Atuma apolisi kuti athane ndi opposition & social media

  Рет қаралды 66,781

Bakili Muluzi TV

Bakili Muluzi TV

Күн бұрын

Пікірлер: 758
@mosesphakamisa5406
@mosesphakamisa5406 2 ай бұрын
The Best TV in Malawi 🇲🇼.... BMTV Bringing yout the hidden secrets, Historian 100%
@kidaadams
@kidaadams 2 ай бұрын
Koma anthu zinthuzi mumazitengela chibwana, ngati Dziko this is an alarm to wake us up
@JonesChingaya-yf4gg
@JonesChingaya-yf4gg 2 ай бұрын
Ndipo live zimafunika tikamva chonchi tizichitapo kathu, koma vuto ndi apolice ndi a army coz ndiomwe akugwirisidwa ntchtooo
@Mtonga-m9b
@Mtonga-m9b 2 ай бұрын
You are right.... Koma basi kaya mkutani? Tonse tikumamvera daily koma basi kaya ozindikira ndi ophunzira akutani kaya
@SaidyKamala-jj7lo
@SaidyKamala-jj7lo 2 ай бұрын
Kk😂😂 guys mpaka gondolosi ayii chakwela asowe guys bola tivotele bakili muluzi tv 😂
@ganizankabango
@ganizankabango 2 ай бұрын
BAKILI MULUZ TV FANS LET'S GATHER HERE
@peterchipala1822
@peterchipala1822 2 ай бұрын
@IshmaelNesta-rb8dx
@IshmaelNesta-rb8dx 2 ай бұрын
Here we are....💪
@Mohammed-sk1fy
@Mohammed-sk1fy 2 ай бұрын
Power
@IsmaelBilal-lh1pi
@IsmaelBilal-lh1pi 2 ай бұрын
Freedom fighter 💪
@HappinessKapombeza-ut9mo
@HappinessKapombeza-ut9mo 2 ай бұрын
We are HERE.
@VictorCustom-my1nv
@VictorCustom-my1nv 2 ай бұрын
Akamuna
@ChimwemweKondowe-nj4lx
@ChimwemweKondowe-nj4lx 2 ай бұрын
God is using you in our generation to bring light to the blind. May good Lord keep protecting you
@usherjamson174
@usherjamson174 2 ай бұрын
Inuyo man ndinu machine mumadziwa zisisi za zitsilu izi 💪💪
@jonathanphiri-t2i
@jonathanphiri-t2i 2 ай бұрын
😂😂😂😂😂😂😂😂😂
@JafaliChiwimbi
@JafaliChiwimbi 2 ай бұрын
Kkkkkkk ❤❤❤
@PaulKagona
@PaulKagona 2 ай бұрын
Osamachemerera zopusa
@usherjamson174
@usherjamson174 2 ай бұрын
@@PaulKagona poti kupusa umakuona iweyo ukakhala opusa oyamba
@BlessingsBanda-ih4th
@BlessingsBanda-ih4th 2 ай бұрын
​@@PaulKagona zopusa zimeme ukuyankhula iwe zapamutu ziiiiiii😂😂😂😂😂
@VINCENTKADZINJA
@VINCENTKADZINJA 2 ай бұрын
Ulemu wanu amwene koma muzihala utali kuti asazakupezeni timakufilani💪💪💪
@lovemoremandala7420
@lovemoremandala7420 2 ай бұрын
😂 ndiye mwati anadya gondolosi
@StevoZimba
@StevoZimba 2 ай бұрын
😅😅😅😅😂😂😂😂​@@lovemoremandala7420
@mustapherallie6448
@mustapherallie6448 2 ай бұрын
Kunena moopa mulungu nkuluyu amalawife akutifela akusakidwa koma akutiuzabe chilungamo guys lets vote mwanzelu
@Mohammed-sk1fy
@Mohammed-sk1fy 2 ай бұрын
Kwambiri
@petergwetsani1150
@petergwetsani1150 2 ай бұрын
Kwambir man
@paulmgombebanda-mr19sate
@paulmgombebanda-mr19sate 2 ай бұрын
Ndipo Ambuye atitsogolere
@neemahkapatamoyo9563
@neemahkapatamoyo9563 2 ай бұрын
Mposoo
@Evason888
@Evason888 2 ай бұрын
Mashallah
@JamesKhudze
@JamesKhudze 2 ай бұрын
Now ndkugona ndimadkra munthu wamkulu ❤❤❤❤
@BrianMuleke
@BrianMuleke 2 ай бұрын
Muzibwera daily umakwana
@NtloniphoNodimbaza
@NtloniphoNodimbaza 2 ай бұрын
Abisala mmbatata koma mmtsana ukuoneka osawasiya akubawo We love you Mmtola mkhani wathu nambala wani ku Malawi komanso to the World
@JEVICO-MW
@JEVICO-MW 2 ай бұрын
Kuba,kupha ndi kuononga😆🙌 ndilibe lawyer ine
@Sleemsteri
@Sleemsteri 2 ай бұрын
A man with a flowery speech without action
@AlgentChilanga
@AlgentChilanga 2 ай бұрын
Yes that's Mr chikangawa Mr chifunga kapena Kain kkkkk
@JOELMoyo-m6u
@JOELMoyo-m6u 2 ай бұрын
Kkkkkkkk malume ajatu kuno aing'alura eeee saopa ayiiii
@cynthiakananji1608
@cynthiakananji1608 2 ай бұрын
Bakili Muluzi timangokumbukila nthawi yomwe tinkamvera sewero la John chilembwe pa radio.now panopa ukaiona msanga umakhala number 1 kutumizila azinzako kut naonso amvere news ya bakili muluzi.coz he is real not even the comedy.coz mwatsegula Mitu ya anthu ochulika.May the good Lord protect and comforting you with the blood of Jesus where ever you are ❤
@sahasalanje4786
@sahasalanje4786 2 ай бұрын
Umatiimirira chabwino kumalawi kuno kuli maluzi but tikanvera zomwe umatibweresera timazaona ngati tikupasidwa ndarama usazasiye bro GOD bless you
@Evason888
@Evason888 2 ай бұрын
😂😂😂 Mawu okhawo ndi gaiwa paokha
@AngolanChinga
@AngolanChinga 2 ай бұрын
Ndiponso kwambili
@JafaliChiwimbi
@JafaliChiwimbi 2 ай бұрын
Ndi zoona
@rightlombe380
@rightlombe380 2 ай бұрын
Anakomoka ndi agness ku room 😂😂😂 chipongwetu
@coastersRob
@coastersRob 2 ай бұрын
kkkkkkk
@JohnConar-kq4hi
@JohnConar-kq4hi 2 ай бұрын
😂😂😂😂😂 eish amalawi 😢
@zimmekapachika6784
@zimmekapachika6784 2 ай бұрын
😅😅😅😅😅😂😂😂yomweyo mr Chikangawa 😅😅😅😅😅
@victormwamadi2725
@victormwamadi2725 2 ай бұрын
😂😂😂😂😅
@SamKaposa-i5c
@SamKaposa-i5c 2 ай бұрын
Akuti imodzi yokhatu😂😂😂😂
@OFG-th3st
@OFG-th3st 2 ай бұрын
Agnes kukomoketsa wapolisi😂😂 Komatu a Agi mwayaka moto😂😂😢
@SamKaposa-i5c
@SamKaposa-i5c 2 ай бұрын
😂😂😂😂😂😂😂
@DeenesNurudMeke
@DeenesNurudMeke 2 ай бұрын
Kkk
@FrankDingah-if7vz
@FrankDingah-if7vz 2 ай бұрын
Kkkkkk
@HannahNtenda
@HannahNtenda 2 ай бұрын
😂😂😂😂
@ShadyDaHustler
@ShadyDaHustler 2 ай бұрын
Much respect bro ❤❤watching from Nigeria, Lagos
@ronaldordinga6537
@ronaldordinga6537 2 ай бұрын
Akulu a kulu apa sipakufunikaso kumusiyira mulungu ayi,,,,, mulungu mbari yake akuchita daily koma tatiyeni monga ife nzika titengepo gawo pochita ziwonesero kusonyeza Kuti tanyasidwa nazo akupangazi osamangoyamikira wa muluzi tv daily achina big up koma ku ma demo ndikuzakhala nde tapanga chani apopo
@stevemtambalika
@stevemtambalika 2 ай бұрын
Zoonadi Mulungu do amathandiza olimbika so ifeyo tangokhala chete mmal
@NoohNowa
@NoohNowa 2 ай бұрын
Anakomoka ndi ageeness kubedi ndiye angathane ndi Ife 😂😂😂😂😂❤❤
@AlgentChilanga
@AlgentChilanga 2 ай бұрын
Yomweyo our president of information l salute kudya gondolosi ndikukakomoka achepa nanu bigy sangakupezeni akuzinamiza kwabasi kkk
@webstermbewe8395
@webstermbewe8395 2 ай бұрын
We have been waiting for this continue to give us the best analysis of what is happening around the world
@JeanBanda-zy6wu
@JeanBanda-zy6wu 2 ай бұрын
Akomoka bwanji ku room atatafuna gondolosi 😂😂😂😂😂😂😂😂😂 yomweyoooo chigangawa, we love bakili muluzi TV ❤
@P.Bilali
@P.Bilali 2 ай бұрын
Bakili Muluzi TV... asazafe.... U keep us updated and mwina zina zimakanika kuti zitike poopa kuti uying'alula
@InnocyLee
@InnocyLee 2 ай бұрын
Koma inuyo you are brotherhood best tv in Malawi
@SannyChifambi
@SannyChifambi 2 ай бұрын
Keep good work of inspiring the nation
@lingsonmitunda293
@lingsonmitunda293 2 ай бұрын
Maso ndi makutu za dziko la Malawi. Thank you BMTV.
@SamKaposa-i5c
@SamKaposa-i5c 2 ай бұрын
Exactly
@lysonkaselema7321
@lysonkaselema7321 2 ай бұрын
Malume uyu waposa pa makutu koma mapilikanilo asaa
@ChikumbutsoJohn-rs4tt
@ChikumbutsoJohn-rs4tt 2 ай бұрын
You're the best thank you for Good job
@MathewsMafaiti
@MathewsMafaiti 2 ай бұрын
Keep it up my boss matimilira big man ✊✊
@LamieTiger
@LamieTiger 2 ай бұрын
Achoke chakwera we don't want him anymore
@Laurent-h9u
@Laurent-h9u 2 ай бұрын
Thank you so much for updating us as Malawian wake up 😢😢😢
@MrBanda-w6o
@MrBanda-w6o 2 ай бұрын
Uncle osaopa mulungu Ali mbali yanu amatetenza anthu ake inuyo ndiwosakhidwa😊❤❤❤
@kubengovender6996
@kubengovender6996 2 ай бұрын
Tell us more and more, chakwera ndichitsilu mbolo yamake !!
@OusmanDavie
@OusmanDavie 2 ай бұрын
VUTO malawi kugona Hrdc. Pac onse ndi agaru awa anagulidwa
@philipoga2401
@philipoga2401 2 ай бұрын
silute fadah much love asakufuna asiye iwe ndi wathu wathu bakili muluzi tv machine amphepo
@PeterMoloko-lr3wq
@PeterMoloko-lr3wq 2 ай бұрын
Kkkk and I quote 'anadya gondolosi mkukakumana ndi hule ku lodge kumenya round imodzi mkukomoka'.......
@Benson-cf6qd
@Benson-cf6qd 2 ай бұрын
😅....mpaka kukomoka chifukwa cha Agnes 😊😊
@BrightZionga
@BrightZionga 2 ай бұрын
😂😂😂😂 koma big inuyo mumatha❤❤❤ just stay alert please
@Aisha-db6ds
@Aisha-db6ds 2 ай бұрын
Iponden fadah , kukomoka ku room ndi Agnes Sha😮
@MadaBuleya
@MadaBuleya 2 ай бұрын
Chilima may your soul continue resting in peace.dziko pano ndimasanje
@MohammadShek-u4k
@MohammadShek-u4k 2 ай бұрын
Akuluwa amakamba chilungamo chifukwa sikanakala zonama bwesi asqkusakidwa komano kusakidwako akuwaulula somwe akupa zonama bwesi akuti ndiwamisala komano sangamukwanise ndipo tikumufunira wabwino sonse
@watchman731
@watchman731 2 ай бұрын
Exactly....sangakhale busy kumamusaka had it been kuti sakunena chilungamo , ndekuti chilipo...
@DavieNhlane
@DavieNhlane 2 ай бұрын
Koma man inuyo mmmm .unadziwa bwanj zot akuluwa anakomoka atamenya round imodzi 😂😂😂😂😂.thats why i always say that you are speaking from heaven
@actuarialscience2283
@actuarialscience2283 2 ай бұрын
Agness, chonde chepetsa kunyekhulira mbolo. Usaphe apolisi ambiri. Chepetsa kunyekhulira mbolo agi.
@GiftMlinde
@GiftMlinde 2 ай бұрын
Iweee ndikatunduuu GOD protecttt u
@AyandaPhungula-bg9ql
@AyandaPhungula-bg9ql 2 ай бұрын
The best and truth TV ❣️ mumatiyimilira big
@MussahNamalomba-e3p
@MussahNamalomba-e3p 2 ай бұрын
Ndiye mwati anakomoka ndiimozdi😂 eeee koma Agnes 😊😂
@REECEMw-o9s
@REECEMw-o9s 2 ай бұрын
❤❤❤❤❤ bakili muluzi TV ndiozindikila kuposa chewa ameneyi
@user-Grant260
@user-Grant260 2 ай бұрын
Much respect elder ❤❤watching from Venezuela in Caracas
@manzyhetekele8697
@manzyhetekele8697 2 ай бұрын
Keep it up brother 💪 we love your work 👏 😊
@gifahumphrex2454
@gifahumphrex2454 2 ай бұрын
Our best Chanel ❤
@MilitaryYusuf
@MilitaryYusuf 2 ай бұрын
Respect to u .history is a best teacher
@KassoCompany
@KassoCompany 2 ай бұрын
Being first to watch!!!!❤❤ Ndipaseni udindo bwana bakili muluzi tv😂😂
@JacksonMoyo-tm8dv
@JacksonMoyo-tm8dv 2 ай бұрын
Father of history like herodotus, you are the one
@khambisan
@khambisan 2 ай бұрын
Kkkkkk now its time to open a eyes thi is true massage 💪💪💪💪💪
@DimoraMvalo
@DimoraMvalo 2 ай бұрын
Koma inuyo big ndi number 1 ❤❤ ndimakunyadilani heavy
@JasperKaleni-dx6nn
@JasperKaleni-dx6nn 2 ай бұрын
Ife sitingakusiye wekha ❤❤best tv
@MichaelJannah-hn9qv
@MichaelJannah-hn9qv 2 ай бұрын
God bless you Bakili muludzi tv
@livinesspasseli5044
@livinesspasseli5044 2 ай бұрын
Kkkkkkk apa ndye mamalidza machedza bosss Mpaka kukomoka ndi gondolosss for 3 days kkkk
@MillieMalakam
@MillieMalakam 2 ай бұрын
Iweyo umaziwa history ndithu ndikuhala Khani bwino aaaa maulemu ako basi Allah guide u
@emmanuelkampira6950
@emmanuelkampira6950 2 ай бұрын
❤❤❤ it's our prayer for you to be safe always. 👑
@jonathanphiri-t2i
@jonathanphiri-t2i 2 ай бұрын
😂😂😂😂😂😂Anakomoka ndi Agness koma Agnes ai zikomo kkkkkkkkk 🤣🤣
@JosephSamson-g1h
@JosephSamson-g1h 2 ай бұрын
Popanda inu ife tili m'mazi bro kept up🙏🙏
@idrisshtambala
@idrisshtambala 2 ай бұрын
Koma iweyo umakwana ❤❤❤ndiwewachikondi chodzadza usazasiye timakhala ndithawi yokuvetsela ndipo timakudalilakwambili
@RiteRoderick
@RiteRoderick 2 ай бұрын
Malawi Chikangawa Party out in the name of Jesus. Ndipo mademo mwezi unowo tinyetetsa zedi pa 31
@DeenesNurudMeke
@DeenesNurudMeke 2 ай бұрын
Kuchema kkk
@PeterLemani-jk3mw
@PeterLemani-jk3mw 2 ай бұрын
You're the best tv in the world
@AustinYusuf-do4vz
@AustinYusuf-do4vz 2 ай бұрын
😅😅😅😅😅 ati ngati anakumoka ndi agines kuli bwanji Bakili mulunzi TV Kkkkk kkkkk 😂😂
@mayesoedisonmatama86
@mayesoedisonmatama86 2 ай бұрын
Inuyo big ulemu wanu, mumasata zinsisi zonse za dziko lathuli, may God protect you always, boma la mcp ndi la nkhanza koopsa
@robertrichman9376
@robertrichman9376 2 ай бұрын
You and Kalindo are the only heros we have in Malawi
@mikemakamo7360
@mikemakamo7360 2 ай бұрын
One round fent 😂😂😂 sangamake ndimafana amenewa. Big up BM TV 📺
@Anthonymendos
@Anthonymendos 2 ай бұрын
Ilove you bakili muluzi TV, you is One
@PatriceKaomba
@PatriceKaomba 2 ай бұрын
God bless you mulungu akupatseni zosowazanu mudzina la yesu
@thokoayami6934
@thokoayami6934 2 ай бұрын
Ife tizapanga ma demo akazakugwirani, much respect to you brother
@Gorilla-k8e
@Gorilla-k8e 2 ай бұрын
Munthu wa mkulu kwambili bakili muludzi tv big up big bro
@EmmanuelZiba-qz6ug
@EmmanuelZiba-qz6ug 2 ай бұрын
l love you from Lusaka Zambia 🇿🇲🇿🇲 kucharo
@Addih_calyx_music
@Addih_calyx_music 2 ай бұрын
😂😂😂TELL DEM .FIRE BURNING #bakili TV to di world
@Justin_Nano
@Justin_Nano 2 ай бұрын
Best TV❤❤much love
@matembamadadada8291
@matembamadadada8291 2 ай бұрын
Respect captain love you to much 🎉🎉🎉
@matembamadadada8291
@matembamadadada8291 2 ай бұрын
❤❤
@ulemuchisale
@ulemuchisale 2 ай бұрын
History is the best teacher
@uzaleuzale8603
@uzaleuzale8603 2 ай бұрын
Pakufunika game kuyiwonera patali mapeto ake bomali kuti lidzalamulireso tidzakukuta mano that's why I love bakili muluzi tv every day
@MuhammadInack
@MuhammadInack 2 ай бұрын
Kkkkkkkk Agnes ayi zikomo🙌🙌🙌🙌
@FisherAction
@FisherAction 2 ай бұрын
God bless you big man keep it up
@dalitson3558
@dalitson3558 2 ай бұрын
We love you our own brother be safe wherever you are,
@lyiemax
@lyiemax 2 ай бұрын
The only number 1 TV station ❤❤❤❤
@giftjamali8204
@giftjamali8204 2 ай бұрын
Kkkkkk inuyo ndi katundu boss eee tataya kantengooo boss mwawiba basiiii
@Dee-h7c
@Dee-h7c 2 ай бұрын
LONG LIVE BAKILI MULUZI TV 🎉🎉🎉🎉
@Deajay-jn8cf
@Deajay-jn8cf 2 ай бұрын
😂😂😂😂😂Koma adah iweyo aaaah kayaa😂😂😂😂😅😅
@AnnaPhiri-b8t
@AnnaPhiri-b8t 2 ай бұрын
Mr chikangawa akuzimvera
@JoshuaNamauti-py4up
@JoshuaNamauti-py4up 2 ай бұрын
Kwambil big man inuy ndinuyo bc mumakwanila guy's tiyen tivote bwino bwino good night timadikila imeneyi❤❤
@joshuamasulani1190
@joshuamasulani1190 2 ай бұрын
Am just thinking during voting period muzinanena komwe akubera
@OZIELBLESSINGS
@OZIELBLESSINGS 2 ай бұрын
much proud of you sir🎉❤
@stevemtambalika
@stevemtambalika 2 ай бұрын
Koma chikangawayu eshhh see you 2025,bakili TV morefire and be strong
@jerryl.chadziwika8527
@jerryl.chadziwika8527 2 ай бұрын
Following from Libya
@hopembendela
@hopembendela 2 ай бұрын
You are are the number one bro
@DeenesNurudMeke
@DeenesNurudMeke 2 ай бұрын
Anthu wa kuasekerera ationongera dziko li ndithutu mmm zomvesa chisoni kwambiri esh
@JOELMoyo-m6u
@JOELMoyo-m6u 2 ай бұрын
Mumankhala malume you are number one
@innocentmabedi3850
@innocentmabedi3850 2 ай бұрын
Apapa ndigonano, bravo BM tv
@johnkatapeh7182
@johnkatapeh7182 2 ай бұрын
Tilibe chisisi pa dziko lapansi........❤❤❤❤❤❤bakili tv
@AffickChaona
@AffickChaona 2 ай бұрын
Best TV in Malawi bakiri Muluzi TV ❤❤
@Prodbysix40
@Prodbysix40 2 ай бұрын
<a href="#" class="seekto" data-time="179">2:59</a> u killed me 😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂🎉🎉
@StevoZimba
@StevoZimba 2 ай бұрын
Voice to the voiceless😊
Adaferanji mkulu wa asilikali a nkhondo, General Manken Chigawa
19:53
Bakili Muluzi TV
Рет қаралды 127 М.
РОДИТЕЛИ НА ШКОЛЬНОМ ПРАЗДНИКЕ
01:00
SIDELNIKOVVV
Рет қаралды 3,9 МЛН
小丑家的感情危机!#小丑#天使#家庭
00:15
家庭搞笑日记
Рет қаралды 32 МЛН
Mom had to stand up for the whole family!❤️😍😁
00:39
didn't manage to catch the ball #tiktok
00:19
Анастасия Тарасова
Рет қаралды 33 МЛН
Incredible Moments Caught on Camera
30:40
UNSORTED
Рет қаралды 4,6 МЛН
Ip Man 2 | The Boxing Competition
15:57
Cinewatch
Рет қаралды 8 МЛН
Abale ake a John Chilembwe ali kuti?
15:36
Bakili Muluzi TV
Рет қаралды 44 М.
Khothi la ICC likumufuna Zikhale Ng'oma; Mbava zovala ma suit ku Malawi
8:01
Zomwe Zinachitika Kut Ndege Isowe
5:19
Sam Malvitha
Рет қаралды 270 М.
Ong Bak | Fight Club Scene
15:05
Cinewatch
Рет қаралды 75 МЛН
РОДИТЕЛИ НА ШКОЛЬНОМ ПРАЗДНИКЕ
01:00
SIDELNIKOVVV
Рет қаралды 3,9 МЛН