MA AMERICANS ONSE NDI AMODZI NDI ISRAEL.CHIFUKWA MA AMERICANS ONSE NDI ANA A ABRAHAM.+ ISAAC + JACOB.NDIPO MALO ATACHEPA ENA ANAPITA KU AMERICA .KUKAPEZA MALO OWAKWANA.KUTI ADZIKALIMAKO..KOMA ISRAELNDI AMERICA NDI AMODZI.MA JEWS.KUPATULA MA RED INDIANS ONWE ALI AENI AKE A KU AMERICA KO
@AlexManuelMisomali-sv1vn5 күн бұрын
Zoonadi bola America itenge Malawi popedza talephera kuzilamulira tokha
@GoodsonMtambo-e9g4 күн бұрын
Ndipo love atenge maliwiyi bs
@kennedybanda5 күн бұрын
Koma ndiye
@MelvinShawa5 күн бұрын
Mmmm a Malawi kutengeka basi
@YassimineRasheedКүн бұрын
Bora atengenso malawi, chonde tikufuna tikhare ma mericans
Aaa wachedwa ameneyo ife achakwera yatipeleka kale ku tadzaniya apa gati tatsogoza nyanja tatsala patiso
@shukurajaaffarie-cr2nm5 күн бұрын
Mmesa iwowo ndi amodzi. Ine sindikulola mawo ndipangapo kanthu...
@Felista-m4q5 күн бұрын
Tikunzunzika atitenge
@ERNESTONANSONGOLE-m5pКүн бұрын
😂😂😂😂
@JulietLizziePhiri4 күн бұрын
Eya ifenso please
@AchinaKellz5 күн бұрын
Yes 😂
@ChikuMega5 күн бұрын
Atitenga pokhapokha chakwela akachoka pa mpando
@PempheloAmoni5 күн бұрын
Fuso langa nali athuwo akawachotsa kutengedwa ndimayiko ena kenako akamaliza kumanga adzawabwelezetsaso mmalo mwawo kapena ayikamo athu aku America???
@FahzKananji5 күн бұрын
Welcome to Malawi Trump
@DanielShaba-z6s5 күн бұрын
🎉
@AlwayneH5 күн бұрын
Atengedi Ineyoso ndavomeleza mmmm malawi is not a country only but also a though prison
@rashidadan25335 күн бұрын
Not allowed America to invade GAZA , let palestinian's to have their state , let them be free , Ku malawi kunonso azabwele , zinthu ziyamba kuyenda bwino Professor Peter muthalika akayambanso kulamulila