirwa8839 16 күн бұрын
Program yokoma kwabasi.....komano Brian Banda akakhalapo....bwezi zakomesesa
@rafiqlimbilira940
@rafiqlimbilira940 20 күн бұрын
Munagwirizana kuti lero muvale Uniform pa program yanu😄
@user-zo3bf3ec3g
@user-zo3bf3ec3g 21 күн бұрын
Malamulo akuno kumalawi kawili kawili timapanga pofuna kuthana ndi ndiwina Kapena Pofuna kusangalasa wina
@AustiniHendersoni
@AustiniHendersoni 20 күн бұрын
Nosenu dzitsilu mungamaganize zot munthu akukhudzidwa ndikatangale akhaleso president zaziii
@beinhardkausiwa7107
@beinhardkausiwa7107 21 күн бұрын
Dpp❤
@alicemalika677
@alicemalika677 21 күн бұрын
Ndizolowele ndikudyere mwana
@user-fb6kh2dk1y
@user-fb6kh2dk1y 17 күн бұрын
my die hard SKC
@giftbanda7690
@giftbanda7690 21 күн бұрын
Chilima abwerele ku DPP izizi nde zikhoza kumuyendela kupezaso Chiyembekezo chose cha amalawi than ukuku alike ndithu
@user-jd9yz5hp7y
@user-jd9yz5hp7y 21 күн бұрын
MCP and UTM onsewa sitikwafuna atikwana azipita akangwele
@user-pl8kw3dc9d
@user-pl8kw3dc9d 22 күн бұрын
Chakwera ndi chilima ndimanyi pakholo panu
@MozzyBSaimon
@MozzyBSaimon 22 күн бұрын
Koma ma guy inuyo ndinu 1 mumakambilana nkhani zogwila mtima komanso zomasula mtundu wa Malawi. From RSA
@WezzieBaloyi
@WezzieBaloyi 22 күн бұрын
Nde ife a UTM tsitikuyifunaso
@osmanwanja3733
@osmanwanja3733 21 күн бұрын
Kkkk
@user-xx4jb9se3z
@user-xx4jb9se3z 21 күн бұрын
Mbava izi zikuganiza ngat ziwinanso zofanana mapiko mbalame zimaulukira limodzi. Komanso chilima nso naye was wandikhumudwitsa.achilima losing mwaila???????
@marryphili5419
@marryphili5419 20 күн бұрын
Munthu wakuba kukharaso president zosatheka iesh
@PatrickMailos
@PatrickMailos 19 күн бұрын
UTM bwerelani ku DPP kuti Zanu zikuyendelani
@MozzyBSaimon
@MozzyBSaimon 22 күн бұрын
Chilima ndi chakwela mapolo awo ndi omwe akuononga ndalama za a Malawi
@prettytambala5687
@prettytambala5687 22 күн бұрын
Asatinyase, pa keliyala zaka zingati? Azitenga laws lammanja beru
@giftbanda7690
@giftbanda7690 21 күн бұрын
Ndipo inu zaziii ati mene anayambila kutiuza mawu awa a akwana
@user-yh3ys3qn6p
@user-yh3ys3qn6p 20 күн бұрын
Chisilu galu iwe, mwana wa hule ya zelu
@ChimwemweGwape
@ChimwemweGwape 15 күн бұрын
Nzeru zake zatha chilimayyo
@jamesgama5489
@jamesgama5489 21 күн бұрын
Chilima ndi tambwali
@Zaid-ut4ob
@Zaid-ut4ob 22 күн бұрын
😮
@user-xz7mo8zy8f
@user-xz7mo8zy8f 21 күн бұрын
Propaganda against UTM
@Henry-vw2cz
@Henry-vw2cz 20 күн бұрын
Mbava😂😂😂😂😂😂
@lloydmalenga305
@lloydmalenga305 16 күн бұрын
Atambwali sametana
@FatimaUmali-pc8sy
@FatimaUmali-pc8sy 21 күн бұрын
😅😅😅😅
@ishmaeldama8906
@ishmaeldama8906 22 күн бұрын
Kariat is not good woman
@Abdul-xk8dq
@Abdul-xk8dq 21 күн бұрын
Koma mukunenazi amalawi ziwapindulilanji mumangolimbana za chilima eee chakwela atolankhani inu useless
@levisonmthawanji4232
@levisonmthawanji4232 21 күн бұрын
This is bringing people into reality of what is on the ground politically
2024 Elections | 3D analysis of the election data
10:54
SABC News
Рет қаралды 357 М.
ZOMWE ZIKUCHITIKA KU NTCHERU 🙌🙌
24:02
HOT 265
Рет қаралды 16 М.
Кәріс өшін алды...| Synyptas 3 | 10 серия
24:51
kak budto
Рет қаралды 1,3 МЛН
PINK STEERING STEERING CAR
00:31
Levsob
Рет қаралды 20 МЛН
Whyyyy? 😭 #shorts by Leisi Crazy
00:16
Leisi Crazy
Рет қаралды 19 МЛН
Jack Barsky: KGB Spy | Lex Fridman Podcast #301
3:37:34
Lex Fridman
Рет қаралды 6 МЛН
KULONDOLOZA ZA IMFA YA AGNESS KATENGEZA...@MibawaStudios
18:50
LIKI-LIKI TELEVISION
Рет қаралды 40 М.
JOHN KAPITO WATOPA NAYE CHAKWERA. Ityoke ityoke Osabisa mau // PART 1
33:23
GWEDE-GWEDE WA LERO KWAYAKA MOTO🔥🔥21 May 2024
28:02
HOT 265
Рет қаралды 30 М.
MAI JANE ANSAH (TIPPEX) part1....
41:52
LIKI-LIKI TELEVISION
Рет қаралды 34 М.
Bingu from Perth & Asia Part 8 - Press Questions 1
13:21
Nkhani Digest
Рет қаралды 205 М.
Кәріс өшін алды...| Synyptas 3 | 10 серия
24:51
kak budto
Рет қаралды 1,3 МЛН