We are reacting and commenting on what the former MCP publicity secretary is saying about Tonse Alliance Government failure to fulfill campaign promises.. Malawi is Worse off than it was 5 years ago...he admits!!
Пікірлер: 23
@FrancesMitengo-p2d6 ай бұрын
Mai inu God bles you mai navicha
@KCS-vk3ce6 ай бұрын
Wanzeru Akuona apa kuti vuto ndi Muthalika. Ana kufika pokunthana paguru kholo lawo limawalangiza zichani?
@estherkauyange65486 ай бұрын
Warembembawe ndiwe wa mcp..... Iwe vuto siukuona kuti botomani akuombera mmanja za age limit poti akufuna kukhaulisa muntharika poti adachosedwa kuchipani Ali ngati oima paokha!
@AndrewMdala6 ай бұрын
Achinyamatawo ndiyawo zawanyela😂😂😂
@FrancesMitengo-p2d6 ай бұрын
Dziko la Malawi chibwana chikuchuluka kwambiri
@GiboTakondwa6 ай бұрын
Age limite ma mp nawonso
@AndrewMdala6 ай бұрын
Nayeso speaker sadziwa ntchito hule la chabe chabe
Zamanyazi kudpp nawoso asuleman nkhalidwe alibe zoona mpaka kumenyana nkhani yongokambilana chipani cha chikwanje lero ayamba kumenyana okha okha kudpp
@juniortsegula38476 ай бұрын
Botoman ndi chirenga mboli ya manu mufa
@VenançioZocueza6 ай бұрын
I we achakwera ali ndi mphamvu ngati mnyamata koma boma likuwanyera.nkhanza kwa anthu anzeru oti amatha ntchito.samalani amalawi umphawi sudzatha,mbambadi.
@giftphiri5956 ай бұрын
Kodi Joe Biden ali ndi zaka zingati tiuzeni tiziwe phindu la age Limit!.
@kondwanimunthali74016 ай бұрын
Achita bwino kumukuntha Botoman.Chilengayo nayonso he is very useless 😊
@PaulMvuma6 ай бұрын
Dpp sichipani ndi nkhondo, zoona aliyese azingochokela ku thyoro mulomwe, dyakanani mwekha wa dpp, my vote to Mcp